Mmmm angawine Awa, support alibe ngati chinalephera chipan cha chilima ku wina iwe ndiwe ndani kandondocha ka chakwera iwe😮😮😮😮 unapha chilima, ukanapangitsa colour yako ya green not za anzako, kuchikamwa😮😮😮
HlS exllent professor Peter muthalika The president of the republic of MALAWl 🇲🇼🇲🇼🇲🇼 2025 to 2030 Chuluke wazipani koma zikoli likufunika professor basi .
Ku mulanje anathawako manganya ndipo last election anali pa 3rd position, pa 2 panali kondwani, pa 2 panali Damson Chilewani, 3 panali iyeyo ndipo pa 4 panali mayi oti anthu amamukondanso, and remember this is the same constituency yomwe Brown Mpinganjira anayimira
Chipani cha manganya, chinayamba 2012, chinazilala posowa support, this year, wafikanso pa ground to boost or to amplify chakwela movement, my appeal to my fellow malawians, don't be fooled again, he is up to no good, keep your eyes on the ball, rise Malawi rise!!!!!
Manganya alibe molalo ndi mwana wa chikangawa asakupuiseni ndichifukwa alibe plan ndi zake nakhumwa ndichifukwa al kupanga msalu dzofana ndi zipani zina koma akunama achepa nazo
Colour doesn't matter, what matters are the words, there's no UTM there, so what's long with you DPP and UTM people? Mukumuwopa Dr. Usi eti, vuto a DPP munayimisa nkhalamba and this time ayitchetcha mosavuta anyamatawa.
Manganya ndi chitsilu kwambili yudasi anamupeleka chilima
Kukubweraku aliyense akhala ndi chipani pakhomo pake😂😂😂😂😂
Lonseri ndi dyela
Kkkk
Ekezakitile😂
Zankutu bas mabi eni eni 😂😂😂😂😂zaziiii akakhuta mang'ina atinyasepo apa fotsekii
😂😂 chipani chazimai
😂😂😂😂😂 tchaiii ku malawi anthu aphana ndi ndale😂😂😂😂
Anthu akumulanje Mitu sikukwera koma ifeyo alomwe sitimapanga zimenezo 😂😂😂😂😂😂😂manganya ndi nakhumwa anthu amenewa khaya anachokera kuti khaya
Pepani si tonse
Uyuyu ndiwa Mcp akungofuna kuchepesa chiwelengelo Cha dpp ndi utm cholinga Mcp izaduse moyela
Hahaha manganya ndi iwe chitsilu aaaw😅😅
akufuna kt kummwera kukhale zipqni zambiri cholinga adulirane number ya anthu cholinga dpp izalephere
Mmmm angawine Awa, support alibe ngati chinalephera chipan cha chilima ku wina iwe ndiwe ndani kandondocha ka chakwera iwe😮😮😮😮 unapha chilima, ukanapangitsa colour yako ya green not za anzako, kuchikamwa😮😮😮
kkkkk awanso ndi a kape kwambiri,kukula mtima ngati ali ndi manyi pakhosi
Ndiye osabwera poyera ndichani kumazembera mumbali. Pawoka sangapange ndale ndizobvuta. Why sanapange green color ya odya zake alibe mulandu.
Tiyeni nazoni si amakuchememelelani mukamavina dance nde mukuona ngati mwafikapo kkkkkk or dzina la chipanicho kuchita kuwoneka kt saliyekha mulandu ulipo ndithu
Zangoyamba kuziwika kwa anthu SOPANO ZOMWE bwana a isi amaganiza koma akulu akulu achipani cha UTM anazitulukila kale kuti awa cholinga chawo kunali kusokoneza chipani. Apaso sanati ngati yudasi anazipachika yekha nawoso awa muwawona. Kuti Malawi aziwe kutidi awa anapeleka zawo uja
Manganya chipanichi sichanyuwani ayi anayambisa kale chilima asanafe manganya poyambilila anapanga ngwilizano chapani chake ndicha chilima
Wachita bwino kutuluka awasiire akaporowo ubwino uss sikaporo
Uyu ndi mpaka kwabasi odya zake colour inali ya green lero yasanduka red kkkkkk mbuzi yamunthu
Musiyeni usi Mesa anamuchotsa Ku UTM
wachita bwinotu mesa ku UTM anamuchosa nde vuto ndichani
Ithink usi is a genius
Ndipo better apite yenkha awina
Malawi akuonesta kuti chikondi chidatithawa dziko lochepa koma zipani mbweeeeee ine zimenezi zikundinyasa ndithu
Koma mulanje central mpaka zipani zitatu constituency ya anthu adyera
HlS exllent professor Peter muthalika
The president of the republic of MALAWl 🇲🇼🇲🇼🇲🇼 2025 to 2030
Chuluke wazipani koma zikoli likufunika professor basi .
Anthu akumulanje amitsala OKHA OKHA kunalitso pinganjila apa ali ku MCP nankhumwa MANGANYA otsewa a MCP agalu KWABASI
Chiikangawa Pali winanso
UTM iphangepo nkandu asumilleni manganya 👊👊👊
Malawi can be ashamed manganya akaputa yenkha ndipo antha kuwina uyu
Alliance y ujeni iyi , ndani sakudziwa.
BAMBO A SIKONO
AZIPITA KU ZIMBABWE AKAJOYINE ZANUPF
Tirinaye limozi not DPP
UYU NDI WAMISALA CHAKWERA AKUNGOMUGWIRITSA NTCHITO KOMA PALIBE ANGAMUSATILE ANTHU AKUFUNA KUNGOMUDYERA
Woyipa Zimbabwe ameneyu
I blame saulos chilima
Wapopa manganya ndi chikangawa anthu amene adzavotele manganya wa votela MCP
B13
Kusokoneza anthu apa kuli 50- 50.okalamba sadza siyanitsa po vota.
Okudya zake alibe mulandu ndiyakalekale ngakhale UTM isanayambe km nkhan ikhale ya colour chfkwa panthawiyo makaka ake anali a green
Usi ndi oopsya muvutika naye simu ati
Wazinva koko ma za zalama zaboma
Ku mulanje anathawako manganya ndipo last election anali pa 3rd position, pa 2 panali kondwani, pa 2 panali Damson Chilewani, 3 panali iyeyo ndipo pa 4 panali mayi oti anthu amamukondanso, and remember this is the same constituency yomwe Brown Mpinganjira anayimira
Mbuyache mayikolo usi watopa kuyamwa magazi amchipani chija choweta ng'ona , wachita bwino wayambisa chake ,,,,,
Kkkkkk ase umaniwaza
Chipani cha manganya, chinayamba 2012, chinazilala posowa support, this year, wafikanso pa ground to boost or to amplify chakwela movement, my appeal to my fellow malawians, don't be fooled again, he is up to no good, keep your eyes on the ball, rise Malawi rise!!!!!
Chipani cha azimayi chikupita ku alliance ya MCP
Jacob juma wakumalawi kkkkkk
Musholozi (Umshini wami)
Ku Malawi kwachuluka drama serious
Mmmmm koma kadziko kamalawi
Saulos chilima ndiye chitsilu kobasi Lazarous ndi one
Palibe wamupopa koma ndiwamisala
Mental box 2 ,Zomba
Manganya alibe molalo ndi mwana wa chikangawa asakupuiseni ndichifukwa alibe plan ndi zake nakhumwa ndichifukwa al kupanga msalu dzofana ndi zipani zina koma akunama achepa nazo
Kodi za odya zake alibe mlandu ndi za lero?
Azimayi atipwetekesa chifukwa chotengeka
Colour doesn't matter, what matters are the words, there's no UTM there, so what's long with you DPP and UTM people? Mukumuwopa Dr. Usi eti, vuto a DPP munayimisa nkhalamba and this time ayitchetcha mosavuta anyamatawa.
Kkkkk km eeeee 😂😂😂😂
Don't you know that he started Odya zake before joining UTM?
NDALE ZA UKAKA
Satana kwake ndi kupha,kuba nkuononga kusongonyeza ...alomwe mwatani kodi?
Ndigaru kwambili
Ndale Zaki Malawi 🇲🇼
Nkhumba iyi yandikwana bwanji
Sawina ameneyo akungotaya nthawi
Ndalama zukoma kudya
Takhala tikunena Kuti uyu ndi Traitor. Chikangawa kuyetsetsa Kuti UTM tithe basi. Wadya Bibi yake yomwe
Plan yake ndiyoti kachipani kakeko akalowe Nako mu mgwirizano ndi MCP cholinga Chakwera akamutenge ngati running mate
Watumidwa!
Mabvuto alipo
m c p yamupopa usi koma akunamakwambili
Zazii maiko usi alibe sogolo
Ndale it's dirty game sungazivese
wakhoza,atenge,masapota,a,utm
Waba zambiri ameneyo
Koma moyo uno
Kutha kwa dziko
Chakuvutani ndi chiyani aliyese ali ndi ufulu
Tiana ta chikagawa iti
kunja kuno kulidi anthu oipa ndaoners apapa
Kkkk
Akanakhala dolo akadayika makaka ake a green osati kutengera za Utm izi zikusonyeza kuti alibe Chikoka pandale
Anthu mmm! Akadapanga makaka a green bwezi mwati ndi MCP
Musiyeni Micheal naye ndi munthu
Omwe akuyenda ndi manganya ndi wa mcp afune asafune
Kamanganya ndikadolo
X
P
B
B13