Размер видео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показать панель управления
Автовоспроизведение
Автоповтор
That time ziko likuyenda bwino,, atola nkhani amasowa chofusa
Akatundu atse
The leader , the greatest
Uyu adali munthu
Mr president ❤❤❤
Nthawi imeneyo...atolankhani amasowa chofunsa chifukwa chokhuta kwambiri nsima
Kkkkkk 😂😂😂 uli ndi vuto 😂
Journalists opoira munthu azipumako asapite ku holiday
A very foolish question,so u want the president to report to you
You are the one foolish. Anthu ngati Inu ndi amene mumapepeletsa president. President ndi servant wa Anthu osati bwana wawo.
When MBC was worthy to watch
I wish if that question for pirilan from zodiak to ask chakwera now about civil cevants salary as of now
A man with good leadership, bingu may his soul rest in peace
mmalawi ngati anataya muthu wolemekeza athu onse posatengera ndale , sitizapezaso wina, onse amene anatenga gawo pa imfa ya legend ameneyi adzakayakha ngati sadalape, ine ndinagwirana nawo mzanja atabwera kuzapephera pa nguludi parish ku chiradzulu.mzimu wawo uwuse ndi mtendere.
Big man ameneyu anayenela kukhala life president
Ndipo zenizeni
Anayaambitsa trabalism in Malawi.
Iii8ii0lp@@HellingsMughogho
This is time i saw my my parents never struggling to put food on table for me
Pro bingu anar mtsogoleri wamphavu mu ulamuliro democracy anariso okondedwa ndi anthu.
Awa adali machine mu kaganizidwe ndithu... MHSRIP
Bingu anari Genius ❤
This was a heroic speech spoken by the late president of the Republic of Malawi that was a warm heart of Africa before which is now a hell of Africa
We miss you
People love the dead....when alive you hate hi
Mtolankhani koma anakuwidwa😂😂😂
Munthu Wamkulu
May his soul continue 🤞 rest in peace 🕊️🕊️
Bingu anali Chawulere chamulungu kumtundu wamalawi
Bingu,, the greatest president seconded by Kamuzu,
Uyu nde anali president watsogolo mbili yonse yamalawi
Continue rest well. We didn’t understand you 🙏🏾
Continue resting in peace Ngwazi
Nthawi imeneyo sugar ali pa K450 1 kg eeeeh..... RIP Dr Bingu
Will forever miss this man..may his soul rest in peace😢
Madala Bingu munthu wachikulire.tikukusowani ndi ulamuliro wanu.anthu oipa anatisaukitsa.tidzakusowani mpaka kale kale
Akanakhala kuti nthawi amabweza m'buyo,akanazizwa pamenepo dziko liliri lelo...
mulungu amudalitse bingu
Hamble president pano tingomangidwa tikalankhula zakukhosi
Awa adali katundu wabwino kudziko laMalawi koma pokhala Mulungu salakwitsa, tizingoti rest in peace mfumu
Anapulumutsa a Malawi for 9 years
Dickson Kashoti wa congress😂😂
Bwana pumani mumtendere dziko munaliyendetsa bwino heavy
Bingu was just lucky economy padziko lapansi inali bwino. Koma anali wakuba just like ma president ena. Anayambitsaso tsankho mmalawi muno. Komaso anapha anyamata 20plus mu jully. Plus Robert Chasowa. May their soul rest in peace❤
Ngati ankaba koma mumakhuta,Bakili anapeza economy ili bwino kwambiri koma anapanga chiyani chanzeru.
Bingu anali president wamphamvu ndipo amathandiza amphawi aliyense nthawi yake anali ndichakudya pakhomo. Otsati awatikuwaona pano
For the love of late Bingu
Kunena zoona umbuli wathu wakumalawi ndagoma nawo kumangokuwa zilizose
Uyu mulungu apase chilango
Mulungu tatidzutsireni uyi ife tikupasani chakwera
The right President ❤
rest in peace Dad
Big hand to the late Bingu wa Mutharika
This man was having charismatic power
This was not right intimidating the journalists
I loved this guy since and nothing has changed up to date
Ndakunyandilani koma mudzimuwanu wupumemumtendele
True meaning of leadership
Pamene lero atola nkhani akuchita kuopa Galu uyu alipoyi
Media freedom was suppressed 😢
This man was indeed ordained by God to lead us, when God is in control no wonder hunger, outbreaks are nowhere.
the great leader and we miss you Dad may your soul rest in peace.
Bingu anali omvesesana ndi anthu ake
Uyu analiphuradi zikoli pa moto😢
DPP inali ndi mbuli za ma supporter
Mkuluyu amkakondedwa hvy eeeeee😂
The presidential
A leader very humble....May your soul keep resting in peace
Eeeee km akulu awa tidzawasowa ndithu
RIP BINGU
Osati zisilu zili lerozi aaaaa mbala zenizeni
Munthu wamkulu ,mzimu wake uuse mu mtendere
Gk
Munthu wankulu kwambili tidzakusowani😢
Chonchi nkunali ulamuliro wamtendere, koma atolankhani apa sanagwire ntchito yawo mwamtendere.
Visionary Leader
Sitinamuvetsetse BINGU
Continue resting in peace Dad ❤❤❤
Anali Amfumu AWA osapha Anthu ai
Awawa anali machine a three phase😢
anali wakulu
Ameneu an2 amachta manyaz
Wina adaiwonera patali kungoyankhula chingerezi onse ziii
😂😂😂❤
My vote
Eeee mn
Hahahaha
Great speech
he was wise man and may his soul rest in peace.
Kkkkkk
We're still missing this great man
GOAT
Koma zidaliko
Mathers
uyu anali Munthu guys
Kmkmm
Shasha kwambiri ❤
He was a great leader
Mzimu wake uwuse mundendere
Muimaso madala
Legend never die
Mumakwana dad
Uku kunali kuntunda osati zibwana
Legends never Died
M'makwana
Bingu
Bingu😢😢
kugaya
That time ziko likuyenda bwino,, atola nkhani amasowa chofusa
Akatundu atse
The leader , the greatest
Uyu adali munthu
Mr president ❤❤❤
Nthawi imeneyo...atolankhani amasowa chofunsa chifukwa chokhuta kwambiri nsima
Kkkkkk 😂😂😂 uli ndi vuto 😂
Journalists opoira munthu azipumako asapite ku holiday
A very foolish question,so u want the president to report to you
You are the one foolish. Anthu ngati Inu ndi amene mumapepeletsa president. President ndi servant wa Anthu osati bwana wawo.
When MBC was worthy to watch
I wish if that question for pirilan from zodiak to ask chakwera now about civil cevants salary as of now
A man with good leadership, bingu may his soul rest in peace
mmalawi ngati anataya muthu wolemekeza athu onse posatengera ndale , sitizapezaso wina, onse amene anatenga gawo pa imfa ya legend ameneyi adzakayakha ngati sadalape, ine ndinagwirana nawo mzanja atabwera kuzapephera pa nguludi parish ku chiradzulu.mzimu wawo uwuse ndi mtendere.
Big man ameneyu anayenela kukhala life president
Ndipo zenizeni
Anayaambitsa trabalism in Malawi.
Iii8ii0lp@@HellingsMughogho
This is time i saw my my parents never struggling to put food on table for me
Pro bingu anar mtsogoleri wamphavu mu ulamuliro democracy anariso okondedwa ndi anthu.
Awa adali machine mu kaganizidwe ndithu... MHSRIP
Bingu anari Genius ❤
This was a heroic speech spoken by the late president of the Republic of Malawi that was a warm heart of Africa before which is now a hell of Africa
We miss you
People love the dead....when alive you hate hi
Mtolankhani koma anakuwidwa😂😂😂
Munthu Wamkulu
May his soul continue 🤞 rest in peace 🕊️🕊️
Bingu anali Chawulere chamulungu kumtundu wamalawi
Bingu,, the greatest president seconded by Kamuzu,
Uyu nde anali president watsogolo mbili yonse yamalawi
Continue rest well. We didn’t understand you 🙏🏾
Continue resting in peace Ngwazi
Nthawi imeneyo sugar ali pa K450 1 kg eeeeh..... RIP Dr Bingu
Will forever miss this man..may his soul rest in peace😢
Madala Bingu munthu wachikulire.tikukusowani ndi ulamuliro wanu.anthu oipa anatisaukitsa.tidzakusowani mpaka kale kale
Akanakhala kuti nthawi amabweza m'buyo,akanazizwa pamenepo dziko liliri lelo...
mulungu amudalitse bingu
Hamble president pano tingomangidwa tikalankhula zakukhosi
Awa adali katundu wabwino kudziko laMalawi koma pokhala Mulungu salakwitsa, tizingoti rest in peace mfumu
Anapulumutsa a Malawi for 9 years
Dickson Kashoti wa congress😂😂
Bwana pumani mumtendere dziko munaliyendetsa bwino heavy
Bingu was just lucky economy padziko lapansi inali bwino. Koma anali wakuba just like ma president ena. Anayambitsaso tsankho mmalawi muno. Komaso anapha anyamata 20plus mu jully. Plus Robert Chasowa. May their soul rest in peace❤
Ngati ankaba koma mumakhuta,Bakili anapeza economy ili bwino kwambiri koma anapanga chiyani chanzeru.
Bingu anali president wamphamvu ndipo amathandiza amphawi aliyense nthawi yake anali ndichakudya pakhomo. Otsati awatikuwaona pano
For the love of late Bingu
Kunena zoona umbuli wathu wakumalawi ndagoma nawo kumangokuwa zilizose
Uyu mulungu apase chilango
Mulungu tatidzutsireni uyi ife tikupasani chakwera
The right President ❤
rest in peace Dad
Big hand to the late Bingu wa Mutharika
This man was having charismatic power
This was not right intimidating the journalists
I loved this guy since and nothing has changed up to date
Ndakunyandilani koma mudzimuwanu wupumemumtendele
True meaning of leadership
Pamene lero atola nkhani akuchita kuopa Galu uyu alipoyi
Media freedom was suppressed 😢
This man was indeed ordained by God to lead us, when God is in control no wonder hunger, outbreaks are nowhere.
the great leader and we miss you Dad may your soul rest in peace.
Bingu anali omvesesana ndi anthu ake
Uyu analiphuradi zikoli pa moto😢
DPP inali ndi mbuli za ma supporter
Mkuluyu amkakondedwa hvy eeeeee😂
The presidential
A leader very humble....May your soul keep resting in peace
Eeeee km akulu awa tidzawasowa ndithu
RIP BINGU
Osati zisilu zili lerozi aaaaa mbala zenizeni
Munthu wamkulu ,mzimu wake uuse mu mtendere
Gk
Munthu wankulu kwambili tidzakusowani😢
Chonchi nk
unali ulamuliro wamtendere, koma atolankhani apa sanagwire ntchito yawo mwamtendere.
Visionary Leader
Sitinamuvetsetse BINGU
Continue resting in peace Dad ❤❤❤
Anali Amfumu AWA osapha Anthu ai
Awawa anali machine a three phase😢
anali wakulu
Ameneu an2 amachta manyaz
Wina adaiwonera patali kungoyankhula chingerezi onse ziii
😂😂😂❤
My vote
Eeee mn
Hahahaha
Great speech
he was wise man and may his soul rest in peace.
Kkkkkk
We're still missing this great man
GOAT
Koma zidaliko
Mathers
uyu anali Munthu guys
Kmkmm
Shasha kwambiri ❤
He was a great leader
Mzimu wake uwuse mundendere
Muimaso madala
Legend never die
Mumakwana dad
Uku kunali kuntunda osati zibwana
Legends never Died
M'makwana
Bingu
Bingu
Bingu😢😢
kugaya