I heard this from my mother. When I was young I use to attend Glory to God ministry, lords willing one of the faithful days wants to return their once again. Hearing from UAE Dubai❤
Mulungu akudaliseni chifukwa cha cha umboni wamphavu. Mu u bomboni wanu ndarimbikiskika mu zambiri. Zimozi mwa izo pa zimene mulungu anakuwoneskani. Naneso zina ananiwoneskapo. Nthawi za mbiri nimakayika kuti. Zoona izi ambuye mundikhululukire pokayika. Amen ambuye akhare nanu mai mawindo pa zonse 🙏
I heard this from my mother. When I was young I use to attend Glory to God ministry, lords willing one of the faithful days wants to return their once again. Hearing from UAE Dubai❤
Tipstseniko manambala a Mai maeindo chinde
Mulungu akudaliseni chifukwa cha cha umboni wamphavu. Mu u bomboni wanu ndarimbikiskika mu zambiri. Zimozi mwa izo pa zimene mulungu anakuwoneskani. Naneso zina ananiwoneskapo. Nthawi za mbiri nimakayika kuti. Zoona izi ambuye mundikhululukire pokayika. Amen ambuye akhare nanu mai mawindo pa zonse 🙏
Tilape ndithu kuti ambuye atikhululukire
Amen
Umbon umeneyo wapangisa kut ndidziwa zambiri Ambuye aremekedzeke
Ku mwamba kulemekezeke
Ndiomboni umenewu mtima wanga ufunafuna nkhope ya Ambuye Yesu nthawi zose.
Nanga mkukupezani bwanji kuti tifuse zambiri zonkhudza umboni umenewu
Chonde anthu tiyeni tilapedi kuti tisakapezeke ku gehena Malo amazuzo.
Ambuye aleme kezeke
Amen!! God help me
Umboni uwu wasuntha moyo wanga Ambuye alemekezeke
Zonama mukunenazo mai simungandiopsezeso
Amayi mumandidalitsa kwambili
Umboni umenewu wasitha moyo wanga
Zikomo kwambiri abusa chifukwa cha uthenga wanu.
Ambuye andichitile chifundo