ZOCHITIKA KU DPP🙌🙌🙌🙌

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 3 окт 2024

Комментарии • 111

  • @MuhammadSamson-yz1kl
    @MuhammadSamson-yz1kl 3 месяца назад +10

    APM my vote sitikufuna achikambelembere ayi APM ❤❤❤❤❤

  • @Drmuhammadchiwona
    @Drmuhammadchiwona 3 месяца назад +5

    Apm my vote

  • @chakakachaka-man
    @chakakachaka-man 3 месяца назад +4

    ADADI A.K.A FAZALA HOZA HOZA MY VOTE

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 3 месяца назад +2

    Apm the great man!!!! My vote achosedwe tisanyengelere zisiru za anthu ife zauthira kuwiri ayi!!

  • @GiboSunset
    @GiboSunset 3 месяца назад +5

    Kawawa achoke basi APM my vote

  • @danielmsowoya9107
    @danielmsowoya9107 3 месяца назад

    This man has a beautiful future in the circles of journalism, KEEP IT UP

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 3 месяца назад +4

    Bon Kalindo is good guy

  • @MaryMlomba
    @MaryMlomba 3 месяца назад +1

    More fire malawi dziko loop mulungu ilo . Ayerekeze wa kumidima kuvomeleza zopusazo.

  • @Leo-fj6gz
    @Leo-fj6gz 3 месяца назад +3

    APM activated 💙💙💙💙💙

  • @lyiemax
    @lyiemax 3 месяца назад +1

    Powerful!!!! inuyo mumatha guys, proud of you ❤❤❤

  • @KassimWilson-o8h
    @KassimWilson-o8h 3 месяца назад +4

    Peter si munthu wamba akuxiwa chomwe akupanga mukuwona ngat nd mcp

  • @Costance-nf7ue
    @Costance-nf7ue 3 месяца назад +4

    Yaaa Dpp sikusunga kape bwino masewela

  • @DouglasDazuKamwendo
    @DouglasDazuKamwendo 3 месяца назад +8

    DPP sikusunga kape or m'modzi

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 3 месяца назад +2

    APM is the only hope for Malawi

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga 3 месяца назад +2

    we love u peter mutharika❤❤

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 3 месяца назад +3

    Program ya Gwede-gwede ili very hot Masiku ano🔥🔥 YOHANE 8:32 Coonadi cidzakumasulani..

  • @DanielnachanzaBanda
    @DanielnachanzaBanda 3 месяца назад +1

    Apm my vote

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 3 месяца назад +2

    Tikufuna kuti tidziwe zoona komaso akamatiuza zomwe zinachitika kuti ndege igwe adziwe kuti sife Ana komaso sife Anthu osaganiza bwino and mikuluwiko timayidziwa 😢

  • @Chisomo-dh2gq
    @Chisomo-dh2gq 3 месяца назад +1

    Apm my vote

  • @AnnastasiaChakwiya
    @AnnastasiaChakwiya 3 месяца назад +3

    Apm my vote

    • @dalitson3558
      @dalitson3558 3 месяца назад

      Ifeso ndi a Dpp komano zomwe zikuchitika muchipanichi sizabwino ali zii or kususa boma lokubali

  • @peterkinsLekera
    @peterkinsLekera 3 месяца назад +1

    Awasiye koma dziwani kuti pali madera ena amawinira dzina la chipani ngati kumwanza balaka ndi thyolo mulanje lilongwe tchisi ndi dowa

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 3 месяца назад +1

    Eeeee achoke ndithu amenewo bwana ...
    APM vote vote vote

  • @SamuelMponda-y3d
    @SamuelMponda-y3d 3 месяца назад

    Nzeru yabwino aku Mibawa kuthandiza cipani cacitetezo, cilungamo ndi citukuko.

  • @retirementtoafrica
    @retirementtoafrica 3 месяца назад +4

    Ma cross over omwewo

  • @NoreenNaituri
    @NoreenNaituri 3 месяца назад

    Dpp inatha kale,nde bolanso chikomeni kk aphunguwo sakuonamo sogolo ata

  • @Aubreysekeyah
    @Aubreysekeyah 3 месяца назад

    Apm bomaaaAa

  • @PeterThomas-lw3io
    @PeterThomas-lw3io 3 месяца назад +3

    Malawi tivotele Atupele muluzi chifukwa his mind is very fresh
    Osati Chakwera

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 3 месяца назад

    DPP ikanawasiya anthu amenewa, tionana chaka cha mawa. Nthawi yatha kale.Bola taona mawanga awo. Akaime ngati independent tizaone ngati atazawine.

  • @PatrickGonagona
    @PatrickGonagona 3 месяца назад +1

    We a wise man like APM🙏

  • @jamesguduza
    @jamesguduza 3 месяца назад

    Chimkuza mau ….kukapanga gwedwe gwede kuti Aunt Tiwo akhaleno…. UNCLE TIWO…..😝💃🕺

  • @PatrickGonagona
    @PatrickGonagona 3 месяца назад

    We need a wise man like APM ❤❤

  • @MaxwellDzaone-ym1vg
    @MaxwellDzaone-ym1vg 3 месяца назад +2

    Fire💥💥💥

  • @owenmoses9434
    @owenmoses9434 3 месяца назад +1

    Page iyi ndayamba kuinyumwa!

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 3 месяца назад +1

    Ukuchita kudziwa kuti mkaziyu sakugwilika waponda mwala za iwe sakusamala umuyitane amveke ndili buzy bwerani tikambirane ndatanganidwa ndiye chopangira za ukwati ndi chani kuthetsa kupeza wina APM simwanatu ayi ndiye enanu mukungolubwa apa zamkutu achotse ma virus mu chipan amene angaononge kusogoloku .

  • @Zelinakhisswell
    @Zelinakhisswell 3 месяца назад +1

    Steve amandiwaza ati aise honorable uyerekeze 😂😂😂😂

  • @ramseycrown483
    @ramseycrown483 3 месяца назад

    I like you guys you talk and don't fear anyone. ❤

  • @MarthaMtonga-qt6tc
    @MarthaMtonga-qt6tc 3 месяца назад

    Adad vote yanga yilipo

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 3 месяца назад +1

    Peter anakalamba mutu wake udasiya kugwira ntchito bwino bwino

    • @GeraldChisamba
      @GeraldChisamba 3 месяца назад

      😂😂😂😂 just imagine 90 yrs kumafunabe u president musiyen adzagwa ndi BP gogo ameneyi

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms 3 месяца назад

    Vuto ndi respect aphunguwo alibe respect nd chipani chawo dpp kuchotsa anthu amenewa ine ndikuwona kuti vuto palibe what we need is respect.

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 3 месяца назад

    Guys mumavala boo big up.

  • @KhalideNerve-mu1eq
    @KhalideNerve-mu1eq 3 месяца назад +2

    Ndipo live zusonga makape thawi imeneyo tilibe

  • @LoganKulupando
    @LoganKulupando 3 месяца назад

    voterani adadi mulungu satayawache chipepeso 1biliyoni ngatizonama ndiyeeasawine mbavazozichoke

  • @CharlesPhiri-ds1rk
    @CharlesPhiri-ds1rk 3 месяца назад

    😂😂😂😂😂😂kkkkkkkkkk uyelekeze....udzasamuka muno Malawi....ukwat umakhara pakat pa mwamuna ndi mkazi

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 3 месяца назад

    Tizaifera mbendera iyi wina aziwaso

  • @robertkalima874
    @robertkalima874 3 месяца назад +1

    Cadet wafa basi

  • @StevenMjMbama
    @StevenMjMbama 3 месяца назад

    Steve apoo ponkha Nde wakwiya ndiyamathanyula 😂😂😂😂😂😂😂 amene azayelekeze tizamponda oyankhula zamathanyula

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma 3 месяца назад

    Pita muthalika simuthu wamba akudziwa chomwe akuchita pothamangitsa agalu amenewo

  • @PatrickGonagona
    @PatrickGonagona 3 месяца назад

    💪💪💪💪💪 DPP my vote 💪❤

  • @TomasDzifoole
    @TomasDzifoole 3 месяца назад

    Osamasunga njoka

  • @ProsperDaniel-kb2yc
    @ProsperDaniel-kb2yc 3 месяца назад

    Kkkkk zawo izoi😂😂😂

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 3 месяца назад

    Musamazimbaise omwe azakumangeyo ndiyemwe anapha

  • @anthonynkhoma4265
    @anthonynkhoma4265 2 месяца назад

    Chipani chombwambwana dpp. Mwayiwala 2005 dpp chitangopangidwa chinalibe phungu ngakhale mmodzi. Aphingu anapeza ochoka kuzipani zina. Bingu anakanitsitsa kuti section 65 igwire ntchito. Musatinyanse

  • @WilfredChinkono
    @WilfredChinkono 3 месяца назад +1

    Mpaka ayitane aphungu a mcp zachmba eti

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 3 месяца назад

    Good Messnge guys

  • @patriciap.bandah3385
    @patriciap.bandah3385 3 месяца назад

    Usi suyaka popanda moto, zauku mwapita uku mwapita tataya nazo Achilima, amenewo achoke akuphesani chifukwa mutamange uku Iwo azipita nazo kuchipani chinacho kukamasula ganizanipo bwino pamenepo dziko lake si ili

  • @YoweliChipapaChipapa
    @YoweliChipapaChipapa 3 месяца назад

    Khonswe owononga ntedza wambeu amaphedwa bas sakalamba, amenewa achoke ndikonswe

  • @MaryMlomba
    @MaryMlomba 3 месяца назад

    Achotsedwe basi chifukwa ndi anthu adyera amenewo .

  • @ChristopherKawilam
    @ChristopherKawilam 3 месяца назад

    Steve iwe pano wafikamo 😂😂😂

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 3 месяца назад

    ❤😂❤😂❤ very nice 😂😂😂no man to man no guys no lesbian ❤❤❤😂😂

  • @RhodrickPhula
    @RhodrickPhula 3 месяца назад +1

    Koma dpp ikuganiza bwanji kumabudulabe anthu mchipani zowina zitheka bwanji abale?????

  • @EllahChikwatu
    @EllahChikwatu 3 месяца назад

    🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @blessingmnomanda
    @blessingmnomanda 3 месяца назад

    Kkkkkkkk

  • @NikolasNanawe
    @NikolasNanawe 3 месяца назад

    DPP mukuchosa anthu Osayiwalatu kuli 50+1 mukwanisa km 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @SaeedHurzrut
    @SaeedHurzrut 3 месяца назад

    vuto anthu Andale ndi ozikonda especially when to black leadership

  • @felixjoseph8161
    @felixjoseph8161 3 месяца назад

    Awachotse and anthu amenewa sazawinaso ku madera awo aphungu oyipa akufuna azikapha anthu ndi anzao a mcp

  • @MaxonKambazithe
    @MaxonKambazithe 3 месяца назад

    Wina anakhuza ni Mr khafula womwe anachoka ku mcp kupita ku UDF

  • @MoosaDawood-l5c
    @MoosaDawood-l5c 3 месяца назад

    Aphungu Adelaide amenewo

  • @wellingtonnkhoma-wr6nc
    @wellingtonnkhoma-wr6nc 3 месяца назад

    Pano ndi mthawi yot zonyasa zonse zichoke sakulakwa, tisanayike mpunga mumpoto timasankha miyara .

  • @YoweliChipapaChipapa
    @YoweliChipapaChipapa 3 месяца назад

    Sefa WA DPP Ali boo siwamataya akunyodola boo

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 3 месяца назад

    Bingu anaphwanya gawo 65 kuchoka ku UDF ramulo silinagwire ntchito bwanji??

  • @JackMvura-ik2td
    @JackMvura-ik2td 3 месяца назад

    Nkhanga zinapangana kusanapse chokaniko Ku DPP kulibe chilipo pitala ndimu lomwe watsankho chitulukeni chamunthu icho chakwera bomaaa ufune usafune

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 3 месяца назад +1

    Galu ndi Peter muthalika musogoleri wopanda nzeru

    • @ZionekaMember
      @ZionekaMember 3 месяца назад

      😂😂😂😂😂😂Cadet wa MCP

    • @TriciaManase
      @TriciaManase 3 месяца назад +1

      Kuyankhula kwa bwanji kumeneko uli ndi umunthu koma iweyo?

    • @patrickmacheso5062
      @patrickmacheso5062 3 месяца назад

      Even Makolo ako ndi apanda nzeru, mchifukwa anabereka mwana opusa ngati iweyo.

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 3 месяца назад

    As a DPP supporter, I agree with your idea of not fighting those members of Parliament because it's pointless anyway.
    It's better just to leave them to finish their remaining period and find their replacement peacefully and smartly

  • @grantjossam
    @grantjossam 3 месяца назад

    My vote

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 3 месяца назад

    Khani yogonana amuna okha okha kapena amkazi okha okha amipingo kwanthu kuno muzinena zoona madziwapo Kathu chifukwa Bingu dziko muno atakana khani imeneyi simunamuyikire kumbuyo kapana kunena ma church kuti asapange ziwonetsero akukana zopusa koma inuyo munali kulemba ma katala kwa Bingu zili zopusa

  • @KassimWilson-o8h
    @KassimWilson-o8h 3 месяца назад

    😂😂😂akumanga tu

  • @MatolaAwalu-x3g
    @MatolaAwalu-x3g 3 месяца назад

    Kodi mnyumba mwako mwana wako akamasapota mdani wako ungasangalale naye?

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 месяца назад

    Koma dpp ikuthani ndithu ziganizo za dad kaya tiziona 2025

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 3 месяца назад

    Chosan basi AAA atibowe

  • @FrancisStima-sc7zs
    @FrancisStima-sc7zs 3 месяца назад

    Amaitha ameneo

  • @DicksonLutere-p9k
    @DicksonLutere-p9k 3 месяца назад +1

    Paja DPP ndi Briefcase party osamadabwa zizindikilo zakutha kwa chipani

  • @MadalitsoGama
    @MadalitsoGama 3 месяца назад

    Ause muntendele amenewo alute

  • @omarajibu860
    @omarajibu860 3 месяца назад

    Why apply to others, and not others?

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 3 месяца назад

    Cadet kuzngulira mutu

  • @MoosaDawood-l5c
    @MoosaDawood-l5c 3 месяца назад

    ❤❤❤❤❤❤ dpp sakulakwa

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 3 месяца назад

    Achita bwino awachose apeze awo aDPP

  • @KondwaniLungu-x5l
    @KondwaniLungu-x5l 3 месяца назад

    Mbola zonse kumeneko azichose basi .

  • @Uncle_B265
    @Uncle_B265 3 месяца назад

    Ndipo live akazitape kuno aiii

  • @languitoneelias9972
    @languitoneelias9972 3 месяца назад

    Kkkkkkk his brother dump udf for dpp why not impeshed wakula uyu

  • @RachelDongolosi
    @RachelDongolosi 3 месяца назад

    Awachotse osanyengelela

  • @MaxonKambazithe
    @MaxonKambazithe 3 месяца назад

    Anali a nsanje central

  • @brendakamvabingu-rr4fg
    @brendakamvabingu-rr4fg 3 месяца назад

    😂😂😂😂

  • @Freedomchennl47
    @Freedomchennl47 3 месяца назад +2

    Kma agalu A dpp amatikwana bwanj

    • @Chisomo-dh2gq
      @Chisomo-dh2gq 3 месяца назад +2

      Galu ndiiwe uli ku mcp weee

    • @Freedomchennl47
      @Freedomchennl47 3 месяца назад +1

      @@Chisomo-dh2gq Aise ine siwa MCP ine ndwa UDF kmano timaona chinsogolo nde nd DPP ngakhale ine ndli wa UDF popanda DPP ife a UDF sitingawine ndchifukwa ine ndmadalila DPP kut mwina 2025 ngakhale ndli wa UDF

    • @EllahChikwatu
      @EllahChikwatu 3 месяца назад

      ​@@Freedomchennl47ndechifukwa can muku nyozo muli wa UDF sibho

    • @Stuartkachali45
      @Stuartkachali45 3 месяца назад

      Msiyen ameneyo mutu wake sugwira ntchito galu ndiyeyo

  • @GiftJulius-ro9ev
    @GiftJulius-ro9ev 3 месяца назад

    Dpp namalomba panyapako ndi gogo wanuyo...

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 3 месяца назад

    Bon kalindo simuthu wa bwino pkhani ya ndare chifukwa ndi munthu amene amangofuna zabwino zikhare zake basi alibe fundo zeni zeni zoti ineyo ndi ngavepo or pang'ono

  • @robsontyg3928
    @robsontyg3928 3 месяца назад

    We don't care

  • @PaulMvuma
    @PaulMvuma 3 месяца назад

    I don't like Peter munthalika

    • @Zelinakhisswell
      @Zelinakhisswell 3 месяца назад

      He doesn't even know that you exist 😂😂😂😂

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 3 месяца назад

    I love you Selina , I need your number ❤