Bon Kalindo Response To H E Chakwera's SONA.

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 8 сен 2024
  • His Excellency the President Dr Lazarus Chakwera was at Parliament in Lilongwe to make his State of the Nation Address (SONA) and here is what Bon Kalindo had to say about it.
    Olemekezeka a President Dr Lazarus Chakwera anali ku Nyumba ya Malamulo ku Lilongwe kukakamba nkhani ya boma la dziko lino (SONA) ndipo izi ndi zomwe Bon Kalindo ananena pankhaniyi.
    Note: We Apologize, we mentined in the intro that Bakili Muluzi TV had a copy of the but it turns out they too do not have the full copy. Tikayipeza we will post it or tikupatsani Link kuti nanunso muyimvele.

Комментарии • 119

  • @nyasavoicebox
    @nyasavoicebox  7 месяцев назад +5

    Note: We Apologize, we mentioned in the intro that Bakili Muluzi TV had an Audio/Visual copy of the SONA but it turns out they too do not have the full copy. Tikayipeza we will post it or tikupatsani Link kuti nanunso muyimvele. If you would like get the PDF version please email us at nyasavoicebox@gmail.com and we will make that available to you.

  • @user-is5dl7np9g
    @user-is5dl7np9g 7 месяцев назад +4

    Ine ndiye chakwera wandikwana😮😮

    • @giftdulamkalenga7344
      @giftdulamkalenga7344 7 месяцев назад

      Ndipo opha, chakwera pano angakhale herooo

    • @user-jk8sh7fh2d
      @user-jk8sh7fh2d 7 месяцев назад

      Empty brain

    • @user-jk8sh7fh2d
      @user-jk8sh7fh2d 7 месяцев назад

      Koma analidi m'busa uyu ? Fuso zikupeleka pic yanji ya azitumiki achauta. This is are bad people not all 90%bad 10 are good.

  • @munashemoyo4190
    @munashemoyo4190 7 месяцев назад +8

    Ine ndye saname president uyu amandinyasa zed since kulowa boma mbudzi

  • @charlurquhart5788
    @charlurquhart5788 7 месяцев назад +1

    Akanakhalako anthu ten kumalawi ngati born kalindo pano kumalawi kutasintha akapange kwa mache ximenezo galu ameneyo

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN 3 месяца назад

    The king master, the DC bon kalindo

  • @ephraimkadamika
    @ephraimkadamika 7 месяцев назад +1

    Mwana owopsya kwambiri ❤❤ the Dc

  • @MphatsoDuncan-gh2vc
    @MphatsoDuncan-gh2vc 7 месяцев назад +1

    Fire

  • @charlurquhart5788
    @charlurquhart5788 7 месяцев назад

    ❤born kalindo ndikukanika kupta kwathu kumalawi chifukwa cha Boma iri mmm ai

  • @dingim1234
    @dingim1234 7 месяцев назад

    Those who don't value their words, will never value your wishes.

  • @user-xv5pr3ji6w
    @user-xv5pr3ji6w 7 месяцев назад +1

    A chakwera zikufunika musazike ndithu inuyo nthawi yanu yatha,.. ine patrick nampota, South Africa

  • @HildatoweraMhango-et4mz
    @HildatoweraMhango-et4mz 7 месяцев назад +1

    Pa campagn ndi chilima anatiuza kale kuti adzamanga airtell yabwino

  • @ThandieWaMalungaseda-rd1bg
    @ThandieWaMalungaseda-rd1bg 7 месяцев назад +2

    Chilungamo chenicheni

  • @PreciousHenderson-qc1hq
    @PreciousHenderson-qc1hq 6 месяцев назад

    God guide malawi🎉❤

  • @user-oo5bx1rl3j
    @user-oo5bx1rl3j 7 месяцев назад

    Nkhani yaikulu a bwana president Boni Kalindo monga athu amene mukutiimilira ifeyo anthu osauka. Ndimaona ngati kuti akawakana mai Mary Navitcha kuti akhale leader of opposition; ndimaona ngati kuti inuyo ndi gulu la Malawi First. Mungopita ku court kukatenga injunction chifukwa MCP ikuwadelera a Malawi kwambili. Kulibwino parliament imeneyi ingoimitsidwapo. Chifukwa anthuwa akuwatola a Malawi ngati alibe tsogoleli monga inuyo bwana Boni Kalindo. Thanks mr President Boni Kalindo

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 7 месяцев назад

    Thank you Mr kalindo

  • @IsaacPhakaya
    @IsaacPhakaya 2 месяца назад

    Mwanaa opsa kwambili Bon kalindo

  • @user-qw4pk7wj8i
    @user-qw4pk7wj8i 7 месяцев назад +1

    Ndithandizeni guys liu lot DR wakuti limatanthauzanji anzathu mumatha kuona dictionary

    • @user-to8pv7ph9g
      @user-to8pv7ph9g 7 месяцев назад

      It stands for Doctor, mainly used in health field like physician,or with phd.just an abbreviation like, Mr which stands for mister.

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 7 месяцев назад +1

    Tidya chizungu chachakwera chaka chino

  • @Bkathira
    @Bkathira 7 месяцев назад

    Nice one Mr DC waiting ma Demo

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 7 месяцев назад +1

    DC ndimunthu wachilungamo anthu wotere ndi amene akufunika ku parliament

  • @oliviamphande1900
    @oliviamphande1900 7 месяцев назад +1

    Waiting ma demo Mr bon kalindo

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r 6 месяцев назад +1

    Koma chakwera amalingalira kt azafa ndikukakuman ndi fum ya mafum?mm koma ukuxuza ndithu

  • @user-xo5mq7wl7t
    @user-xo5mq7wl7t 7 месяцев назад

    A KALINDO KEEP IT UP

  • @thefather007
    @thefather007 7 месяцев назад

    🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉the dc!!!!!!!!!!!!!!!!!!!! Umakwanatu

  • @user-dt8nr1zx6e
    @user-dt8nr1zx6e 7 месяцев назад

    ❤❤❤❤❤ Bon kalindo
    Mawu amenewo

  • @user-jp2qg2ww7r
    @user-jp2qg2ww7r 7 месяцев назад

    Dc❤❤

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 7 месяцев назад

    ❤❤❤❤❤ mr bon kalindo

  • @PrinceMapemba-fn4cw
    @PrinceMapemba-fn4cw 6 месяцев назад

    One day will bath together at state house 😎😎😎

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 7 месяцев назад +1

    Chakwela mulungu adzamulanga kwambili chifukwa athu akuzuzika ndipo athu akufa ndi njala

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga7344 7 месяцев назад

    Dc plz come tulusa ndodo

  • @HappyMwase-w7f
    @HappyMwase-w7f 2 месяца назад

    szilimbino dzikolawola

  • @user-mk7fh5ml8s
    @user-mk7fh5ml8s 7 месяцев назад

    Umakwana DC❤❤❤

  • @AllanCharlesNgona-wm5xs
    @AllanCharlesNgona-wm5xs 6 месяцев назад

    Mr kalindo ❤❤❤😂😂😂😂😂😂😂😂 neco

  • @BrightNkhoma-xz4bg
    @BrightNkhoma-xz4bg Месяц назад

    Kod .mesa anat akalephera 2 years azatula pas udindo?? Tinenekut akukwanisa kusatula pasi udindowu?

  • @user-jw5rx9ze8k
    @user-jw5rx9ze8k 7 месяцев назад

    The DC ❤

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 7 месяцев назад +3

    Mbewu iyiyi ya Chakwera yi isazabwerenso yatizunza ngat tili mu chipani chimodzi.

  • @PreciousHenderson-qc1hq
    @PreciousHenderson-qc1hq 6 месяцев назад

    Viva malawi Viva malawi

  • @user-qm1qb2jp4s
    @user-qm1qb2jp4s 6 месяцев назад

    Ndipo chakwera palibe chilipo ine ndie wa kwa gwanda chakuambayo ndi bodza kwathu sanaikeko nseu DPP ndi lomwe idzakonze nseu

  • @TiyaMtete
    @TiyaMtete 7 месяцев назад

    ❤❤❤❤Mr bon kalindo

  • @AlickNdeketeya
    @AlickNdeketeya 7 месяцев назад

    Ku gaza

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 7 месяцев назад +1

    Achakwela tikufa ndi njala komwe tikupita basi musala nokha

  • @johncassimu5433
    @johncassimu5433 7 месяцев назад +1

    Ine chakwela ai ndi mbudz

  • @eliasmgala8469
    @eliasmgala8469 6 месяцев назад

    Akuluwa ndale zawalowa kwambiri. Angokhala leader of opposition basi

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 7 месяцев назад +1

    Chakwera kukamwa kobwafikako

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d 7 месяцев назад

    Kwa ine zomalandila ndalama za ulerezi si zabwino kwen kwen, chifukwa zimapwetekesa anthu ozilimbikila pa okha chifukwa ndi pamene misonkho imakwela kwambili ovutika amakhala ozilimbikila uja olandila za ulere sadandaula coz nzaulele. Program imenei ndingakhale osangalara itakhala only okalamba bsi not aliese and big problems amalembana pa chibale anthu ake ndi omweomweo choncho nzosakoma.

  • @abdulirichard260
    @abdulirichard260 7 месяцев назад

    viva D.C. ❤❤❤

  • @storytambala6088
    @storytambala6088 7 месяцев назад

    Chakwera usanamize anthu kuti, ungamange njanji yoti sitima iziyendera magetsi. Pakalipano, ikulira boma la south africa anthu atadula mawaya onse a copper mu njanji ikutha 3yrs pakali pano madera ena kulibe sitima zonyamula wanthu. Ndiye ukawanamize anthu lero, tamawopa Chakwera kumwambaku kuli mulungu udziwe kuti, unayamba bwino koma tsopano utha udyo.

  • @user-pu3sb2xw6z
    @user-pu3sb2xw6z 7 месяцев назад

    ❤❤❤Kalindo

  • @peterkuliyanimbewe
    @peterkuliyanimbewe 7 месяцев назад

    Moto kuti buuuuuuuuu kalondo yemweyooo

  • @custommantchombe-rn1oo
    @custommantchombe-rn1oo 7 месяцев назад

    The kalindo DC ....Umatha

  • @tiunzanenganimunomwaafrican
    @tiunzanenganimunomwaafrican 7 месяцев назад

    🎉 Ndiye wina aliyese😂akulira naye❤ chakwela olo kufusa mwana amangotu kwana kuti ansavele virus ya chakwela ayenda ndi kurangura zonsa kwana Oro kakebe ka feteresa.🎉😂❤

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 7 месяцев назад +1

      😂😂😂😂😂Ndipo aliyense anadi akudana naye Akumamutukwana coz chaufiti wake

  • @user-pe7lo1fe9b
    @user-pe7lo1fe9b 7 месяцев назад +1

    Tikufera chizungu

  • @user-qd2uy9fp9v
    @user-qd2uy9fp9v 7 месяцев назад

    Bwana kuyakhula kumeneko kwa nzeru awawa akufunika ku pita koko atulukeko si ana ife

  • @user-ny3it3jp9l
    @user-ny3it3jp9l 6 месяцев назад

    Hy

  • @kennethkaunda3636
    @kennethkaunda3636 6 месяцев назад

    Mumaona Ngati achimwene aakulu ndi wazisuzo munya muona

  • @georgemponda
    @georgemponda 7 месяцев назад +1

    Speech yagalu uyu(chakwera) its copy and paste speech ya president wa South Africa 🇿🇦 😂😂😂😂

  • @user-qy5sh4di7t
    @user-qy5sh4di7t 7 месяцев назад

    Iya

  • @user-ec3xh4pc6t
    @user-ec3xh4pc6t 7 месяцев назад

    Wawa ambwiye

  • @lawrencetenthani5547
    @lawrencetenthani5547 7 месяцев назад

    Or iweyo Kalindo ndichani unapangako uli MP kwanuko. Leave Chakwera alone tidamuvotera tokha

  • @davietembo7935
    @davietembo7935 7 месяцев назад

    Don't talk about Kalindo for everyone here in Malawi is able to see .Ifetu ndi anthu akuluakulu tikuona zonse bwana though mukusapota manyaka

  • @georgednthala-wh3pf
    @georgednthala-wh3pf 7 месяцев назад

    Kuyanba kuwapatsa150k simwano, bcoz amadikila apange budget through parliament bcoz thy needed a gud amount of money. Iwe ili ndi nsanje whatever speech angayankhule u criticize it bcoz u want to deal with the president posakupatsa udindo m'boma

  • @user-ce6hy6tp7e
    @user-ce6hy6tp7e 7 месяцев назад

    Kod inu amalawi muli pati paliposo mukangonyoza zili zonse mwatan kod nanuso mitu yanu sikugwira ntchito pitani uko ndi chakwera wanuyo machende ake, bon kalindo ndi katundu payekha ife tili ndi abon kalindo

    • @user-qv4ko6ps4j
      @user-qv4ko6ps4j 7 месяцев назад

      Dikila ndi wa tukwaneno zenizeni, mboli zanu,machende anu,nyini zanu, mikongo yanu ,kuda ngati kuseli kwa tchende nonse otsutsana ndi bon kalindo ,chakwela galu wa munthu, nankhumwa mwana wa mbuzi okakamila kuyamwa galu chakwela koma munya campaign ikayamba mpamene muone mkwiyo wa a Malawi,,,,,machende anu nonse ! Chakwela kukamwa ngati mpheto, mkazi wako kukamwa ngat kumtumbo agalu inu mwatizunza kwakwana manyi anu

  • @BrazioBauleni-sq9pu
    @BrazioBauleni-sq9pu 7 месяцев назад

    The DC more fire sonayi ndi manyaka

  • @fridaymtembo1304
    @fridaymtembo1304 7 месяцев назад

    Akafuse nyamilandu akati azamanga 5star hotel mu nthawi yowonjezela zimene akayesa kuti Malawi wa lero ndi wa zana anthu ndiwokwiya ndi anthu opusa onga wawa

  • @IdritsaHanudan-dg3gi
    @IdritsaHanudan-dg3gi 6 месяцев назад

    Ndpo chaakwela sukunya sunny wako

  • @evansevas119
    @evansevas119 7 месяцев назад

    Kalindo asakupusitseni amalawi choti mudziwe palibe chingasinthe mavuto wabe adzapita patsogolo chimene akufuna born kalindo ndichakuti boma limene likubwelalo lizamuganizile udindo winauliwonse akadzatelo simudzamuwonaso wapita basi mavutowabe adzati tsalila yinu ndiyene

  • @user-gh1yc3mu5r
    @user-gh1yc3mu5r 7 месяцев назад

    Umakwanira the DC

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp 7 месяцев назад

    Nasongoleyi ayende byake biiiiii

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b 7 месяцев назад

    Chakwera inachuluka ndi jerasi nkhwidzi kupangira APM koma kunena zoona walephera kusogolera wanthu

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o 7 месяцев назад

    A kalindo even u mp unakulephelani anakuchosan mukanakhala kut anthu akwanu mumawathandiza bwenzi sanaku choseni pa u mp leave our president alone ,jealous lakuvutan mumafuna unduna

  • @AlickNdeketeya
    @AlickNdeketeya 7 месяцев назад

    Chakwera ndi batile linja lizigona Pa charge basi

  • @user-qw4pk7wj8i
    @user-qw4pk7wj8i 7 месяцев назад

    Kod uyu chidzungu chake chakut bible courage yomweyi kkkkkk Kom chisoni kobs

    • @user-qv4ko6ps4j
      @user-qv4ko6ps4j 7 месяцев назад

      Satanic, imamusintha munthu mu zambiri ndipo English yi ndi silang ya pansi pa nyanja

  • @ronexmcdonald8742
    @ronexmcdonald8742 7 месяцев назад

    The DC

  • @charlurquhart5788
    @charlurquhart5788 7 месяцев назад

    Cionse akulandila machende ache galu amenei achoke bs

  • @josephMandala-hk4xs
    @josephMandala-hk4xs 7 месяцев назад

    Kodi a Boni K Alindo ndiotani ?Is he a Malawian or Mozambican

  • @PSTPerivoli-xd1ot
    @PSTPerivoli-xd1ot 7 месяцев назад +1

    kodi umangosusa zilizose basi? ziyamikilani zinazi akulu ifet tikuonako ubwino winawake

  • @jonathanmbewe4246
    @jonathanmbewe4246 7 месяцев назад

    Nyengo yakutswakutswa

  • @user-fs1ox7ou1b
    @user-fs1ox7ou1b 5 месяцев назад

    Chisilu ichi

  • @user-nc4vi1jt5g
    @user-nc4vi1jt5g 7 месяцев назад

    Abonikalindo akachoka achakwera chakachamawa amene abwereyo simudzayimililanso nkuyamba kutukwana ndikungokuonani mulungu akadzatisunga tidzakusekani

    • @user-qv4ko6ps4j
      @user-qv4ko6ps4j 7 месяцев назад

      Iwe ndi chitsilu eti! Bon satukwana koma kutsuka bodza la boma

    • @user-nc4vi1jt5g
      @user-nc4vi1jt5g 7 месяцев назад

      @@user-qv4ko6ps4j tachenjera ndiweo mudamuchotsa apm lelo mukulankhula zachakwera mukusonyeza kuchenjera kodi kumuitana munthu kuti mbuzi sikutukana?

    • @user-qv4ko6ps4j
      @user-qv4ko6ps4j 7 месяцев назад

      @@user-nc4vi1jt5g chokaaaaaa iweso mbuzi

  • @user-kr1kg5hy9l
    @user-kr1kg5hy9l 7 месяцев назад

    Zokotani mfumu.

  • @PSTPerivoli-xd1ot
    @PSTPerivoli-xd1ot 7 месяцев назад +2

    i think bon kalindo you just opposes for the sake of opposing!! see things with positive lens! akulu kususa kwanu nkopanda nzeru

  • @MathewsKamphambe
    @MathewsKamphambe 7 месяцев назад

    Komatu amene akudyelela misokho yathu ni azathu akumwela koma izi anena ABorn Kalinndo nizosaveka kodi anapeleka Fredy ndi a boma ? anthu amafa ninjala ninali boma liti ?inu mukulimbana mokho ku DPP kwanuko .ukuwuzani kuti mukakhale kwina mukana kuzolowela kundila zawulele

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga 7 месяцев назад

    timayembekeza kut tikumva kuti akalindo athandiza anthu 50 pakuwagawila chimanga aaa zokamba ulibe mbava yamunthu

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 7 месяцев назад

    Chimangoziwa kuyankhura chisiru chi boza basi mbuzi ya munthu. Nthawi yako yatha basi.

  • @nellikkmwenda7087
    @nellikkmwenda7087 7 месяцев назад

    Achakwela ndi aboza

  • @lawrencetenthani5547
    @lawrencetenthani5547 7 месяцев назад

    Kusokoneza Parliament ukalowera kuti ndipo khomo lake litilo.

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o 7 месяцев назад

    Kalindo has nothing and doesn't know anything chitsiru Cha chabechabe

  • @user-xs3pk1vp8i
    @user-xs3pk1vp8i 7 месяцев назад

    Kalindo ngwakufuntha akufuna ndalama wakavuka uyu zaziii

  • @user-og3dp9di7e
    @user-og3dp9di7e 6 месяцев назад

    Kalindo mmmmm kumangotsutsa zilizose, ulire ndiweyo ,chifukwa chakwera akuwinaso,

  • @user-rk3uo5fs6g
    @user-rk3uo5fs6g 6 месяцев назад

    Am failing to get your argument. U trash the SONA and same u recommend the SONA to the extent kuyitchula yokongola and mwayichekenera kuti can induce maiko akunja kuti apange support. Nkhani ikukambidwayi Ndi commenting on SONA is totally different. I expected you analyzing the SONA and isolate issues of great important and bring alternatives that can help to shape the situations. Waste of precious time

  • @user-xs3pk1vp8i
    @user-xs3pk1vp8i 7 месяцев назад

    Kalindo chilichonse kutsutsa mmmm asatipusitse mutu wake sulibwino akuluwa

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 7 месяцев назад

    IMF, world bank, European union komanso the whole donor community is fully behind the president's economic policy...
    Anthu amenewa sapanganawo zandale so give credit where its due.
    Iweyo Kalindo what do u know about economy?
    Your audios are just a source of entertainment basi osati muzinamapo apa 😅😅😅

  • @robertharawa9203
    @robertharawa9203 7 месяцев назад

    The most useless guy in Malawi is Bon Kalindo after realising whatever problems the Malawi are facing what have you done to the people of you area to areaviate some of these problems do you really see what your friends like Bushiri are doing to help the poeple of this country but they have never been here to talk the nosense you talking about here

  • @johnchicoti
    @johnchicoti 7 месяцев назад

    Bon kalindo adazowela kubwebweta kungomuzolowela basi alibe ninzelu zomwe ngati iweyo Ali plasntent wawanthu osawuka bwanji suwathandiza anthu osawukawotu

  • @user-cw8ue6qp8w
    @user-cw8ue6qp8w 7 месяцев назад

    Kod inuyo a born kalindo ndiy tivotele ndan koz mukutisokonedza ndiy mwina muine inuyo

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r 7 месяцев назад

    Akalindo ndiwopusa komaso chamba chamvuta

  • @user-lc9bm6li6z
    @user-lc9bm6li6z 7 месяцев назад

    Ndiwopusa kwambiri uyu

  • @peterkuliyanimbewe
    @peterkuliyanimbewe 7 месяцев назад

    Moto kuti buuuuuuuuu kalondo yemweyooo

  • @user-mk4lo7bd6f
    @user-mk4lo7bd6f 7 месяцев назад

    Iwe ukusowa zolakhula kagone nichamba cakocho