I never miss your daily talks. Keep on being REAL. MALAWIANS need your voice and eyes. Malawi tavutika for too long. Yet we are a country full of human resources with HUGE POTENTIAL AND LOVE FOR OUR COUNTRY❤
From Mozambique to Zimbabwe antill Germany how much did he spend muzipatala mabedi, mankhwara mulibe mzimu wothandiza anthu wovutika alibe, koma ziwani zoti nthawi yimasitha.
Kodi a Peter Mutharika angakwela njinga???? Ako ndi kachinyamata nsanje ikuphani,,,,ufuna udindo wauponda palibe udindo wako Bon kalindo vuto ulibe ivini JCE koma ukufuna udindo
What kind of president playing like that so which means he don't think about country why he's going to playing like that no no we must think guys his playing so much
Sitikutanthauza kuti a president kukwela njinga ndi vuto ayi koma ndalama zomwe akuonongazo kumayenda ndi anthu ochuluka ku maiko akunjazo ndi misonkho ya amphawi yomwe ikanathandiza kugula mankhwala muzipatala inuyo simukuona nokha pamenepa anthu omwe ali ndi ana sangatenge kandalama kochepa komwe angathe kugulila chakudya ndikumakayendaka juga ayi apa sitikunyoza president but it doesn't make sense for a president leaving his own country and doing rubbish to other countries that's very nasty and not good at all guys be wise before you support this nonsense please
I never miss your daily talks. Keep on being REAL. MALAWIANS need your voice and eyes. Malawi tavutika for too long. Yet we are a country full of human resources with HUGE POTENTIAL AND LOVE FOR OUR COUNTRY❤
The DC ❤❤❤❤❤ bon kalindo mwana woyipa kwambiri
Ayi
Ng'alulayizeshoni booooooni kalindoooooo the DC
We all love you Mr Dc
Ulemu wanu honorable kalindo friend from liwonde
Ndipo iyeyu chomwe waona cha nzeru nkukayendesa njinga ku German? Asayendesa kuno njingayo bwanji? Ndiye ife zitipindulira chani zokayendesa njinga ku German pomwe kuno akungotigwetsera kwacha ife nkumasauka?
Am watching you from Lusaka Zambia 🇿🇲🇿🇲 kucharo 🎉🎉
From Mozambique to Zimbabwe antill Germany how much did he spend muzipatala mabedi, mankhwara mulibe mzimu wothandiza anthu wovutika alibe, koma ziwani zoti nthawi yimasitha.
You are the BEST🌺💜🙌🏽💯🥇
Very true sir
Bon Kalindo ambassador given to poor Malawi from heaven for free.. Go Go Go
😂😂😂😂😂
Mizimu yonse 9 ikumuona mr chikangawa
Kikikikikiiiii koma Amoyaaaaa matong'aluratu!!!!
😅😅😅kulibe even company yopanga thabwa ya ndege 😂😂😂😂😂😂😂these is word make mi following u bon kalindo
Uyu ndi dolo koma vto sakambako momwe aphuzitsi akuvutikira....mphuzitsi kuchitidwa promote February koma mpaka PANO osasinthiridwa malipiro
DC❤
Zooʻna zoona man good speech
😂😂😂😂😂😂 Ndege ya Manu kkkkk
Kodi a Peter Mutharika angakwela njinga???? Ako ndi kachinyamata nsanje ikuphani,,,,ufuna udindo wauponda palibe udindo wako Bon kalindo vuto ulibe ivini JCE koma ukufuna udindo
😂😂
Push Mr kalindo
😂😂😂😂 Ndege ya Manu
Komartu amanena zoona dc mpamene tikumunyoza tidzAmkumbukila ndithu
Funso,,,,,kodi a Peter Mutharika angakwele njinga???
The dc is very strong man in malawi athu amenewo ndi amene tikuwafuna ku malawi zigawo zonse zakumalawi
A Bon kalindo alibe fundo ndinasiya kale kuwanvela palibe chimene ma data anga akutengapo pa Bon kalindo
Kikikikikk😂😂😂😂😂😂😂 matama a vera
We are with you the DC
Umakwana boni kalindo❤❤❤
The DC
Koma inuyo nda nyoooooodiiiiiii big up
Koma ambwiye chemuruphale 😅😅😅😅😅 iyayizikomo ambwiye
We just have a president but not leader like it or not i don't care
Kkkkkk uku ndy kung'alura 😅😅😅
Kkkkkkkkk km bon kalindo
Umakwana koma
Yes maka yamdzio muibweleze
Simatama koma ndi nthawi akuyendamoyo ikuwoneka ngati matama
Umakwana do ❤❤❤❤❤
Kkkkkkkkkkkk koma ndaseka
The Dc mwana mulanje
Bt kumvetsa chisoni madera ena like Bangwe anthu kumamwa madzi apachitsime ngati simtauni
Iwe ndiwe chitsilu wava: usamanyoze chakwera, munthu amayenera akugwila ntchito.
Kuwononga mitsonkho yathu kumakwera njinga ku Italy koma umbuzi siyachikumba yokha iyiso ndimbuzi yeniyeni Mr chikangawa chakwera 😅😅😅😅😅😅
Chikangawa ndiwochitisa manyazi kenako azakamukweza wilibala zaziiii
BON KALINDO NDI KAPE UYU MXEEE
Boni kalindo puliz tandisiye ine chonde 😂😂😂😂😂 ndatopa nkuseka ine
Dyela azisongoleli
Kumalawi kuno nsanje idzatipha kwabasi, kudzikonda ndi ndi kudzikundikira, chavuta nchiyani munthu kukwera njinga aaaa
kaya kkk
Eti abale 😂😂 zinazi umangozindikila data yapita pachabe ndizinthu zozizila
Muli ndi vuto ndinu anthu akupha inu
@@Eric-gb9ms iyi ndi social media akulu, osamapusa nazo
@@miccah81 l don't care about social media bro the guy is talking the truth vuto anthufe timadana ndichilungamo
Ati what really happene wa chani😂😂😂😂😂😂 iwet ndiwa ntopola😂😂😂😂
Vuto utsogoleli wa matama, wamata 😅😅😅😅nthawi yolandira ndalama yo chonde a kalindo mudzandikondole😅😅😅, vuto kudzimva akamayenda ngati sanamweko madzi apachitsime
Kodi ameneyu ngotani? Chomwecho anthu abandu kuno amawalipitsa nsonkho
Boni kalindo chitsiru chamunthu,kuphatikizapo omwe amachemerera munthu wamisala,
Kalindo 🔥
Mboni kalindo winaso ndi umbuli sopano, mvuto simukisiyanisa zabwino ndi zoipa mukungofuna kutchuka bas
Osauka nzako ndani galu iwe uli mu hummer ...mabodza basi
Apa ndiye wationjeza nkuluyu
😂😂😂😂 dziko lotii even thabwa ndege lilibe😂🤣🤣
😂😂😂😂😂😂😂 auze Bon
Hon kalindo tikuyamikireni, ntchito yanu yoimilira amalawi osaukafe mukuigwira, ndipo mwainu mulibe dyera.. mmbuyomu achina Ben longwe anaesetsa kukuonongerani mbiri kuti mumalandira ndalama kwa andale, koma ife amalawi tinapeza umboni kuti amakunamizilani.
What kind of president playing like that so which means he don't think about country why he's going to playing like that no no we must think guys his playing so much
Ndipo palibe fundo apa zamisala Basi zayamba relo pule kuenda pa kovoi
Ina ndi sanje naye kapolo uyu,, ukhala 5 years Ina ukutulutsa audio, MCP my vote
Yeah akhalira dzimenezi 😂😂😂😂
Enanu umbuli ndiumene wakula sindimakudabwani chakwela sitsogoleli sakudziwaso chimene akuchita
Kapolo koma iweyo
Ungafanane ndi a Bon kalindo iweyo
Kuvutikaku kukuphetsani ndimaumboniwo Achakwera wo
A Bon Kalindo, Dziwani kuti nyengo imasintha. Nasuso kwerani yanu njinga
Why do you mean
Usilu umenewo
😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊
😂😂😂😂nde wat ma MP a kazi 8.8
Ulemu wanu Big
Boni kalindo inu mumakwanira
KkK koma Bon
Ndipo akanagwa
Chisiru chimandikwana heavy sanje basi ngat uli phawi osangopita kumunda kukalima bwanji
I weyo ndi mphawi
Ungafanane ndi Bon kalindo
Olima ndi iweyo
😂😂😂😂😂😂 nde mwati vuto ma tttaaaaaamah😂
Zosekhala bwino
Zaziii
Fuso lopusa limenero
Y you got body guards iŵeyo?
😂😂😂
Umatisokosela iwe anakumana unduna ndiye utikwanepo apa aliyese amachita matama ndimene wapezela ndi nthawi yake chakwela
Mbuli zimangolira chilichonse zimaganiza kuti munthu akakhala president basi chilichonse asiye aziwaphikira ngakhale nsima,Malawi womvetsa chifundo anthu ozolowera kupatsidwa chilichonse
Auze bon
The DC😂😂😂😂
The Dc
Ine uyu amandi bowa sanje thoooo mcp my vote
Go ahead
Why you telling us
Funk off
futsek
Go and mop the lake
Ndie utani chifukwa ndie Ali ndi anthu omkondatu meaning or MCP yakoo singapange mistake yomupha,
Wamisala osagenda
Galu wachiwewe uyu adachita khungu sakuona🎉
Ndibwino kubadwa mphawi kudzafa olemera not kubadwa mphawi kudzafa mphawi 😮😮😮
Achitsilu mmalo mothandza dziko akulisya mkumakazendewela njinga koma mmutumu muli nzeru?ma supporter mkumaombela mmanja chonsecho nao akufa ndi umphawi zikutithandza chian iz tangomupatsen kalindo amalize kwatsalaku kuendetsa dzikoli aaaaa
@@Biath-m4b zomwe wayendela kwaife ndizamphindu kwambiri km inuyo mbuzi njinga inuyo simungakwele chifkwa chamatama palibepo zachilengo km umbuli ndiuphawi ndi chifkwa mukuona ngati zolakwika
Mmene mumadyela ifetu tiliku magobo sitimalimbana ndi zimenezo zoti kuli njala mankhwala kulibe zimenezo zikusangalatsa amene dziko akulimva bwino koma kumwamba kudzayankhula
Ndikape bon uyu timachenji taku dpp tampengetsa ndiyekukwela njinga mchifukwa kkkkk koma masala inayi
Kuyikira umboni wauchigaru
Ndalama izi zikumphani
Zikomo kwambiri bwana, mwatiyankhulila ife aku chitipafe ndipo tikuzunzika kwambiri ndinkhani ya mafuta, ndipo kulibiletu mafuta kuno
Akutherani bandu wakuuzani nindani kuti muvere zaziiiii zopanda nimuchere akuchita bwino kukupasanjinga akuziwa kare kuti ndiwe mbava inde karindo umatiyimira
Eish anatilodzayo ayi ndinthu adatilakwira ndinthu 😅😅😅😅
Iwe karido ngati ulibe chochita tengani khasu pitani kumunda muzika sosa ndiwe mbwewa
Akupasani zingati? a Mr chikax anuwo?
Wayamba kabanza kunja
Ndipodi ndi amphawi
Sitikutanthauza kuti a president kukwela njinga ndi vuto ayi koma ndalama zomwe akuonongazo kumayenda ndi anthu ochuluka ku maiko akunjazo ndi misonkho ya amphawi yomwe ikanathandiza kugula mankhwala muzipatala inuyo simukuona nokha pamenepa anthu omwe ali ndi ana sangatenge kandalama kochepa komwe angathe kugulila chakudya ndikumakayendaka juga ayi apa sitikunyoza president but it doesn't make sense for a president leaving his own country and doing rubbish to other countries that's very nasty and not good at all guys be wise before you support this nonsense please
Auze the dc
Bon Kalindo ndi President wa Amphawidi
@@PETERSINKADZIWA mbali akwanuko osati enafe km mbuzi nu
Mavutowa mwawawona lero?vuto mumaganiza zopusa
Wamisala uyu
😂😂😂😂 koma moyo
ukharira yomwey namabwebweta lwe onyooooooo
Nawetso ukhalira yomangoyikira umboni wachikangawawo