Musalimbane ndi peter komanso Atupele ...pakampeni paja amaneneratu poyera kut MUSAVOTERE MCP ...nde anthu sanamve akut umafuna change...This is the change..the change can be positive or negative....asiyeni a MCP alamulire chifukwa ndie zimene munavotera...tichimine kaye a malawi...Pena Mulungu amapanga zoti anthu aphunzire kwambiri
Ndiye ngati akutero kut samatengapo gawo nkwabwino asayime asiye omwe angamathandizire kumamenyanawo nkhondo bcz we are in democracy no words kupembezana
Sanayankhule di bwino bambo amene aja Peter ndi atupere komanso former president Bakili Muluzi anayankhula po za mcp koma anthu kusambva lero ndi izi nde akamayankhula aziyamba aganuza kaye osamangobwebwetuka
Iyeyo akuona ngati a opposition angokhala? A Peter ndi atupele TU siopusa akumuwelenga kaye chakwela yu AKUFUNA amlize kaye uchitsiru wakewo kenako adzuke koditu campaign sinayambe kukhala zinthu a opposition mukuwanyozawo simuwafuna
Tinawakana amapha ma albino amenewo asiye akalamba panopa sitikumvako kuti agwira ziwaro za anthu boma la peter linalibe security ndiposo wakalamba wapume zina mumangonama mulizambiri mu malawi panopa tikuwona zachilendo kale kunalibe ngati ndikukwera kwazinthu si malawi yekha ife tikufuna chitukuko basi zimene mukulankhurazo sizikumveka bora chakwera ndi anthu anuwo
Zoona Peter atupele si ozikonda vuto ndife amalawi ovota mitu inawuma mtanyiwa kalindo bakili TV Peter atupere ndi ena ofunila Malawi zabwino alankhula za mcp koma sitinave. Panopa mukuona mcp ikugwirisa ngongole and ikugawa ndala and amalawi tawona mumene wafera chilima ndi abale athu koma still tikusapota bomalo amalawi tili ndivuto loganiza bwino. Munthu kuti mumuziwe kuti zeru alibe boma kuyakhula mwamatama kuzikona kupereka ndalama kuti anthu amuvotere
Iwe ukuyankhulawe ndi Peter muthalika kapena Atupele akupatsa chani chitsiru iwe kagwade wekha kupepera eti kuzolowera kunyambita nsapato .Khala pansi asiyire anthu ozindikira aziyankhula. IWE SINNENERI WA ANTHU AWIRIWA
Musalimbane ndi peter komanso Atupele ...pakampeni paja amaneneratu poyera kut MUSAVOTERE MCP ...nde anthu sanamve akut umafuna change...This is the change..the change can be positive or negative....asiyeni a MCP alamulire chifukwa ndie zimene munavotera...tichimine kaye a malawi...Pena Mulungu amapanga zoti anthu aphunzire kwambiri
Zoonad anthu amageya mwano kwambiri akuti tisithe zithu ndie zasithaditu
Koma boss ndiiwe ozindikira koopsa keep it up, mavutowa tinachita kubwelesa tokha. Anatiuza ndipo anatilangiza koma kusanva ndipo ananena Peter Muntharika kuti mukupanga inuzi akubwerawo muona Nyekhwe. Lero ndiizi kaaah
Good comment. Truly these two Gentlemen are real country men.
Zikomo amwene papani Mr pita ndi Tupele muzitikhululukila zoona vuto ndi ife ndithu🙏🙏🙏🙏🙏
Good correction sir ❤❤
Zoona brother uyu walankhura odiyo iyi ndi mbudzi ya Mano kunsi, ndipo samadziwa chomwe amanena. I love you u ndipo mau anga mwandinenera ndinu❤❤
More fire mr D takunyadilani kwambiri mwalankhulabwino
Kmaso number one ozikonda ndameneo akuyakhulayo waku mangochiyo ndamene ali adyela
Abwana osaganiza ndi inuyo don't trust akunena zoona apeter ndi atupele ndi anthu osathandiza anthu akulephela kutuluka kulimbikisa anthu boni kalindo akulimba naye ekha sakumuona mzawo uja chihana akuyenda kumalankhula pa steji dziko ndi kumamva koma peter ndi atupele ndipamene kubisala iwo akuti aopa kuphedwa ndi mcp kodi mufuna muzangonyamulilidwapo pampandopo muzidya misonkho ya amalawi
Ase wayankhura bwino mmanja mwako 🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🤝🤝🤝🤝🤝🤝
Ameen Iweyo mulungu akudalisene moyo ukuyangula zabwino mau amuna asitero amavuna dala athuwo
Zoona kuyankhur mosacheuka bwana komaso chilungamo anthuwa tithanenao tokha Peter and atupele asiyeni ananyozedwa ngat alibe mitu ngat alibe uzimu asiyen imfa ya saulosi chilima yaripweteka Ndye mikono yanthu tikutsamir kwa a2 awawa Ndye njara ikatikhaulitsa ndipamene tingapite pa mseu
Ndiye ngati akutero kut samatengapo gawo nkwabwino asayime asiye omwe angamathandizire kumamenyanawo nkhondo bcz we are in democracy no words kupembezana
Ndipo Muthu ndiobvuta ndithu tinya ndizomwe tinkafuna ngati ana akhanda oti nkhongelesiyo yabwela lero hahahahaha
Moti inu mwavotelaso mavuto aaaa zikozeni nokha kumeneko Peter atupele siwolakwa
Thanks D phiri
Auzeni ana amahurewa,
Ndiomwe atifikitsa pa manyiwa.
Bu shit, anthu amanyi amenewa. Azimuloza Chala ntambo.
Mai woputsa iwe umafuna azingoyenda wamba iweyo siukuziwa kuti mcp ili ndi chiwembu chachikulu kodi mcp yakutuma ? Ugaluwako
D.phiri wanena zoona,,,ife tinalakwisa
This is true boss,, atupere or munthalika asiyeni mavutowa ndiifeyo amalawi kusamva lero ndi izi
Pure answer
Ndipo APM anatiuza kut mukavotera MCP muzalira, lero nzimenezi munkafuna anyamata paja, ulemu wanu akulu mwayankhula bwino kwabas,
Izi nde ndizoonad osapanga complain pa anthu awa ayi vuto ndamene anachotsa dpp kukavotela mcp
Akulu inu mulibe zelu ndipo zomwe mukunenazo chipani cha dpp udf ngati akhala ndimaganizo akowo basi dpp yapita sizalowaso boma ndiwe chisilu basi dpp ndaituluka kuli zitsilu ndichifukwa chake mukongoluza zisakho shupit
Ndipo Apm ndi atupele 2025 anatisiya tikhaule tinapanga chipongwe tokha
Peter wakalamba sangathamange osazemba ai ndipotu inuyo mukakakamila peter ndiye zolowa boma iwalani ndithu
Chachikulu ife amalawi sitikufuna kukhutitsi pazimene Dr piter amatipangira ndiye anthu athira kuwiri
Mcp 2025 boma cadet akhaula ndipo iwe cadet ukanalila musobva😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅
Powerful 👊
Uku nde kuyakhura mopanda nzeru😅😅😅😅😅😅 kod adpp abalalika eti
Musiyeni uyo wadya banzi walandila ndalama.Mangochi singavotele mcp ai
Ayi ndizakale zomwezija ndikwabwino azilankhulapo asakhale zii
Muiyu afuna kukoza mbili yachakwela kodi Apm sadanene kuti mudzaona nyenkhwe atupele ndi apm sindikuwapeza ndi mulandu ovulala ife bandi akamange atupele ndi apm ndizoona
Good correction
Mr phiri .mwandizizilitsa mtima mwarankhura bwino kwambiri.nditamva vn yonyodza ija ineyo mtima unawawa
Sitinva ife Anthony awa Antananarivo don't vote ❎ theme ife makan
Mungobvutika boma ndilomweli ndipo sitikusintha apa mungotaya nthawi kulongolola palibe chomwe mungachite
Kagwileni ntchito mupeza nalondalama boma lachakwera koma mulesi alipamavuto
Wa mcp ameneyo akufuna kut a peter ndi atupele atuluke akawaphe a mcp wabunya
Alomwe muli patchito chakwela ndukuzani pano simungamuchotse mulakhula mutopa chitsazo ma by election mukungoluza daily
Peter amapanga kampeni
Ndpo zoona bro mwayankhula bwino
Bodza len leni ifetu sitikupanga complain chifukwa chilungamo tikuchidziwa inu izi mukuzitenga kut
Tsono mukuona ngati mcp ingachoke boma ndi kutukwana kwa ma akitivisinu anthu muli ndichibwana kwabwasi tiye nazoni mukhala ku kotsutsa konko
Iwe usabvutike anthu sangabvoteleso dpp kulibe ndipo ndukuuza pano dpp sizabwelelasi boma pezani zina zochita izi mutayanazo nthawi
Mau akulu akoma akagonela
Kusankha kwanu a Malawi , muziwona konko. Iwowo analemela kale awa ,mabvuto ndife
Chisilu ndamene anavotela mcp yo ine ndinavotela my lovely dad Mr p ndiposo pano it's my vote no matter wat
Walandira ndarama za mcp amenyo
Zonadi. Zimenez
O
❤❤❤
Choka ukuyankha zosaveka azako akuti kampeni osati zimene mukuyankha ndizina zimene akunena aazanu ndi kampeni
Ndare za nepotism ku Malawi we need federal system of government otherwise no change to people that's why Malawi is the poorest country in the world.
Malawi ngakhale wuyifele ,aaa ,chilima anapita ,nkhani yake kufera Malawi . Malawi si woufela
Peter muthalika ndi nkhalamba munthu oti akuziyipitsira yekha pomwe akhala angapange kampen
Tiyeni tingoyang'ana kutsogolo
Munthu amadikira chopereka church kuti akhale ndi ndalama ndie mumaganiza kuti angalamulire dziko
Lero ndi izi dziko latsala masanza okhaokha
Chakwela ndi wamizala wamanyi
Zoona man, mai awa ndi hule wachabe
Sanayankhule di bwino bambo amene aja Peter ndi atupere komanso former president Bakili Muluzi anayankhula po za mcp koma anthu kusambva lero ndi izi nde akamayankhula aziyamba aganuza kaye osamangobwebwetuka
Kusamva kwathu. Don't put the blame on Peter and Atupele. Tinavota tokha
Iyeyo akuona ngati a opposition angokhala? A Peter ndi atupele TU siopusa akumuwelenga kaye chakwela yu AKUFUNA amlize kaye uchitsiru wakewo kenako adzuke koditu campaign sinayambe kukhala zinthu a opposition mukuwanyozawo simuwafuna
Tinalakwisa tinavotela ena ndiyekuti tisadzudzule? Usanena kuti musakonze ayi ,,wa Aodio sanalakwise,,,tisawagwadile Oro kuwachonderela,,Iwo nde azamwe mkaka,,
Choka mboliyako...mkamwa mopindikamo...
Kma iwe ngati ndiwe mukazi ndiwe hule wangoifuna Boro yaminthuyo asa😊
Ulemu wanu guys mwayakhula bwino kwambili mulungu adzikhala nanu thawi zose onyazao asiyeni azinyoza amachita kutumidwa ndi chakwela kuti adzisusa athu akayakhula chilungamo chachikulu tiyeni tiike zise m, manja mwa chauta akuva kulila kwathu chakwela akadapanda kulamulila dzikoli mukanakhala khondo yoopsa kwambili koma mulungu adalola kuti kutelo kuti ukulu wake uonekele 🙏🙏
Amene uja machende ake ndipo ozikonda ndi iye uja ndi chakwera wakeyo
Ndi mbuzi imeneyo mutharika ndi atupele ndi sogolo la dziko lamalawi
Koma amalawi tilindimavito, chonyasa chija chayamba kuoneka chabwino kkkkk akangolowa adadi. Muzayambe kunenaso kuti bora chakwera
Tinawakana amapha ma albino amenewo asiye akalamba panopa sitikumvako kuti agwira ziwaro za anthu boma la peter linalibe security ndiposo wakalamba wapume zina mumangonama mulizambiri mu malawi panopa tikuwona zachilendo kale kunalibe ngati ndikukwera kwazinthu si malawi yekha ife tikufuna chitukuko basi zimene mukulankhurazo sizikumveka bora chakwera ndi anthu anuwo
Opusa
Gulu la mahure opanda mzeru ndimanena aja ndi m'modzi mwaiwo ndiweyo.
Hule
Ndi munthu opepera iyeyo ngati wapatsidwa ndalama azingodya
Amai amene aja atumidwa inu satipusise ife eetu ndpo alikomweko kwachakwerako
Kma ndiye akuchita kuonekadi kuti awapatsa kenakake chifukwa nde akulubwalubwatu
Ndiwekape munya 2025 bomasitokusintha
Ndie ngati ali ndi mantha asiye ndale kuti akhale moyo wautali umene akuufunao
Watiyakhulila mwene
Mwayankhula bwino kwambiri
Zoona Peter atupele si ozikonda vuto ndife amalawi ovota mitu inawuma mtanyiwa kalindo bakili TV Peter atupere ndi ena ofunila Malawi zabwino alankhula za mcp koma sitinave. Panopa mukuona mcp ikugwirisa ngongole and ikugawa ndala and amalawi tawona mumene wafera chilima ndi abale athu koma still tikusapota bomalo amalawi tili ndivuto loganiza bwino. Munthu kuti mumuziwe kuti zeru alibe boma kuyakhula mwamatama kuzikona kupereka ndalama kuti anthu amuvotere
Komanso umuuze kut watikwana
Muuze chimbuzi chimenechi mmesa amakuuzani kusamva kwani
Ndipo big amai amenewa ndi chimbuzidi zedi Amai opanda nzeru
Zaka 84 angathamange.? Anthu osazindikira inu Peter akanangotuluka tsiku limodzi mukuganiza khansala wa DPP akanaluza? Tulo basi
Nzeru ulibe
Iwe ukuyankhulawe ndi Peter muthalika kapena Atupele akupatsa chani chitsiru iwe kagwade wekha kupepera eti kuzolowera kunyambita nsapato .Khala pansi asiyire anthu ozindikira aziyankhula. IWE SINNENERI WA ANTHU AWIRIWA
Asiye ayankhe okha
A dpp mbuzi yagalu iwe ukuyakha
Tsono iwe wadya banzi ya pitala munthu wadyewa uku one kuziro 2025 mukunya chakwera bomaaa iwe mulomwe mwachepa achewa ndayao atumbuka simuwatha komaso ozindikila alomwe ena Asari Ngati iwe samuvotera pitila DPP yatha Palibe akuifuna tanganizani Mangochi zikumvekanso Kuti mwina pitala akhoza Ku votela chakwera😂😂😂😂😂😂
Abwana osaganiza ndi inuyo don't trust akunena zoona apeter ndi atupele ndi anthu osathandiza anthu akulephela kutuluka kulimbikisa anthu boni kalindo akulimba naye ekha sakumuona mzawo uja chihana akuyenda kumalankhula pa steji dziko ndi kumamva koma peter ndi atupele ndipamene kubisala iwo akuti aopa kuphedwa ndi mcp kodi mufuna muzangonyamulilidwapo pampandopo muzidya misonkho ya amalawi
Inutu ndiye munyee, mukhaule agaluu Inu.