Osanamapo apa. DPP loves using UDF to achieve their political goals. After Bakili muluzi spent his time, money and energy he was dumped like piece of s…..t. Apa DPP,MCP,UDF,UTM,PP,Aford aliyense ayime payekha then after failing to get 50+1 you can form concrete alliances. Ma alliances opanga nthawi zino ndi aja mukangowina mmayamba kuwaudza ena kuti mukanawinabe popanda iwowo. Komanso why should youthful leaders with energy and vision throw away their ambitions because of old failed leaders. Chakwera has failed and Muntharika analephera kale. We need to be moving forward and way from these failed politicians.
Nkhani yonvetsa chisoni, si paja ali pa mpando iye ankati MCP chipani chakupha? A Malawi akufyza CHITERZE, iye akuononha ndalama kugula anthu ndi kumakopera anthu anthuwo
Do not be bothered by Bakili Mluzi's actions. His speech at UDF convention revealed it. He was Kamuzu"s henchman. One could not just hold the post of SG in the MCP of Kamuzu. Bakili anali chief planner wakuponyera anthu kung'ona ndikupa anthu. During his time in MCP, he oversaw the death of Albert Muwalo, Gadama, Matenje, Focus Gwede, Sangala, Chisiza brothers and many others
Oh,ndiye kuti chipanicho tikusiyileni ndi chani aku Machinganu eti?,iwowo ndiofunika aphatikizane ndi zipani za ku m'mwera kuti anthu aku Machinga adye?,aMalawi ena alibe ntchito or atafa ndi njala?.Khala nachoni chipani chanu cha a Yao.
Bakili muluzi atupele ndi anthu adyera ndi mbuzi za anthu akufuna iwowo azilemela amalawi azivutika agalu a udf wosavotela ndipo atupele sazalamula dziko la malawi chifukwa ndi wadyera machende ake
Pamtumbo oako iwe wa Ku Tysolo iwe. Ahlomwe muli pa tchito galu iwe, without UDG mukanakhala ndani ? Kulira uku pamtumbo pako chaka chonse. Okupha Albino pamtumbo pako
Kodi bwanji alomwe aliense amene sakuchita za DPP ndi mdani wao? Inu a DPP democracy mumaidziwa. Nthawi imene anthu amamenyera kuti kubwere democracy DPP ILIPO? Simudziwa democracy ndi chifukwa chake mungofuna kuti dziko lonse la Malawi likhale la DPP. SHAME ON YOU
Inuyo a dpp ndinu ana pandale…MCP inakuphumitsani Boma APM atalumbiritsidwa kale nde what makes u think mungawine pano muli kunja kwa boma? Alomwe inu joke too much 😅
JESUS IS ON THE THRONE Mbewu zomwe timazala ndi zomwe timakolora... Mukudabwa chani? Mbewu zomwe timazala 2020 ndi zomwe tikukolora Panopa. Come 2025 mbewu zomwe tizazare ndizomwe tidzakolore zaka za kusogolo zikubwerazo. Ubwino wa Mulungu amavomereza chiganizo chomwe iwe mwini wapanga ndicholinga choti uzasowe ponamizira. Tiyeni nazoni.
Abalalitsa anthu okonda udf cause iwo omwe a Bakili Muluzi anankhala akulalikira kwa nthawi yaitali za kuipa kwa mcp lero sangatiuzenso za ubwino wa mcp awa never
Koma wina amalira ndi alomwe bwanji ndne waku Mangochi makukondan alomwe nonse all Lomwez live long love u from the moon to the back all alomwe
Alunena zoona ife a MCP ndi UDF ndi PP tili limodzi moti Atupele azakhara vice president
Koma bwanji tisafurumire kuwerudza chifukwa nthawi idakalipo.and Atcheya ndale sanayambe lero and onse omwe akupanga ndale panowa aziziwa ndi Atcheya ..and nkuru uja ndalama alinaxo choncho palibe wandale angawanyengere kuti apange gwilidzano ndi MCP.koti mukuganidza kuti imfa ya Shanil ija Atcheya akuigonera turo .😊
@@RaffickAllie Zikom komazo athu akudabwa ndichani apa tupere ananena kuti ali ndi mcp ananena woka kut ayenda woka ndiyeno pali mvutoso
@@JohnJohn-og8rt nkhani ndiyakuti .sakufuna kutapidwa kamwa mudakali mawa .akudziwa kuti .kungoyerekedxa kurankhura monyedza apasa Wallet arrest cholinga kumufoora .iye uja zorankhura alinaxo koma tidikire campaign...
@@JohnJohn-og8rt kumasintha kuja bwanji anatisegura maso
Ndizoona
Ndaitsika udf
Dpp my vote
Osanamapo apa. DPP loves using UDF to achieve their political goals. After Bakili muluzi spent his time, money and energy he was dumped like piece of s…..t. Apa DPP,MCP,UDF,UTM,PP,Aford aliyense ayime payekha then after failing to get 50+1 you can form concrete alliances. Ma alliances opanga nthawi zino ndi aja mukangowina mmayamba kuwaudza ena kuti mukanawinabe popanda iwowo. Komanso why should youthful leaders with energy and vision throw away their ambitions because of old failed leaders. Chakwera has failed and Muntharika analephera kale. We need to be moving forward and way from these failed politicians.
Hear his toung Mlomwe weni weni. Apostle ogwilira anatu. Mneneli onyenga Mphatso ya utumiki ulibe galu
Zoona Apostle Austin vuto pa Malawi anthu saziwa
Atupele muluzi Mai Ake ndiaku lilongwe musiyeni apite Ku MCP koma ife sitingavotere mcp
Komatu mwavutika. Kodi chisankho muwinira nkhani zolenga basi. Apostle for propaganda 😂😂😂
Komanso sikoyamba ,a Muluzi anapangapo m'gwilizano ndi MCP mu 2009
Muluzi ndiwa MCP,,😂😂 u are right bro😂
Atupele Muluzi alibe utsogoleli ,analuza u MP kusonyeza kuti ,alibe Chitukuko
Atupele sazalamulila malawi chifukwa ndimuthu opusa chisilu chomangomvela zilizose komaso iwe muluzi uzikula kod ndalama zonsezo uzanyamula kumanda
Sono nde mukunyozatu Ngati kuti zomwe akuyankhula gang'a wanuyi ziri ndi umboni 100%. Alomwe mukamanyoza Muluzi mmandimvesa chisoni komaso kusayamika kwanu kumawonekera poyera. Alomwe munali ndani Inu kupanda Muluzi? Si munali agalu akapolo achabechabe Inu? Ankakudziwani ndani anyapapi achabechabe Muluzi asanakufukuleni pamatope? Anthu munkachita manyazi even kutchula ntundu wanu. Osamangomuyamika Bakili bwanji
Chifukwa choti Atupele wanena kuti ayima payekha wabwela opanda Usogolele kodi mukutiona ngati ndife ana?
Nkhani yonvetsa chisoni, si paja ali pa mpando iye ankati MCP chipani chakupha? A Malawi akufyza CHITERZE, iye akuononha ndalama kugula anthu ndi kumakopera anthu anthuwo
Nanga mukufuna UDF ijoine chipani chopha ma albino cha DPP? Chosafunanso anthu akumpoto. UDF mdani wawo weni weni ndi DPP asaisekerere. It's payback time ife a UDF sitingalodzedwenso kuvotera ndi DPP
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤🙏
Izizi nzoona Bakili Muluzi ankayankhula yekha pa statement yake okumva anamva
Ndekutiso DPP yagula aford
Galu iwe paribe chomwe ungatiuze ife anthu akuluakulu,osalowelera udani wa anthu awiri bwanji iwe ukulowelela za udani wa anthu awiri??
Aliyese osapota DPP ndimulonwe Kodi?? This is nonsense aaaaa,,zamitunduzo tizisiye Kaye uko,coz mavuto tonse tikuvutikila limodzi,,enanu mungopanga pretend apa yet mwadya chitedze aaaaah tikhalire imeneyo ife😢
ATUPELE MULUZI Mutu wake sumayenda bwino 😂
Do not be bothered by Bakili Mluzi's actions. His speech at UDF convention revealed it. He was Kamuzu"s henchman. One could not just hold the post of SG in the MCP of Kamuzu. Bakili anali chief planner wakuponyera anthu kung'ona ndikupa anthu. During his time in MCP, he oversaw the death of Albert Muwalo, Gadama, Matenje, Focus Gwede, Sangala, Chisiza brothers and many others
Ine wa udf koma ine sinikuifuna mcp ndikufuna dpp mupita nokha Atupele kumeneko ku mcp kma mcp inagwa mbiri yoipa😂😢
Ineyo pandekha ndugwirizananazo zimenezoo,ndipo ndi Zoona,
Atupele uganizebwino Kumachingako anthu akufa ndinjala,mulibe chisoni zoona kugulisa anthu mwakonda ndalama mwandinyasa kwambili
Oh,ndiye kuti chipanicho tikusiyileni ndi chani aku Machinganu eti?,iwowo ndiofunika aphatikizane ndi zipani za ku m'mwera kuti anthu aku Machinga adye?,aMalawi ena alibe ntchito or atafa ndi njala?.Khala nachoni chipani chanu cha a Yao.
Nanga chair pano ndi Bakili?
Ameneo amcp Agula bakili muluzi ndi mwana wa abakili basi osati anthu oza vota ayi ozavota azasakha kuvotela dpp
Wagula muluzi okha osati ife a udf tipita ku dpp my vote
Satan iwe wabodza ukufaritsa bodza kamba kofuna kuti UDF isankhe kufuna kwako??
ndiinu muthu waboza kwambili
Atupere yo akamufunse Chilima, ngat MCP imasunga pangano
Kodi UDF idakalipobe?Munthu kuvotera UDF kumati ingawine?bola kutaya voteyo
Chisakho aliyese ndichake ,
Inu nde mwalandila kwandani ndalama kuti
Muwauze athu kuti asaza votele udf
Anyozeni azanu akudya ndalama
Amalawi kulubwa lubwa bas
Atupele walakwa UDF idzabvata chipani china
5b ndiyochepe
Bakili muluzi atupele ndi anthu adyera ndi mbuzi za anthu akufuna iwowo azilemela amalawi azivutika agalu a udf wosavotela ndipo atupele sazalamula dziko la malawi chifukwa ndi wadyera machende ake
Pamtumbo oako iwe wa Ku Tysolo iwe. Ahlomwe muli pa tchito galu iwe, without UDG mukanakhala ndani ? Kulira uku pamtumbo pako chaka chonse. Okupha Albino pamtumbo pako
Mlomwe ndiwe uli ndi mvuto. Bwanji mungomulola peter ndi dpp ingothandiza Atupeleyo ngati zukuwawani.
Kodi bwanji alomwe aliense amene sakuchita za DPP ndi mdani wao? Inu a DPP democracy mumaidziwa. Nthawi imene anthu amamenyera kuti kubwere democracy DPP ILIPO? Simudziwa democracy ndi chifukwa chake mungofuna kuti dziko lonse la Malawi likhale la DPP. SHAME ON YOU
Muluzi is Mcp guy shadow
Kupusa uneneli onama😮😊😅😅😅
Eya ndizoonad wakunva wanva osanva sazanvanso
Bali Muluzi si bambo wathu kuti angatitsogolele zochita ayi
Iwe khala buzy ndi maitanidwe Ako osati za ndalezi
Pano akuterera anyani okhaokha basi mabwana anasiya
Or ku votera udf or not sazasaukaso panyopako
Kodi Austin nthawi imene UDF inapanga mgwirizano ndi DPP inu munali musanabadwe? Ndafunsa chochifukwa UDF inapanga mgwirizano ndi DPP ili mboma bwanji siunadzuke kuti DPP yagula UDF? Iwe ingonena kuti zikundipweteka kuti mwina UDF ikhoza kupanga mgwirizano ndi MCP. Palibe zanzeru ukukamba apa. Iwe isiye UDF payokha iwenso uzipanga za DPP yakoyo
Austin ndiwe chitsilu Cha munthu kwambili
Iwe tupere nde mbuli zoona m,paka ku mcp eee bassi suzalamulanso kumalawi kuno ndiwe kape
ndipo sindikusapotanso
OLO ATAPITA KU CHIKANGAWA BOYS KO SANGAWINE ADZAWAVOTERA NDANI WAPITAKO NDI ATUPERE NDI BAMBO AKE ANTHU OWATSATIRA SANGAPANGE MANYAKA AMENEO
UDF sitilola kukhala munkhwapa mwa MCP or DPP sitikuifuna tipita tokha kumasakho win or lose
Ukunama m'bale
UDF tidalowa iwe usanabadwe galu wa munthu iwe ndiwe ndani iwe
Inuyo a dpp ndinu ana pandale…MCP inakuphumitsani Boma APM atalumbiritsidwa kale nde what makes u think mungawine pano muli kunja kwa boma?
Alomwe inu joke too much 😅
Koma mukamati simukulola kukhala munkhwapa ndizipani zina mukafika ulendo wanu chifukwa or kutsutsanso simaysutsa nao
Munthu amadananacho chilungamo
Ufulu wa Atupele ndi umenewo. VN yake yopanda mfundoyi.
Choka
Ife tidatuluka kale
JESUS IS ON THE THRONE
Mbewu zomwe timazala ndi zomwe timakolora... Mukudabwa chani? Mbewu zomwe timazala 2020 ndi zomwe tikukolora Panopa.
Come 2025 mbewu zomwe tizazare ndizomwe tidzakolore zaka za kusogolo zikubwerazo.
Ubwino wa Mulungu amavomereza chiganizo chomwe iwe mwini wapanga ndicholinga choti uzasowe ponamizira.
Tiyeni nazoni.
Stupid Apostle bwanji osangonena kuti ndiwe wa DPP bwanji??
Kupusa uneneli onama
Stupid wa DPP iwe ungolira lira Mesa iwe DPP ndimene inasokoneza UDF....alomwe oyipa inu wodzikonda.
Anthu amenewa ndi afiti, osayamika, asankho, ndi ozikonda osati masewera. Zikuwawawa za UDF kkkkk, amva bwino.
Mabodza mwakalamba inu
Uziti Aford ikuima ndi alomwe osati ikuimira aMalawi
Aford ilibe mojo(support)kumpoto. DPP is wasting its time
Muli ndi umboni wanji
Ndiye ngati alibe utsogolleri nanga nanga Atupele ukulimbana naye chofukwa chiyani . Leave Atupele alone.
Aaaa munthu angavotele ppp
Pepani kwambili
Agalu a Dpp anthu osowa khalidwe munatiphela chipani mbolizanu..
Ameneyu alibe fundo.
Kuyankhula kwa muluzi kunali kubwelesa umodzi monga malawi.
Komanso ameneyo wadya ndalama ku Dpp kut alimbane kunena za UDF.
Mmene tazuzikila ife a udf ndi Dpp. Chopangila ngwilizano sindikuchiwonanso
Iwetu ndi modzi mwa abuli.amenene sukuziwa kathu
Lather keep quiet.
🎉zoona Zikom uyu chisilu
Abalalitsa anthu okonda udf cause iwo omwe a Bakili Muluzi anankhala akulalikira kwa nthawi yaitali za kuipa kwa mcp lero sangatiuzenso za ubwino wa mcp awa never
Mudzachiona chikadzakula even achina kalindo anena zimenezi
Man bakili muluzi ndiwadyela Muthu amene amangosamala zake ndichifuka chipanichi chinatha kukonda ndalama
Vuto lawo apostle austin ndichani mmesa chipanichi ndichawo anayambitsa wokha
Zabodza😅😅😅
Zabodza akunenazi uneneli onama kufuna kinchuka
Don't bring your personal issues with Atupele and Bakili to all of us. Iwe ndi galu God will punish you for this lie mark my words
Ndiye udziunikile wekha Kodi DPP ndipaniso mwatisokonezakale inu
Ineyo pandekha ndugwirizananazo zimenezoo,ndipo ndi Zoona,