Размер видео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показать панель управления
Автовоспроизведение
Автоповтор
To me welcome back Mr muluzi we know ur dad was a Hero in politics be like him atupele my vote
Kodi Atupere akuthawathawa bwanji akafunsidwa za a Chakwera
I think he might be the right candidate
My vote 🗳
Sakundigwira mtimabe ine, nkhani ya economy sakuyifotokoza momveka
We need alliance please 🙏🙏🙏😭😭
We love you ❤boss
Uyu ndiolephera sayankha futso😊
Mantha ake ameneo mungalamulire dziko inu ngakhale Mulungu amafuna munthu odziwa mchimene ali kulephera kuyankha funso lophweka
Booom atupere muluzi❤❤❤❤
Let's work together as one Chikangawa asowe basi
My vote...
Interigent Man 🔥
Mmene Chilima adayendera 2019, ndikukhulupirira kuti adaphunzira pamene paja and ayenda mmidzi😂😂😂😂😂😂
Boma ❤❤❤❤ tupele
one thing I like about this guy, samapanga nawo politics yonyozana....ndi mfana wa look sharp
Atupele you can't be a president on this country because yo are too young on compain
M'malawi muno timaluza azisogoleli abwino chifukwa cha kuzikonda kwaoyambisa zipani,,, kunena chilungamoh bwanawa ndale anazisiya,, chimene abwelelaso ndichyn please
Wina mwa andale opanda mbili yonyansa pa ndale mfana uyuyu,frankly speaking.
@@SamuelThanganyika that's true my bro
Kukanika kupeleka % ya mzanke kungot 1/10 nzovutaso izi? Kapena sakuzzsata zinthuzi, naye wakanika basi sangatenge boma npake amafuna mcp yibwere ku convention banzi lamvuta uyu
😂😂😂 mumafuna amene chani ngati timamva akayankhula???
Bingu anayimalidza UDF singazawineso mdziko muno pawokhaa
@@kennethnasteve4721 udf ndi malemu achipan
Awa utsogoleli mulibe thandizilani MCP poti ndalama mwatenga kale
Mmmm zamumtima nzawekha choona chili muntima mwawomo
Akuluwa tawayezeka, kumenya kugwesa 😅
❤❤❤❤ Boma
Komatikuyeseni bwana
Agulitsa chipani awa ku congress
He is not answering questions
Tupele ndi munthu oganiza za patsogolo
@@MjombaMoosa l am with you big man
Ndinayiwala paka munaunikira kuti tizankhe molondola chifukwa enawa azalowa m'boma pofuna kuti abe mwakwijo munatiunikiradi
😂😂 Mantha poyankha atupele.Very simple futso hw marks amene mungawapatse achakwera?.Yankho dololo😂😂
Koma ndipo 😅
Akuti upereke malikisi iwe ukuyankha zako mmmm uyu wabisala mmasamba zipita kuchikangawa partyko kutha kwa UDF
Funsoyi ayilephera kuyamkha akudodoma dodoma
Palibe cha nzeru wakambapo apa.
Awunope tunyakule
Akuthawa fuso lachakwera
Ali ndi utsogoleri
Onyoza makolo ake afe ndithu......Bingu adaba u president wa udf Mulungu adzabweza
Inunso ndi mbuli yophunzila
Komaso awa iye amafuna kuwonetsa ntchito zake payekha osati adzilamulidwa ndi anthu
Akuzembatu mayankho atupele
Yankhani funso atupele
Akulephera kuyankha bwino bwino mafunso......uyutu akuzapanga mgwirizano ndi Congress
Atupele sakulephela kuyankha zacha chakwela, koma musaiwale kuti atupele safuna ndale zonyozana koma ifeyo ovota ndiomwe tione muthu omuvotela
Ndipo kwambili thawi zambili samenya kampen onyoza
Teroni
Cadet wa mcp iwe atupele muluzi
Atupele amayankhula zogwila mtima koma bwanji sapasidwa mpata kuti alamule?
Amalawi kuyankhula bwino sikulamulira dziko
weyi ndilunga anemeyi sitingamusape upule
..
Sakuyankha funso
Lolani mwanayu alamure
Awa mfundo alibe adzingopita kumakadya ndalama zomwe anaba bambo ake
IWEO UKANDAKHAL ULINDIFUNDO BWENZ UKUVUTIK CHOCHO NO PAIN NO GAIN
Iwe ndi nfundo zakozo bwanji osakamuchotda chikangawa ukalamulire meina anthu adiye kudya chitedze .?
@@cjaylucky munthu ovutika samakhala ku Singapore, I'm enjoying in Singapore 🇸🇬 bro
Aaaaaah opusa iwe anthu amavutika ku 🇺🇸 ukufuna utiuze chani in life
@@mcsellahntv6896 ine ndi dolo siine kape ngati atupele muluzi
My vote atupere muluzi
Akunama awa. Atumidwa kuti agawe ma vote akummwera kuno nkuona akukana alliance. Akufuna athandize chipani china kuti chidutse.
Chakwela 0/10
To me welcome back Mr muluzi we know ur dad was a Hero in politics be like him atupele my vote
Kodi Atupere akuthawathawa bwanji akafunsidwa za a Chakwera
I think he might be the right candidate
My vote 🗳
Sakundigwira mtimabe ine, nkhani ya economy sakuyifotokoza momveka
We need alliance please 🙏🙏🙏😭😭
We love you ❤boss
Uyu ndiolephera sayankha futso😊
Mantha ake ameneo mungalamulire dziko inu ngakhale Mulungu amafuna munthu odziwa mchimene ali kulephera kuyankha funso lophweka
Booom atupere muluzi❤❤❤❤
Let's work together as one Chikangawa asowe basi
My vote...
Interigent Man 🔥
Mmene Chilima adayendera 2019, ndikukhulupirira kuti adaphunzira pamene paja and ayenda mmidzi😂😂😂😂😂😂
Boma ❤❤❤❤ tupele
one thing I like about this guy, samapanga nawo politics yonyozana....ndi mfana wa look sharp
Atupele you can't be a president on this country because yo are too young on compain
M'malawi muno timaluza azisogoleli abwino chifukwa cha kuzikonda kwaoyambisa zipani,,, kunena chilungamoh bwanawa ndale anazisiya,, chimene abwelelaso ndichyn please
Wina mwa andale opanda mbili yonyansa pa ndale mfana uyuyu,frankly speaking.
@@SamuelThanganyika that's true my bro
Kukanika kupeleka % ya mzanke kungot 1/10 nzovutaso izi? Kapena sakuzzsata zinthuzi, naye wakanika basi sangatenge boma npake amafuna mcp yibwere ku convention banzi lamvuta uyu
😂😂😂 mumafuna amene chani ngati timamva akayankhula???
Bingu anayimalidza UDF singazawineso mdziko muno pawokhaa
@@kennethnasteve4721 udf ndi malemu achipan
Awa utsogoleli mulibe thandizilani MCP poti ndalama mwatenga kale
Mmmm zamumtima nzawekha choona chili muntima mwawomo
Akuluwa tawayezeka, kumenya kugwesa 😅
❤❤❤❤ Boma
Komatikuyeseni bwana
Agulitsa chipani awa ku congress
He is not answering questions
Tupele ndi munthu oganiza za patsogolo
@@MjombaMoosa l am with you big man
Ndinayiwala paka munaunikira kuti tizankhe molondola chifukwa enawa azalowa m'boma pofuna kuti abe mwakwijo munatiunikiradi
😂😂 Mantha poyankha atupele.
Very simple futso hw marks amene mungawapatse achakwera?.
Yankho dololo😂😂
Koma ndipo 😅
Akuti upereke malikisi iwe ukuyankha zako mmmm uyu wabisala mmasamba zipita kuchikangawa partyko kutha kwa UDF
Funsoyi ayilephera kuyamkha akudodoma dodoma
Palibe cha nzeru wakambapo apa.
Awunope tunyakule
Akuthawa fuso lachakwera
Ali ndi utsogoleri
Onyoza makolo ake afe ndithu......Bingu adaba u president wa udf Mulungu adzabweza
Inunso ndi mbuli yophunzila
Komaso awa iye amafuna kuwonetsa ntchito zake payekha osati adzilamulidwa ndi anthu
Akuzembatu mayankho atupele
Yankhani funso atupele
Akulephera kuyankha bwino bwino mafunso......uyutu akuzapanga mgwirizano ndi Congress
Atupele sakulephela kuyankha zacha chakwela, koma musaiwale kuti atupele safuna ndale zonyozana koma ifeyo ovota ndiomwe tione muthu omuvotela
Ndipo kwambili thawi zambili samenya kampen onyoza
Teroni
Cadet wa mcp iwe atupele muluzi
Atupele amayankhula zogwila mtima koma bwanji sapasidwa mpata kuti alamule?
Amalawi kuyankhula bwino sikulamulira dziko
weyi ndilunga anemeyi sitingamusape upule
..
Sakuyankha funso
Lolani mwanayu alamure
Awa mfundo alibe adzingopita kumakadya ndalama zomwe anaba bambo ake
IWEO UKANDAKHAL ULINDIFUNDO BWENZ UKUVUTIK CHOCHO NO PAIN NO GAIN
Iwe ndi nfundo zakozo bwanji osakamuchotda chikangawa ukalamulire meina anthu adiye kudya chitedze .?
@@cjaylucky munthu ovutika samakhala ku Singapore, I'm enjoying in Singapore 🇸🇬 bro
Aaaaaah opusa iwe anthu amavutika ku 🇺🇸 ukufuna utiuze chani in life
@@mcsellahntv6896 ine ndi dolo siine kape ngati atupele muluzi
My vote atupere muluzi
Akunama awa. Atumidwa kuti agawe ma vote akummwera kuno nkuona akukana alliance. Akufuna athandize chipani china kuti chidutse.
Chakwela 0/10