Ulemu wanu bambo aife mwatilela zambiri talandila zaulele moti nyengo ya makolo athu samakwanisa kugura respect for you our father and thanks Brian potionesa atcheya
That's true His Excellence Dr Bakili Muluzi could stop just to give someone a lift in his Ministerial Car. For example is my Father (Late Stephen Eliya Banda) and myself, His Excellence the Former President gave us a lift in his Official Car while he was the Administrative General of the Mighty Malawi Congress Party.
This man! Ayayayay.....the humour is just great. Brian on a lighter note question eish.....ayayayay ndaseka mpaka misonzi. Mpaka odziponyaponya eti? 😂😂😂😂😂
Sitinaone nawo utsogoleri wanu komabe timanyadira chifukwa Cha zithu zochepa zomwe tinapeza kamba ka utsogoreri wanu taona ma k50 opanda mitu ife ndalama mumkatigaira ndi manja Anu akulu inu osati zinazi
The first program kuonera ndikuseka nawo limodzi 😊 pamene enawa kumangokhala kulozana zala basi. What a great man
Long live our former president
Respect to you our X President Dr Bakili Muluzi🙏🙏🙏💕
what a wonderful interview, ViVa a tcheya, the best well dressed president in Malawi
Pule amene anawafesa kukoma amalawi paka nthawi yochepa😢😢 mulungu akudaleseni mr muluz ndi wumoyo ndimakukondan❤❤❤❤❤
Ulemu wanu bambo aife mwatilela zambiri talandila zaulele moti nyengo ya makolo athu samakwanisa kugura respect for you our father and thanks Brian potionesa atcheya
Long live Dr Bakili Muluzi❤❤❤❤❤❤
Atcheya tsopanoooo!!! timakunyadirani president wamsangala odziwa kuseka, osakhala zinazi aaaah
Bakili knows how to choose but bingu was the best ayao simuziwa economy
Long live Dr. Bakili Muluzi
Abwanawa ndi munthu wabwino
Well spoken Dr Bakili Muluzi atsogoleri azitero tikufunilani moyo wautali pamodzi ndi family yanu Mulungu azikudalisani nthawi zonse
That's true His Excellence Dr Bakili Muluzi could stop just to give someone a lift in his Ministerial Car. For example is my Father (Late Stephen Eliya Banda) and myself, His Excellence the Former President gave us a lift in his Official Car while he was the Administrative General of the Mighty Malawi Congress Party.
This man! Ayayayay.....the humour is just great. Brian on a lighter note question eish.....ayayayay ndaseka mpaka misonzi. Mpaka odziponyaponya eti? 😂😂😂😂😂
Nantahala ife muthawi yanu long life atcheya
This man his is another level just hear his voice 😊
Malawi ndi dziko lokhalo lomwe mapresident opuma akumva kukoma. Ulemu wanu a Chakwera.
Taonani a Muluzi,mayi JB, Khumbo, APM, Chilupha n ena.
We will always Love you a chair.❤❤
Long live.
Quran on shelf mashala habibi
To be honest this man is a greatest man,,,,,,,,,,,,,,,,,long live Dr Bakili Muluzi we love you very much ❤❤❤❤
Munthu amene anapangitsa Malawi kukhala owawa kwambiri panopa. Chomwe ankagulitsira ma company kwa amwenye sichikudziwika
I like his voice
Long live Muluzi
Long live atcheya❤
Government doesn't run a business. It should create atmosphere for people to do business.
Ndani wamva zimenezi bwinobwino?
Ine ndinamva, tcheya si munthu wamba baba anakonza
umenewu ndi ntondo endeed
Achalume kuchitekete God be with you
Watching live from SA Durban KZN
Kuti enafe tisakhuzidwe ndi nkhaza za chipani chimodzi for that time Achair,,,munatinvetsa kukoma mu nthawi yanu❤❤❤❤❤
Much respect to our granny mumakwana 🎉🎉🎉🎉
Anamva mtunda ukufotokoza, anamva zonsezo ( I remember Mkasa's song. A Chair ndi mtunda)
The most likeable PULE of Malawi kuseka continuous
Bakili vuto linapo ndi umbuli komanso business yake o i hope anali kupikulitsa bonya. Nfi masamba
Long live achair!we love u!
A Gama we love you,long live
kuntunda 🔥
The great man 🎉❤
😮
Sizaiwa former President pa free education primary sizophweka
Big man ever
Big man tsopano ❤❤❤
10:20
Watch live from Nyambadwe
Allah akudalitseni a chair
Achair Allah bless you ❤❤❤❤❤
Ulemu wanu acheya timakunyadirani kwambiri potibweretsela ufulu Allah bless you more
Ndale ndi tchimodi cz muli kuba muli bodza
Mumakwana acheir
Great man
Mr fake money... Kape wina amene anazesa mavuto mmalawi.kugulitsa ma company chitsiru
Long live former president a chair anthu
putin waku malawi bakili
Pa town kumachenjela ❤❤❤achalume
Simungathe kusangalatsa aliyese koma ndinu big man muthu wa bwino kwambili
Mwana wakwathu
Nice
Sogoreri aziseka abale .Atcheya inuyo ndati inuyo inuyo Atcheya mulungu azikudalitsani
Kuchitekete
Sitinaone nawo utsogoleri wanu komabe timanyadira chifukwa Cha zithu zochepa zomwe tinapeza kamba ka utsogoreri wanu taona ma k50 opanda mitu ife ndalama mumkatigaira ndi manja Anu akulu inu osati zinazi
Kumtunda
By mentioning Late Chikufwa Chihana he was being honest, that name contributed a lot to Malawi democracy!
Mukatero ndinu mtumbuka , mumapopanatu
Ku machinga Kwa chikweo ndiye kwathu 😂😂😂
Kholo pa ndale
Big man
Bambo anagwila ntchito yotamandika awa. Mulungu adziwapatsa dza bwino iwowa
President olankhula zonveka bwino,,,not zinaziyi
Atcheya woeeee!
Achalume koma atcheya mmm amathandiza
Achair ine ndilipo nkubwera konko ndithu
❤❤❤
Achakulungwa wachiyao
Awa ndatcheya kuchikweza kkkkkk
Uyu ndi amene anayamba kugwirisana ndi amwennye nkhani yobera amalawi
Achisilu inu
Atcheya
Muthu wakulu kwambiri
A Chair palibenso
Tcheya ndikaswiri
Atcheya mmakwanila
Kungogulitsa ma company a boma basi ndalama kupochera achalume anali ochenjera
professor
Bigy...
Kungocho kela kuchalichi kuvuna udndo ngamti chakwera
Byson mwaona
Tionele zimenezi
Tate wokondeka
Awa anali adindo
M,tunda wa m,ndale
Mbava iyi ndi yomwe inaononga zuko lamalawi
Achisilu inu you know not
Umbuli
Owononga sukumuona
Achalume🥸
munali munthu
Munthu wamkulu
Munthu wamkulu ❤❤
The worst present ever
Anakulamulirabe 10 yrs for sure