KODI OIPAYO NDI MUTHARIKA KOMASO ATUPELE KAPENA ILI NDI BODZA?

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 7 сен 2024

Комментарии • 91

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Месяц назад +11

    Musalimbane ndi peter komanso Atupele ...pakampeni paja amaneneratu poyera kut MUSAVOTERE MCP ...nde anthu sanamve akut umafuna change...This is the change..the change can be positive or negative....asiyeni a MCP alamulire chifukwa ndie zimene munavotera...tichimine kaye a malawi...Pena Mulungu amapanga zoti anthu aphunzire kwambiri

    • @user-rp9wy6rd1q
      @user-rp9wy6rd1q Месяц назад +3

      Zoonad anthu amageya mwano kwambiri akuti tisithe zithu ndie zasithaditu

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x Месяц назад +8

    Koma boss ndiiwe ozindikira koopsa keep it up, mavutowa tinachita kubwelesa tokha. Anatiuza ndipo anatilangiza koma kusanva ndipo ananena Peter Muntharika kuti mukupanga inuzi akubwerawo muona Nyekhwe. Lero ndiizi kaaah

  • @macrinenduna1024
    @macrinenduna1024 Месяц назад

    Good comment. Truly these two Gentlemen are real country men.

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi Месяц назад +4

    Zikomo amwene papani Mr pita ndi Tupele muzitikhululukila zoona vuto ndi ife ndithu🙏🙏🙏🙏🙏

  • @MonicaSteve-t5p
    @MonicaSteve-t5p Месяц назад +3

    Good correction sir ❤❤

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3i Месяц назад +1

    Zoona brother uyu walankhura odiyo iyi ndi mbudzi ya Mano kunsi, ndipo samadziwa chomwe amanena. I love you u ndipo mau anga mwandinenera ndinu❤❤

  • @user-ou9jz8pr4m
    @user-ou9jz8pr4m Месяц назад +2

    More fire mr D takunyadilani kwambiri mwalankhulabwino

  • @Freedomchennl47
    @Freedomchennl47 Месяц назад

    Kmaso number one ozikonda ndameneo akuyakhulayo waku mangochiyo ndamene ali adyela

  • @LeonardChinomba
    @LeonardChinomba Месяц назад +2

    Abwana osaganiza ndi inuyo don't trust akunena zoona apeter ndi atupele ndi anthu osathandiza anthu akulephela kutuluka kulimbikisa anthu boni kalindo akulimba naye ekha sakumuona mzawo uja chihana akuyenda kumalankhula pa steji dziko ndi kumamva koma peter ndi atupele ndipamene kubisala iwo akuti aopa kuphedwa ndi mcp kodi mufuna muzangonyamulilidwapo pampandopo muzidya misonkho ya amalawi

  • @PetroMatias
    @PetroMatias Месяц назад +1

    Ase wayankhura bwino mmanja mwako 🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🤝🤝🤝🤝🤝🤝

  • @JohnJohn-og8rt
    @JohnJohn-og8rt Месяц назад +1

    Ameen Iweyo mulungu akudalisene moyo ukuyangula zabwino mau amuna asitero amavuna dala athuwo

  • @HezekiahItz
    @HezekiahItz Месяц назад

    Zoona kuyankhur mosacheuka bwana komaso chilungamo anthuwa tithanenao tokha Peter and atupele asiyeni ananyozedwa ngat alibe mitu ngat alibe uzimu asiyen imfa ya saulosi chilima yaripweteka Ndye mikono yanthu tikutsamir kwa a2 awawa Ndye njara ikatikhaulitsa ndipamene tingapite pa mseu

  • @FisherAction
    @FisherAction Месяц назад

    Ndiye ngati akutero kut samatengapo gawo nkwabwino asayime asiye omwe angamathandizire kumamenyanawo nkhondo bcz we are in democracy no words kupembezana

  • @MaggieCement
    @MaggieCement Месяц назад +1

    Ndipo Muthu ndiobvuta ndithu tinya ndizomwe tinkafuna ngati ana akhanda oti nkhongelesiyo yabwela lero hahahahaha

  • @user-vn3ty1yg9l
    @user-vn3ty1yg9l Месяц назад

    Moti inu mwavotelaso mavuto aaaa zikozeni nokha kumeneko Peter atupele siwolakwa

  • @LovemoreSalima
    @LovemoreSalima Месяц назад

    Thanks D phiri
    Auzeni ana amahurewa,
    Ndiomwe atifikitsa pa manyiwa.
    Bu shit, anthu amanyi amenewa. Azimuloza Chala ntambo.

  • @EdsonKamwendo
    @EdsonKamwendo Месяц назад +1

    Mai woputsa iwe umafuna azingoyenda wamba iweyo siukuziwa kuti mcp ili ndi chiwembu chachikulu kodi mcp yakutuma ? Ugaluwako

  • @user-bq8gb7tb1l
    @user-bq8gb7tb1l Месяц назад

    D.phiri wanena zoona,,,ife tinalakwisa

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 Месяц назад

    This is true boss,, atupere or munthalika asiyeni mavutowa ndiifeyo amalawi kusamva lero ndi izi

  • @mozesaine6677
    @mozesaine6677 Месяц назад

    Pure answer

  • @MrsNankhumwa
    @MrsNankhumwa Месяц назад +1

    Ndipo APM anatiuza kut mukavotera MCP muzalira, lero nzimenezi munkafuna anyamata paja, ulemu wanu akulu mwayankhula bwino kwabas,

  • @shazirahJafali
    @shazirahJafali Месяц назад

    Izi nde ndizoonad osapanga complain pa anthu awa ayi vuto ndamene anachotsa dpp kukavotela mcp

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад

    Akulu inu mulibe zelu ndipo zomwe mukunenazo chipani cha dpp udf ngati akhala ndimaganizo akowo basi dpp yapita sizalowaso boma ndiwe chisilu basi dpp ndaituluka kuli zitsilu ndichifukwa chake mukongoluza zisakho shupit

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba Месяц назад

    Ndipo Apm ndi atupele 2025 anatisiya tikhaule tinapanga chipongwe tokha

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад

    Peter wakalamba sangathamange osazemba ai ndipotu inuyo mukakakamila peter ndiye zolowa boma iwalani ndithu

  • @IshumaerWazakile-u5d
    @IshumaerWazakile-u5d Месяц назад

    Chachikulu ife amalawi sitikufuna kukhutitsi pazimene Dr piter amatipangira ndiye anthu athira kuwiri

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад

    Mcp 2025 boma cadet akhaula ndipo iwe cadet ukanalila musobva😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm Месяц назад

    Powerful 👊

  • @AlliSaiti
    @AlliSaiti Месяц назад

    Uku nde kuyakhura mopanda nzeru😅😅😅😅😅😅 kod adpp abalalika eti

  • @user-jc5tf8jl1m
    @user-jc5tf8jl1m Месяц назад

    Musiyeni uyo wadya banzi walandila ndalama.Mangochi singavotele mcp ai

  • @FisherAction
    @FisherAction Месяц назад

    Ayi ndizakale zomwezija ndikwabwino azilankhulapo asakhale zii

  • @zaidimussa
    @zaidimussa Месяц назад

    Muiyu afuna kukoza mbili yachakwela kodi Apm sadanene kuti mudzaona nyenkhwe atupele ndi apm sindikuwapeza ndi mulandu ovulala ife bandi akamange atupele ndi apm ndizoona

  • @AiameAdamo-su1nt
    @AiameAdamo-su1nt Месяц назад

    Good correction

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw Месяц назад

    Mr phiri .mwandizizilitsa mtima mwarankhura bwino kwambiri.nditamva vn yonyodza ija ineyo mtima unawawa

  • @HassanMbalaka-gb5sv
    @HassanMbalaka-gb5sv Месяц назад

    Sitinva ife Anthony awa Antananarivo don't vote ❎ theme ife makan

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад

    Mungobvutika boma ndilomweli ndipo sitikusintha apa mungotaya nthawi kulongolola palibe chomwe mungachite

  • @ShearstonNyirenda
    @ShearstonNyirenda Месяц назад

    Kagwileni ntchito mupeza nalondalama boma lachakwera koma mulesi alipamavuto

  • @user-el8to1te3l
    @user-el8to1te3l Месяц назад

    Wa mcp ameneyo akufuna kut a peter ndi atupele atuluke akawaphe a mcp wabunya

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад

    Alomwe muli patchito chakwela ndukuzani pano simungamuchotse mulakhula mutopa chitsazo ma by election mukungoluza daily

  • @user-qk2hw4ex3c
    @user-qk2hw4ex3c Месяц назад

    Peter amapanga kampeni

  • @lutfieabrahams1465
    @lutfieabrahams1465 Месяц назад

    Ndpo zoona bro mwayankhula bwino

  • @user-lk8kj9zv6x
    @user-lk8kj9zv6x Месяц назад

    Bodza len leni ifetu sitikupanga complain chifukwa chilungamo tikuchidziwa inu izi mukuzitenga kut

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад

    Tsono mukuona ngati mcp ingachoke boma ndi kutukwana kwa ma akitivisinu anthu muli ndichibwana kwabwasi tiye nazoni mukhala ku kotsutsa konko

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад

    Iwe usabvutike anthu sangabvoteleso dpp kulibe ndipo ndukuuza pano dpp sizabwelelasi boma pezani zina zochita izi mutayanazo nthawi

  • @MalungaSteven-i2o
    @MalungaSteven-i2o Месяц назад

    Mau akulu akoma akagonela

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Месяц назад

    Kusankha kwanu a Malawi , muziwona konko. Iwowo analemela kale awa ,mabvuto ndife

  • @LindaMakalani
    @LindaMakalani Месяц назад

    Chisilu ndamene anavotela mcp yo ine ndinavotela my lovely dad Mr p ndiposo pano it's my vote no matter wat

  • @CassimMbalaka
    @CassimMbalaka Месяц назад +1

    Walandira ndarama za mcp amenyo

  • @francebanda-du9yk
    @francebanda-du9yk Месяц назад

    Zonadi. Zimenez
    O

  • @Mahamudu-q6b
    @Mahamudu-q6b Месяц назад

    ❤❤❤

  • @user-qk2hw4ex3c
    @user-qk2hw4ex3c Месяц назад

    Choka ukuyankha zosaveka azako akuti kampeni osati zimene mukuyankha ndizina zimene akunena aazanu ndi kampeni

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q Месяц назад

    Ndare za nepotism ku Malawi we need federal system of government otherwise no change to people that's why Malawi is the poorest country in the world.

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Месяц назад

    Malawi ngakhale wuyifele ,aaa ,chilima anapita ,nkhani yake kufera Malawi . Malawi si woufela

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o Месяц назад +1

    Peter muthalika ndi nkhalamba munthu oti akuziyipitsira yekha pomwe akhala angapange kampen

  • @HUMPHREYBALANGWE
    @HUMPHREYBALANGWE Месяц назад

    Tiyeni tingoyang'ana kutsogolo
    Munthu amadikira chopereka church kuti akhale ndi ndalama ndie mumaganiza kuti angalamulire dziko
    Lero ndi izi dziko latsala masanza okhaokha

  • @YusufuUsumani
    @YusufuUsumani Месяц назад

    Chakwela ndi wamizala wamanyi

  • @MustapherLino
    @MustapherLino Месяц назад

    Zoona man, mai awa ndi hule wachabe

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Месяц назад

    Sanayankhule di bwino bambo amene aja Peter ndi atupere komanso former president Bakili Muluzi anayankhula po za mcp koma anthu kusambva lero ndi izi nde akamayankhula aziyamba aganuza kaye osamangobwebwetuka

  • @SellinaSanena
    @SellinaSanena Месяц назад

    Kusamva kwathu. Don't put the blame on Peter and Atupele. Tinavota tokha

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn Месяц назад

    Iyeyo akuona ngati a opposition angokhala? A Peter ndi atupele TU siopusa akumuwelenga kaye chakwela yu AKUFUNA amlize kaye uchitsiru wakewo kenako adzuke koditu campaign sinayambe kukhala zinthu a opposition mukuwanyozawo simuwafuna

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Месяц назад

    Tinalakwisa tinavotela ena ndiyekuti tisadzudzule? Usanena kuti musakonze ayi ,,wa Aodio sanalakwise,,,tisawagwadile Oro kuwachonderela,,Iwo nde azamwe mkaka,,

  • @GiftJulius-ro9ev
    @GiftJulius-ro9ev Месяц назад

    Choka mboliyako...mkamwa mopindikamo...

    • @VarietyNkhata
      @VarietyNkhata Месяц назад

      Kma iwe ngati ndiwe mukazi ndiwe hule wangoifuna Boro yaminthuyo asa😊

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Месяц назад

    Ulemu wanu guys mwayakhula bwino kwambili mulungu adzikhala nanu thawi zose onyazao asiyeni azinyoza amachita kutumidwa ndi chakwela kuti adzisusa athu akayakhula chilungamo chachikulu tiyeni tiike zise m, manja mwa chauta akuva kulila kwathu chakwela akadapanda kulamulila dzikoli mukanakhala khondo yoopsa kwambili koma mulungu adalola kuti kutelo kuti ukulu wake uonekele 🙏🙏

  • @EsnartMartin
    @EsnartMartin Месяц назад

    Amene uja machende ake ndipo ozikonda ndi iye uja ndi chakwera wakeyo

  • @ChiefJustin-cl8jl
    @ChiefJustin-cl8jl Месяц назад

    Ndi mbuzi imeneyo mutharika ndi atupele ndi sogolo la dziko lamalawi

  • @ThulaniPrince
    @ThulaniPrince Месяц назад

    Koma amalawi tilindimavito, chonyasa chija chayamba kuoneka chabwino kkkkk akangolowa adadi. Muzayambe kunenaso kuti bora chakwera

  • @SlindiryLoveness
    @SlindiryLoveness Месяц назад

    Tinawakana amapha ma albino amenewo asiye akalamba panopa sitikumvako kuti agwira ziwaro za anthu boma la peter linalibe security ndiposo wakalamba wapume zina mumangonama mulizambiri mu malawi panopa tikuwona zachilendo kale kunalibe ngati ndikukwera kwazinthu si malawi yekha ife tikufuna chitukuko basi zimene mukulankhurazo sizikumveka bora chakwera ndi anthu anuwo

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn Месяц назад

    Ndi munthu opepera iyeyo ngati wapatsidwa ndalama azingodya

  • @StellaCharles-dq8db
    @StellaCharles-dq8db Месяц назад

    Amai amene aja atumidwa inu satipusise ife eetu ndpo alikomweko kwachakwerako

    • @shazirahJafali
      @shazirahJafali Месяц назад +1

      Kma ndiye akuchita kuonekadi kuti awapatsa kenakake chifukwa nde akulubwalubwatu

  • @MaikNkhoma
    @MaikNkhoma Месяц назад

    Ndiwekape munya 2025 bomasitokusintha

  • @patassonelucaszovuta3431
    @patassonelucaszovuta3431 Месяц назад

    Ndie ngati ali ndi mantha asiye ndale kuti akhale moyo wautali umene akuufunao

  • @user-pv2xx3lu8b
    @user-pv2xx3lu8b Месяц назад

    Watiyakhulila mwene

  • @user-ev6bi7jr7g
    @user-ev6bi7jr7g Месяц назад

    Mwayankhula bwino kwambiri

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Месяц назад

    Zoona Peter atupele si ozikonda vuto ndife amalawi ovota mitu inawuma mtanyiwa kalindo bakili TV Peter atupere ndi ena ofunila Malawi zabwino alankhula za mcp koma sitinave. Panopa mukuona mcp ikugwirisa ngongole and ikugawa ndala and amalawi tawona mumene wafera chilima ndi abale athu koma still tikusapota bomalo amalawi tili ndivuto loganiza bwino. Munthu kuti mumuziwe kuti zeru alibe boma kuyakhula mwamatama kuzikona kupereka ndalama kuti anthu amuvotere

  • @yotamumahomed1313
    @yotamumahomed1313 Месяц назад

    Komanso umuuze kut watikwana

  • @user-lw4hw9ce4w
    @user-lw4hw9ce4w Месяц назад

    Muuze chimbuzi chimenechi mmesa amakuuzani kusamva kwani

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x Месяц назад

      Ndipo big amai amenewa ndi chimbuzidi zedi Amai opanda nzeru

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Месяц назад

    Zaka 84 angathamange.? Anthu osazindikira inu Peter akanangotuluka tsiku limodzi mukuganiza khansala wa DPP akanaluza? Tulo basi

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Месяц назад

    Iwe ukuyankhulawe ndi Peter muthalika kapena Atupele akupatsa chani chitsiru iwe kagwade wekha kupepera eti kuzolowera kunyambita nsapato .Khala pansi asiyire anthu ozindikira aziyankhula. IWE SINNENERI WA ANTHU AWIRIWA

  • @KestonNGUBO
    @KestonNGUBO Месяц назад

    A dpp mbuzi yagalu iwe ukuyakha

  • @JackMvura-ik2td
    @JackMvura-ik2td Месяц назад

    Tsono iwe wadya banzi ya pitala munthu wadyewa uku one kuziro 2025 mukunya chakwera bomaaa iwe mulomwe mwachepa achewa ndayao atumbuka simuwatha komaso ozindikila alomwe ena Asari Ngati iwe samuvotera pitila DPP yatha Palibe akuifuna tanganizani Mangochi zikumvekanso Kuti mwina pitala akhoza Ku votela chakwera😂😂😂😂😂😂

  • @LeonardChinomba
    @LeonardChinomba Месяц назад

    Abwana osaganiza ndi inuyo don't trust akunena zoona apeter ndi atupele ndi anthu osathandiza anthu akulephela kutuluka kulimbikisa anthu boni kalindo akulimba naye ekha sakumuona mzawo uja chihana akuyenda kumalankhula pa steji dziko ndi kumamva koma peter ndi atupele ndipamene kubisala iwo akuti aopa kuphedwa ndi mcp kodi mufuna muzangonyamulilidwapo pampandopo muzidya misonkho ya amalawi

    • @LovemoreSalima
      @LovemoreSalima Месяц назад

      Inutu ndiye munyee, mukhaule agaluu Inu.