Powerful talking from our beloved president, president for the poor always there for poor Malawian citizens the Dddddd Cccccc!!!!, proud of you always. May the good Lord continue to guide and protect you always 🔥🔥🔥🔥
Akuti apolice adzisilira mpunga WA Ana school koma ADC inuyo ndi wa wani long live a kalindo anya manyi achakwera achitsiru amenewo , nde bwino akalindo ineso maganizo amenewo nariwo kuti athu asavotere chauzika akalindo inuyo inuyo ambuye akudaritseni ife kwakwataine sitikupanga nawo zopusazo tikulira ife ku Ntcheu😢😢😢 koma God knows chakwera adzafa imfa yowawa
This two much guyz..koma kuli Mulungu amatha kumuchitsa munthu pa mpando ndikuthamangitsa kukamusiya ku ntchire..koma mmawelenga baibulo????? Inalipo mfumu ina imachita zimenezi koma ngati simusamala Mr president ndi nduna zanu mupalanura mkwiyo wa Yehova....take my note
Mr Bonnnnnnnnnnn kalindo DC big up kodi bwanji osayambisa madem bwanji kumalawiko galu ameneyo ife kuno atikwana kwambiri ndithu tiye nazo Mr bonnnnnn kalindo the DC
Timanva nanu kukoma nsaname🎉🎉 ndipo mau anu amatitothoza ifeo,ndiposo pa mpando wa upresident inuo mwafika kale bwana,zolembalemba zangosala tsiku loyikika bas
A kalindo tiyankhulileni ife tili nanu mcp ndi yoipadi ifeyo a malawi amenetili kuno ku Mozambique tili o khuzika ndi zomwe likuchita boma la a chakwela , ku vuula mchenga mpaka laicence zinachitikako kuti ? Keep it up a kalindo.
Iyayi na ya mchenga yokhayo boma likunena zoona chifukwa mchenga is in the group of minerals and any mineral is a government property which is minored through the government permission. Everywhere in the world illegal mining is prohibited citizens are allowed to collect sand ndi wilibala basi not with a thipa truck then you have to go face the law which is in the constitution every country.
Aborn kalindo nde mumatiziwisa nkhani zambili mumatiyimilira koma or mukuyankhula anthuwa palibe chomwe akuva bwanji kuti kupangike mademo poti apo akuwona ngati tikusangalala ndi ulamuliro wawoo kukufunika ma demo kuti Ave ngati mumene anapangila azathu ku Kenya lizaini sangapange popanda ma demo 😢
Apa nde chakwela akutitola kwambiri mulungu mumve kulilira kwa amalawife mupaka kugilitsa mutchenga uli wachilengendwe ayi zikomo magamuro anu chakwera adutsa muyetso mitsozi yanthu kuvutika kwanthu dzikhare pa panja lanu achakwera 🥲🥲 inu aboni kalindo keep it up kutiuza anthu opepelawa 🔥🔥🔥🔥
Koma boma ili lafika posauzana n'chenga umene akulesa wayamba kuvuula lero ameneyu galu kwabasi chakwera atimaliza tonse
Powerful talking from our beloved president, president for the poor always there for poor Malawian citizens the Dddddd Cccccc!!!!, proud of you always. May the good Lord continue to guide and protect you always 🔥🔥🔥🔥
Akuti apolice adzisilira mpunga WA Ana school koma ADC inuyo ndi wa wani long live a kalindo anya manyi achakwera achitsiru amenewo , nde bwino akalindo ineso maganizo amenewo nariwo kuti athu asavotere chauzika akalindo inuyo inuyo ambuye akudaritseni ife kwakwataine sitikupanga nawo zopusazo tikulira ife ku Ntcheu😢😢😢 koma God knows chakwera adzafa imfa yowawa
😂😂😂😂😂 DC ndiyakatundu zoona
Anatiloza ndi malemu chilima aise pomuchita follow achinyamata ife😢😢
Uku nde kung'alulatu 10,000% ayi zikomo ndithu💪💪💪💪💪💪💪
Big mulungu akudaliseni ndipo pitirizani kutiombola kuwachosa amalawi mw agaluwa a mcp
God bless you Mr DC you always stand for the poor this government of chakwala is useless ever
The Dc Bon Kalindo anthileni fire anthu osowa umunthuwa osanyengelera ayi
This two much guyz..koma kuli Mulungu amatha kumuchitsa munthu pa mpando ndikuthamangitsa kukamusiya ku ntchire..koma mmawelenga baibulo????? Inalipo mfumu ina imachita zimenezi koma ngati simusamala Mr president ndi nduna zanu mupalanura mkwiyo wa Yehova....take my note
Mr kalindo u are a hero, the opposition the very week, the opposition is in deep slumber,
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤go deeper mr kalindo you are the best ❤❤❤❤❤❤
Mr president the DC we love you and greetings from North London UK
Tell dem the dccccc!!! Never stop fighting for the poor innocent people we vote for purposes Mr born we are on ur side
Kalindo we are failing to thank you but only God will thank you
Koma Mulungu ngati kunali kufuna kwanu kuti munthu uyu awulawe u president ayi pafikapa ife anthu anu timveni kulira kwathu 😢, Ife anthu akumuzi kuti tigule sopo timadalira kuvuwula mchenga omwewo kuti tichape, onani pomwe zinthu zafikapa Yehova, ingobwerani muzaweruzepo dziko lanuli Ambuye
Booooon kalindooooo 🔥🔥
Mr Bonnnnnnnnnnn kalindo DC big up kodi bwanji osayambisa madem bwanji kumalawiko galu ameneyo ife kuno atikwana kwambiri ndithu tiye nazo Mr bonnnnnn kalindo the DC
Timanva nanu kukoma nsaname🎉🎉
ndipo mau anu amatitothoza ifeo,ndiposo pa mpando wa upresident inuo mwafika kale bwana,zolembalemba zangosala tsiku loyikika bas
It's the sikusinja Gwenembe song for me
Akubwila fodya wamagogo wakuzino uja,(maganga).
The DC 🔥🔥💕 Chakwera atule pansi udindo..., Palibe zoti asintheso ai.., tikumunyengelela uyuh.. _
Kung'alula big man,ife Angoni kuntcheu ndife oganiza kkkkk😂
Allowance ya manebbtatenga koma ndiyochepa kobasi....polingalira ndi mmene zinthu zakweleramu
Muli bwino koma Anthu Ena sakukhulupilira inuyo boss munatitenga kutisiya ku sewo inuyo munapita kunja nokha mukadya ndalama zatha lero mwabwera 😂😂😂😂😂😂
Our president more fire 🔥 Booooon kalindoooo 🔥 🙌
❤❤❤ ndimakunyadilani 👏👏
The dc our poor president in Malawi
Make mbuuu mwana mbuuuuu long live the DC
😂😂😂😂 ati kufuna kumangidwa!! Komadi ndiwe DC
A kalindo tiyankhulileni ife tili nanu mcp ndi yoipadi ifeyo a malawi amenetili kuno ku Mozambique tili o khuzika ndi zomwe likuchita boma la a chakwela , ku vuula mchenga mpaka laicence zinachitikako kuti ? Keep it up a kalindo.
Aaaah koma izizi ndiye chakwera wationjedza zedi ,koma chifukwa chani kweni kweni?
Khaaaaaa wafika the DC
And it's the song for me😂😂😂😂Winiko Ayi ndithu
ULEMU WANU MR, THE DC..... BON KALINDO 💪✊✊✊📡🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Boooon Kalindo , Pangolin mwana womvuta kwambiri
Kalindo 🎉🎉 iweyo ndi 1,,,ku Egypt kuja timadya kwabasi ❤❤
Tikufuna mademo bwana osamunyengerera Chakwera
Koma mpaka chenga mmmm mawonjeza
Mafuta ayamba kuchoka ku Mozambique kukafika ku area 50 ku Lilongwe kudzela pa njanje ai zikomo
Ife dzuro timadikira mademo, agalu amenewa atitopesa
Born kalindo more 🔥
😅😂ayi ziliko mpaka boma kugulitsa ntchenga😂😂😂😂
Kkkkkkk koma DC kkkkk gwenembe
Zoonadi mboni ndineyo nditachita ngoz ku Queens ndinalipira kut andithandize
Njira ya ld pokavota sitikavota nkhondo ichitike ichitike
The DC boooooon kalindoooooooo
Chakwera nkongo wamako ,mboli Yako ,machende ako ,alipwisi alitongo.
Kkkkkk
Uchitsilu ndiye umeneo
Sizidachitikepo
Kkkkk koma ndipo akavoteraa nda amawooo hiyaa mau Mr Bon
Akufuna kutimpha agalu amenewa.go deeper
Kkkk Boma amalawi kutifinya tiwona zinthu shop chaine chasala ndi maepute katoni okhaokha ndatawira kunnjenga ndiyemukulesa mukufuna kundipha chani mukandiphera kuzenje komweko 😮😮😮😮
Uyu ndi nyoooo kwa nyooo ulemu wanu aaaa mchenga athu anayambira kale za mchenga athu amadyera momo abale eishh sambi
MCP ikufuna kuzabela ma vote chifukwa sizidachitikepo ku voter without ID ngakhale kuno ku South Africa
Mmatha madhala madhala inu mungoyimila koma zikhala bwino
Kuswakuswa big osaopa😊
We only need solutions not only kulalika
Ambuye nditengeni
Mafumu aku ntcheu mtima wawo ukuwawa alibe dyera ndi mafumu odziwa kulira moyo wa munthu sizocheza
Following boss
Mulungu adalenda dothi osati Chakwera ai
Where are we going to make our hustle now😭😭😭 mpakana nchenga omweu tkatenge chilolezo? 🔥🔥🔥🔥🔥
Ndizisilu zaathu zathu ananyerapo chenga iyewo chakwera
Koma funso nkumati kuti,
Kodi Chakwela ndi Zikhale wacheyo, samachita manyazi konse akamamva izi? kapena umunthu wanu unatha??
The DC tell them shit
Mau awaa sikalindoo
The DC himself 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Umakwana booooon kalindo
Totally agree the dc
Ine nyimbo ndi zomwe zimandi waza koophya ati Sikusinja ndi Gwenembe amkaimba agogo awake DC popita ku Mzuzu akudutsa mu chikangawa 😂😂😂😂😂 DC makina 😂😂
Iyayi na ya mchenga yokhayo boma likunena zoona chifukwa mchenga is in the group of minerals and any mineral is a government property which is minored through the government permission. Everywhere in the world illegal mining is prohibited citizens are allowed to collect sand ndi wilibala basi not with a thipa truck then you have to go face the law which is in the constitution every country.
Koditu uku mcp kwangokula mbuzi za anthu
The Dc bon kalindo good Messnge
Anthu amene amabweresa Mbatata Ku nsika wa Limbe Ku chokers Ku Mulanje akuzunzidwa kwambiri akafika kuti asise a Police akuchosa misonkho akuti alakwa akalipire. K20 Pamene anthu akupangira mavuto mafuta anadula Palibe chomwe akupindula
Gwenembe ND sikisinje yemweyo 😂😂😂😂
😂😂😂 book la gwenembe kodi kkk
Ndipo zoonadi chonsecho sanapangile anthuwo chochita
😅😅😅😅kumalawi mkokoma ndithu bwanawa akutiposa zochita
Ng'alula DC
Sikusinja ndi Gwenembe😅😅😅😅😅😅😅 Nyengo yokhadxula kukhazula
Born kalindo more fire
Koma mkulu uyu kkkkkkkk sikusinja sikusinja kkk
Mr kalindo munafika aaaah kukanapezeka ambiri ngati inu bwezi dzikoli titaona zina aaaah
😂😂😂😂😂. Zosatheka sizidzatheka nanga chenga ndichani uyo wasala pang'no kt amfe ameneyo chisilu chamunthuyo muuze ambere Ku muloza border kuno aone kt angatile ife kuvuula chenga.
Osakhala presdent bwanji abon kalindo
Tayambitsani chipani cha amphawi
😂😂😂😂 azingomwadi ambuye mtengeni 😂😂😂😂😂
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥
🙌🙌🙌ay zikomo
Ing'alureni 🔥🔥
😂😂 Akalindo nyimboyo ndayikonda
Mpakana licence 😂😂😂😂😂🙌🙌🙌🙌 zili kumalawi nzatose akatenge licence ndi driver 😂😂😂😂
Big Bos DC mumakwa
Ati pedza madzi mu tikuvula chenga tikhapanamo
Sure
Aborn kalindo nde mumatiziwisa nkhani zambili mumatiyimilira koma or mukuyankhula anthuwa palibe chomwe akuva bwanji kuti kupangike mademo poti apo akuwona ngati tikusangalala ndi ulamuliro wawoo kukufunika ma demo kuti Ave ngati mumene anapangila azathu ku Kenya lizaini sangapange popanda ma demo 😢
Kalindo umatitsekula maso
The DC .....
Tiyambe mademo.... Ulemu wathapo apa
Zoona aliyense akavote opanda cha unzika basi nanga izizo nchilungamo
Ndipo live eeee a police eeee akuwo jeza
Zoona Born Kalindo auzeni ife tikuvutika kwambirii pa msewu kuno ku Kasungu chamama
Good
Koma m,chenga wa mulungu abale koma chakwela ambuye mutengeni watituza mokwanila mulungu mulangeni galu ameneu