A Bakili Muluzi Agulitsa Chipani Chifukwa Cha Mtima Wadyera - Apostle Austin

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 8 окт 2024

Комментарии • 92

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani Час назад +1

    Koma wina amalira ndi alomwe bwanji ndne waku Mangochi makukondan alomwe nonse all Lomwez live long love u from the moon to the back all alomwe

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 2 часа назад +1

    Alunena zoona ife a MCP ndi UDF ndi PP tili limodzi moti Atupele azakhara vice president

  • @RaffickAllie
    @RaffickAllie 3 часа назад +2

    Koma bwanji tisafurumire kuwerudza chifukwa nthawi idakalipo.and Atcheya ndale sanayambe lero and onse omwe akupanga ndale panowa aziziwa ndi Atcheya ..and nkuru uja ndalama alinaxo choncho palibe wandale angawanyengere kuti apange gwilidzano ndi MCP.koti mukuganidza kuti imfa ya Shanil ija Atcheya akuigonera turo .😊

    • @JohnJohn-og8rt
      @JohnJohn-og8rt 2 часа назад

      @@RaffickAllie Zikom komazo athu akudabwa ndichani apa tupere ananena kuti ali ndi mcp ananena woka kut ayenda woka ndiyeno pali mvutoso

    • @RaffickAllie
      @RaffickAllie 2 часа назад

      @@JohnJohn-og8rt nkhani ndiyakuti .sakufuna kutapidwa kamwa mudakali mawa .akudziwa kuti .kungoyerekedxa kurankhura monyedza apasa Wallet arrest cholinga kumufoora .iye uja zorankhura alinaxo koma tidikire campaign...

    • @RaffickAllie
      @RaffickAllie 2 часа назад

      @@JohnJohn-og8rt kumasintha kuja bwanji anatisegura maso

    • @JumaKachala
      @JumaKachala Час назад

      Ndizoona

  • @Sofi-p1v
    @Sofi-p1v 2 часа назад +1

    Ndaitsika udf
    Dpp my vote

  • @driano763
    @driano763 Час назад

    Osanamapo apa. DPP loves using UDF to achieve their political goals. After Bakili muluzi spent his time, money and energy he was dumped like piece of s…..t. Apa DPP,MCP,UDF,UTM,PP,Aford aliyense ayime payekha then after failing to get 50+1 you can form concrete alliances. Ma alliances opanga nthawi zino ndi aja mukangowina mmayamba kuwaudza ena kuti mukanawinabe popanda iwowo. Komanso why should youthful leaders with energy and vision throw away their ambitions because of old failed leaders. Chakwera has failed and Muntharika analephera kale. We need to be moving forward and way from these failed politicians.

  • @TamUs-u2h
    @TamUs-u2h 32 минуты назад

    Hear his toung Mlomwe weni weni. Apostle ogwilira anatu. Mneneli onyenga Mphatso ya utumiki ulibe galu

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 2 часа назад

    Zoona Apostle Austin vuto pa Malawi anthu saziwa

  • @ziwani3682
    @ziwani3682 3 часа назад +3

    Atupele muluzi Mai Ake ndiaku lilongwe musiyeni apite Ku MCP koma ife sitingavotere mcp

  • @McDonaldMuyombe
    @McDonaldMuyombe 2 часа назад +1

    Komatu mwavutika. Kodi chisankho muwinira nkhani zolenga basi. Apostle for propaganda 😂😂😂

  • @ShillahLawrence
    @ShillahLawrence Час назад

    Komanso sikoyamba ,a Muluzi anapangapo m'gwilizano ndi MCP mu 2009

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 Час назад

    Muluzi ndiwa MCP,,😂😂 u are right bro😂

  • @ShillahLawrence
    @ShillahLawrence Час назад

    Atupele Muluzi alibe utsogoleli ,analuza u MP kusonyeza kuti ,alibe Chitukuko

  • @GoldenNamanguya-q9u
    @GoldenNamanguya-q9u 2 часа назад +1

    Atupele sazalamulila malawi chifukwa ndimuthu opusa chisilu chomangomvela zilizose komaso iwe muluzi uzikula kod ndalama zonsezo uzanyamula kumanda

    • @mauricechembe
      @mauricechembe Час назад

      Sono nde mukunyozatu Ngati kuti zomwe akuyankhula gang'a wanuyi ziri ndi umboni 100%. Alomwe mukamanyoza Muluzi mmandimvesa chisoni komaso kusayamika kwanu kumawonekera poyera. Alomwe munali ndani Inu kupanda Muluzi? Si munali agalu akapolo achabechabe Inu? Ankakudziwani ndani anyapapi achabechabe Muluzi asanakufukuleni pamatope? Anthu munkachita manyazi even kutchula ntundu wanu. Osamangomuyamika Bakili bwanji

  • @MACDONADLITIA
    @MACDONADLITIA 2 часа назад

    Chifukwa choti Atupele wanena kuti ayima payekha wabwela opanda Usogolele kodi mukutiona ngati ndife ana?

  • @EdwardSteven-t6h
    @EdwardSteven-t6h 2 часа назад

    Nkhani yonvetsa chisoni, si paja ali pa mpando iye ankati MCP chipani chakupha? A Malawi akufyza CHITERZE, iye akuononha ndalama kugula anthu ndi kumakopera anthu anthuwo

  • @PatrickChirwa-cv5cd
    @PatrickChirwa-cv5cd 52 минуты назад

    Nanga mukufuna UDF ijoine chipani chopha ma albino cha DPP? Chosafunanso anthu akumpoto. UDF mdani wawo weni weni ndi DPP asaisekerere. It's payback time ife a UDF sitingalodzedwenso kuvotera ndi DPP

  • @HamzaAyame-ch3et
    @HamzaAyame-ch3et 2 часа назад

    ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤🙏

  • @EvanceWame-v7v
    @EvanceWame-v7v 5 минут назад

    Izizi nzoona Bakili Muluzi ankayankhula yekha pa statement yake okumva anamva

  • @AdyanaAjidah
    @AdyanaAjidah 33 минуты назад

    Ndekutiso DPP yagula aford

  • @Adamuson
    @Adamuson Час назад

    Galu iwe paribe chomwe ungatiuze ife anthu akuluakulu,osalowelera udani wa anthu awiri bwanji iwe ukulowelela za udani wa anthu awiri??

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 Час назад

    Aliyese osapota DPP ndimulonwe Kodi?? This is nonsense aaaaa,,zamitunduzo tizisiye Kaye uko,coz mavuto tonse tikuvutikila limodzi,,enanu mungopanga pretend apa yet mwadya chitedze aaaaah tikhalire imeneyo ife😢

  • @NoohNowa
    @NoohNowa Час назад

    ATUPELE MULUZI Mutu wake sumayenda bwino 😂

  • @asahelmachila3026
    @asahelmachila3026 Час назад

    Do not be bothered by Bakili Mluzi's actions. His speech at UDF convention revealed it. He was Kamuzu"s henchman. One could not just hold the post of SG in the MCP of Kamuzu. Bakili anali chief planner wakuponyera anthu kung'ona ndikupa anthu. During his time in MCP, he oversaw the death of Albert Muwalo, Gadama, Matenje, Focus Gwede, Sangala, Chisiza brothers and many others

    • @MahometAli-e8w
      @MahometAli-e8w 8 минут назад

      Ine wa udf koma ine sinikuifuna mcp ndikufuna dpp mupita nokha Atupele kumeneko ku mcp kma mcp inagwa mbiri yoipa😂😢

  • @JohnWame-u3l
    @JohnWame-u3l Час назад

    Ineyo pandekha ndugwirizananazo zimenezoo,ndipo ndi Zoona,

  • @WitnessCharles-s7p
    @WitnessCharles-s7p 2 часа назад +1

    Atupele uganizebwino Kumachingako anthu akufa ndinjala,mulibe chisoni zoona kugulisa anthu mwakonda ndalama mwandinyasa kwambili

    • @Okalekale
      @Okalekale Час назад

      Oh,ndiye kuti chipanicho tikusiyileni ndi chani aku Machinganu eti?,iwowo ndiofunika aphatikizane ndi zipani za ku m'mwera kuti anthu aku Machinga adye?,aMalawi ena alibe ntchito or atafa ndi njala?.Khala nachoni chipani chanu cha a Yao.

  • @HenriqueFrancis-cv6zc
    @HenriqueFrancis-cv6zc 2 часа назад

    Nanga chair pano ndi Bakili?

  • @emilynthite6545
    @emilynthite6545 2 часа назад

    Ameneo amcp Agula bakili muluzi ndi mwana wa abakili basi osati anthu oza vota ayi ozavota azasakha kuvotela dpp

    • @MahometAli-e8w
      @MahometAli-e8w Минуту назад

      Wagula muluzi okha osati ife a udf tipita ku dpp my vote

  • @Adamuson
    @Adamuson 2 часа назад

    Satan iwe wabodza ukufaritsa bodza kamba kofuna kuti UDF isankhe kufuna kwako??

  • @RichardChitenje
    @RichardChitenje Час назад

    ndiinu muthu waboza kwambili

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 3 часа назад

    Atupere yo akamufunse Chilima, ngat MCP imasunga pangano

  • @ShillahLawrence
    @ShillahLawrence Час назад

    Kodi UDF idakalipobe?Munthu kuvotera UDF kumati ingawine?bola kutaya voteyo

  • @MustafaAjalu
    @MustafaAjalu 2 часа назад

    Chisakho aliyese ndichake ,
    Inu nde mwalandila kwandani ndalama kuti
    Muwauze athu kuti asaza votele udf
    Anyozeni azanu akudya ndalama
    Amalawi kulubwa lubwa bas

  • @AbdullnoorCassim
    @AbdullnoorCassim 2 часа назад

    Atupele walakwa UDF idzabvata chipani china

  • @WitnesAkimu
    @WitnesAkimu 6 минут назад

    5b ndiyochepe

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Час назад

    Bakili muluzi atupele ndi anthu adyera ndi mbuzi za anthu akufuna iwowo azilemela amalawi azivutika agalu a udf wosavotela ndipo atupele sazalamula dziko la malawi chifukwa ndi wadyera machende ake

  • @TamUs-u2h
    @TamUs-u2h 35 минут назад

    Pamtumbo oako iwe wa Ku Tysolo iwe. Ahlomwe muli pa tchito galu iwe, without UDG mukanakhala ndani ? Kulira uku pamtumbo pako chaka chonse. Okupha Albino pamtumbo pako

  • @stainbanda2424
    @stainbanda2424 3 часа назад

    Mlomwe ndiwe uli ndi mvuto. Bwanji mungomulola peter ndi dpp ingothandiza Atupeleyo ngati zukuwawani.

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 3 часа назад

    Kodi bwanji alomwe aliense amene sakuchita za DPP ndi mdani wao? Inu a DPP democracy mumaidziwa. Nthawi imene anthu amamenyera kuti kubwere democracy DPP ILIPO? Simudziwa democracy ndi chifukwa chake mungofuna kuti dziko lonse la Malawi likhale la DPP. SHAME ON YOU

  • @StevenFombe
    @StevenFombe 2 часа назад

    Muluzi is Mcp guy shadow

  • @MicahNjeleka
    @MicahNjeleka 2 часа назад

    Kupusa uneneli onama😮😊😅😅😅

  • @PeterMaulana-f4g
    @PeterMaulana-f4g 2 часа назад

    Eya ndizoonad wakunva wanva osanva sazanvanso

  • @ShillahLawrence
    @ShillahLawrence Час назад

    Bali Muluzi si bambo wathu kuti angatitsogolele zochita ayi

  • @mikesandali8425
    @mikesandali8425 2 часа назад

    Iwe khala buzy ndi maitanidwe Ako osati za ndalezi

  • @DaudBonomali
    @DaudBonomali 3 часа назад

    Pano akuterera anyani okhaokha basi mabwana anasiya

  • @ThembaShandu-m9m
    @ThembaShandu-m9m Час назад

    Or ku votera udf or not sazasaukaso panyopako

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 3 часа назад +1

    Kodi Austin nthawi imene UDF inapanga mgwirizano ndi DPP inu munali musanabadwe? Ndafunsa chochifukwa UDF inapanga mgwirizano ndi DPP ili mboma bwanji siunadzuke kuti DPP yagula UDF? Iwe ingonena kuti zikundipweteka kuti mwina UDF ikhoza kupanga mgwirizano ndi MCP. Palibe zanzeru ukukamba apa. Iwe isiye UDF payokha iwenso uzipanga za DPP yakoyo

    • @MCAnthonyNdau
      @MCAnthonyNdau 3 часа назад

      Austin ndiwe chitsilu Cha munthu kwambili

  • @AbdulazizWyson-dq3ce
    @AbdulazizWyson-dq3ce 2 часа назад

    Iwe tupere nde mbuli zoona m,paka ku mcp eee bassi suzalamulanso kumalawi kuno ndiwe kape
    ndipo sindikusapotanso

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 3 часа назад

    OLO ATAPITA KU CHIKANGAWA BOYS KO SANGAWINE ADZAWAVOTERA NDANI WAPITAKO NDI ATUPERE NDI BAMBO AKE ANTHU OWATSATIRA SANGAPANGE MANYAKA AMENEO

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 3 часа назад

    UDF sitilola kukhala munkhwapa mwa MCP or DPP sitikuifuna tipita tokha kumasakho win or lose

  • @KapoloWachitsanzo
    @KapoloWachitsanzo Час назад

    Ukunama m'bale

  • @Adamuson
    @Adamuson Час назад

    UDF tidalowa iwe usanabadwe galu wa munthu iwe ndiwe ndani iwe

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 Час назад

    Inuyo a dpp ndinu ana pandale…MCP inakuphumitsani Boma APM atalumbiritsidwa kale nde what makes u think mungawine pano muli kunja kwa boma?
    Alomwe inu joke too much 😅

  • @DaudBonomali
    @DaudBonomali 3 часа назад

    Koma mukamati simukulola kukhala munkhwapa ndizipani zina mukafika ulendo wanu chifukwa or kutsutsanso simaysutsa nao

  • @ChimwemweMathyola
    @ChimwemweMathyola 3 минуты назад

    Munthu amadananacho chilungamo

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 2 часа назад

    Ufulu wa Atupele ndi umenewo. VN yake yopanda mfundoyi.

  • @ConradccjSokoSoko
    @ConradccjSokoSoko 10 минут назад

    Choka

  • @ClementsKamanga
    @ClementsKamanga 3 часа назад

    Ife tidatuluka kale

  • @JenalaMsowoya
    @JenalaMsowoya Час назад

    JESUS IS ON THE THRONE
    Mbewu zomwe timazala ndi zomwe timakolora... Mukudabwa chani? Mbewu zomwe timazala 2020 ndi zomwe tikukolora Panopa.
    Come 2025 mbewu zomwe tizazare ndizomwe tidzakolore zaka za kusogolo zikubwerazo.
    Ubwino wa Mulungu amavomereza chiganizo chomwe iwe mwini wapanga ndicholinga choti uzasowe ponamizira.
    Tiyeni nazoni.

  • @Adamuson
    @Adamuson 2 часа назад

    Stupid Apostle bwanji osangonena kuti ndiwe wa DPP bwanji??

  • @MicahNjeleka
    @MicahNjeleka 2 часа назад

    Kupusa uneneli onama

  • @starneckkulemero7548
    @starneckkulemero7548 2 часа назад

    Stupid wa DPP iwe ungolira lira Mesa iwe DPP ndimene inasokoneza UDF....alomwe oyipa inu wodzikonda.

    • @tasmania527
      @tasmania527 Час назад

      Anthu amenewa ndi afiti, osayamika, asankho, ndi ozikonda osati masewera. Zikuwawawa za UDF kkkkk, amva bwino.

  • @johnkambala692
    @johnkambala692 3 часа назад

    Mabodza mwakalamba inu

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 3 часа назад

    Uziti Aford ikuima ndi alomwe osati ikuimira aMalawi

    • @tasmania527
      @tasmania527 Час назад

      Aford ilibe mojo(support)kumpoto. DPP is wasting its time

  • @ChiefJustin-l5p
    @ChiefJustin-l5p 3 часа назад

    Muli ndi umboni wanji

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 3 часа назад +1

    Ndiye ngati alibe utsogolleri nanga nanga Atupele ukulimbana naye chofukwa chiyani . Leave Atupele alone.

  • @ClementsKamanga
    @ClementsKamanga 3 часа назад

    Aaaa munthu angavotele ppp

  • @WonganiKatchale
    @WonganiKatchale 2 часа назад

    Pepani kwambili

  • @GiftJulius-ro9ev
    @GiftJulius-ro9ev 3 часа назад +1

    Agalu a Dpp anthu osowa khalidwe munatiphela chipani mbolizanu..

  • @RichardNsanama-m4q
    @RichardNsanama-m4q 3 часа назад +2

    Ameneyu alibe fundo.
    Kuyankhula kwa muluzi kunali kubwelesa umodzi monga malawi.
    Komanso ameneyo wadya ndalama ku Dpp kut alimbane kunena za UDF.
    Mmene tazuzikila ife a udf ndi Dpp. Chopangila ngwilizano sindikuchiwonanso

    • @MchachaGoodson
      @MchachaGoodson 3 часа назад

      Iwetu ndi modzi mwa abuli.amenene sukuziwa kathu
      Lather keep quiet.

    • @JohnJohn-og8rt
      @JohnJohn-og8rt 2 часа назад

      🎉zoona Zikom uyu chisilu

    • @Evelyn-q1o
      @Evelyn-q1o 2 часа назад

      Abalalitsa anthu okonda udf cause iwo omwe a Bakili Muluzi anankhala akulalikira kwa nthawi yaitali za kuipa kwa mcp lero sangatiuzenso za ubwino wa mcp awa never

    • @mercerblair4841
      @mercerblair4841 2 часа назад

      Mudzachiona chikadzakula even achina kalindo anena zimenezi

    • @GoldenNamanguya-q9u
      @GoldenNamanguya-q9u 2 часа назад

      Man bakili muluzi ndiwadyela Muthu amene amangosamala zake ndichifuka chipanichi chinatha kukonda ndalama

  • @abdulhameed7808
    @abdulhameed7808 2 часа назад +1

    Vuto lawo apostle austin ndichani mmesa chipanichi ndichawo anayambitsa wokha

  • @MicahNjeleka
    @MicahNjeleka 2 часа назад

    Zabodza😅😅😅

    • @MicahNjeleka
      @MicahNjeleka 2 часа назад

      Zabodza akunenazi uneneli onama kufuna kinchuka

  • @Adamuson
    @Adamuson Час назад

    Don't bring your personal issues with Atupele and Bakili to all of us. Iwe ndi galu God will punish you for this lie mark my words

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 3 часа назад

    Ndiye udziunikile wekha Kodi DPP ndipaniso mwatisokonezakale inu

  • @JohnWame-u3l
    @JohnWame-u3l Час назад

    Ineyo pandekha ndugwirizananazo zimenezoo,ndipo ndi Zoona,