I'm very proud with this man and I love him so much ,samadzipanga proud ku ma social media moyo wake za family yake ayi ,komanso ngati muthu woti wagwira ntchito m'boma simudzamva any speach ina iriyonseyo ayi , amachita kukhala ngatinso ku Malawiko anachoka koma ayi ,amawonetsa kuti ziii ameneyo amakhala busy kumasamalira zopanga tsogolo la ana ake ,ndi momwe mwamvera apapa za mamphunziro awana ake ,uhule ngati anthu woyimbawa momwe timamvera iyeyu ayi ndithu ,ndimamumva kukoma mkati mwangamu koopsya ada awawa
Ati ku ndale sikoti kuli ndalama zoti ukhoza kuphunzisila ana aaaah ndie kuti zimveke bwanji? Iweyo billy anthu ambili amakuziwila mu music and umaimba bwino and kuimba uku kunapeleka chidwi kwa anthu ovutika kukuika mu m'boma ndi maganizo oti ukhoza kusintha ziko, koma anakaziwa kuti umapanga za moyo wake ndi family koma pa chilungamo ndiwe munthu oipisisa kwambili pa ndale ziko lako sumalikonda wadyela sangatukule ziko.
Ndietu ukayankhula amati ndiwe wa nsanje aaah zichani umakhala umakhala kuti pena ukunena chilungamo. Uyu anthu samamuziwa bwino bwino coz sanakhale nae , amamuziwila mu nyimbo and kwa ine ku nyimbo amaimba bwino mumakhala nfundo , koma kumuonesesa amapanga za family not ziko ndi munthu oipa kwambili
I'm very proud with this man and I love him so much ,samadzipanga proud ku ma social media moyo wake za family yake ayi ,komanso ngati muthu woti wagwira ntchito m'boma simudzamva any speach ina iriyonseyo ayi , amachita kukhala ngatinso ku Malawiko anachoka koma ayi ,amawonetsa kuti ziii ameneyo amakhala busy kumasamalira zopanga tsogolo la ana ake ,ndi momwe mwamvera apapa za mamphunziro awana ake ,uhule ngati anthu woyimbawa momwe timamvera iyeyu ayi ndithu ,ndimamumva kukoma mkati mwangamu koopsya ada awawa
kuphudzitsa Ana mopereka chidwi kwa anthu omvera ndikutha kuona kuti palibe mphwepwa mwa Ana onse
Munthu wamkulu kwambiri , A bwana ozichepesa kwambiri . Inuyo big ,God bless you .
Ulemu wanu Mr billy ndimakunyadirani kwambir ❤❤❤
BK my legend... We love you honourable here in Zambia. Your music is so classic.
I thank God I was part of your generation as well as your music, we are blessed by your art
Ndine emweuja,my favorite song
My favorite artist n the role model himself
Ndiye emwe uja… watching in the States.
I like Billy Kaunda mainly the number NALIYERA
Opanda mbiri yoipa Billy kaunda pitilizani kukhala munthu wa bwino achimwene ❤❤❤❤❤ from Capetown
Eeee iwe phe ameneyu timadziwa kuti ndinu biggy Inu🔥
onabo bile mkaunda voice very nice ❤❤ Mr. nkhumani
Few seconds into the interview and yep. Great voice from the host
Munthu wodzichepetsa kwambli ndiyamba kumvela nyimbo za billy kaunda mucha 1999
Ndangosilila maphudzisidwe a ana ooo God bless you big and humble man
two
How can i access the book "Hills and Valleys"'?
Billy u stil young boy lv ur music
The old legend still lives on.
My favourite musician Bill Kaunda
I like your songs MR
Cool man yoh ilove the personality
Well done Mr BK, we love you more
A classmate timakunyalani
May God bless you all the time
Big respect to Billy kaunda 💚🇲🇼💪
❤❤❤watching from south Africa sand
Zikomo kwambiri oyimba yemwe sanavekepo ndi nkhani zanyasi ndi Billy kaunda ndipo ndioyimba okhazikira pa luso lake timakunyadirani malume k
Very inspired ❤
Mwacheza ndi Munthu wa bwino uyu kwambiri
Oyimba opanda matukutuku God bless you
Munthu odekha ndi dzeru zache ,I really like him, with his songs too
I like that guy so much
Ndi big man pophunzitsa Ana ake sukulu
Very humble man ❤
Bless you Bro
THIS MAN IS CALM.
I remeimber when I was a kid pa chiwembe
The best
A humble Man
Uli boh bily
Ulemu wanu Mr presidente 🙏🙏🙏🙏
Ati ku ndale sikoti kuli ndalama zoti ukhoza kuphunzisila ana aaaah ndie kuti zimveke bwanji? Iweyo billy anthu ambili amakuziwila mu music and umaimba bwino and kuimba uku kunapeleka chidwi kwa anthu ovutika kukuika mu m'boma ndi maganizo oti ukhoza kusintha ziko, koma anakaziwa kuti umapanga za moyo wake ndi family koma pa chilungamo ndiwe munthu oipisisa kwambili pa ndale ziko lako sumalikonda wadyela sangatukule ziko.
Cool man
Legend
Humble mn ❤❤❤❤❤
Nice 🔥
Ahhhh mwakafupikisatu abale
Mawu a billy kaunda takumbuka amalawitonse
Amandidalisa kwambili wakwanthu kupoto ndine symon phetera munthu imozi amandisangalatsa
Ndi oimba yemwe sayangana pansi pa nyimbo zake ,.. amatha
Humble man
Abily timakunyadirani mwasinthisa zambiri mziko muno
Ana sachuluka man🔥
50+ koma looking fresh...
My man.
Aaaa nde kachepatu ka inteviewko
Our new MP
Master
Awawa kungowataya basi palibe angamasule zingwe Nsapato zawo
It is his music career not carrier.
Wa akulu tsopano timakunyadirani mumatha.
Timati Mzimba osati Nzimba😮
Zazelu basi
mwimbanga makola akulu tingateta yayi
Nthawi inachepa koma.
Komatud makolo anu anabeleka mpaka ana 11,,ayi ntchito anaigwira
Oh koma wabeleka
Munthu ozichepesa kwambiri komaso wanzelu
Billy uli ndi Ana 7 ine ndiri ndi 8 ndichitsomo cha namalenga
Sikefa chimoto
In politics ku Blantyre palibe chomwe tingaloze chomwe amapanga chothandiza
Ndietu ukayankhula amati ndiwe wa nsanje aaah zichani umakhala umakhala kuti pena ukunena chilungamo. Uyu anthu samamuziwa bwino bwino coz sanakhale nae , amamuziwila mu nyimbo and kwa ine ku nyimbo amaimba bwino mumakhala nfundo , koma kumuonesesa amapanga za family not ziko ndi munthu oipa kwambili
Koma nde unasosolatu man, ana 7 alone?, kkkkkkk
Amavuta kuphunzira ndi kulela osati kubeleka kkk
Kwabac
I love this man,and i wish him to contact me (please got your message).