Bon Kalindo Response To H E Chakwera's SONA.
HTML-код
- Опубликовано: 8 сен 2024
- His Excellency the President Dr Lazarus Chakwera was at Parliament in Lilongwe to make his State of the Nation Address (SONA) and here is what Bon Kalindo had to say about it.
Olemekezeka a President Dr Lazarus Chakwera anali ku Nyumba ya Malamulo ku Lilongwe kukakamba nkhani ya boma la dziko lino (SONA) ndipo izi ndi zomwe Bon Kalindo ananena pankhaniyi.
Note: We Apologize, we mentined in the intro that Bakili Muluzi TV had a copy of the but it turns out they too do not have the full copy. Tikayipeza we will post it or tikupatsani Link kuti nanunso muyimvele.
Note: We Apologize, we mentioned in the intro that Bakili Muluzi TV had an Audio/Visual copy of the SONA but it turns out they too do not have the full copy. Tikayipeza we will post it or tikupatsani Link kuti nanunso muyimvele. If you would like get the PDF version please email us at nyasavoicebox@gmail.com and we will make that available to you.
😊😊😊😊😊
Ine ndiye chakwera wandikwana😮😮
Ndipo opha, chakwera pano angakhale herooo
Empty brain
Koma analidi m'busa uyu ? Fuso zikupeleka pic yanji ya azitumiki achauta. This is are bad people not all 90%bad 10 are good.
Ine ndye saname president uyu amandinyasa zed since kulowa boma mbudzi
Akanakhalako anthu ten kumalawi ngati born kalindo pano kumalawi kutasintha akapange kwa mache ximenezo galu ameneyo
The king master, the DC bon kalindo
Mwana owopsya kwambiri ❤❤ the Dc
Fire
❤born kalindo ndikukanika kupta kwathu kumalawi chifukwa cha Boma iri mmm ai
Ngakhareso ine mmm galu uyu
Those who don't value their words, will never value your wishes.
A chakwera zikufunika musazike ndithu inuyo nthawi yanu yatha,.. ine patrick nampota, South Africa
Sure kkk
Pa campagn ndi chilima anatiuza kale kuti adzamanga airtell yabwino
Chilungamo chenicheni
God guide malawi🎉❤
Nkhani yaikulu a bwana president Boni Kalindo monga athu amene mukutiimilira ifeyo anthu osauka. Ndimaona ngati kuti akawakana mai Mary Navitcha kuti akhale leader of opposition; ndimaona ngati kuti inuyo ndi gulu la Malawi First. Mungopita ku court kukatenga injunction chifukwa MCP ikuwadelera a Malawi kwambili. Kulibwino parliament imeneyi ingoimitsidwapo. Chifukwa anthuwa akuwatola a Malawi ngati alibe tsogoleli monga inuyo bwana Boni Kalindo. Thanks mr President Boni Kalindo
Mau amphamvu
Thank you Mr kalindo
Mwanaa opsa kwambili Bon kalindo
Ndithandizeni guys liu lot DR wakuti limatanthauzanji anzathu mumatha kuona dictionary
It stands for Doctor, mainly used in health field like physician,or with phd.just an abbreviation like, Mr which stands for mister.
Tidya chizungu chachakwera chaka chino
Nice one Mr DC waiting ma Demo
DC ndimunthu wachilungamo anthu wotere ndi amene akufunika ku parliament
Waiting ma demo Mr bon kalindo
Koma chakwera amalingalira kt azafa ndikukakuman ndi fum ya mafum?mm koma ukuxuza ndithu
A KALINDO KEEP IT UP
🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉the dc!!!!!!!!!!!!!!!!!!!! Umakwanatu
❤❤❤❤❤ Bon kalindo
Mawu amenewo
Dc❤❤
❤❤❤❤❤ mr bon kalindo
One day will bath together at state house 😎😎😎
Chakwela mulungu adzamulanga kwambili chifukwa athu akuzuzika ndipo athu akufa ndi njala
Dc plz come tulusa ndodo
szilimbino dzikolawola
Umakwana DC❤❤❤
Mr kalindo ❤❤❤😂😂😂😂😂😂😂😂 neco
Kod .mesa anat akalephera 2 years azatula pas udindo?? Tinenekut akukwanisa kusatula pasi udindowu?
The DC ❤
Mbewu iyiyi ya Chakwera yi isazabwerenso yatizunza ngat tili mu chipani chimodzi.
Viva malawi Viva malawi
Ndipo chakwera palibe chilipo ine ndie wa kwa gwanda chakuambayo ndi bodza kwathu sanaikeko nseu DPP ndi lomwe idzakonze nseu
❤❤❤❤Mr bon kalindo
Ku gaza
Achakwela tikufa ndi njala komwe tikupita basi musala nokha
Ine chakwela ai ndi mbudz
Akuluwa ndale zawalowa kwambiri. Angokhala leader of opposition basi
Chakwera kukamwa kobwafikako
Kwa ine zomalandila ndalama za ulerezi si zabwino kwen kwen, chifukwa zimapwetekesa anthu ozilimbikila pa okha chifukwa ndi pamene misonkho imakwela kwambili ovutika amakhala ozilimbikila uja olandila za ulere sadandaula coz nzaulele. Program imenei ndingakhale osangalara itakhala only okalamba bsi not aliese and big problems amalembana pa chibale anthu ake ndi omweomweo choncho nzosakoma.
viva D.C. ❤❤❤
Chakwera usanamize anthu kuti, ungamange njanji yoti sitima iziyendera magetsi. Pakalipano, ikulira boma la south africa anthu atadula mawaya onse a copper mu njanji ikutha 3yrs pakali pano madera ena kulibe sitima zonyamula wanthu. Ndiye ukawanamize anthu lero, tamawopa Chakwera kumwambaku kuli mulungu udziwe kuti, unayamba bwino koma tsopano utha udyo.
❤❤❤Kalindo
Moto kuti buuuuuuuuu kalondo yemweyooo
The kalindo DC ....Umatha
🎉 Ndiye wina aliyese😂akulira naye❤ chakwela olo kufusa mwana amangotu kwana kuti ansavele virus ya chakwela ayenda ndi kurangura zonsa kwana Oro kakebe ka feteresa.🎉😂❤
😂😂😂😂😂Ndipo aliyense anadi akudana naye Akumamutukwana coz chaufiti wake
Tikufera chizungu
For sure
Bwana kuyakhula kumeneko kwa nzeru awawa akufunika ku pita koko atulukeko si ana ife
Hy
Mumaona Ngati achimwene aakulu ndi wazisuzo munya muona
Speech yagalu uyu(chakwera) its copy and paste speech ya president wa South Africa 🇿🇦 😂😂😂😂
Iya
Wawa ambwiye
Or iweyo Kalindo ndichani unapangako uli MP kwanuko. Leave Chakwera alone tidamuvotera tokha
Don't talk about Kalindo for everyone here in Malawi is able to see .Ifetu ndi anthu akuluakulu tikuona zonse bwana though mukusapota manyaka
Kuyanba kuwapatsa150k simwano, bcoz amadikila apange budget through parliament bcoz thy needed a gud amount of money. Iwe ili ndi nsanje whatever speech angayankhule u criticize it bcoz u want to deal with the president posakupatsa udindo m'boma
Kod inu amalawi muli pati paliposo mukangonyoza zili zonse mwatan kod nanuso mitu yanu sikugwira ntchito pitani uko ndi chakwera wanuyo machende ake, bon kalindo ndi katundu payekha ife tili ndi abon kalindo
Dikila ndi wa tukwaneno zenizeni, mboli zanu,machende anu,nyini zanu, mikongo yanu ,kuda ngati kuseli kwa tchende nonse otsutsana ndi bon kalindo ,chakwela galu wa munthu, nankhumwa mwana wa mbuzi okakamila kuyamwa galu chakwela koma munya campaign ikayamba mpamene muone mkwiyo wa a Malawi,,,,,machende anu nonse ! Chakwela kukamwa ngati mpheto, mkazi wako kukamwa ngat kumtumbo agalu inu mwatizunza kwakwana manyi anu
The DC more fire sonayi ndi manyaka
Akafuse nyamilandu akati azamanga 5star hotel mu nthawi yowonjezela zimene akayesa kuti Malawi wa lero ndi wa zana anthu ndiwokwiya ndi anthu opusa onga wawa
Ndpo chaakwela sukunya sunny wako
Kalindo asakupusitseni amalawi choti mudziwe palibe chingasinthe mavuto wabe adzapita patsogolo chimene akufuna born kalindo ndichakuti boma limene likubwelalo lizamuganizile udindo winauliwonse akadzatelo simudzamuwonaso wapita basi mavutowabe adzati tsalila yinu ndiyene
Umakwanira the DC
Nasongoleyi ayende byake biiiiii
Chakwera inachuluka ndi jerasi nkhwidzi kupangira APM koma kunena zoona walephera kusogolera wanthu
A kalindo even u mp unakulephelani anakuchosan mukanakhala kut anthu akwanu mumawathandiza bwenzi sanaku choseni pa u mp leave our president alone ,jealous lakuvutan mumafuna unduna
Chakwera ndi batile linja lizigona Pa charge basi
Kod uyu chidzungu chake chakut bible courage yomweyi kkkkkk Kom chisoni kobs
Satanic, imamusintha munthu mu zambiri ndipo English yi ndi silang ya pansi pa nyanja
The DC
Cionse akulandila machende ache galu amenei achoke bs
Kodi a Boni K Alindo ndiotani ?Is he a Malawian or Mozambican
kodi umangosusa zilizose basi? ziyamikilani zinazi akulu ifet tikuonako ubwino winawake
Nyengo yakutswakutswa
Chisilu ichi
Abonikalindo akachoka achakwera chakachamawa amene abwereyo simudzayimililanso nkuyamba kutukwana ndikungokuonani mulungu akadzatisunga tidzakusekani
Iwe ndi chitsilu eti! Bon satukwana koma kutsuka bodza la boma
@@user-qv4ko6ps4j tachenjera ndiweo mudamuchotsa apm lelo mukulankhula zachakwera mukusonyeza kuchenjera kodi kumuitana munthu kuti mbuzi sikutukana?
@@user-nc4vi1jt5g chokaaaaaa iweso mbuzi
Zokotani mfumu.
i think bon kalindo you just opposes for the sake of opposing!! see things with positive lens! akulu kususa kwanu nkopanda nzeru
Ndipo ine amandikwana Winiko wanuyi
Komatu amene akudyelela misokho yathu ni azathu akumwela koma izi anena ABorn Kalinndo nizosaveka kodi anapeleka Fredy ndi a boma ? anthu amafa ninjala ninali boma liti ?inu mukulimbana mokho ku DPP kwanuko .ukuwuzani kuti mukakhale kwina mukana kuzolowela kundila zawulele
timayembekeza kut tikumva kuti akalindo athandiza anthu 50 pakuwagawila chimanga aaa zokamba ulibe mbava yamunthu
Chimangoziwa kuyankhura chisiru chi boza basi mbuzi ya munthu. Nthawi yako yatha basi.
Achakwela ndi aboza
Kusokoneza Parliament ukalowera kuti ndipo khomo lake litilo.
Kalindo has nothing and doesn't know anything chitsiru Cha chabechabe
Kalindo ngwakufuntha akufuna ndalama wakavuka uyu zaziii
Kalindo mmmmm kumangotsutsa zilizose, ulire ndiweyo ,chifukwa chakwera akuwinaso,
Am failing to get your argument. U trash the SONA and same u recommend the SONA to the extent kuyitchula yokongola and mwayichekenera kuti can induce maiko akunja kuti apange support. Nkhani ikukambidwayi Ndi commenting on SONA is totally different. I expected you analyzing the SONA and isolate issues of great important and bring alternatives that can help to shape the situations. Waste of precious time
Kalindo chilichonse kutsutsa mmmm asatipusitse mutu wake sulibwino akuluwa
IMF, world bank, European union komanso the whole donor community is fully behind the president's economic policy...
Anthu amenewa sapanganawo zandale so give credit where its due.
Iweyo Kalindo what do u know about economy?
Your audios are just a source of entertainment basi osati muzinamapo apa 😅😅😅
The most useless guy in Malawi is Bon Kalindo after realising whatever problems the Malawi are facing what have you done to the people of you area to areaviate some of these problems do you really see what your friends like Bushiri are doing to help the poeple of this country but they have never been here to talk the nosense you talking about here
Bon kalindo adazowela kubwebweta kungomuzolowela basi alibe ninzelu zomwe ngati iweyo Ali plasntent wawanthu osawuka bwanji suwathandiza anthu osawukawotu
Kod inuyo a born kalindo ndiy tivotele ndan koz mukutisokonedza ndiy mwina muine inuyo
Akalindo ndiwopusa komaso chamba chamvuta
Ndiwopusa kwambiri uyu
Moto kuti buuuuuuuuu kalondo yemweyooo
Iwe ukusowa zolakhula kagone nichamba cakocho