ANANDIKWATIRA NDILI NDI ANA ATATU KALE...true love

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 1 окт 2024

Комментарии • 46

  • @mirriamwilliam-nq9wg
    @mirriamwilliam-nq9wg 4 месяца назад +9

    Zikuchit kukoma ngat zisathe mmmmm ndazikonda kobas,,, inenso chisomo chindigwere Amen

  • @bandacharles82may
    @bandacharles82may 4 месяца назад +8

    Very interesting story. I hope this story will inspire alot of people. Provided that its belt on the basis of true love.

  • @EmercianahKasiku-en6hl
    @EmercianahKasiku-en6hl 4 месяца назад +9

    Zabodza Anthu opephera amanama kwambiri mmalo moti anene zoona amanama ponamizira dzina la Mulungu

    • @ChristinaLigomeka
      @ChristinaLigomeka 4 месяца назад +1

      Osamathamangila kuweruza sionse abodza ena ndiophera km Ali asatanic amenewo ndye abodza osamatenga opephera ose ndabodza ena akupemphera Ali thumwi zasatana ena akupemphera Ali ake Eni Eni aMulungu samalani poyakhula

    • @jennyx6914
      @jennyx6914 4 месяца назад +1

      she cant keep the secret of dreams to her husband akuti zamaloto akumvera pompa
      boza boza leni leni ili onse amafunana kale

    • @LeendaDeborah2005
      @LeendaDeborah2005 3 месяца назад

      Nde anthu a Satanic ndi achilungamo?? Nanunso mumayankhula mopepela bwanji. Adakulodzani mukamugwadire

    • @violetpotani
      @violetpotani 2 месяца назад

      ​@jennyx6914😅😅😅😅

  • @SinyoroMoyo
    @SinyoroMoyo 4 месяца назад +2

    Komatu nyimbo zinazi ndiutumiki eish, am not here to judge but sometimes we have to ask yourself about your position .mkazi wabusa kukonda nyimbo za anthu ovula kuchita kuyitsata

  • @HortencioSamuelOfessi-e5c
    @HortencioSamuelOfessi-e5c Месяц назад

    Koma zodabwitsa bwanji zimenezi zosangalatsa kwambiri mwanipatsa chitsanzo chabwino niyerekeze NDI ABRÃO NDI SARA ZIKOMO 🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @JuniorHala-vf9ov
    @JuniorHala-vf9ov 4 месяца назад +1

    Komaso ukapedza nkazi okulilapo ummm amakakamilatu kkkk abusa kupanga ukwati nkazi woti ndiobelekapo kare

  • @CatherineMtchona
    @CatherineMtchona 4 месяца назад +2

    Ndazikonda ambiri tikuvula chifukwa cha ana mmmmmm ambuye tsegulani makomo

  • @jennyx6914
    @jennyx6914 4 месяца назад +1

    12 years nkukhala uli pa banja? after might prayers anakhailita yekha yekha ndi family ya abusa zoona? anali ndi mission mzimayiyu
    ulape ulape plz mzimayi iwe chonde

  • @jennyx6914
    @jennyx6914 4 месяца назад +1

    inenso ndikuona boza mu story iyi bcz sanali maneba how come osungitsa key. adutse wapafupi kwambiri? again munthu omukonda ngati akuthetsa chibwenzi akanafunsa why? whats wrong? ndiwachimaso maso pastor ameneyo

  • @EnifaJosafati
    @EnifaJosafati 4 месяца назад +2

    Zili bwino kwambili God is good

  • @ElizabethKazambwe
    @ElizabethKazambwe 4 месяца назад +1

    Kupeleka madzi kwa bambo chogwada ai zikomo

  • @violetpotani
    @violetpotani 2 месяца назад

    Apa tivene kaye zinazo pambuyo😅😅😅

  • @GracePhirie
    @GracePhirie 3 месяца назад

    Nde bambowa anali virgin ok😂

  • @chisomodouglas2084
    @chisomodouglas2084 4 месяца назад

    Mayiwa nyimbo asankhayo ndimmene akutanthauzilira sindikuwonapo vuto enanu mumathamangila kuweruza ena chonsecho nyimbo mukuti zachikunjazi mu 4n mwanu zilimo ndipo mumavera kma akavera wina walakwitsa

  • @richardbanda3677
    @richardbanda3677 3 месяца назад

    Great couple; friendly, kind and full of advice. Timakunyadirani anthu inu!

  • @nifaKutaumbe
    @nifaKutaumbe 3 месяца назад

    Taziwa zimene zinali behind the journey of this wonderful couple

  • @EthelOsman
    @EthelOsman 4 месяца назад

    Mmmm mulungu alipodi anthu tikugwila zibalo poti ana tilele tonse ambuye Zikomo

  • @Catherinembowe
    @Catherinembowe 4 месяца назад

    Atumwi munasonyeza kukhwima mmaganizo ndinu chitsanzo chabwino

  • @GeorgePatels-go7wj
    @GeorgePatels-go7wj 4 месяца назад

    Ndiye mai busa kusankha nyimbo yachikunja why?? Mmmm ayi zikomo utumiki

  • @GeorgePatels-go7wj
    @GeorgePatels-go7wj 4 месяца назад

    Ndiye mwamuna wa mai busa oyamba kumwalilira kutulo mmmm ??? Akuti mzimu wa amuna awo ngati akumva , akufa sadziwa kanthu bii

  • @vatineseduwin
    @vatineseduwin 4 месяца назад

    banja ili landisangalasa kwambili mulungu segulani makomo

  • @PetroKachingwe-jf7dh
    @PetroKachingwe-jf7dh 4 месяца назад

    That's interesting story
    God bless our families

  • @BerthaChisoni
    @BerthaChisoni 4 месяца назад

    Ndinaphunzila nawo abusa akazi ku primary school

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba 4 месяца назад

    Waana awili atha kundi hala zisomo zilipo kuno 😂

  • @NaomiGondwe-og5hg
    @NaomiGondwe-og5hg 4 месяца назад

    God bless your marriage ❤

  • @ishmaelbofa1159
    @ishmaelbofa1159 4 месяца назад

    Koma abusa inuyo musangalala ndimoyo owawawu

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 4 месяца назад

    Ai musamatero kuchepetsa nthawi

  • @BilaliMatemba
    @BilaliMatemba 3 месяца назад

    True love indeed 💕💕💕

  • @PiliraMlaviwa
    @PiliraMlaviwa 3 месяца назад

    So interesting.

  • @frankchiwawa4795
    @frankchiwawa4795 3 месяца назад

    Hoooo

  • @NaomiGondwe-og5hg
    @NaomiGondwe-og5hg 4 месяца назад

    Interesting ❤

  • @MgGondwe
    @MgGondwe 4 месяца назад

    Amen

  • @Omwale
    @Omwale 4 месяца назад

    timaina ta mBaiBulo😀

  • @oburybindula-nf7ek
    @oburybindula-nf7ek 4 месяца назад

    Aaaa Linda ulipo mmmm missing

  • @RabeccaGama-f7m
    @RabeccaGama-f7m 4 месяца назад

    Zosagalasa

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w 4 месяца назад

    Ambuye chimodzi modzi

  • @highcallingglobalministries
    @highcallingglobalministries 4 месяца назад

    komatu anthu inu,,,

  • @JosephChikoko-to3ji
    @JosephChikoko-to3ji 4 месяца назад

    Do as the spirit leads

  • @Richardmkandawire-vm6id
    @Richardmkandawire-vm6id 4 месяца назад

    Good lesson guys

  • @pemphokatembe443
    @pemphokatembe443 4 месяца назад +1

    Eeeeh! Nkhani yopatsa chidwi❤❤

  • @Desmond-q7r
    @Desmond-q7r 4 месяца назад

    Mabodza kkkkkk mazitumiki who ever mapemphero zokolo mbeta ndiye zolingazawo aaaa