Interview ndi Norman Chisale

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 5 фев 2025

Комментарии • 433

  • @Catherinesmart-xk4zx
    @Catherinesmart-xk4zx Год назад +8

    Chisale ndimunthu wabwino kwambiri wamanga ma church wachita zambiri Ambuye akudalitsen achisale long live

  • @RuthNankumba-ux3sw
    @RuthNankumba-ux3sw Год назад +22

    Big up Norman Chisale ,I love your courage 🔥 Ambuye apitilize kukumenyeran nkhondo ,,,I'm one of your supporters

    • @NzeruDesign-ut1go
      @NzeruDesign-ut1go 11 месяцев назад +2

      Ndpo nthawvyamayankho ikubwela big tipanga zobwezera ntoporao

  • @paulgodfrey3361
    @paulgodfrey3361 Год назад +10

    Leah you the best journalist...well done to Me Chisale

  • @mengokumwenda3832
    @mengokumwenda3832 Год назад +25

    The lady was carefully selected to handle this interview am impressed with how she has handled this heavy interview. Professional indeed

  • @ChristinahNkwanda
    @ChristinahNkwanda 4 месяца назад +1

    Norman ooooye.Please Please please Mr N Chisale keep it up God will help help you, always pray, praise him Amen Amen Amen

  • @hectortambuli605
    @hectortambuli605 Год назад +4

    Great man Norman Chisale. Oceans of luv to you and your family.

  • @LetsSeePlaces43
    @LetsSeePlaces43 Год назад +11

    Interviewing a well trained professional soldier should be different with interviewing a well trained professional economist💪🏾💪🏾Bravo snipper Norman Paulosi Chisale🤣🎉🎉💥💥

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 Год назад +12

    Chisale akumva zowawa chifukwa cha anthu ansanje but Chisale is the best Man in Malawi he spend his money to help the orphans and community, God bless you always and protect you Mr Chisale.

    • @AngellahKunsanama
      @AngellahKunsanama Год назад

      Zoonad ol evn Ines zimandiwaw, km Amalawi if nsanje😢

    • @Homeofpeace321
      @Homeofpeace321 Год назад

      @@AngellahKunsanama amalawi amamukonda munthu akafa, that's why dzikoli lili lobwerera mbuyo,

    • @AubreyKennethchingamba-gq6et
      @AubreyKennethchingamba-gq6et 6 месяцев назад

      Titakhala ndi anthu 20 nziko lino ngati Mr Chisale Malawi atha kusintha I proud of you Mr Chisale ndimakunyadilani chifukwa chakulimba ntima kwanu

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza5802 8 месяцев назад +6

    Komano pa point ya human rights Peter Muthalika he really respects

  • @matembanevermind-po3me
    @matembanevermind-po3me Год назад +1

    Gud interview love you questioner and Mr interviewer Norman

  • @mijerimasiye7310
    @mijerimasiye7310 Год назад +8

    Azodiak tamakhalani ndi ma bottle amadzi mukamapanga interview ndi anthu please

  • @JamesKamanja
    @JamesKamanja 7 месяцев назад +1

    God bless Mr chisale komano mokupemphani ndithu pepani uyu akufuna kut mumukhululukileyu imvani kulila kwake kut ukulu wayehova ukhalebe pa inuyo yesu anat muwakhululukile chifukwa sakuziwa chimene akuchita
    Musaiwale kut munthu payekha alibe vuto koma satana akamulowa amapangisa munthu kuchita zimene choipa chili mwa iyeyo chikufuna please ndikuziwa ndithu ululu ndi ochuluka kwambili koma khululukani ambuye apitilize kukupasani moyo wamphanvu madaliso avumbebe kut wamasiye apeze popumila

  • @JohminMatick-c9h
    @JohminMatick-c9h Год назад +1

    Msilikari adzakhare msilikari mpaka kare. Big up bro N. Chisare❤❤

  • @thomluciouss7360
    @thomluciouss7360 Год назад +13

    The one who talk the truth doesn't fear and it's really true that the truth pains big up Mr Chisale

  • @indiAisha-q2o
    @indiAisha-q2o 25 дней назад

    Ambuyechonde dalitsani achisale, chifukwa siolakwa chonde ambuye❤❤❤

  • @JosephKavalo-f5q
    @JosephKavalo-f5q 14 дней назад

    Keep it up umakwana Norman chisale

  • @cosmasmaya-z6w
    @cosmasmaya-z6w Месяц назад +1

    ulemu wanu bwana mr chisare big pp

  • @DairesBaina
    @DairesBaina Год назад +4

    Chisale your number 1 well trained soldier

  • @GodfreyMphaya
    @GodfreyMphaya 11 месяцев назад +1

    Bravoooo big man chisale i salute you

  • @CresentShaba-k3q
    @CresentShaba-k3q 11 месяцев назад +2

    Mr Chisale isn't my relative but ndawamvesa he is a real soldier, BRAVO CHISALE. BULL Sheet kayun.

  • @EmmanuelKamwagha-m5u
    @EmmanuelKamwagha-m5u Год назад +2

    Courage muli nayo...komano kusa kululukako kuchita kuoneseratu kuti muli ndi mtima wakupa

    • @happyzumatembo2174
      @happyzumatembo2174 Год назад

      😢 or uli iweyo kut munthu akunamizele mulandu wa murder. Uthakumukhululukira?

    • @DouglasDazuKamwendo
      @DouglasDazuKamwendo 7 месяцев назад

      Sukudziwa chomwe ukunena, sukuona kuti Chisale amuzuza popanda zifukwa?

  • @ThomasKawina-o5n
    @ThomasKawina-o5n 4 месяца назад

    Ana achepa ulemu wanu bwana chisale 👏👏👏👏👏👏

  • @falayichitsotso5371
    @falayichitsotso5371 Год назад

    Mr Chisale I hear ur story it's very bad and am very happy with u ustand with God dnt give up mukuyakhula kwako mulungu akumva ndipo mulungu amalora Kuti ana Ake andutse mmavuto ndicholinga Choti ukulu wake ukaonekere God will be with u mwaiwe muli usogoleri

  • @LevisonSimssimbeye
    @LevisonSimssimbeye Год назад +1

    Watching from zambia

  • @AlfredSaulosi
    @AlfredSaulosi 25 дней назад

    Zoona zake zake za Norman Chisale.Kunena yekha mwini wake.

  • @NodiceChakwala-tz5gg
    @NodiceChakwala-tz5gg Год назад +1

    great mtolankhani , kip the fire burning girl

  • @Edgar.RatheilKapalamula
    @Edgar.RatheilKapalamula Год назад +5

    Akuzuzika ngati yesu chisare ndi Good Samaritan athu abwino amazuzika

  • @blessedmichael5124
    @blessedmichael5124 Год назад

    I like sir Norman Chisale he's been good in speech osamaopa pa chilungamo

  • @dumisanimoyo3152
    @dumisanimoyo3152 Год назад +1

    Chisale usatiuze kuti akhale wo opa mulungu suyo chakwera wo opa mulungu akutizunza

  • @jumazabula2908
    @jumazabula2908 Год назад +1

    Definition of having readership, fire 🔥 chisale

  • @mordecaikachale2497
    @mordecaikachale2497 Год назад +10

    I like the energy tht u hv Mr chisale as a soldier...big up❤

  • @kannockRichy
    @kannockRichy Год назад +4

    Mr chisale attitude in this interview shows kuti bambowa ndionama..😂

    • @magdalenachipeta2394
      @magdalenachipeta2394 Год назад

      Ndipo sukunama uku ndiwabodza auze mtundu wa a Malawi kuti ma billions a chuma anawapaeza bwanji osamangobwebweta zopanda phindu, kufuna anthu akumvele chisoni.

    • @DouglasDazuKamwendo
      @DouglasDazuKamwendo 7 месяцев назад

      Ndinu mabulutu guys

  • @ndalamaandrew
    @ndalamaandrew Год назад +2

    Koma Chisale uyuyu eeeeeeh 🙌🙌🔥🔥🔥

  • @KennedyBanda-p9x
    @KennedyBanda-p9x 17 дней назад

    Matama.ndarama zakuba mbara ziku ikuru mmarawi chisare komaso pitara kabambe mwAnaveka chaponda mutharika bingu ndege supar jet

  • @GodfreyMphaya
    @GodfreyMphaya 11 месяцев назад

    One thing i like this guy he talk straight

  • @ChifundoSaikonde
    @ChifundoSaikonde 29 дней назад

    God is great chhisale

  • @SifoMvalaudza
    @SifoMvalaudza 2 месяца назад

    Big up bro pitirizan ntchito

  • @AcacioWilsonPhezula-t8l
    @AcacioWilsonPhezula-t8l 6 месяцев назад

    Wn am the of them amene ndimamva kuwawa ndikamva kuti mwamangidwa,sinakumane nanu ,sitinayankhulako koma zimkandiwawa koopsa

  • @Chief-Phungwako
    @Chief-Phungwako Год назад +1

    This was nice chisale seems a good one though ndindale

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki 8 месяцев назад +1

    Mr Chisale i understand your pain please please firgive him isbus for your own good, you saud you are Christian our master jesus taught us to forgive those who do us wrong before we ask to be forgiven

  • @AndrewBiliat
    @AndrewBiliat 7 месяцев назад

    Big up Soldier

  • @SolomoniTiyesi
    @SolomoniTiyesi 6 дней назад

    Ifee that's straight tolk and being honest kuti a chisale akuyakhula mopanda chigamba ndazikonda kwambiri and please kaimeni bwana chisale

  • @chawagondwe6404
    @chawagondwe6404 Год назад +1

    Those who are saying bravo chisale you need special prayers..this guy stole our money tax payers money....he accumulated wealth within a short period of time....hotels cars houses etc he is backing himself apa he can't admit it.....and you are busy kumunyadira 😮Malawi ndife ogona too much.....he is lucky he is outside otherwise he belongs inside

  • @Liam-ky5cu
    @Liam-ky5cu Год назад +1

    Bravo Bravo 👏 😁 Soldier...

  • @RodreckChisoso
    @RodreckChisoso Месяц назад

    Love one chisale

  • @MisheckChangata
    @MisheckChangata 7 месяцев назад

    Great man ,i like u

  • @Maxielyies
    @Maxielyies Год назад +6

    Powerful talking and intelligent, proud of you @Norman Chisale

    • @henryhenry6632
      @henryhenry6632 Год назад

      Intelligent ya ku machende amalawi mapanga support zingawenga bwanji, kupusa

    • @yamikanijames6915
      @yamikanijames6915 Год назад

      Mukuyamikila chisale man? After all what he did now you're embracing his work.... don't you know people lost trust in DPP and one of the biggest reason ndi iyeyu

    • @LetsSeePlaces43
      @LetsSeePlaces43 Год назад +2

      People never lost trust with DPP...anthu tinanamizidwa kuti tizaona zabwino...pano misozi yatha mmaso yayamba kutuluka ndi misozi ya magazi chifukwa Cha bodza la CHAKWERA ndi chilima.

  • @pempherokatakwala6451
    @pempherokatakwala6451 Год назад

    Norman chisale iweyo ndi number 1 moto kuti buuuuu!!

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr Год назад +2

    Ndamva chisoni pokumva nkhani yanu bambo Chisale 😢 koma chilungamo chilipo ndipo momwe mwadutsa inumo enanso adutsamo ili ndidziko. Abale whyyy a police athu mmatero, olo ndiliineyo ndingaophwezetu ndipo ndikanamizilidwa ndimakwiya kuposanso achisalewo 😂😂

  • @NkhumbuSichela
    @NkhumbuSichela Год назад

    😂😂😂 so in love with his courage 🤦🥰

  • @EUGINEMWADALA
    @EUGINEMWADALA 28 дней назад

    Ndinu ochenjere nkulu ndinudi nsilikali weniweni osazi njoka luzi tuziona panozi

  • @peterbyson6269
    @peterbyson6269 10 месяцев назад

    respect to you both you building Malawi in this interview ..

  • @paulgodfrey3361
    @paulgodfrey3361 Год назад +1

    Your the best Leah

  • @tisuhmakhwah7085
    @tisuhmakhwah7085 Год назад +1

    Kkkkkk ayayaya malawi tingogulisa tigawane dollar zo

  • @chifunirosaka9077
    @chifunirosaka9077 Год назад +12

    Soldier never die chisale more 🔥

  • @AngozoMalunga
    @AngozoMalunga Месяц назад

    Mbambande Mr chisale

  • @quintonmutume82
    @quintonmutume82 Год назад

    Dpp yangoyenera kubweler 💓💓🙌🙌

  • @AngellaAnge-p7x
    @AngellaAnge-p7x Год назад

    Keep it up Mr chisale

  • @EnelessBanda-x5n
    @EnelessBanda-x5n 2 месяца назад

    Aaa zaxiiiii kod kukhala msilikali ife tiope

  • @patrickjoda2165
    @patrickjoda2165 Год назад +2

    Mulungu akhale patsogolo basi Mr chisale Angoni

  • @GiftMeja
    @GiftMeja Год назад +1

    Komatu chisale ndye akumulakwla

  • @YohaneGauti
    @YohaneGauti 6 месяцев назад +1

    Bwana chisale ineyo ndikuti pepani kwambili pa zomwe munazunzidwa
    Ifenso timamvanso kuwawa

  • @paulvimbamvula9508
    @paulvimbamvula9508 29 дней назад

    Norman akadzalowa muboma yes... Azabwezera

    • @PromiseChombo
      @PromiseChombo 24 дня назад

      Hahhahahahhahahahah ndipo live azabweza ndithuuu

  • @YusufAjida-t8r
    @YusufAjida-t8r 3 месяца назад

    Mr chisale mulungu akudaliseni posamala Ana masiye ndipo akuonjezere zambili

  • @vitumbikocobysinyiza-5116
    @vitumbikocobysinyiza-5116 Год назад +1

    Big up Mr chisale

  • @MjombaMjuba
    @MjombaMjuba Год назад +1

    Akunama uyu, wakupha komanso wakuba, chitsiru chimangidwa chisiyeni, sakudziwa kuti apita kundende.

  • @chrisscapper-zw5rk
    @chrisscapper-zw5rk Год назад

    Bravo Mr Chisale

  • @SydneyRajab
    @SydneyRajab Год назад

    Leah , bravo 💪

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel2541 Год назад

    Haters will always blame you my brother just because all the enemies of APM can't be happy with your speech. Even the way this woman is interviewing you just shows that she is one of the haters because of this ( I feel bad and hate those ones who are blaming APM for useless things or political reasons and I handle him as my biological father) but no stress brother you're a real and very strong soldier and you're humble man otherwise stupid questions this woman was asking you if it was I, I would just fu....k off from that interview. Your character is a real good courage and discipline soldier and we love you and everything is going to be good

  • @paulmakaula4937
    @paulmakaula4937 Год назад +6

    Political prosecution has ever been in existence since our independence....please follow the rule of the law always! Clear conscious is the medicine...God is watching and will judge everyone right..

  • @DouglasDazuKamwendo
    @DouglasDazuKamwendo 7 месяцев назад

    Am watching this interview kachikenaso Norman Chisale yu ndi #1 kwa amene alipa chilungamo akudziwa kuti big wa ndi real man osangoti mwakati poti umadana naye.

  • @LingstonManjolo
    @LingstonManjolo 4 месяца назад

    Amalekano zikomo chifukwa Cha machezedwe anu ndi achisale mkazi odziwa kufusa ngati iwe thanks

  • @MikeGama-j6j
    @MikeGama-j6j Год назад +2

    Tikukuvesesani mr chisale.

  • @maonekedweDaniel
    @maonekedweDaniel Год назад +3

    Kma this interview must be repeated even pa wailesi , nice Leah keep on going more fire

  • @SolomoniTiyesi
    @SolomoniTiyesi 6 дней назад

    Leah malekano powerful katundu omanga ndi mawaya

  • @enipherphiri207
    @enipherphiri207 Год назад +2

    Chisale oopsya eeeee. Bible mmanja koma Bullshit pakamwa mbweee ashiii

  • @ChrissyThawani
    @ChrissyThawani 2 месяца назад

    Oh Kodi nsewu uja nza pita etiiii.....lozani zanu ife tione a china Boma ndi lomwelo

  • @magdalenachipeta2394
    @magdalenachipeta2394 Год назад +1

    1986 he was already working as a soldier but he is saying is 42 years old eeeeeish!!! 😂😂😂komatu munthuyu akuoneka ndiokakala mtima mayankhulidwewa atha kupanga zoophsya. He is saying kuti ndiopemphela koma akuti sangakhululukile aSteven Kayuni 😭😭 chonsecho amayenda ndi bible , mawu a Mulungu mwamunthuyu mulibemo.

  • @EUGINEMWADALA
    @EUGINEMWADALA 28 дней назад

    I have never liked u soldier but i feel your pain.

  • @williammaseko8542
    @williammaseko8542 Год назад +3

    He is very emotional and trying to run away from facing justice. No one accepts to be guilty in public and whatever is doing here is normal for suspects. 42years doesn't match with the way he looks unless he tells us kuti amasamba Nyanga.

  • @paulvimbamvula9508
    @paulvimbamvula9508 29 дней назад

    Chisale more fire

  • @lonjiekaselera9651
    @lonjiekaselera9651 Год назад

    The real legend khaaa wauuza ngamo

  • @NishaMakwiya-l1x
    @NishaMakwiya-l1x Год назад +1

    Koma poti APM ayimezo nde tasephana basi aaaa..mwachidure kumalawi ndare zithe

    • @DouglasDazuKamwendo
      @DouglasDazuKamwendo 7 месяцев назад

      Iweso khala chete mapazi opotokawo ngati milomo yako ikuyankhula mopotokayo

  • @johnsong7236
    @johnsong7236 Год назад +2

    chisale ndiozipopa mwachamba

  • @NovemberMmangathayo
    @NovemberMmangathayo Год назад +2

    Mbavaizi aaaaaa awonongachumachamalawikwambili

  • @MadalitsoNaluso
    @MadalitsoNaluso 11 дней назад

    Steven Kayuni😂😂😂😂

  • @HamisiPatrick-m6f
    @HamisiPatrick-m6f 18 дней назад

    Zoonadi tamakhalani ndimabotolo amadzi ameneyo chisale ndimunthu wabwino

  • @JuliusSantos-l7h
    @JuliusSantos-l7h Год назад +4

    This guy is some how mad

  • @lukainnocent5380
    @lukainnocent5380 Год назад +1

    mbuzi chisale ukuona ngati bambowakowo sangawine ameneyo wapha albino wakwa na

  • @shupikayintuwaluwa-5899
    @shupikayintuwaluwa-5899 Год назад

    Kkkkkkk aaa zoona. Msilikali kiching, amba chilungamo n how he's feeling with de way they r treating him

  • @samaxodala7587
    @samaxodala7587 Год назад +1

    Chisale💪💪💪🇲🇼🇲🇼

  • @JosephMussa-gz9co
    @JosephMussa-gz9co Год назад

    Nice interview

  • @Johnybegood260
    @Johnybegood260 Год назад +9

    This woman is brave

  • @Discar_mw
    @Discar_mw Год назад +2

    This was a hot 🔥 one lol 😂

  • @AndisonSaidiKhunjuh
    @AndisonSaidiKhunjuh Год назад

    Big up boss

  • @yusufqassim2020
    @yusufqassim2020 Год назад

    Ee achisale anapsa mtima💪

  • @kondwamlungu8384
    @kondwamlungu8384 Год назад

    Yeah azayakha zomwe amamangila Norman chisale

  • @SalomyKamnkhwani-c7l
    @SalomyKamnkhwani-c7l Год назад

    This lady 🙌🙌🙌🙌🙌

  • @Gorilla-k8e
    @Gorilla-k8e Год назад +2

    😂😂😂😂😂😂😂moto kuti buuuuu L malekano umatimilila koma bwinotu akubandula mbakela bwana ameneyo 😂😂😂😂😂

  • @KennedyBanda-p9x
    @KennedyBanda-p9x 17 дней назад

    Adayamba kare kuba amarawi.ndibwino kuba