BON KALINDO LERO PA 16 JULY 2024 |

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 22 авг 2024

Комментарии • 150

  • @user-lz4kc5ob1t
    @user-lz4kc5ob1t Месяц назад +2

    Ife tamupasa kale mai kaliyati president of utm

  • @user-ig9ip8jq7v
    @user-ig9ip8jq7v Месяц назад +1

    Watching from S A port Elizabeth timakunyadilani bwana pitilizani kuti imilira Mr Bon kalindo l Salute u bwana

  • @EnittaDavison
    @EnittaDavison Месяц назад +2

    Umatiymilra iweyo ulemu wako bon 🔥🔥🔥🔥👏👏👏👏👏👏

  • @justinmakiyi4189
    @justinmakiyi4189 Месяц назад +10

    As UTM and Malawi as whole country we are luck having this guy as somehow a prophet or advisor to the difference parties. The choice is in our hands to take the advise or leave them. But one day we shall remember Him. That's the free advise indeed. Regards

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Месяц назад +6

    😅😅 zapana ndithu ndipo sanati and who is Manganya??? U don't know Bonnnnnn Kalindooooo mwana oopsa kwambiri ndiponso mumumva, the DC mwana woyankhulira pa mchombo pa Malawi, alibe mantha ndipo saopa Unyolo kaya mfuti😅😅😅

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Месяц назад +5

    President wathu wathu amangoyima pachilungamo🎉

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Месяц назад

      @@Lazarus-qo1sl president wa zitsilu zokhazokha ndi mbuli zophumzila koma makolo awo fees anagowononga ngati mmene DPP inawonongera dzikoli

    • @VungaQueen
      @VungaQueen Месяц назад

      Mmmmmmmm inu Bon Kalindo musiye nde zitsilu tili ambili inu anthu abwino Kharani km siwani kt choyipa chitsata Mwini nadutsa sindinyoza ine

  • @christopherphiri8476
    @christopherphiri8476 Месяц назад +3

    Born kalindo will help UTM if anything engenge him to assist he is a man of action Christopher phiri from Zambia

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer Месяц назад +3

    DC born kalindo more fire 🎉

  • @SteveSamson-t9d
    @SteveSamson-t9d Месяц назад

    following kalindo Diiiiiìiiiiiiii siìiiiiiiiiiiii

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s Месяц назад +3

    Awa ndiye amkamuna a UTM zili ndiinu kunyozera km Bon ndiye walangiza.

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Месяц назад +5

    The DC, Mr booooooon kalindo 🎉🎉🎉

  • @TooNajahInsideKoshah
    @TooNajahInsideKoshah Месяц назад

    Iwe ndiye president wathu wathu

  • @DalitsoTwalick
    @DalitsoTwalick Месяц назад +2

    Thanks my president for ur information

  • @user-yk5qd6sk8e
    @user-yk5qd6sk8e Месяц назад +2

    the dc 🎉🎉 mwana ooopsa kwambili

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i Месяц назад +2

    Kodi a UTM mukuitana athu kwana chifukwa ninji Kodi menemo mulibeathu oti angayendese chipani ?bwinonazotu ndalama inampha mwanawamuthu zayekha ananyika sima m'mazi

  • @vincentkhunsanama584
    @vincentkhunsanama584 Месяц назад +2

    Yeah, the DC is not making mistake to advice the utm fam big up the DC

  • @JosephLemani-qq1is
    @JosephLemani-qq1is Месяц назад +3

    Mwayankhula bwino bon kalindo ena akufuna kugwetsa chipani cha UTM koma bola abwelele komwe anachokela

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r Месяц назад +1

    Inetu ndimaganiza Kuti boni kalindo ndi mamuna koma ayi eti ndi wamkazi or kuganiza kwake ndimadabwa nako aaah lero ndamumvetsetsa ndi mkazi paja amavalaso ma browsers amamangaso tsitsi 😅😅😅😅😅 koma MCP yamulela bwinji because popanda MCP sibwenzi ali miss kalindo lero ayi akuyenera ponyoza MCP uku ndlama zikulowa kuchokera kwa anthu a ndale opposition 😅😅😅😅😅 uyithokoze MCP ukuchita bwino kwambili keep it up moto kuti buuu Satana akugwila ntchito yowatsogolela anthu ku moto ndi pakamwa kulankhula sosakondweretsa ambuye work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die

    • @JusticeNyirenda
      @JusticeNyirenda Месяц назад

      Thanks for the information about Jesus, but the rest is senseless

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Месяц назад

      @@JusticeNyirenda so it's better not to take part to these people we can die in sins we are in the last days all things must come to pass like economy James 5 the whole chapter famine, wars, disease all these they contribute financial crises all over the world Mathew 24 vs 5 to 8 then you will here about the national Sunday Law to combat all the crisses mentioned above by force in the name climate change and the pope will rule the world for 3 and half years but he will be overflow by all nations when they will see that no change but hypocrisy leading people to destruction and people will be against him work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die follow Jesus not politicians ndi abodza Ngati omwe akuchulikitsa machimo awo pa social media

  • @ElizaJames-by8ef
    @ElizaJames-by8ef Месяц назад +4

    African man ❤❤❤

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi Месяц назад

    Muzibwereza mau aoooooopsya kwambiri 😅😅😅 ndi iiiiiii

  • @KondwaniBilliat-t4g
    @KondwaniBilliat-t4g Месяц назад +1

    A DC tikupempha Mulungu wa kumwamba akupaseni moyo wautali ndi ntchito zanu zabwino pitilizani tilipambuyo panu nga!nga!nga!!!!!!!

  • @EdwinMabviko
    @EdwinMabviko Месяц назад

    Unayankhula zimenezo ,galu iwe!!!

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x Месяц назад +2

    Very sensible message bwana #DC♥️🔥🔥🔥

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx Месяц назад +2

    Good advice Mr President

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Месяц назад +1

    The DC we are with you Mr president wa anthu osawuka ❤❤

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Месяц назад +1

    Wolimbana ndi Boooo Kalindo oooo the DC atembenuke ndipo azilume kunsana more 🔥🔥🔥 Kalindooooo the DC 😅😅

  • @LuckyMhlanga-m1u
    @LuckyMhlanga-m1u Месяц назад

    Kalindo you are true

  • @HajjiSufiyani
    @HajjiSufiyani Месяц назад

    Pitilizani. Kutisogolela. Ndithu kuyakhula koveka bwana

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x Месяц назад

    Ndizona osangotenga zili zonse km a Malawi asanhhe

  • @user-wu8kp7ui5j
    @user-wu8kp7ui5j Месяц назад +3

    The DC 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @AliajoeAliajoe-vv1wo
    @AliajoeAliajoe-vv1wo Месяц назад

    Great man

  • @violetpotani
    @violetpotani Месяц назад

    Eeeish koma information mumayipeza 😅😅😅anthuwa bwenzi atangokhala coz akunyozeka

  • @Judah-zb6sl
    @Judah-zb6sl Месяц назад

    The DC ❤🎉🎉🎉🎉🎉

  • @ErickMambelera
    @ErickMambelera Месяц назад

    Umakwana kalindo

  • @WanangwaVwalika
    @WanangwaVwalika Месяц назад

    More fire!!

  • @eliaschinoko2086
    @eliaschinoko2086 Месяц назад

    The Dc Booooooooooooooooooooooooooooooooooon Kalindo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @OmrahGeraldOmrahGerald
    @OmrahGeraldOmrahGerald Месяц назад

    ❤❤❤❤ The DC kungalula

  • @davidmzee2205
    @davidmzee2205 Месяц назад

    Nde mwati Pepe Kale ?😂😂

  • @annamazingashaibuh6276
    @annamazingashaibuh6276 Месяц назад

    The DC kkkkkkkkk🔥🔥🔥🔥

  • @KingLunda-u1t
    @KingLunda-u1t Месяц назад

    Big man hooooooo

  • @Lemankais
    @Lemankais Месяц назад

    Bon ndi kampani simunthu wamba

  • @SteveZimba-e8s
    @SteveZimba-e8s Месяц назад

    Gwiritsani ntchito malangizo amene wakupatsani DC osazitaya muononga chipani chanu chabwino bwino

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb Месяц назад +1

    Ng''alula m'bale.

  • @user-oy6dl1pv9e
    @user-oy6dl1pv9e Месяц назад +1

    Following kwa Diiiiiiiiiiiisiiiiiiiiiiiiiiiiii

  • @SanidaChirwa
    @SanidaChirwa Месяц назад

    Ing'alilen fada ,osaopa ay Malawi ndiwathu uyu

  • @FelixKazembe-wi5zb
    @FelixKazembe-wi5zb Месяц назад

    Ndizosantheka kutuluka anthu onse chipani" choti mudziwe chipani cha UTM chamwazikana! Pepho langa ndiloti osalawo asachuluke zomwe zitapangise chipani kuchepa mphavu...manganizo anga.😢

  • @sulleahmnyimbili1362
    @sulleahmnyimbili1362 Месяц назад

    Thanks for the advice Mr kalindo

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma Месяц назад

    Akunamizana kwambili athu amenewa mcp ikutula udindo pasi

  • @Raph-kayRaph-kay-g5v
    @Raph-kayRaph-kay-g5v Месяц назад

    Utm samalani ndi kabambe ndi brocko yati musabwerere Ku DPP matchera chenjerani mafana

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw Месяц назад +11

    The DC 🎉🎉🎉🎉🎉

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Месяц назад

    Ur right the DC akapusa kulowa mikangano

  • @user-sk3ld2ss7s
    @user-sk3ld2ss7s Месяц назад

    Boni kalindo ndi chilata chopanda kanthu, chomangosokosera...

  • @Maliko-bp1xn
    @Maliko-bp1xn Месяц назад

    Mukulankhula zooonadi

  • @PetroMatias
    @PetroMatias Месяц назад +1

    Ndinzoonadi asangotora munthu

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Месяц назад

    The DC mwana wowopsya kwambiri Bon kalindo

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 Месяц назад

    The DC mnyamata oopya kwambiri 😅😅

  • @EmmanuelMalata-r4j
    @EmmanuelMalata-r4j Месяц назад

    Mumatiyimilira bwana❤

  • @YolliyajeerasYeeras
    @YolliyajeerasYeeras Месяц назад

    Mwana ooooooooooopsa kwambili

  • @RuthMoto
    @RuthMoto Месяц назад

    Mukhalise comrade Bon kalindo

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Месяц назад +2

    Amp alibe nawe nthito kambwe iwe chisilu

  • @user-pb6wb3iz7z
    @user-pb6wb3iz7z Месяц назад

    Well narrated

  • @BrightNkhoma-xz4bg
    @BrightNkhoma-xz4bg Месяц назад

    Athu opusa kwambiiri akuona ngat tikugona......... Our president Bon Kalindo 🇲🇼🇲🇼🇲🇼 😂😂😂😂 pepekale

  • @user-mk4ju6iw7c
    @user-mk4ju6iw7c Месяц назад +1

    Mwathandidxa akafunakunyodxela anyodxele okha

  • @SHABBASELEMANI-o8d
    @SHABBASELEMANI-o8d Месяц назад

    Ati PEPE KALE... koma DC

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma Месяц назад

    We folow

  • @jacksonmaster2288
    @jacksonmaster2288 Месяц назад

    Kalindo UTM amaikonda kwambili

  • @EstherBailoni
    @EstherBailoni Месяц назад

    DC , tiye Nazo usaope

  • @DICODIDICODI
    @DICODIDICODI Месяц назад

    No☝️THE DC

  • @richardjumah198
    @richardjumah198 Месяц назад

    UTM malangizo a ulele awa please

  • @user-rr7je1zi8t
    @user-rr7je1zi8t Месяц назад

    Kuti nkhaaaa wabwela bon kalindo

  • @KondwaniBilliat-t4g
    @KondwaniBilliat-t4g Месяц назад

    Backward never forward ever ❤

  • @PeterNamphwanya
    @PeterNamphwanya Месяц назад

    Chi booooon kalindooooooo🎉🎉🎉🎉🎉

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo Месяц назад

    The DC

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7v Месяц назад

    Sakumudziwa Boooon Kaliindo

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Месяц назад

    Bola mwachenjez ali ndi khutu ambve

  • @Momweekly
    @Momweekly Месяц назад

    Well spoken

  • @MecyMalothi
    @MecyMalothi Месяц назад

    The D C our pangolin

  • @jumahgeorge
    @jumahgeorge Месяц назад

    Following

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon Месяц назад

    Born kalindo the deceeee

  • @user-rr5nq2uo6i
    @user-rr5nq2uo6i Месяц назад

    Big up the DC

  • @AnyumbaJulias
    @AnyumbaJulias Месяц назад

    Ulemu wako iweyo bon kalindo

  • @user-zl5wv8ix8u
    @user-zl5wv8ix8u Месяц назад

    Kalindoo akunena dzoona

  • @jumahgeorge
    @jumahgeorge Месяц назад

    The DC more 🔥

  • @JohnWindford-jv8ls
    @JohnWindford-jv8ls Месяц назад

    Kma azipumako Tizimvako zina.

  • @marcelolemos1484
    @marcelolemos1484 Месяц назад

    THE DC

  • @ClementJosephy
    @ClementJosephy Месяц назад

    Inuyo munavaya patali ana achepa,... Eeeeee

  • @BrightonKamwendo-db1ci
    @BrightonKamwendo-db1ci Месяц назад

    Mau onveka zeeed mbuyanga

  • @GiftJulius-ro9ev
    @GiftJulius-ro9ev Месяц назад

    Kabambe simunthu ..

  • @MaxwellKananji-r5d
    @MaxwellKananji-r5d Месяц назад

    Makamaka pamene wanena kut pakufunika mery chilima amutenge kut agwile naye ntchito pamenepo Mr DC mwanena zoona ndipo mzimu wa SKC utha kuusa mumtendele

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Месяц назад

      Chifukwa chamkazi wakeyo?
      Mukunama ....za Mulungu amaweruza yekha ndipo sapanga pangano ndimunthu...Za dziko lapansi musaphatikize Mulungu

    • @FelixKazembe-wi5zb
      @FelixKazembe-wi5zb Месяц назад

      Ndichaka amalawi dale zimativuta chifukwa mumafuna anthu omwewo azipanga dale. banja lonse abambo akakhala president mwanaso akufunaso wu president omweyo ayi😂😂😂😂 dale sichoncho.

  • @user-hq6dq7zr1e
    @user-hq6dq7zr1e Месяц назад

    Auzeni a utm azinyozela wokha

  • @TalazanGamah
    @TalazanGamah Месяц назад

    We follow

  • @lydiagadama4887
    @lydiagadama4887 Месяц назад

    The Dc

  • @YusufIbrahim-w1g
    @YusufIbrahim-w1g Месяц назад

    Boooon kalindo is not sepro man is big man chizulo chat ambawi Allah bless him

  • @RhodaNombo
    @RhodaNombo Месяц назад

    Mmatiimilila the dç

  • @oskidooscar7468
    @oskidooscar7468 Месяц назад

    Aaaaaaaaaa awa amaopa manganya ndamzawo

    • @Raph-kayRaph-kay-g5v
      @Raph-kayRaph-kay-g5v Месяц назад

      Manganya nkanyama kanji? Phwala lako wamva

    • @oskidooscar7468
      @oskidooscar7468 Месяц назад

      @@Raph-kayRaph-kay-g5v manganya olo nda bambo ako angafanane iwenso chisilu et
      Manganya is a vp of malawi
      You like it or not

  • @TemwaKabisa
    @TemwaKabisa Месяц назад

    The DC 🎉🎉🎉🎉🎉❤❤

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn Месяц назад

    Pepekale ameneyo wakumalawi?kapenawaku ithiopia

  • @JosephyMagombo-t7d
    @JosephyMagombo-t7d Месяц назад

    The DC ✊️

  • @stormchatepa134
    @stormchatepa134 Месяц назад

    bwana nyo

  • @ellensambo6323
    @ellensambo6323 Месяц назад

    ❤❤❤