Some laws in Malawi seem to be invalid. Is section 65 really abided in the parliament? It was only Hon.late JZU Tembo the political hero who validated this law.May his soul RIP
Mp ngati wakomedwa ndi ndalama za MCP achosedwe Basi coz amapanga zithu zoti lamulo lake akulidziwa tikudziwa kuti ma mp amenewo analandila ndalama zokwana 50 million kwacha
Kom DPP imayenera kungochimva ,,, osat kulimbananso
Amarawi akundikirira inua Dpp ooyeeee
Akuyenera kuchosedwa chifukwa akanafuna kulowa M C P akanalowa b4 chisankho chapita pamenepo akuputsitsa dziko
Some laws in Malawi seem to be invalid. Is section 65 really abided in the parliament? It was only Hon.late JZU Tembo the political hero who validated this law.May his soul RIP
Bola asasokoneza athu ena kupita nawo ku mcp please the must go the self not with others
Joyce chitsulo usakane ayi iweyo akupotoza adausi koma waila momwe timavutikilamu muja kuti uwine sorry uzatifuna
Achita bwino kuwachotsa, alondole mbuzi zizawo zija😂😂😂 Peter nd oganiza bho safuna zachibwana.
🎉ndiye muwina bwanji politics is the game of numbers ndinu mbuli yeti bwanji kuchotsa antu muluza chifukwa changondo mayambitsa ngondo ina
A choke
We don't need alyance
Again we need to change a better president
Dpp🤔💪💪😍😍apatu ndiyemwazukanotu
Akuyenera kuchotsedwa chifukwa athuwa Ari Madera achewa Komaso awonetsa zatsakho lá choramura ndilhera lamuro ligwire nchito basi
Washoke nadi
Achosedwe basi amenewo
Joyce chitsuro ndiwa mcp to be honest achoke kumene
asiyeni akakhale kuchipani chokuphacho osalimbana nawo dpp 2025 bomaaaaaaaaa
AChoke chifukwa tinawasangha kuzela chipani chomwe akutuluka, athu amenewo angosatila komwe azipeza chuma okha bas
DPP 2025 BOMA ❤❤❤❤
Aliyense azayime payekha akalephelana ndiye azizapanga zagwilizanozo
A DPP sazatheka osangokhalabwanji
Mukatha kuchotsa ma mp wo mudzuke mupange ZOKUPYA CHONDE PLEASE
Azivaya anthu akupha
Agalu mbava azipita ku mcp konko mbuzi
MUMUUZE CHAKWERA KUTI AWAPHE MWA LUSO MUJA ONSEO 4 NDI ADYELA GWILA TCHITO YAKO CHAKWERA AZIMISE
Malawi akuvutika koma Nkhani zikhale zokangana basi zazipani basi koma Malawi ee ee tikadali kuvutika
DPP ndi mbambande imadana ndiopepera zedi
Achoke apite. Kuchipani chokuphacho
Mp ngati wakomedwa ndi ndalama za MCP achosedwe Basi coz amapanga zithu zoti lamulo lake akulidziwa tikudziwa kuti ma mp amenewo analandila ndalama zokwana 50 million kwacha
Yakwiya ndi mizimu
achoke bass Mesa ampwanya lamolo
DPP INABWERA KUZAKHALA, APM FATHER OF MALAWI ❤❤❤❤
Mp opusa ife sitikuwafuna,azipita ku ng'onazo😂
Zopusa basi bwanji sanachosedwe pa u president mukulu wake atachoka ku udf
Dpp 2025 Bomaaaaa
Dpp ndi chipani chodzindikira
Koma mbuzi Zina DPP Ina bwera kudzakhala KO tsutsa visiyeni MCP tengani mp onse amenewo Komanso lamuro lija la two years lija MCP ikanaimitsa Kaye kumenekumso malamuro ankhwima 2025 kuli mbola
Akudziwa kuti ku mcp akaruza
Achoke apite. Kuchipani chokuphacho