CDEDI PRESS BRIEFING LIVE TODAY - NAMIWA WAPEMPHA PRESIDENT CHAKWERA KUTI ALANKHULE A MALAWI LERO

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 8 фев 2025
  • CDEDI PRESS BRIEFING LIVE TODAY - NAMIWA WAPEMPHA PRESIDENT CHAKWERA KUTI ALANKHULE A MALAWI LERO

Комментарии • 268

  • @afritouch4660
    @afritouch4660 Месяц назад +10

    Malawi should support Israel because the land was owned by Israel before Palestine claimed it & bible can teach you better. We don’t support terrorists. Shame on you

    • @catherinec1861
      @catherinec1861 Месяц назад

      Uku ndikusamvetseta history and Bible.
      These are Jews fighting and killing Christians.

    • @WakuMalawi
      @WakuMalawi Месяц назад +6

      That bible that you're referring to says it's ok to kill innocent women & children...? I thought killing was one of the commandments "not to do"...? Please exlplain.

    • @Accountants615
      @Accountants615 Месяц назад +6

      Mwapupulumatu kunena kuti Shame on you, 😂😂😂😂😂😂😂😂, Killing is not a good act, Thy shall not murder! Komanso ndiwe wa MCP nde kupha sivuto

    • @AHAMADUJRAminie-c6q
      @AHAMADUJRAminie-c6q Месяц назад +1

      Machende ako iweyo shame for yourself

    • @ReeqoVescan
      @ReeqoVescan Месяц назад

      Munthu osazindikira uyu musiyeni

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Месяц назад +10

    Bravo namiwa ndi team yanu yonse tili kumbali yanu simulinokha ❤❤

  • @FebbieNjewa-g3k
    @FebbieNjewa-g3k Месяц назад +5

    Cded group,,keep it up!God bless n protect yu in Jesus christ name

  • @RosinaPatel
    @RosinaPatel Месяц назад +12

    Viva Comrade Namiwa..enough is enough

  • @aggogokina8992
    @aggogokina8992 Месяц назад +2

    Akulu akulu Namiwa ndi chibinyira chokanika kusenza awa ndi akamunadi amene ayima pa cholungamo mopanda mantha. Power to that💪💪💪👍

  • @JanatuCarlos
    @JanatuCarlos 29 дней назад

    Mr namiwa and his team may good lord protect them and continue their job in the name of Jesus,,,,

  • @GraceShaibu-i9d
    @GraceShaibu-i9d Месяц назад +2

    Viva comrade namiwa big up

  • @ThomasMaulana-u4p
    @ThomasMaulana-u4p Месяц назад +7

    Nsaname ine Chakwerayi amandisowesa choyankhura eeeish☹.

  • @SuccessorMupangami
    @SuccessorMupangami Месяц назад +8

    Landilan Maluwa anu Mr Namiwa,Amalawi ochuluka tili mbali yanu.

  • @thomasmember2485
    @thomasmember2485 Месяц назад +5

    Big up Comrade Namiwa Osaopa Osafooka Osatopa.

  • @miraclejohnphiri7687
    @miraclejohnphiri7687 Месяц назад +4

    Question kodi abwana athuwa analidi aku church kapena amkagwila ntchitito basi zikudabwisa???

  • @FrancisMcJossam
    @FrancisMcJossam 17 дней назад

    Namiwa he is my favourite person

  • @catherinec1861
    @catherinec1861 Месяц назад +2

    Why fight over the lake when we are not making any profitable use of it? Africa should continue to look to unity not divisions.
    I agree 100% with the Israel/Palestinian issue. We are on the wrong side of history for as long as our government supports Israeli genocide.

  • @WellosMoyo
    @WellosMoyo 17 дней назад

    Umatiimirila more fire Namiwa

  • @EmmanuelNgambi-y6h
    @EmmanuelNgambi-y6h 29 дней назад

    Very wise and intelligent Namiwa go on,,,, osaopa osafooka osatopa 🔥

  • @felixnyirongo5265
    @felixnyirongo5265 29 дней назад

    Please go ahead Mr Namiwa

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Месяц назад +1

    Powerful our saviour
    God bless you namiwa

  • @WitnessChimera-r4i
    @WitnessChimera-r4i Месяц назад +9

    Apa tinaimbila mfiti m'manja tilibe mau a 🇲🇼 malawi

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os Месяц назад +1

      Ndipo zoonadi tinayimbira mfiti m'manja ndi chani chomwe chinatilodza ife? Tinapusitsika ndi ubusa, anavala chigoba cha ubusa

    • @WitnessChimera-r4i
      @WitnessChimera-r4i Месяц назад

      @VeronicaChirwa-ct4os ndipo kwambili

  • @WestonMakiyi-s9l
    @WestonMakiyi-s9l Месяц назад +3

    Great man

  • @Edward-y3v
    @Edward-y3v Месяц назад +1

    May God bless you Comrade

  • @Moses51
    @Moses51 Месяц назад +8

    Chilungamo poyela together with Malawi

  • @AlbertNambwale-sm9qe
    @AlbertNambwale-sm9qe Месяц назад +3

    Nice briefing

  • @AggieKwekwesa
    @AggieKwekwesa Месяц назад +1

    God z with u comrades ❤

  • @MussaRafael-d4q
    @MussaRafael-d4q Месяц назад +9

    never give up Namiwa

  • @DavienBanda
    @DavienBanda Месяц назад +3

    Atola nkhani nawonso zuwakhuza that's why akusowa mafunso. We need God's presence on this..........

  • @lewisdicksonmlozi130
    @lewisdicksonmlozi130 Месяц назад

    God bless you guys ❤

  • @NyanguPaul
    @NyanguPaul Месяц назад +7

    Let's continue comrade never give up

  • @DAGAMAaaaa
    @DAGAMAaaaa 29 дней назад +1

    Worm heart of Africa ija ikusapota nkhondo chifukwa cha chakwera

  • @felixnzunda1961
    @felixnzunda1961 Месяц назад +1

    The other problem we have in Malawi is that we employ soldiers who are our very young children who cannot withstand the pressure and fight.

  • @JohnChikuni-cr1xy
    @JohnChikuni-cr1xy Месяц назад +3

    Namiwa is a true Malawian

  • @ShukuraniTonex
    @ShukuraniTonex Месяц назад

    God bless you guys ✊️

  • @BornfaceMponda-ny9tw
    @BornfaceMponda-ny9tw Месяц назад +5

    Go go go

  • @LawrenceDickens-jk3zx
    @LawrenceDickens-jk3zx Месяц назад +2

    Mr Namiwa big up bro

  • @AmosBandula-up4yb
    @AmosBandula-up4yb Месяц назад

    Number 1

  • @nthawigolowa5158
    @nthawigolowa5158 Месяц назад +1

    I like the confidence from Mr. Phiri.. Good composure

    • @KumbukaiMtawaliWaMoffat
      @KumbukaiMtawaliWaMoffat Месяц назад

      @@nthawigolowa5158 Why is Israel in Gaza?

    • @nthawigolowa5158
      @nthawigolowa5158 29 дней назад

      @KumbukaiMtawaliWaMoffat why are u asking me that? Didn't u hear from the briefing

    • @InnocentMtafya-c6b
      @InnocentMtafya-c6b 29 дней назад

      ​@@nthawigolowa5158, Kodi awa ndi azibusa mumati Ojiya waja akusiyana bwanji?

  • @fysonmalola383
    @fysonmalola383 Месяц назад

    We have had a lot of briefings......are we making progress??

  • @ezekieljambo4255
    @ezekieljambo4255 Месяц назад

    Comrade Phiri mu kunveka ngat Namadingonamadingo eeh😊
    Big up!

  • @MolesBrown
    @MolesBrown Месяц назад +11

    Kodi asilikaliwa ncthito yayo ndichiyani Kodi iwowo siwoteteza dziko chaka ndi chaka kulemba asilikali akati ateteza dziko ndikumademo zoona ndalama zathu zikungopita ndizowona asilikali athu adzisiya kuteteza dzi dzikolawo adzikateteza mayikol akunja zoona kunsanke analanda kumachinga analanda kumwanza analanda sizoonayi anamiwa mwayitenga bwino koma musakhale mwasamila chipani musawonetse mbali nenani chalakwikacho mbalizose mukatelo amalawi ose adzikuvetselani Imani panokha chonde mupange zadziko lose

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os Месяц назад +1

      Ndi opepera awa amangodziwa kupita ku DRC

    • @FRANKMKWAILA
      @FRANKMKWAILA Месяц назад +1

      Asilikali amayendera ma orders, ngati atsogolero ali chete, asilikali sangangopakira mifuti ulendo ayi. Nyanja yapita basi. Alandira bwanji map achilendo nkukhala chete?

    • @BerthaWasi
      @BerthaWasi Месяц назад +1

      Honestly asilikali akumalawi ndopepela maiko ena kukamachitika zopusa kuboma amatha kuchosa president ndkukonza dziko koma athuwa mmmmmmmm

    • @NurjChilawo
      @NurjChilawo Месяц назад +1

      Asilikali athu pano ali ngati Tambala onyowa

    • @AchinaKellz
      @AchinaKellz Месяц назад

      Ayi alowa ndale ngati police

  • @FreddieKanyerere-u2z
    @FreddieKanyerere-u2z Месяц назад +1

    Comrade Namiwa big Up ana anthu adzavutika ndi ziganizo zopusa.

  • @Hildamanda-e2x
    @Hildamanda-e2x Месяц назад

    God bless you guys ❤ mulungu azikutetezani kuti malawi amulumuke kunzela mwainu chiyembekezo cha amalawi chili pa inu ❤❤❤❤❤

  • @ThokoMsonkho-hy4uc
    @ThokoMsonkho-hy4uc Месяц назад +6

    Namiwa anabadwa kudzapereka chiyembekezo kwa olema ndi othodwa. Ndimamumvetsetsa pazomwe amapanga,amafuna zabwino zizichitikira pa a Malawi

  • @GrecianWyson
    @GrecianWyson Месяц назад +1

    Namiwa uremu 🎉🎉🎉 mukutiyimiriradi my God bless you

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 Месяц назад +4

    Elder ....Nàmiwa ....Respect....❤🔥🔥🔥🔥

  • @georgeaiwa8661
    @georgeaiwa8661 Месяц назад +5

    Mr. Namiwa mulisinthadi dzikoli

  • @MikeNguluwe
    @MikeNguluwe 29 дней назад

    Kwa ine Mike Nguluwe Anamiwa ndi amzanu ulemu wanu anthu Azeru wow ona patli a chikondi wosazikonda wonganizira za athu ena wosakonda ndalama tikuyamikilen tithanzeni kukoza zikoli tiili ndi ana tonse tikupita ku tsongolo ulemu

  • @ThandiswaMqakai-v4i
    @ThandiswaMqakai-v4i Месяц назад

    Am second tired with Chakwera
    Go to Ntcheu Dzunje area
    No good roads
    No good infrastructure
    No clean water
    I am here now
    Where is Malawi government?
    This is the home of my father
    But authorities please give them good tarmac road
    Thank you

  • @PETROLJ-n1t
    @PETROLJ-n1t Месяц назад

    Mr namiwa timakunyadilani pokhala nafe amalawi❤

  • @EUGINEMWADALA
    @EUGINEMWADALA Месяц назад +1

    Ndipo mai olemekezeka dr Joyce Banda solved it very well ndipo muthawi yochepa. It may look simple kokano that boundary tizalira tizapanga regret malawi will still remain poor and land locked. We already have few resources and we are failing to manage then instead tikungobetsa kwa azungu ndi maiko oyandikana nao thats being unreasonable

  • @CharlyChigwembele
    @CharlyChigwembele Месяц назад +1

    Big up namiwa

  • @LastbornEnd-r9c
    @LastbornEnd-r9c Месяц назад +3

    Koma awawa ayankhura kachiwiriwo akufunika adziyankhura yankhura plz mr Namiwa

  • @aishamakisudi3220
    @aishamakisudi3220 Месяц назад +1

    Our hero Mr

  • @chimwemwenkute3839
    @chimwemwenkute3839 Месяц назад +2

    Katundu waboma uyu he's a freedom fighter

  • @PromiseKhenzo
    @PromiseKhenzo Месяц назад +1

    NAMIWA THE BIG MAN🎉😊

  • @LimbikaniTambala-z1y
    @LimbikaniTambala-z1y Месяц назад +1

    Mukhalira yomweyo Chakwera mukunenayo awinanso

    • @GraceShaibu-i9d
      @GraceShaibu-i9d Месяц назад

      muza winila kubela osati za chilungamo mukunama man

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer Месяц назад +4

    Mutu wao sungwir ntchito pan aprezident anth ndip sakudziwa chomwe akuchit akufunik kumtemela srs

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 Месяц назад +3

    I trust namiwa hiro

  • @DannieChimenya
    @DannieChimenya Месяц назад

    Baba Namiwa god bless ❤️

  • @JosephyStain-ty9oo
    @JosephyStain-ty9oo Месяц назад +1

    I like your voice namiwa you are one continue nyanja ndi yathu not Tanzania apo bii ikhalapo nkhondo M v T tiona kut zikutha bwanja amene angavomeleze zanyanja asowa on this year 😢

    • @FidelisKumwenda
      @FidelisKumwenda Месяц назад

      Tanzanians are our relatives, and nobody from around the border with Tanzania will want any conflict with our relatives over a useless topic which only serves people who have no relatives from either side of the border.

  • @TokozaniBanda
    @TokozaniBanda Месяц назад +2

    Kodi munthu ngati amakonda anthu ake angadane naye chakwera ndi galu kapena mbuzi iweso ukusapota chakwera ndiwe galu kwabasi munthu osaganiza komaso wosaganizila ziko kapena amalawi.namiwa continue tili pa mbuyo pano tichela ziko lanthu

  • @NovahiwaInnocent
    @NovahiwaInnocent Месяц назад

    Namiwa ndi deal, keep it up

  • @WellosMoyo
    @WellosMoyo 17 дней назад

    Asilikali,nanuso mukuopa Tanzania?

  • @eunicesaiti
    @eunicesaiti Месяц назад

    Much respect Mr Namiwa 🙏

  • @Nelsonmatenda
    @Nelsonmatenda Месяц назад

    Namiwa timakuyamikani kwambili..mcp ichoke pa 16 Sept 2024

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 Месяц назад

    Nuff respect!....chakwera can not sell the lake ndikuchindila ndalama zonse mahule ndi achina chimwendo kunkuyu ndi zikhale kamajekete...osaiwala hule nanse mbeto

  • @frankchimaliro5981
    @frankchimaliro5981 29 дней назад

    Za nyanja yokhayi asayelekeze ndiyathu amalawi. We will die for it

  • @elishabanda1332
    @elishabanda1332 Месяц назад +1

    Alomwe awa they want muthalika mu longwe nzawo agalu

    • @Geraldmkwewu
      @Geraldmkwewu Месяц назад

      galu ndiweyo nose ndi chakwera fiti lnu

  • @GiftSoko-w4h
    @GiftSoko-w4h Месяц назад

    Big up Namiwa mumatiyimilila

  • @JosephHill-fy1bb
    @JosephHill-fy1bb Месяц назад +2

    Nyanja imeneyo lazaro adzabweza ndalamazo...

  • @AubreyShaba-b5d
    @AubreyShaba-b5d Месяц назад +3

    Hei, Malawi is just a grain of sand full in a wheelbarrow..we aren't even counted worldwide... Check, all presidents except Her Excellency Joyce Banda and Kamuzu Banda,have had fuel crisis shortages of fuel supply..We see no angels here apart from the exceptional two.... Was it not Bingu who said, *Kagoneni pa mseu ngati galimoto sizikupondani* Is this a lie? Or he sounded Eddie Murphy?... Lake Malawi issue: Tanzania Government cannot just change boundary.. Neither Malawi nor TZ can just wake up and draw new boundaries... Country boundaries were a colonial baby, not a single African country drew its boundaries...Go back to Archieves in Zomba and check boundaries as demarcated by colonialists... Northern Malawi border was an agreement for reasons discussed between the British and Germans...Mbeya was part of Nyasaland (Malawi) while North east of Lake Nyasa(Malawi)..belonged to Tanganyika(Tz) The British and Germans settled for a swap... The British released Mbeya to the Germans,(Tanganyika), likewise the Germans released North East of Lake Nyasa (Malawi)to the British... What you must know is that no single country can just wake up and make new boundary without international consultation... it's not an easy process...I see no reason why politicians and some NGOs are shaking knees for nothing.. Those who made such boundaries, the British and Germans governments must negotiate it on a round table..If Tz wants North East of Lake Malawi,then Tz must secede Mbeya City back to Malawi as was the agreement between the British and Germans... International Law on Common Waters was born after this agreement.. They give us back Mbeya City and be part of Common Waters..No such a thing will work until Tz gives back Mbeya City to Malawi... unedited text...

  • @MosesTangwe-q8o
    @MosesTangwe-q8o Месяц назад

    Ngati anatseka admark zogulitsa nyanja tisakaikire tilindi gwape wa president oti mmutu mwake mulibemo kanthu

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt Месяц назад +1

    This chakwera regime is not chifuniro cha Mulungu yes,

  • @LukeMapukusa
    @LukeMapukusa Месяц назад +4

    Chakwera wamaliza dziko lathu zed Nyanja yapita bas

  • @AarongeoffreyKaluwa-eb7ot
    @AarongeoffreyKaluwa-eb7ot Месяц назад

    MCP is a cased party. Any one who joins MCP, no matter how blessed he or she is but will be cased as well. You must pray and watch Which party to join.

  • @AwetuAmidu-u2j
    @AwetuAmidu-u2j 26 дней назад

    👊✊💪🏿💪🏿

  • @RickBanda-p3m
    @RickBanda-p3m Месяц назад

    Ngati malire amavuta a Munda mzere umodzi mpaka zikwanje nde mukanene dziko we have defence force and their major responsibility is to defend the territory akuchedwa pati let them go their anyamata a mmadzi akateteze nyanja go

  • @royalimagecreations
    @royalimagecreations Месяц назад

    Namiwa and his team are just more than Chilembwetu pena

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Месяц назад +2

    Zamphavu 🔥

  • @GiftPaulMaononga
    @GiftPaulMaononga Месяц назад +1

    Bwerela zokhazokha, palibe cha nzeru chimwe ndatolapo

    • @hannah-gs2kh
      @hannah-gs2kh Месяц назад

      Muchira simunati muzingomwa mwandondomeko

  • @SheriffBakili
    @SheriffBakili Месяц назад +1

    Anthu akufa kumeneko sasilamu okha ena ndi achi khilisitu

  • @enosmanganda327
    @enosmanganda327 Месяц назад

    Timakusapotani a Namiwa, Komano history ya Palestine anena awo a supporter a Hamas wo ndi yabodza. Mwina sakudziwa.

  • @abangaabanga4677
    @abangaabanga4677 Месяц назад +1

    Mawu......Mawu.....!

  • @mansonchinkhuzi
    @mansonchinkhuzi Месяц назад +2

    Uyu atule pansi udindo wa HRDC sakukwana wangokhala odzazidwa ndiukali koma mulibe utsogoleri pasankhidwe wina basi

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule Месяц назад

    Namiwa Big man ❤

  • @GhamaJohnus-b7x
    @GhamaJohnus-b7x 29 дней назад

    Abiti mumakwana landlani maluwa anu (achakwela asatibwezelese m'mbuyo)

  • @lacfunnytv1251
    @lacfunnytv1251 Месяц назад

    Koma uyo Asabuni, be careful with that guy.

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz Месяц назад

    That's the point icc ukufunika ndithu

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete Месяц назад

    Free Palestine chakwera anavotela Israel Kuti izipha ana Ku Palestine mapwala ake chakwera panyapakepo ndintu 😢😢

  • @AlihIbrahim-s7v
    @AlihIbrahim-s7v Месяц назад +7

    Akristu ena ndiwozitsata eeee 😂😂😂😂

    • @NdaonaMsowoya
      @NdaonaMsowoya Месяц назад +4

      Kristy nsilam tosefe ndi amozi palibe kusiyana apa km chigawenga ichi mumati chakwela azafa ifa yowawa kwambili

    • @AlihIbrahim-s7v
      @AlihIbrahim-s7v Месяц назад +2

      @NdaonaMsowoya 😂😂😂😂😂adzafa ngati chitete chofela pa tsekela

  • @LeyvanSamuel-pe5tc
    @LeyvanSamuel-pe5tc Месяц назад +2

    Keep it up good work 😇 Namiwa no peace for the wicked chikangawa akapuma kumwamba 😅

  • @LameckGamah
    @LameckGamah Месяц назад

    Sulute CDEDI💪

  • @vivianmkwate8536
    @vivianmkwate8536 Месяц назад

    Bravo CDEDI

  • @EUGINEMWADALA
    @EUGINEMWADALA Месяц назад +2

    2025 CDEDI yoyeeeee yanyanjayi tikhalitsepo

  • @TimexKaufa
    @TimexKaufa Месяц назад

    Zanyanja aprezident a Tanzania ndi wankazi mkutheka amadziwana mwanseli ndi chifukwa akusowa poyakhulala.

  • @AlexanderTraffick
    @AlexanderTraffick Месяц назад +2

    Wachiwiri kurankhurawe mmmmm ndakupatsa ulemu .uli ndimfundo komaso umadziwa kutambasura nkhani.History it's a best teacher

  • @DeavncKapesi
    @DeavncKapesi Месяц назад +1

    So sad 😢😢

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 Месяц назад +1

    Nthawi ya malemu Kamuzu ankalimbikisa ubale ndi Israel apa awanso akupanga chimodzimodzi chilipo amapindula no doubt about that

  • @JoyceMoyo-mp3de
    @JoyceMoyo-mp3de Месяц назад

    Namiwa your the best for me with your comrade

  • @macdonaldkainga
    @macdonaldkainga Месяц назад +1

    Namiwa umatha

  • @mikechasowa5915
    @mikechasowa5915 Месяц назад +3

    A Mtondo Namiwa

  • @MlaziJames
    @MlaziJames Месяц назад +1

    Atule pansi udindo mr chikangawa