Размер видео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показать панель управления
Автовоспроизведение
Автоповтор
Moto Mr Boni 🎉🎉🎉🎉🎉❤❤❤
Bon kalindo iweyo ife timagula madata kuti tivele inu ma bigy l love ❤❤❤❤
❤❤❤mwana wa mama Malawi muno bon kalindo God ahead u my brother. from Cape Town mitchells plain town centre
Moto 🎉🎉🎉🎉🎉 Dc Bon Kalindo auseni kuti aziwe zeneni kuti achite bwino fire ❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
The DC boooooooorn kalindooo ❤
Manganya, Nankhumwa ndinu makapa
Mumatiyimilila akalindo❤❤❤❤
Bon kalindo wathu wathu waku mulanje kuno👉🏔️
Booon Kalindo the DC 🔥🔥💪💪 mwana wachabe kwambili 💪
DPP idasosolera pa msampha imafuna chithandizo pakalowa njoka.Zikatheka basi mmati paliponse pakhale wanu wachilomwe.UDF ndiye mudaichita chipongwe kale singabwerezeso.Boma ndilomweli ndipo palibe kusinth.Mufune musafune Dr Chakwera mpaka 2030 woooo
THE DC OSUTSA BOMA CHONDE MUTIPETSA AMALAWI KU MCP IYU CHIPANICHO ANALEPHELA KUWINA ACHILIMA KAMABE NDANITSO ATUPELE SANGAWINE PANGANI CHIMODZI MUTIPULUMUTSE AMALAWI KUYIPHELA APA MCP BASI CHIPANI CHIMODZI UYU NDIKAGAME ATSIYANA ADZIMA PA VOTE PAKA KALE
The DC ❤..Zoona zokhazokha ❤❤❤❤❤❤
AA DC KUNENA ZONA MUMALANKHULA CHILUNGAMO KOMA AZIPNI ZOSUSA SAMVA AYI M'BUSA WINA KWA VUMBWE AMAWAWUZA LIVE PA MALILO A MWANANVEKA KUTI NGATI AKUFUNA KUWINA OFUNIKA ,M,NGWILIZANO KOMA ANTHU AKEWA KUDZINVA TOO MUCH
Mulipachi ntchito bwana😂. Zikomo tikumverako zambiri
Aopparition"wa atipweteketsa chifukwa chosamva
A opposition kukula mtima kwambiri malangizo akupasidwa kusamva
Mwauze big
DC 🔥🔥🔥
Truly ❤
💥💥💥💥💥💥 bon kalindo machine kasongo one
The DC mwana owoopsa kwa mbili
Kuswa×2 mosayang'ana chipani kapena nkhope oposition nkhani ndimeneyo mu umodzi muli mphamvu
DC🔥😊
The DC,Mulungu akudalitseni kwambiri,anthuwa mumaamudza chilungamo koma sakumva,vuto kusamva kwao kuzaika a Malawi mavuto.
❤❤❤❤❤❤❤
Ausen boss ❤
Osaopa osatopa osafooka comrade the dc
Mumakwana Bwana DC Honorable Kalindo..Pitilizani kuwayimirira a Malawi
❤
Powerful ❤
Awuzen chilungamo akhumudwe akhumudwe chilungamo mutanena madala bola ava andale kkk
Bas ntchito kumanga anthu mmalo mothesa njala anyani amenewa
True
😂😂😂😂😂😂😂
The DC mwana owoopysa kwambili
Denis Mahata ndiye Yankho la tsala ku malawi. Ibrahim Traore wa ku Malawi
I hope amva asadzalile pa mawa kuti zisankho sizinayende bwino
Ife nde tudzakupangan follow m'ka kale
Awuzeni aopposition ife tikudalira iwowo
the DC akatundu 🔥 chesaopa ukali wanu ❤❤❤❤❤💪💪🔥
Osazinyenga ndchala ohooo
Koma wawawuza wanzelu atorepo kanthu
Chilungamo chilungamo
The Dc mumakwana
Ati kasongo 😂
Zipani zakumana zokumana zokula mitima zokha zokha
Bon kalindo machine operator,
Mumakwana Apure athu
The DC power
Mumatiimilila
Ndinu one a kalindo
Koma chakwera ndioyipa
The DC
Moto Mr Boni 🎉🎉🎉🎉🎉❤❤❤
Bon kalindo iweyo ife timagula madata kuti tivele inu ma bigy l love ❤❤❤❤
❤❤❤mwana wa mama Malawi muno bon kalindo God ahead u my brother. from Cape Town mitchells plain town centre
Moto 🎉🎉🎉🎉🎉 Dc Bon Kalindo auseni kuti aziwe zeneni kuti achite bwino fire ❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
The DC boooooooorn kalindooo ❤
Manganya, Nankhumwa ndinu makapa
Mumatiyimilila akalindo❤❤❤❤
Bon kalindo wathu wathu waku mulanje kuno👉🏔️
Booon Kalindo the DC 🔥🔥💪💪 mwana wachabe kwambili 💪
DPP idasosolera pa msampha imafuna chithandizo pakalowa njoka.Zikatheka basi mmati paliponse pakhale wanu wachilomwe.UDF ndiye mudaichita chipongwe kale singabwerezeso.Boma ndilomweli ndipo palibe kusinth.Mufune musafune Dr Chakwera mpaka 2030 woooo
THE DC OSUTSA BOMA CHONDE MUTIPETSA AMALAWI KU MCP IYU CHIPANICHO ANALEPHELA KUWINA ACHILIMA KAMABE NDANITSO ATUPELE SANGAWINE PANGANI CHIMODZI MUTIPULUMUTSE AMALAWI KUYIPHELA APA MCP BASI CHIPANI CHIMODZI UYU NDIKAGAME ATSIYANA ADZIMA PA VOTE PAKA KALE
The DC ❤..Zoona zokhazokha ❤❤❤❤❤❤
AA DC KUNENA ZONA MUMALANKHULA CHILUNGAMO KOMA AZIPNI ZOSUSA SAMVA AYI M'BUSA WINA KWA VUMBWE AMAWAWUZA LIVE PA MALILO A MWANANVEKA KUTI NGATI AKUFUNA KUWINA OFUNIKA ,M,NGWILIZANO KOMA ANTHU AKEWA KUDZINVA TOO MUCH
Mulipachi ntchito bwana😂. Zikomo tikumverako zambiri
Aopparition"wa atipweteketsa chifukwa chosamva
A opposition kukula mtima kwambiri malangizo akupasidwa kusamva
Mwauze big
DC 🔥🔥🔥
Truly ❤
💥💥💥💥💥💥 bon kalindo machine kasongo one
The DC mwana owoopsa kwa mbili
Kuswa×2 mosayang'ana chipani kapena nkhope oposition nkhani ndimeneyo mu umodzi muli mphamvu
DC🔥😊
The DC,Mulungu akudalitseni kwambiri,anthuwa mumaamudza chilungamo koma sakumva,vuto kusamva kwao kuzaika a Malawi mavuto.
❤❤❤❤❤❤❤
Ausen boss ❤
Osaopa osatopa osafooka comrade the dc
Mumakwana Bwana DC Honorable Kalindo..
Pitilizani kuwayimirira a Malawi
❤
Powerful ❤
Awuzen chilungamo akhumudwe akhumudwe chilungamo mutanena madala bola ava andale kkk
Bas ntchito kumanga anthu mmalo mothesa njala anyani amenewa
True
😂😂😂😂😂😂😂
The DC mwana owoopysa kwambili
Denis Mahata ndiye Yankho la tsala ku malawi. Ibrahim Traore wa ku Malawi
I hope amva asadzalile pa mawa kuti zisankho sizinayende bwino
Ife nde tudzakupangan follow m'ka kale
Awuzeni aopposition ife tikudalira iwowo
the DC akatundu 🔥 chesaopa ukali wanu ❤❤❤❤❤💪💪🔥
Osazinyenga ndchala ohooo
Koma wawawuza wanzelu atorepo kanthu
Chilungamo chilungamo
The Dc mumakwana
Ati kasongo 😂
Zipani zakumana zokumana zokula mitima zokha zokha
Bon kalindo machine operator,
Mumakwana Apure athu
The DC power
Mumatiimilila
Ndinu one a kalindo
Koma chakwera ndioyipa
The DC
❤