Akulu akulu awa they are intelligent in their own field of study but i think there is a reason why they are not PRO's...or negotiators, literary akulephera kuyankha mafuso pano. simple question, do you have an answer for your proposal? if not why telling their followers kuti Boma has agreed to their demands. they just want to look good to their followers
Nkhani ya mkazi as a classic example in this isuue isn't relevant coz u are not related in any way ..... Auzeni a boma not to give a deaf ear to these unions muphesa nazo anthu osaukafe pomwe inu muzinyamuka wa maiko akunja
Mdalama akupatsa apolice kuti akasake wa bakili muluzi tv malo molipila anthu awa
Ntchito yathu ndiyotopesa,especially Night shifts,chonde hear our cry ,ndalamazo zituluke
Tidakupatsanikale mu COVID, ndite amene yamuchepepa ndalama asiye,
Kunjaku alipo ambili akufuna ntchitoyo.
Very true...
Komanso inu ma doctor mukuyenera nso kumawauza zoti kuchipatalako nso kulibe mankhala
Thanks 🙏👍
Akudya banzi amenewa akhala pansi,,ma mafiya alipo they are planning kuti awaphwetse.
MoH....try to listen to our health workers &help them accordingly, it's not good to have deaf ears
Bola ngati ndalamayo ilipo
Overworked , undervalued. No wonder Malawi has the poorest healthcare in the world 😢
Brian ntchito yosamalila miyoyo ya anthu si ntchito yophweka,ayenela kuyakhidwa mwachangu,ndipo ngati sakuyakha ayenera kutenga action,ndipo anthu otelewa ndiosafunika ma office antchito zaboma
Moto buuuuuu.......ndangokhala pakona kudikira sit in
Akulu akulu awa they are intelligent in their own field of study but i think there is a reason why they are not PRO's...or negotiators, literary akulephera kuyankha mafuso pano. simple question, do you have an answer for your proposal? if not why telling their followers kuti Boma has agreed to their demands. they just want to look good to their followers
Ndipo amene akuti anthuwa adya bans akulakwa kutero. Government is playing tactics of delay.
Brian musalimbike za salary ya May. Mupangitsa kuti salaryo isalowe. Honestly the agreement letter in this case equals the settlement agreement.
Brian ,you must improve on conducting interviews ...😊
Wawa
Ndalama ndizimene akumwaza m'misonkhano zija koma zoona matama onse aja madokotala sakulipidwa😮😮
These guys are not serious as the increases come from Treasury n have a direct bearing on budget numbers. S
Komaso buran iweyo umayiziwa tchitu yachipatala zakazi ndiiz ndizosiyana
Mmmhhh guys athuwa amagwira ntchito yolemesa kwambili .kodi m'boma mukufuna athu amwalire kaye then muzibwera zithu zitavuta kare???shame on you malawi government
brain upolo moto musalangulise anthu pambali mwafa
Ndiye wamwano ndi ndani pamenepa
Awapatse zawo anthu awa amagwila tchito yotamandika
Kkkkkkk Brian musatsamwitse anthu😂
Kodi mukuwapanga chochi madokotala chifukwa mukadwala mumapita zipatala zakunja zipangani koma choyambilira mukanaganiza kuli anthu alibe kalikose pompano muwafuna mulungu akudaliseni zigawani ndalamazo
Kwayaka moto kuti buuu
Brain usawatopese makosanawo please si anthu andaletu awa chepesani moto please
Dziko la malawi timgosithanisa ndi chigubu cha kachaso 😹😹😹
Nkhani ya mkazi as a classic example in this isuue isn't relevant coz u are not related in any way ..... Auzeni a boma not to give a deaf ear to these unions muphesa nazo anthu osaukafe pomwe inu muzinyamuka wa maiko akunja
KOMA MALAWI WAVUTA
Think of poor Malawians before going for a sit in
Them too are poor Malawians!
They have a family to bring up.
They should listen to them.
Even health workers are poor Malawians, let the government think of all poor Malawians
Even health workers are poor Malawians, let the government think of all poor Malawians