BAKILI MULUZI KUCHEZA NDI BRIAN BANDA 11/05/2024.

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 13 сен 2024

Комментарии • 98

  • @osmanmalinda939
    @osmanmalinda939 4 месяца назад +9

    The first program kuonera ndikuseka nawo limodzi 😊 pamene enawa kumangokhala kulozana zala basi. What a great man

  • @TabiaNicks
    @TabiaNicks 4 месяца назад +5

    Long live our former president

  • @GhettohVibies-wn9zo
    @GhettohVibies-wn9zo 3 месяца назад +1

    Respect to you our X President Dr Bakili Muluzi🙏🙏🙏💕

  • @luetec
    @luetec 4 месяца назад +2

    what a wonderful interview, ViVa a tcheya, the best well dressed president in Malawi

  • @user-cy7gd1go6y
    @user-cy7gd1go6y 4 месяца назад +3

    Pule amene anawafesa kukoma amalawi paka nthawi yochepa😢😢 mulungu akudaleseni mr muluz ndi wumoyo ndimakukondan❤❤❤❤❤

  • @waxyamidu5638
    @waxyamidu5638 4 месяца назад +2

    Ulemu wanu bambo aife mwatilela zambiri talandila zaulele moti nyengo ya makolo athu samakwanisa kugura respect for you our father and thanks Brian potionesa atcheya

  • @johnkatapeh7182
    @johnkatapeh7182 4 месяца назад +8

    Long live Dr Bakili Muluzi❤❤❤❤❤❤

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 4 месяца назад +3

    Atcheya tsopanoooo!!! timakunyadirani president wamsangala odziwa kuseka, osakhala zinazi aaaah

  • @user-qe2lz7mx7u
    @user-qe2lz7mx7u 4 месяца назад +1

    Bakili knows how to choose but bingu was the best ayao simuziwa economy

  • @JoshusMbewe
    @JoshusMbewe 4 месяца назад +1

    Long live Dr. Bakili Muluzi
    Abwanawa ndi munthu wabwino

  • @IsmaelRichman
    @IsmaelRichman 4 месяца назад +1

    Well spoken Dr Bakili Muluzi atsogoleri azitero tikufunilani moyo wautali pamodzi ndi family yanu Mulungu azikudalisani nthawi zonse

  • @DonaldBanda-qi7yw
    @DonaldBanda-qi7yw 3 месяца назад

    That's true His Excellence Dr Bakili Muluzi could stop just to give someone a lift in his Ministerial Car. For example is my Father (Late Stephen Eliya Banda) and myself, His Excellence the Former President gave us a lift in his Official Car while he was the Administrative General of the Mighty Malawi Congress Party.

  • @rashiddeula5715
    @rashiddeula5715 4 месяца назад +1

    This man! Ayayayay.....the humour is just great. Brian on a lighter note question eish.....ayayayay ndaseka mpaka misonzi. Mpaka odziponyaponya eti? 😂😂😂😂😂

  • @AdamSteven-ne9hg
    @AdamSteven-ne9hg 4 месяца назад +1

    Nantahala ife muthawi yanu long life atcheya

  • @ImraanYaseen25
    @ImraanYaseen25 4 месяца назад +1

    This man his is another level just hear his voice 😊

  • @stewart.mwamughunda
    @stewart.mwamughunda 3 месяца назад

    Malawi ndi dziko lokhalo lomwe mapresident opuma akumva kukoma. Ulemu wanu a Chakwera.
    Taonani a Muluzi,mayi JB, Khumbo, APM, Chilupha n ena.

  • @magdalinemafunase2440
    @magdalinemafunase2440 3 месяца назад

    We will always Love you a chair.❤❤
    Long live.

  • @EddieBakali
    @EddieBakali 4 месяца назад +1

    Quran on shelf mashala habibi

  • @user-sq2uz6yl3s
    @user-sq2uz6yl3s 4 месяца назад +1

    To be honest this man is a greatest man,,,,,,,,,,,,,,,,,long live Dr Bakili Muluzi we love you very much ❤❤❤❤

  • @mtangaJumbe
    @mtangaJumbe 4 месяца назад

    Munthu amene anapangitsa Malawi kukhala owawa kwambiri panopa. Chomwe ankagulitsira ma company kwa amwenye sichikudziwika

  • @SwidiqLameck
    @SwidiqLameck 3 месяца назад

    I like his voice

  • @victorzakeyuzimba7742
    @victorzakeyuzimba7742 3 месяца назад

    Long live Muluzi

  • @atanasioestevao9707
    @atanasioestevao9707 4 месяца назад +1

    Long live atcheya❤

  • @cristovaoherculano8662
    @cristovaoherculano8662 4 месяца назад +5

    Government doesn't run a business. It should create atmosphere for people to do business.
    Ndani wamva zimenezi bwinobwino?

    • @dannymangawa7511
      @dannymangawa7511 4 месяца назад +1

      Ine ndinamva, tcheya si munthu wamba baba anakonza

    • @geoffreyNkhomah
      @geoffreyNkhomah 4 месяца назад +1

      umenewu ndi ntondo endeed

  • @WellieManonga
    @WellieManonga 4 месяца назад +1

    Achalume kuchitekete God be with you

  • @FrankFrancis-ch3xv
    @FrankFrancis-ch3xv 4 месяца назад +1

    Watching live from SA Durban KZN

  • @user-mz8nw6nx6p
    @user-mz8nw6nx6p 4 месяца назад

    Kuti enafe tisakhuzidwe ndi nkhaza za chipani chimodzi for that time Achair,,,munatinvetsa kukoma mu nthawi yanu❤❤❤❤❤

  • @shakajudahTV
    @shakajudahTV 4 месяца назад

    Much respect to our granny mumakwana 🎉🎉🎉🎉

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 4 месяца назад

    Anamva mtunda ukufotokoza, anamva zonsezo ( I remember Mkasa's song. A Chair ndi mtunda)

  • @darlingtonchimutu8390
    @darlingtonchimutu8390 4 месяца назад

    The most likeable PULE of Malawi kuseka continuous

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l 4 месяца назад

    Bakili vuto linapo ndi umbuli komanso business yake o i hope anali kupikulitsa bonya. Nfi masamba

  • @YamikaniPrince
    @YamikaniPrince 4 месяца назад

    Long live achair!we love u!

  • @CumbuNgoma
    @CumbuNgoma 4 месяца назад

    A Gama we love you,long live

  • @aureliojose763
    @aureliojose763 3 месяца назад

    kuntunda 🔥

  • @jaydee1236
    @jaydee1236 4 месяца назад

    The great man 🎉❤

  • @JuniorJonathan-z1b
    @JuniorJonathan-z1b 2 месяца назад

    😮

  • @JustinPhiri-kq2bb
    @JustinPhiri-kq2bb 4 месяца назад

    Sizaiwa former President pa free education primary sizophweka

  • @jeffchikwapata6933
    @jeffchikwapata6933 4 месяца назад

    Big man ever

  • @MonicaMbwera
    @MonicaMbwera 4 месяца назад

    Big man tsopano ❤❤❤

  • @ElijahHarah
    @ElijahHarah 4 месяца назад

    10:20

  • @user-hx8rr1mq7u
    @user-hx8rr1mq7u 4 месяца назад

    Watch live from Nyambadwe

  • @DonHussein-k7x
    @DonHussein-k7x 4 месяца назад

    Allah akudalitseni a chair

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 4 месяца назад

    Achair Allah bless you ❤❤❤❤❤

    • @user-ub1vt2kq4s
      @user-ub1vt2kq4s 4 месяца назад

      Ulemu wanu acheya timakunyadirani kwambiri potibweretsela ufulu Allah bless you more

  • @Gra898
    @Gra898 4 месяца назад

    Ndale ndi tchimodi cz muli kuba muli bodza

  • @user-fl7br3dw4h
    @user-fl7br3dw4h 4 месяца назад

    Mumakwana acheir

  • @tiongegondwe7219
    @tiongegondwe7219 4 месяца назад

    Great man

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l 4 месяца назад

    Mr fake money... Kape wina amene anazesa mavuto mmalawi.kugulitsa ma company chitsiru

  • @zondiwesinging8001
    @zondiwesinging8001 4 месяца назад

    Long live former president a chair anthu

  • @Oraterbadri
    @Oraterbadri 4 месяца назад +1

    putin waku malawi bakili

  • @ibradaglass8646
    @ibradaglass8646 4 месяца назад

    Pa town kumachenjela ❤❤❤achalume

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 4 месяца назад

    Simungathe kusangalatsa aliyese koma ndinu big man muthu wa bwino kwambili

  • @innocentmabedi3850
    @innocentmabedi3850 3 месяца назад

    Mwana wakwathu

  • @ChristopherKalonga-jt8iz
    @ChristopherKalonga-jt8iz 4 месяца назад

    Nice

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw 4 месяца назад

    Sogoreri aziseka abale .Atcheya inuyo ndati inuyo inuyo Atcheya mulungu azikudalitsani

  • @user-ni4nw1ee2f
    @user-ni4nw1ee2f 4 месяца назад +1

    Kuchitekete

  • @NoelKhwimba-bh3ts
    @NoelKhwimba-bh3ts 4 месяца назад

    Sitinaone nawo utsogoleri wanu komabe timanyadira chifukwa Cha zithu zochepa zomwe tinapeza kamba ka utsogoreri wanu taona ma k50 opanda mitu ife ndalama mumkatigaira ndi manja Anu akulu inu osati zinazi

  • @chawezichipeta5326
    @chawezichipeta5326 4 месяца назад

    Kumtunda

  • @patrickyakobe9685
    @patrickyakobe9685 4 месяца назад

    By mentioning Late Chikufwa Chihana he was being honest, that name contributed a lot to Malawi democracy!

    • @NicholasKwajama
      @NicholasKwajama 4 месяца назад

      Mukatero ndinu mtumbuka , mumapopanatu

  • @imranshaibu1577
    @imranshaibu1577 4 месяца назад

    Ku machinga Kwa chikweo ndiye kwathu 😂😂😂

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw 4 месяца назад

    Kholo pa ndale

  • @user-ud6mz3pf7x
    @user-ud6mz3pf7x 4 месяца назад

    Big man

  • @AlidiMusa
    @AlidiMusa 4 месяца назад

    Bambo anagwila ntchito yotamandika awa. Mulungu adziwapatsa dza bwino iwowa

  • @user-mz8nw6nx6p
    @user-mz8nw6nx6p 4 месяца назад

    President olankhula zonveka bwino,,,not zinaziyi

  • @osmanwanja3733
    @osmanwanja3733 4 месяца назад

    Atcheya woeeee!

  • @christophermukaka7403
    @christophermukaka7403 4 месяца назад

    Achalume koma atcheya mmm amathandiza

  • @user-cb9us2gn9v
    @user-cb9us2gn9v 4 месяца назад

    Achair ine ndilipo nkubwera konko ndithu

  • @respectednation
    @respectednation 4 месяца назад

    ❤❤❤

  • @user-ud6mz3pf7x
    @user-ud6mz3pf7x 4 месяца назад

    Achakulungwa wachiyao

  • @respectednation
    @respectednation 4 месяца назад

    Awa ndatcheya kuchikweza kkkkkk

  • @user-xg2ks9nw5q
    @user-xg2ks9nw5q 4 месяца назад

    Uyu ndi amene anayamba kugwirisana ndi amwennye nkhani yobera amalawi

  • @rexphiri7242
    @rexphiri7242 4 месяца назад

    Atcheya

  • @replacefruittreenursery
    @replacefruittreenursery 4 месяца назад

    Muthu wakulu kwambiri

  • @rtqwtetohedron
    @rtqwtetohedron 4 месяца назад

    A Chair palibenso

  • @SullyBartsony
    @SullyBartsony 4 месяца назад

    Tcheya ndikaswiri

  • @LangretBanda
    @LangretBanda 4 месяца назад

    Atcheya mmakwanila

  • @harrispheleni2205
    @harrispheleni2205 4 месяца назад

    Kungogulitsa ma company a boma basi ndalama kupochera achalume anali ochenjera

  • @chinielstailoring-ro9lu
    @chinielstailoring-ro9lu 4 месяца назад

    professor

  • @ElijahHarah
    @ElijahHarah 4 месяца назад

    Bigy...

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 4 месяца назад

    Kungocho kela kuchalichi kuvuna udndo ngamti chakwera

  • @user-ud6mz3pf7x
    @user-ud6mz3pf7x 4 месяца назад

    Byson mwaona

  • @user-nd8zg6ni7l
    @user-nd8zg6ni7l 4 месяца назад

    Tionele zimenezi

  • @DanMhone-iw6xg
    @DanMhone-iw6xg 4 месяца назад

    Tate wokondeka

  • @MaliamUma
    @MaliamUma 4 месяца назад

    Awa anali adindo

  • @BashielSalade
    @BashielSalade 4 месяца назад

    M,tunda wa m,ndale

  • @user-xg2ks9nw5q
    @user-xg2ks9nw5q 4 месяца назад

    Mbava iyi ndi yomwe inaononga zuko lamalawi

  • @user-xe3xo5mu9k
    @user-xe3xo5mu9k 4 месяца назад

    Achalume🥸

  • @OscarChizula-qr4bi
    @OscarChizula-qr4bi 4 месяца назад

    munali munthu

  • @AllieKaisi-je6rm
    @AllieKaisi-je6rm 4 месяца назад

    Munthu wamkulu

  • @imranshaibu1577
    @imranshaibu1577 4 месяца назад

    Munthu wamkulu ❤❤

  • @kondwanimbewe1317
    @kondwanimbewe1317 4 месяца назад +1

    The worst present ever