A Malawi akuyenera kumpatsa Chakwera masiku osapitilira 10 kuti akhale atapereka lipoti ndipo akapanda kutero, mdziko muno mukuyenera kuchitika ma DEMO okakamiza Chakwera kuturutsa lipoti. Limpopo Fm yalengezanso kuti kuomberedwa kwa nsilikali ku Zomba barracks kuja idali plot yochokera kwa anyamsta a ku STATE HOUSE. DZIKOLI NDILANTHU A MALAWI. Tikulamulidwa ndi chipani cha magazi mudziko muno. Tipempgere kwambiri Ambuye atiturutse mu dziko lino la Farao.
Chakwera watchera kumwezi nkhanga zaona.iye amaona ngati ndiwochenjera koma apapa ndiye wapezeka.akufuna kumpasa deadline 10 days kuti amalawi awapasire report la ngozi ya ndege gulukunyinda ameneyo Dr chikangawa
Kukhala cheteko ndi chitsimikizo choti akudziwa po kanthu president wa dziko ndamene akanakhala oyambirira kutiero koma akuti asankha kukhala chete, nde anthu tingakhulupirile bwanji?
Give him time to meditate on that iissue.It's a very crucial bone of contention.However,he is here in the North accost him democratically to divulge what transpired.It is more than a grief to lose nine Malawians without knowing the apparent cause of the demise.
A Lazarus Chakwerawa akuzolowera pajatu za Sattar Gate iwowatu anali mugulu lomweelo lakubalo ndalama za a Malawi ; inatero utube channel .kuti iwo ndi nduna zao zonse ku parliament .anadya nao. Ndi Sattar yu Anapeza umbavau linali boma mdziko la Britain .koma iwowa anangomupana Saulos chilima yekha kuti chilima anali mbava .koma iwo ndi anzawo onse anadzibisa. Pano ndi apa akubisanso report ya ngozi ya ndege .report from German investigators ..😮😮😮 iwowa aulule nkhani zonse za Sattar Gate kuti anali involved ndi a ndani. Ndipo chilima amuoheranji pangozi ya ndege
Kukhala maiko ena president wa malawi' anthu akadakhala,ataiwala,zoti tidali ndi president ochedwa chakwela.koma, malawi' kaya tinaputsa, bwanji.taonani, anyamata ndi atsikana'aku Kenya Uganda Nigeria, koma kuno tingolidza konono koma kuziwa FB basi.kumangolongolola, kumeneko.
Good Message Dziwe TV
Wakupa ndiyemweyo chakwelayo awawudza andu bwanji 😭😭😭😭 mulungu akulanga Santana iwe
A Malawi akuyenera kumpatsa Chakwera masiku osapitilira 10 kuti akhale atapereka lipoti ndipo akapanda kutero, mdziko muno mukuyenera kuchitika ma DEMO okakamiza Chakwera kuturutsa lipoti.
Limpopo Fm yalengezanso kuti kuomberedwa kwa nsilikali ku Zomba barracks kuja idali plot yochokera kwa anyamsta a ku STATE HOUSE.
DZIKOLI NDILANTHU A MALAWI.
Tikulamulidwa ndi chipani cha magazi mudziko muno.
Tipempgere kwambiri Ambuye atiturutse mu dziko lino la Farao.
Apa ndiye mwadziwikatu mukubisilanji hehehe mwabisara mu kholowa 😂
Dr chikangawa ife musawone ngati tiliphee ngati tayiwala ife tikudikira iwe Dr chikangawa uwona zomwe zinameta chona mchira
Mmesa anapha chilima ndi emweyi machende ake
Chikangawayo akuyenera aturuse lipoti mwangu
UMENEO NDI UMBONI OTI ANAPHADI ANTHU CHAKWERA,UNBONIO NDI WAKE ALENGEZA BWANJI?
Eeeeish koma Malawi wafika potopetsa bodza mmm😅
Mr chikangawa ndiye anapha
Chakwera watchera kumwezi nkhanga zaona.iye amaona ngati ndiwochenjera koma apapa ndiye wapezeka.akufuna kumpasa deadline 10 days kuti amalawi awapasire report la ngozi ya ndege gulukunyinda ameneyo Dr chikangawa
akuziwapo kanthu
Chaka chake ndichino chakwera azimangilira ku tomato kamba kakupanika kkkkk
Good message
Okupha sangaziulule yekha pabwalo lamulandu ,
Chodziwika komanso mosachosela , Saulos Cláuds Chilima anachita kunyongedwa,aphelana udindo
boma la zigawenga zokha zokha atulutse lipoti akubisa chani iye ayaluka timudula mapwala chakwera chaka chake ndichino
Ife tikudikilatu chilungamo kwa iweyo chikangawa😢😢
Koma zingatheke wakupha udziulula kuti ndinedi .
Chikangawa chakwera kaya ngati angatiuze koma tili ufunadi ripoti
Ngati sangawerenge report lo basi apase mkulu wa asilikali awuluse report, mesa iyeyo akuchita mantha
Kkkk chikangawa akuziwa bwino lomwe yeyo
Ayakhe amenewo achikangawawo 😂😂😂😂
This is truth akuyenela kuti ayangule 😢
Kukhala cheteko ndi chitsimikizo choti akudziwa po kanthu president wa dziko ndamene akanakhala oyambirira kutiero koma akuti asankha kukhala chete, nde anthu tingakhulupirile bwanji?
😂😂😂 adalengeza bwanji ndege Itasowa?
Atulutse lipoti akubisa bwaniji pomwe ma Germany ananena,Lazaro akudziwapo kanthu kuti iyeyo ndiyemwe anapanga chiwembucho.black box ilikunyumba kwakeko
Samgatulutse mfiti mulumgu achite naye😮
Liwuzeni dziko chilungamo than kumangokhala chete
Inde ndizowona atuluse liport tilimve
Akusowa poyambira kuti anama motani, anapha yekha galu uyu.
Report ya imfa ya Bingu ,JB sanachedwetse Koma iyi ikuvuta pat?
Give him time to meditate on that iissue.It's a very crucial bone of contention.However,he is here in the North accost him democratically to divulge what transpired.It is more than a grief to lose nine Malawians without knowing the apparent cause of the demise.
Eni anthu anamwalira aja ndi apule amafunika ku pepesedwa ndani?
Awulula bwanji alipo malizasimo cnanga iwowo akuziwa kale 😂😂😂😂😂 alibisa cz chani asadandawule atiwuze basi amenewo asachedweso akubisa chani nanga 😂😂😂😂
Tsono ngakhale muwakakamize adzuka akufawo ?
Bro chakwera ndi munthu oipa kupha zake chifukwa cha 5 year's anzalowe wina kd mavoti achaka chamawa chakwera adzabela km kuti kuvotedwe bwino kutali dzangawine chifukwa moyo umene adaphanga pompha zache
Apasidwe 10 days imeneyo ngati sathero asiye undindo pasi munthu osakonda anthu ake
Ndipo ife tikudikila asakhale chete Amalawi akuyembekezera ndipo akuyenera kupita pa malo amene Chilima anafera
Report yofufuza wins amatulutsanso ndiwina.. umbuli eti mbuzi yamunthu ikufuna Report kwamunthu emwe sikumukhudza
Naye ndiufulu wake
Ayankhe abwanawo zaphinja pa khosi
anthu aku Israel Aja amakatani ku Malawi mr chikangawa plz report muzituluse nokha apa
Anthu awa sazatheka bodza lalowa mmagazi mwawo ndipo sakunda dziko lokhala lawo.
WE NEED A REPORT
Chakwera walikukoma chilima kwene nawe ufwenge no matter what you will go to dei , you will stay longer but the day is coming
zachison liport atulutse maina amene akumutchula mtsogoleli ife tikuchita manyazi monga amalawi lituluke basi
Report Silituluka chifukwa zinali zochita kukonza. Mwachidule achakwera ndiwo anakonza kuti ngoziyi ichitike.
Ngati akukana kupeleka report ndiyekuti akudziwapo kanthu koma akunama amati chouluka chimauluka koma sikulina chizatera
A Lazarus Chakwerawa akuzolowera pajatu za Sattar Gate iwowatu anali mugulu lomweelo lakubalo ndalama za a Malawi ; inatero utube channel .kuti iwo ndi nduna zao zonse ku parliament .anadya nao. Ndi Sattar yu Anapeza umbavau linali boma mdziko la Britain .koma iwowa anangomupana Saulos chilima yekha kuti chilima anali mbava .koma iwo ndi anzawo onse anadzibisa. Pano ndi apa akubisanso report ya ngozi ya ndege .report from German investigators ..😮😮😮 iwowa aulule nkhani zonse za Sattar Gate kuti anali involved ndi a ndani. Ndipo chilima amuoheranji pangozi ya ndege
Akubisilanji report, choncho anthu akamati chakwera akuziwapo kanthu ena ndikumakana
Kukhala maiko ena president wa malawi' anthu akadakhala,ataiwala,zoti tidali ndi president ochedwa chakwela.koma, malawi' kaya tinaputsa, bwanji.taonani, anyamata ndi atsikana'aku Kenya Uganda Nigeria, koma kuno tingolidza konono koma kuziwa FB basi.kumangolongolola, kumeneko.
Sangatulutse iwo Ali gulu lomwelo.
😢😢😢😢
Kodi akuopa chani kuwauza anthu kuti dzinakhala bwanji ifetu tikudikila kuti tinve
Nyawu yajala kwambili
Asakha kukhala chete bwanji
😢
Kodi ngt chikangawa satulusa report nde atulutse mndani
Apatse anthu ena atiuze...akudziwa kut ali mu report lomwelo
Mfiti ys munthu
Palibe kusankha kukhala chete akuthawa nkhani yopeleka report abwana mulimva kuwawa dziko
Naenso azapselera wamoyo
Manipulator... Silent killer.. chakwela inuso muzamwalila either you like it or not...
Report perekani a MCP mesa mukati ndingozi
Chakwela adapha chilima
Chakwela machende ako iwe mbolo yosadulayo big
Wakupha chakwera
Plani imeneyi sikuti bozalo sabwelanalo ayi
ayankhe wasankha chete ife sitikufuna ayankhe by force chimapha Dala
😂😂😂😂
Akabisa report ndiye kut akuzowapo kathu akanakhala kut sakuziwa kathu akadawulusa kale kale
Sikusinja
Mapwalaake chakwela
Mbolo yake Chakwera
Wakupha uyu
Too bad
A bamusi ndiye ndaniso asaaa MCP boma
Timadya ndenge ife zachamba eti
Uzaziona abale ako atachitilidwa chiwembu
Tikufuna zitukuko osati za ndenge zatikwana
Ndipo ife tikudikila asakhale chete Amalawi akuyembekezera ndipo akuyenera kupita pa malo amene Chilima anafera
Ndipo ife tikudikila asakhale chete Amalawi akuyembekezera ndipo akuyenera kupita pa malo amene Chilima anafera
Ndipo ife tikudikila asakhale chete Amalawi akuyembekezera ndipo akuyenera kupita pa malo amene Chilima anafera