Akuti apolice adzisilira mpunga WA Ana school koma ADC inuyo ndi wa wani long live a kalindo anya manyi achakwera achitsiru amenewo , nde bwino akalindo ineso maganizo amenewo nariwo kuti athu asavotere chauzika akalindo inuyo inuyo ambuye akudaritseni ife kwakwataine sitikupanga nawo zopusazo tikulira ife ku Ntcheu😢😢😢 koma God knows chakwera adzafa imfa yowawa
Powerful talking from our beloved president, president for the poor always there for poor Malawian citizens the Dddddd Cccccc!!!!, proud of you always. May the good Lord continue to guide and protect you always 🔥🔥🔥🔥
Timanva nanu kukoma nsaname🎉🎉 ndipo mau anu amatitothoza ifeo,ndiposo pa mpando wa upresident inuo mwafika kale bwana,zolembalemba zangosala tsiku loyikika bas
Mr Bonnnnnnnnnnn kalindo DC big up kodi bwanji osayambisa madem bwanji kumalawiko galu ameneyo ife kuno atikwana kwambiri ndithu tiye nazo Mr bonnnnnn kalindo the DC
A kalindo tiyankhulileni ife tili nanu mcp ndi yoipadi ifeyo a malawi amenetili kuno ku Mozambique tili o khuzika ndi zomwe likuchita boma la a chakwela , ku vuula mchenga mpaka laicence zinachitikako kuti ? Keep it up a kalindo.
This two much guyz..koma kuli Mulungu amatha kumuchitsa munthu pa mpando ndikuthamangitsa kukamusiya ku ntchire..koma mmawelenga baibulo????? Inalipo mfumu ina imachita zimenezi koma ngati simusamala Mr president ndi nduna zanu mupalanura mkwiyo wa Yehova....take my note
Aborn kalindo nde mumatiziwisa nkhani zambili mumatiyimilira koma or mukuyankhula anthuwa palibe chomwe akuva bwanji kuti kupangike mademo poti apo akuwona ngati tikusangalala ndi ulamuliro wawoo kukufunika ma demo kuti Ave ngati mumene anapangila azathu ku Kenya lizaini sangapange popanda ma demo 😢
Apa nde chakwela akutitola kwambiri mulungu mumve kulilira kwa amalawife mupaka kugilitsa mutchenga uli wachilengendwe ayi zikomo magamuro anu chakwera adutsa muyetso mitsozi yanthu kuvutika kwanthu dzikhare pa panja lanu achakwera 🥲🥲 inu aboni kalindo keep it up kutiuza anthu opepelawa 🔥🔥🔥🔥
Koma boma ili lafika posauzana n'chenga umene akulesa wayamba kuvuula lero ameneyu galu kwabasi chakwera atimaliza tonse
Uku nde kung'alulatu 10,000% ayi zikomo ndithu💪💪💪💪💪💪💪
Akuti apolice adzisilira mpunga WA Ana school koma ADC inuyo ndi wa wani long live a kalindo anya manyi achakwera achitsiru amenewo , nde bwino akalindo ineso maganizo amenewo nariwo kuti athu asavotere chauzika akalindo inuyo inuyo ambuye akudaritseni ife kwakwataine sitikupanga nawo zopusazo tikulira ife ku Ntcheu😢😢😢 koma God knows chakwera adzafa imfa yowawa
😂😂😂😂😂 DC ndiyakatundu zoona
Powerful talking from our beloved president, president for the poor always there for poor Malawian citizens the Dddddd Cccccc!!!!, proud of you always. May the good Lord continue to guide and protect you always 🔥🔥🔥🔥
Anatiloza ndi malemu chilima aise pomuchita follow achinyamata ife😢😢
God bless you Mr DC you always stand for the poor this government of chakwala is useless ever
The Dc Bon Kalindo anthileni fire anthu osowa umunthuwa osanyengelera ayi
Kalindo 🎉🎉 iweyo ndi 1,,,ku Egypt kuja timadya kwabasi ❤❤
Born kalindo more 🔥
Timanva nanu kukoma nsaname🎉🎉
ndipo mau anu amatitothoza ifeo,ndiposo pa mpando wa upresident inuo mwafika kale bwana,zolembalemba zangosala tsiku loyikika bas
Mr president the DC we love you and greetings from North London UK
Our president more fire 🔥 Booooon kalindoooo 🔥 🙌
Mr kalindo u are a hero, the opposition the very week, the opposition is in deep slumber,
😂😂😂😂 ati kufuna kumangidwa!! Komadi ndiwe DC
Allowance ya manebbtatenga koma ndiyochepa kobasi....polingalira ndi mmene zinthu zakweleramu
Mr Bonnnnnnnnnnn kalindo DC big up kodi bwanji osayambisa madem bwanji kumalawiko galu ameneyo ife kuno atikwana kwambiri ndithu tiye nazo Mr bonnnnnn kalindo the DC
The DC 🔥🔥💕 Chakwera atule pansi udindo..., Palibe zoti asintheso ai.., tikumunyengelela uyuh.. _
MCP ikufuna kuzabela ma vote chifukwa sizidachitikepo ku voter without ID ngakhale kuno ku South Africa
Big mulungu akudaliseni ndipo pitirizani kutiombola kuwachosa amalawi mw agaluwa a mcp
Kuswakuswa big osaopa😊
A kalindo tiyankhulileni ife tili nanu mcp ndi yoipadi ifeyo a malawi amenetili kuno ku Mozambique tili o khuzika ndi zomwe likuchita boma la a chakwela , ku vuula mchenga mpaka laicence zinachitikako kuti ? Keep it up a kalindo.
Boooon Kalindo , Pangolin mwana womvuta kwambiri
Tell dem the dccccc!!! Never stop fighting for the poor innocent people we vote for purposes Mr born we are on ur side
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤go deeper mr kalindo you are the best ❤❤❤❤❤❤
Koma Mulungu ngati kunali kufuna kwanu kuti munthu uyu awulawe u president ayi pafikapa ife anthu anu timveni kulira kwathu 😢, Ife anthu akumuzi kuti tigule sopo timadalira kuvuwula mchenga omwewo kuti tichape, onani pomwe zinthu zafikapa Yehova, ingobwerani muzaweruzepo dziko lanuli Ambuye
This two much guyz..koma kuli Mulungu amatha kumuchitsa munthu pa mpando ndikuthamangitsa kukamusiya ku ntchire..koma mmawelenga baibulo????? Inalipo mfumu ina imachita zimenezi koma ngati simusamala Mr president ndi nduna zanu mupalanura mkwiyo wa Yehova....take my note
Khaaaaaa wafika the DC
Big Bos DC mumakwa
Uchitsilu ndiye umeneo
Sizidachitikepo
Tikufuna mademo bwana osamunyengerera Chakwera
Kung'alula big man,ife Angoni kuntcheu ndife oganiza kkkkk😂
Make mbuuu mwana mbuuuuu long live the DC
Muli bwino koma Anthu Ena sakukhulupilira inuyo boss munatitenga kutisiya ku sewo inuyo munapita kunja nokha mukadya ndalama zatha lero mwabwera 😂😂😂😂😂😂
Ing'alureni 🔥🔥
Ambuye nditengeni
Kalindo we are failing to thank you but only God will thank you
Following boss
Where are we going to make our hustle now😭😭😭 mpakana nchenga omweu tkatenge chilolezo? 🔥🔥🔥🔥🔥
ULEMU WANU MR, THE DC..... BON KALINDO 💪✊✊✊📡🔥🔥🔥🔥🔥🔥
And it's the song for me😂😂😂😂Winiko Ayi ndithu
Ife dzuro timadikira mademo, agalu amenewa atitopesa
Mpakana licence 😂😂😂😂😂🙌🙌🙌🙌 zili kumalawi nzatose akatenge licence ndi driver 😂😂😂😂
Anthu amene amabweresa Mbatata Ku nsika wa Limbe Ku chokers Ku Mulanje akuzunzidwa kwambiri akafika kuti asise a Police akuchosa misonkho akuti alakwa akalipire. K20 Pamene anthu akupangira mavuto mafuta anadula Palibe chomwe akupindula
Aaaah koma izizi ndiye chakwera wationjedza zedi ,koma chifukwa chani kweni kweni?
Mr kalindo munafika aaaah kukanapezeka ambiri ngati inu bwezi dzikoli titaona zina aaaah
Kkkk Boma amalawi kutifinya tiwona zinthu shop chaine chasala ndi maepute katoni okhaokha ndatawira kunnjenga ndiyemukulesa mukufuna kundipha chani mukandiphera kuzenje komweko 😮😮😮😮
Kkkkk koma ndipo akavoteraa nda amawooo hiyaa mau Mr Bon
Booooon kalindooooo 🔥🔥
Ine nyimbo ndi zomwe zimandi waza koophya ati Sikusinja ndi Gwenembe amkaimba agogo awake DC popita ku Mzuzu akudutsa mu chikangawa 😂😂😂😂😂 DC makina 😂😂
Akufuna kutimpha agalu amenewa.go deeper
Njira ya ld pokavota sitikavota nkhondo ichitike ichitike
The dc our poor president in Malawi
Ng'alula DC
It's the sikusinja Gwenembe song for me
Osakhala presdent bwanji abon kalindo
Tayambitsani chipani cha amphawi
Zoonadi mboni ndineyo nditachita ngoz ku Queens ndinalipira kut andithandize
Mulungu adalenda dothi osati Chakwera ai
Ndizisilu zaathu zathu ananyerapo chenga iyewo chakwera
Chakwera is apus must go
The DC himself 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Mau awaa sikalindoo
Kalindo ndisaname mukuwatsegula anthu koma bvuto opposition ili weak
Koma mpaka chenga mmmm mawonjeza
We only need solutions not only kulalika
Gwenembe ND sikisinje yemweyo 😂😂😂😂
Mumatimilira mr president
❤❤❤ ndimakunyadilani 👏👏
Aborn kalindo nde mumatiziwisa nkhani zambili mumatiyimilira koma or mukuyankhula anthuwa palibe chomwe akuva bwanji kuti kupangike mademo poti apo akuwona ngati tikusangalala ndi ulamuliro wawoo kukufunika ma demo kuti Ave ngati mumene anapangila azathu ku Kenya lizaini sangapange popanda ma demo 😢
A born kalindo mukadikira opposition kuti itisogolere tichedwa inuo tayambisani ife tili mbuyomo
Akubwila fodya wamagogo wakuzino uja,(maganga).
Sikusinja ndi Gwenembe😅😅😅😅😅😅😅 Nyengo yokhadxula kukhazula
😂😂😂😂😂. Zosatheka sizidzatheka nanga chenga ndichani uyo wasala pang'no kt amfe ameneyo chisilu chamunthuyo muuze ambere Ku muloza border kuno aone kt angatile ife kuvuula chenga.
Unabwela kumalawi amenyelen. Nkhondo anthu asauka
Uyu ndi nyoooo kwa nyooo ulemu wanu aaaa mchenga athu anayambira kale za mchenga athu amadyera momo abale eishh sambi
Koma funso nkumati kuti,
Kodi Chakwela ndi Zikhale wacheyo, samachita manyazi konse akamamva izi? kapena umunthu wanu unatha??
The DC tell them shit
Kodi a Pule alibe olo foni ya mmanja kuti azitha kuona zomwe anthu akukamba online incase samadziwa zomwe nduna zake zikugwilira ntchito.What kind of leadership is this.
Ndipo zoonadi chonsecho sanapangile anthuwo chochita
Kalindo umatitsekula maso
😂😂😂😂😂😂😂 DC mkango wapamalawi timenyereni nkhondoyi koma chakwera ameneyi mpaka awaletse anthu kuuvula mchenga zoona
Umakwana booooon kalindo
Mafumu aku ntcheu mtima wawo ukuwawa alibe dyera ndi mafumu odziwa kulira moyo wa munthu sizocheza
Good
Totally agree the dc
Koma mkulu uyu kkkkkkkk sikusinja sikusinja kkk
Mafuta ayamba kuchoka ku Mozambique kukafika ku area 50 ku Lilongwe kudzela pa njanje ai zikomo
Chakwera nkongo wamako ,mboli Yako ,machende ako ,alipwisi alitongo.
Kkkkkk
We are in a Failed State and Chakwera uyuu achoke
Ndipo live eeee a police eeee akuwo jeza
Koma inuu!! Ayi zikomo.
😂😂 Akalindo nyimboyo ndayikonda
Mmatha madhala madhala inu mungoyimila koma zikhala bwino
Kalindo usatitopese machende yako
Koditu uku mcp kwangokula mbuzi za anthu
Zoona aliyense akavote opanda cha unzika basi nanga izizo nchilungamo
❤
Malawi belongs to Malawians and not Chakwera with his incapacitated cabinet
Denkha Born mulungu azikudalisani koma opposition yadekha ndicholinga usadande iwe mulungu azikudalisa
❤❤
Born kalindo more fire
😂😂😂😂😂passport ya fake ya mwana we president❤❤❤