MAYI MAWINDO

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 19 сен 2024
  • MAYI MAWINDO

Комментарии • 18

  • @Sheepfoldfood
    @Sheepfoldfood Год назад +1

    I heard this from my mother. When I was young I use to attend Glory to God ministry, lords willing one of the faithful days wants to return their once again. Hearing from UAE Dubai❤

  • @IsaacJere-w1m
    @IsaacJere-w1m Год назад

    Mulungu akudaliseni chifukwa cha cha umboni wamphavu. Mu u bomboni wanu ndarimbikiskika mu zambiri. Zimozi mwa izo pa zimene mulungu anakuwoneskani. Naneso zina ananiwoneskapo. Nthawi za mbiri nimakayika kuti. Zoona izi ambuye mundikhululukire pokayika. Amen ambuye akhare nanu mai mawindo pa zonse 🙏

  • @astridachirwa7743
    @astridachirwa7743 4 года назад +3

    Tilape ndithu kuti ambuye atikhululukire

  • @BeatriceKhunje
    @BeatriceKhunje 5 месяцев назад

    Amen

  • @vitumbikokaundah2968
    @vitumbikokaundah2968 3 года назад +2

    Umbon umeneyo wapangisa kut ndidziwa zambiri Ambuye aremekedzeke

  • @MaurineFunsani
    @MaurineFunsani Месяц назад

    Ku mwamba kulemekezeke

  • @sibongiresambojere3280
    @sibongiresambojere3280 7 лет назад +3

    Ndiomboni umenewu mtima wanga ufunafuna nkhope ya Ambuye Yesu nthawi zose.

    • @sibongiresambojere3280
      @sibongiresambojere3280 7 лет назад

      Nanga mkukupezani bwanji kuti tifuse zambiri zonkhudza umboni umenewu

    • @jemussijeremias1857
      @jemussijeremias1857 3 года назад

      Chonde anthu tiyeni tilapedi kuti tisakapezeke ku gehena Malo amazuzo.

  • @caiphusgondwe6961
    @caiphusgondwe6961 5 лет назад +1

    Ambuye aleme kezeke

  • @jemussijeremias1857
    @jemussijeremias1857 3 года назад

    Amen!! God help me

  • @jesimoyomoyo3206
    @jesimoyomoyo3206 4 года назад +1

    Umboni uwu wasuntha moyo wanga Ambuye alemekezeke

  • @nditumenichagunda4192
    @nditumenichagunda4192 Год назад

    Zonama mukunenazo mai simungandiopsezeso

  • @knowledgekamanga1011
    @knowledgekamanga1011 4 года назад +1

    Amayi mumandidalitsa kwambili

  • @AlvinJnr-rm6pe
    @AlvinJnr-rm6pe Год назад

    Umboni umenewu wasitha moyo wanga

  • @chifundomopiwa5944
    @chifundomopiwa5944 Год назад

    Zikomo kwambiri abusa chifukwa cha uthenga wanu.

  • @danaziokanjadza6147
    @danaziokanjadza6147 4 года назад +1

    Ambuye andichitile chifundo