Osamathamangila kuweruza sionse abodza ena ndiophera km Ali asatanic amenewo ndye abodza osamatenga opephera ose ndabodza ena akupemphera Ali thumwi zasatana ena akupemphera Ali ake Eni Eni aMulungu samalani poyakhula
Komatu nyimbo zinazi ndiutumiki eish, am not here to judge but sometimes we have to ask yourself about your position .mkazi wabusa kukonda nyimbo za anthu ovula kuchita kuyitsata
12 years nkukhala uli pa banja? after might prayers anakhailita yekha yekha ndi family ya abusa zoona? anali ndi mission mzimayiyu ulape ulape plz mzimayi iwe chonde
inenso ndikuona boza mu story iyi bcz sanali maneba how come osungitsa key. adutse wapafupi kwambiri? again munthu omukonda ngati akuthetsa chibwenzi akanafunsa why? whats wrong? ndiwachimaso maso pastor ameneyo
Zikuchit kukoma ngat zisathe mmmmm ndazikonda kobas,,, inenso chisomo chindigwere Amen
Very interesting story. I hope this story will inspire alot of people. Provided that its belt on the basis of true love.
Zabodza Anthu opephera amanama kwambiri mmalo moti anene zoona amanama ponamizira dzina la Mulungu
Osamathamangila kuweruza sionse abodza ena ndiophera km Ali asatanic amenewo ndye abodza osamatenga opephera ose ndabodza ena akupemphera Ali thumwi zasatana ena akupemphera Ali ake Eni Eni aMulungu samalani poyakhula
she cant keep the secret of dreams to her husband akuti zamaloto akumvera pompa
boza boza leni leni ili onse amafunana kale
Nde anthu a Satanic ndi achilungamo?? Nanunso mumayankhula mopepela bwanji. Adakulodzani mukamugwadire
@jennyx6914😅😅😅😅
Komatu nyimbo zinazi ndiutumiki eish, am not here to judge but sometimes we have to ask yourself about your position .mkazi wabusa kukonda nyimbo za anthu ovula kuchita kuyitsata
Koma zodabwitsa bwanji zimenezi zosangalatsa kwambiri mwanipatsa chitsanzo chabwino niyerekeze NDI ABRÃO NDI SARA ZIKOMO 🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Komaso ukapedza nkazi okulilapo ummm amakakamilatu kkkk abusa kupanga ukwati nkazi woti ndiobelekapo kare
Ndazikonda ambiri tikuvula chifukwa cha ana mmmmmm ambuye tsegulani makomo
12 years nkukhala uli pa banja? after might prayers anakhailita yekha yekha ndi family ya abusa zoona? anali ndi mission mzimayiyu
ulape ulape plz mzimayi iwe chonde
inenso ndikuona boza mu story iyi bcz sanali maneba how come osungitsa key. adutse wapafupi kwambiri? again munthu omukonda ngati akuthetsa chibwenzi akanafunsa why? whats wrong? ndiwachimaso maso pastor ameneyo
😅😅😅😅
Zili bwino kwambili God is good
Kupeleka madzi kwa bambo chogwada ai zikomo
Apa tivene kaye zinazo pambuyo😅😅😅
Nde bambowa anali virgin ok😂
Mayiwa nyimbo asankhayo ndimmene akutanthauzilira sindikuwonapo vuto enanu mumathamangila kuweruza ena chonsecho nyimbo mukuti zachikunjazi mu 4n mwanu zilimo ndipo mumavera kma akavera wina walakwitsa
Great couple; friendly, kind and full of advice. Timakunyadirani anthu inu!
Taziwa zimene zinali behind the journey of this wonderful couple
Mmmm mulungu alipodi anthu tikugwila zibalo poti ana tilele tonse ambuye Zikomo
Atumwi munasonyeza kukhwima mmaganizo ndinu chitsanzo chabwino
Ndiye mai busa kusankha nyimbo yachikunja why?? Mmmm ayi zikomo utumiki
Ndiye mwamuna wa mai busa oyamba kumwalilira kutulo mmmm ??? Akuti mzimu wa amuna awo ngati akumva , akufa sadziwa kanthu bii
banja ili landisangalasa kwambili mulungu segulani makomo
That's interesting story
God bless our families
Ndinaphunzila nawo abusa akazi ku primary school
Waana awili atha kundi hala zisomo zilipo kuno 😂
God bless your marriage ❤
Koma abusa inuyo musangalala ndimoyo owawawu
Ai musamatero kuchepetsa nthawi
True love indeed 💕💕💕
So interesting.
Hoooo
Interesting ❤
Amen
timaina ta mBaiBulo😀
Aaaa Linda ulipo mmmm missing
Zosagalasa
Ambuye chimodzi modzi
komatu anthu inu,,,
Do as the spirit leads
Good lesson guys
Eeeeh! Nkhani yopatsa chidwi❤❤
Mabodza kkkkkk mazitumiki who ever mapemphero zokolo mbeta ndiye zolingazawo aaaa