BON KALINDO 11 JULY 2024 KUNG’ALURA PA THURSDAY

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 19 окт 2024

Комментарии • 223

  • @VungaQueen
    @VungaQueen 3 месяца назад +19

    Apa nde chakwela akutitola kwambiri mulungu mumve kulilira kwa amalawife mupaka kugilitsa mutchenga uli wachilengendwe ayi zikomo magamuro anu chakwera adutsa muyetso mitsozi yanthu kuvutika kwanthu dzikhare pa panja lanu achakwera 🥲🥲 inu aboni kalindo keep it up kutiuza anthu opepelawa 🔥🔥🔥🔥

    • @FRAVIOKUNSANJA
      @FRAVIOKUNSANJA 3 месяца назад

      Koma boma ili lafika posauzana n'chenga umene akulesa wayamba kuvuula lero ameneyu galu kwabasi chakwera atimaliza tonse

  • @StevieChikaonda
    @StevieChikaonda 3 месяца назад

    Uku nde kung'alulatu 10,000% ayi zikomo ndithu💪💪💪💪💪💪💪

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana 3 месяца назад +3

    Akuti apolice adzisilira mpunga WA Ana school koma ADC inuyo ndi wa wani long live a kalindo anya manyi achakwera achitsiru amenewo , nde bwino akalindo ineso maganizo amenewo nariwo kuti athu asavotere chauzika akalindo inuyo inuyo ambuye akudaritseni ife kwakwataine sitikupanga nawo zopusazo tikulira ife ku Ntcheu😢😢😢 koma God knows chakwera adzafa imfa yowawa

  • @lyiemax
    @lyiemax 3 месяца назад +2

    Powerful talking from our beloved president, president for the poor always there for poor Malawian citizens the Dddddd Cccccc!!!!, proud of you always. May the good Lord continue to guide and protect you always 🔥🔥🔥🔥

  • @JasperLloyd-m7o
    @JasperLloyd-m7o 3 месяца назад +4

    Anatiloza ndi malemu chilima aise pomuchita follow achinyamata ife😢😢

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 3 месяца назад

    God bless you Mr DC you always stand for the poor this government of chakwala is useless ever

  • @GoodsonDiwadiwa
    @GoodsonDiwadiwa 3 месяца назад +1

    The Dc Bon Kalindo anthileni fire anthu osowa umunthuwa osanyengelera ayi

  • @PempheroKasimongwa
    @PempheroKasimongwa 3 месяца назад

    Kalindo 🎉🎉 iweyo ndi 1,,,ku Egypt kuja timadya kwabasi ❤❤

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon 3 месяца назад

    Born kalindo more 🔥

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN 3 месяца назад

    Timanva nanu kukoma nsaname🎉🎉
    ndipo mau anu amatitothoza ifeo,ndiposo pa mpando wa upresident inuo mwafika kale bwana,zolembalemba zangosala tsiku loyikika bas

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 3 месяца назад

    Mr president the DC we love you and greetings from North London UK

  • @MoosaSame
    @MoosaSame 3 месяца назад

    Our president more fire 🔥 Booooon kalindoooo 🔥 🙌

  • @EmmanuelMpalagule
    @EmmanuelMpalagule 3 месяца назад

    Mr kalindo u are a hero, the opposition the very week, the opposition is in deep slumber,

  • @pacharokoloviko1694
    @pacharokoloviko1694 3 месяца назад

    😂😂😂😂 ati kufuna kumangidwa!! Komadi ndiwe DC

  • @chimwemwemasamba2880
    @chimwemwemasamba2880 3 месяца назад

    Allowance ya manebbtatenga koma ndiyochepa kobasi....polingalira ndi mmene zinthu zakweleramu

  • @NOORMTUMA
    @NOORMTUMA 3 месяца назад

    Mr Bonnnnnnnnnnn kalindo DC big up kodi bwanji osayambisa madem bwanji kumalawiko galu ameneyo ife kuno atikwana kwambiri ndithu tiye nazo Mr bonnnnnn kalindo the DC

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 3 месяца назад

    The DC 🔥🔥💕 Chakwera atule pansi udindo..., Palibe zoti asintheso ai.., tikumunyengelela uyuh.. _

  • @RashidSaid-lk6bb
    @RashidSaid-lk6bb 3 месяца назад

    MCP ikufuna kuzabela ma vote chifukwa sizidachitikepo ku voter without ID ngakhale kuno ku South Africa

  • @FisherAction
    @FisherAction 3 месяца назад +3

    Big mulungu akudaliseni ndipo pitirizani kutiombola kuwachosa amalawi mw agaluwa a mcp

  • @LovelyJapaneseMaples-xc2bc
    @LovelyJapaneseMaples-xc2bc 3 месяца назад

    Kuswakuswa big osaopa😊

  • @JabesAlfaiate-t4v
    @JabesAlfaiate-t4v 3 месяца назад

    A kalindo tiyankhulileni ife tili nanu mcp ndi yoipadi ifeyo a malawi amenetili kuno ku Mozambique tili o khuzika ndi zomwe likuchita boma la a chakwela , ku vuula mchenga mpaka laicence zinachitikako kuti ? Keep it up a kalindo.

  • @mbewemisoyaanenenji1908
    @mbewemisoyaanenenji1908 3 месяца назад

    Boooon Kalindo , Pangolin mwana womvuta kwambiri

  • @GamaGama-z8p
    @GamaGama-z8p 3 месяца назад

    Tell dem the dccccc!!! Never stop fighting for the poor innocent people we vote for purposes Mr born we are on ur side

  • @vitumbikokamanga5869
    @vitumbikokamanga5869 3 месяца назад +1

    ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤go deeper mr kalindo you are the best ❤❤❤❤❤❤

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya 3 месяца назад +1

    Koma Mulungu ngati kunali kufuna kwanu kuti munthu uyu awulawe u president ayi pafikapa ife anthu anu timveni kulira kwathu 😢, Ife anthu akumuzi kuti tigule sopo timadalira kuvuwula mchenga omwewo kuti tichape, onani pomwe zinthu zafikapa Yehova, ingobwerani muzaweruzepo dziko lanuli Ambuye

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np 3 месяца назад +2

    This two much guyz..koma kuli Mulungu amatha kumuchitsa munthu pa mpando ndikuthamangitsa kukamusiya ku ntchire..koma mmawelenga baibulo????? Inalipo mfumu ina imachita zimenezi koma ngati simusamala Mr president ndi nduna zanu mupalanura mkwiyo wa Yehova....take my note

  • @MussahNamalomba-e3p
    @MussahNamalomba-e3p 3 месяца назад

    Khaaaaaa wafika the DC

  • @Sugerman-tw4do
    @Sugerman-tw4do 3 месяца назад

    Big Bos DC mumakwa

  • @RashidSaid-lk6bb
    @RashidSaid-lk6bb 3 месяца назад

    Uchitsilu ndiye umeneo
    Sizidachitikepo

  • @JaxyKumwenda
    @JaxyKumwenda 3 месяца назад

    Tikufuna mademo bwana osamunyengerera Chakwera

  • @limbanimtitima9170
    @limbanimtitima9170 3 месяца назад +1

    Kung'alula big man,ife Angoni kuntcheu ndife oganiza kkkkk😂

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju 3 месяца назад

    Make mbuuu mwana mbuuuuu long live the DC

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 3 месяца назад +1

    Muli bwino koma Anthu Ena sakukhulupilira inuyo boss munatitenga kutisiya ku sewo inuyo munapita kunja nokha mukadya ndalama zatha lero mwabwera 😂😂😂😂😂😂

  • @FelixMwango-f2y
    @FelixMwango-f2y 3 месяца назад

    Ing'alureni 🔥🔥

  • @OmegaNjati
    @OmegaNjati 3 месяца назад

    Ambuye nditengeni

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope 3 месяца назад +1

    Kalindo we are failing to thank you but only God will thank you

  • @MouriceChimkondo
    @MouriceChimkondo 3 месяца назад

    Following boss

  • @OsmanBakali-s5x
    @OsmanBakali-s5x 3 месяца назад

    Where are we going to make our hustle now😭😭😭 mpakana nchenga omweu tkatenge chilolezo? 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge 3 месяца назад

    ULEMU WANU MR, THE DC..... BON KALINDO 💪✊✊✊📡🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @loycemmadi9303
    @loycemmadi9303 3 месяца назад

    And it's the song for me😂😂😂😂Winiko Ayi ndithu

  • @PatricaTchuwa
    @PatricaTchuwa 3 месяца назад

    Ife dzuro timadikira mademo, agalu amenewa atitopesa

  • @Alice-z7t4z
    @Alice-z7t4z 3 месяца назад

    Mpakana licence 😂😂😂😂😂🙌🙌🙌🙌 zili kumalawi nzatose akatenge licence ndi driver 😂😂😂😂

  • @texonkautera
    @texonkautera 3 месяца назад

    Anthu amene amabweresa Mbatata Ku nsika wa Limbe Ku chokers Ku Mulanje akuzunzidwa kwambiri akafika kuti asise a Police akuchosa misonkho akuti alakwa akalipire. K20 Pamene anthu akupangira mavuto mafuta anadula Palibe chomwe akupindula

  • @AudettaYohanie-fl3oc
    @AudettaYohanie-fl3oc 3 месяца назад +1

    Aaaah koma izizi ndiye chakwera wationjedza zedi ,koma chifukwa chani kweni kweni?

  • @loycemmadi9303
    @loycemmadi9303 3 месяца назад

    Mr kalindo munafika aaaah kukanapezeka ambiri ngati inu bwezi dzikoli titaona zina aaaah

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi 3 месяца назад

    Kkkk Boma amalawi kutifinya tiwona zinthu shop chaine chasala ndi maepute katoni okhaokha ndatawira kunnjenga ndiyemukulesa mukufuna kundipha chani mukandiphera kuzenje komweko 😮😮😮😮

  • @annamazingashaibuh6276
    @annamazingashaibuh6276 3 месяца назад

    Kkkkk koma ndipo akavoteraa nda amawooo hiyaa mau Mr Bon

  • @RidwanAdam-nq6lz
    @RidwanAdam-nq6lz 3 месяца назад +2

    Booooon kalindooooo 🔥🔥

  • @dinahmunthali5324
    @dinahmunthali5324 3 месяца назад

    Ine nyimbo ndi zomwe zimandi waza koophya ati Sikusinja ndi Gwenembe amkaimba agogo awake DC popita ku Mzuzu akudutsa mu chikangawa 😂😂😂😂😂 DC makina 😂😂

  • @IvieMwabile
    @IvieMwabile 3 месяца назад

    Akufuna kutimpha agalu amenewa.go deeper

  • @HannockMesiwni
    @HannockMesiwni 3 месяца назад

    Njira ya ld pokavota sitikavota nkhondo ichitike ichitike

  • @JEFFERYJUMA
    @JEFFERYJUMA 3 месяца назад +1

    The dc our poor president in Malawi

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo 3 месяца назад

    Ng'alula DC

  • @kelvinmphande3754
    @kelvinmphande3754 3 месяца назад +1

    It's the sikusinja Gwenembe song for me

  • @EsnartGirivin
    @EsnartGirivin 3 месяца назад

    Osakhala presdent bwanji abon kalindo
    Tayambitsani chipani cha amphawi

  • @BatsonKadzuwa-tl3rp
    @BatsonKadzuwa-tl3rp 3 месяца назад

    Zoonadi mboni ndineyo nditachita ngoz ku Queens ndinalipira kut andithandize

  • @duncainjimmy
    @duncainjimmy 3 месяца назад

    Mulungu adalenda dothi osati Chakwera ai

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 3 месяца назад

    Ndizisilu zaathu zathu ananyerapo chenga iyewo chakwera

  • @IsraelMtawali
    @IsraelMtawali 3 месяца назад

    Chakwera is apus must go

  • @ChondezVick
    @ChondezVick 3 месяца назад

    The DC himself 🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @densonchiwaya8439
    @densonchiwaya8439 3 месяца назад

    Mau awaa sikalindoo

  • @christophermukaka7403
    @christophermukaka7403 3 месяца назад

    Kalindo ndisaname mukuwatsegula anthu koma bvuto opposition ili weak

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 3 месяца назад +1

    Koma mpaka chenga mmmm mawonjeza

  • @MussaNgoma-r2k
    @MussaNgoma-r2k 3 месяца назад

    We only need solutions not only kulalika

  • @PeterMsukwa-i1n
    @PeterMsukwa-i1n 3 месяца назад

    Gwenembe ND sikisinje yemweyo 😂😂😂😂

  • @KnowledgecGodwin-xo4pw
    @KnowledgecGodwin-xo4pw 3 месяца назад

    Mumatimilira mr president

  • @MartinsKhumalo
    @MartinsKhumalo 3 месяца назад

    ❤❤❤ ndimakunyadilani 👏👏

  • @WitnessPhiri-zr9uf
    @WitnessPhiri-zr9uf 3 месяца назад

    Aborn kalindo nde mumatiziwisa nkhani zambili mumatiyimilira koma or mukuyankhula anthuwa palibe chomwe akuva bwanji kuti kupangike mademo poti apo akuwona ngati tikusangalala ndi ulamuliro wawoo kukufunika ma demo kuti Ave ngati mumene anapangila azathu ku Kenya lizaini sangapange popanda ma demo 😢

  • @SteveKanongwa
    @SteveKanongwa 3 месяца назад

    A born kalindo mukadikira opposition kuti itisogolere tichedwa inuo tayambisani ife tili mbuyomo

  • @HawardStainly
    @HawardStainly 3 месяца назад

    Akubwila fodya wamagogo wakuzino uja,(maganga).

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju 3 месяца назад

    Sikusinja ndi Gwenembe😅😅😅😅😅😅😅 Nyengo yokhadxula kukhazula

  • @TutuAlfred-y2l
    @TutuAlfred-y2l 3 месяца назад

    😂😂😂😂😂. Zosatheka sizidzatheka nanga chenga ndichani uyo wasala pang'no kt amfe ameneyo chisilu chamunthuyo muuze ambere Ku muloza border kuno aone kt angatile ife kuvuula chenga.

  • @JozzyNthinda
    @JozzyNthinda 3 месяца назад

    Unabwela kumalawi amenyelen. Nkhondo anthu asauka

  • @annamazingashaibuh6276
    @annamazingashaibuh6276 3 месяца назад

    Uyu ndi nyoooo kwa nyooo ulemu wanu aaaa mchenga athu anayambira kale za mchenga athu amadyera momo abale eishh sambi

  • @EdwardZuze-r7w
    @EdwardZuze-r7w 3 месяца назад

    Koma funso nkumati kuti,
    Kodi Chakwela ndi Zikhale wacheyo, samachita manyazi konse akamamva izi? kapena umunthu wanu unatha??
    The DC tell them shit

  • @zayedmitawa8345
    @zayedmitawa8345 3 месяца назад

    Kodi a Pule alibe olo foni ya mmanja kuti azitha kuona zomwe anthu akukamba online incase samadziwa zomwe nduna zake zikugwilira ntchito.What kind of leadership is this.

  • @OmegaChingamuka
    @OmegaChingamuka 3 месяца назад

    Ndipo zoonadi chonsecho sanapangile anthuwo chochita

  • @stanfordnsona
    @stanfordnsona 3 месяца назад

    Kalindo umatitsekula maso

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg 3 месяца назад

    😂😂😂😂😂😂😂 DC mkango wapamalawi timenyereni nkhondoyi koma chakwera ameneyi mpaka awaletse anthu kuuvula mchenga zoona

  • @happychimwemwe-1805
    @happychimwemwe-1805 3 месяца назад +1

    Umakwana booooon kalindo

  • @OmegaChingamuka
    @OmegaChingamuka 3 месяца назад

    Mafumu aku ntcheu mtima wawo ukuwawa alibe dyera ndi mafumu odziwa kulira moyo wa munthu sizocheza

  • @ZainuluNsalule
    @ZainuluNsalule 3 месяца назад

    Good

  • @MikeMsosama
    @MikeMsosama 3 месяца назад

    Totally agree the dc

  • @jameskamanga628
    @jameskamanga628 3 месяца назад

    Koma mkulu uyu kkkkkkkk sikusinja sikusinja kkk

  • @GeorgeMphale-n8q
    @GeorgeMphale-n8q 3 месяца назад +1

    Mafuta ayamba kuchoka ku Mozambique kukafika ku area 50 ku Lilongwe kudzela pa njanje ai zikomo

  • @KnowledgecGodwin-xo4pw
    @KnowledgecGodwin-xo4pw 3 месяца назад +2

    Chakwera nkongo wamako ,mboli Yako ,machende ako ,alipwisi alitongo.

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn 3 месяца назад

    We are in a Failed State and Chakwera uyuu achoke

  • @Vascomw
    @Vascomw 3 месяца назад

    Ndipo live eeee a police eeee akuwo jeza

  • @jamesgama5489
    @jamesgama5489 3 месяца назад

    Koma inuu!! Ayi zikomo.

  • @azunguauskay4903
    @azunguauskay4903 3 месяца назад

    😂😂 Akalindo nyimboyo ndayikonda

  • @RafickRaj
    @RafickRaj 3 месяца назад

    Mmatha madhala madhala inu mungoyimila koma zikhala bwino

  • @DeanMakawa
    @DeanMakawa 3 месяца назад

    Kalindo usatitopese machende yako

  • @JamesKambale-s2c
    @JamesKambale-s2c 3 месяца назад

    Koditu uku mcp kwangokula mbuzi za anthu

  • @RadsonTimoteo
    @RadsonTimoteo 3 месяца назад

    Zoona aliyense akavote opanda cha unzika basi nanga izizo nchilungamo

  • @LamseyChimah
    @LamseyChimah 3 месяца назад

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 3 месяца назад

    Malawi belongs to Malawians and not Chakwera with his incapacitated cabinet

  • @chipilirokalison1334
    @chipilirokalison1334 3 месяца назад

    Denkha Born mulungu azikudalisani koma opposition yadekha ndicholinga usadande iwe mulungu azikudalisa

  • @InnocentBanda-g6i
    @InnocentBanda-g6i 3 месяца назад

    ❤❤

  • @SimonMtonga-kf5ht
    @SimonMtonga-kf5ht 3 месяца назад

    Born kalindo more fire

  • @MoosaChirwa
    @MoosaChirwa 3 месяца назад

    😂😂😂😂😂passport ya fake ya mwana we president❤❤❤