Comrade Ntanyiwa Pa Limpopo Fm Pa 26 Jan 2025 "Tamia Ja Wakaniza Kupakulitsa Beans"

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 4 фев 2025

Комментарии • 93

  • @StelliaKachaminga
    @StelliaKachaminga 9 дней назад +5

    Nice song bring more song zixiwawa achimwendo

  • @AlliePaipie
    @AlliePaipie 9 дней назад +15

    Komaso CLIFF CHINYAMA MUSAMAMUYIWALE NDI COMRED WATHU WAPHAMVU

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 9 дней назад +2

    Comrade cc...osamuiwara ...ndinthudi comrade Ntanyiwa...moto kuti buuuuuu🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @Rasheedissa-f3q
    @Rasheedissa-f3q 9 дней назад +7

    Ngani yose ndinanenna my Allah protect you mtanyiwa ndi bakili mulusi TV let's gethas her 🤛👎

  • @Ruthgomonda
    @Ruthgomonda 9 дней назад +5

    Komati Mr Tanyiwa inu ndi One 😅

  • @SamuelMoyenda-p6k
    @SamuelMoyenda-p6k 9 дней назад +1

    Tanyiwa umatiimilila mulungu azikudalitsa 🙏🙏🙏

  • @AndrewChaipa-ub5zu
    @AndrewChaipa-ub5zu 9 дней назад +3

    Abwanawa ndiopepela akulimbana ndi mwana Tamiya mmmmmm bwanji osolimbana ndi the DC . Zachamba.

  • @osmanmdala-uh7xw
    @osmanmdala-uh7xw 9 дней назад +2

    😂😂😂nanga titani nkulenga kwa Mulungu

  • @AndrewChaipa-ub5zu
    @AndrewChaipa-ub5zu 9 дней назад +2

    Dziko lamalawi silachakwela , ndi team yake we are Malawian .

  • @ChikondiBanda-x1o
    @ChikondiBanda-x1o 9 дней назад

    Mr Mtanyiwa inuyo ndikatundu more 🔥🔥🔥

  • @JosephMwadzama-f4u
    @JosephMwadzama-f4u 9 дней назад +1

    Welcome Mr ntanyiwa

  • @daviesweja27
    @daviesweja27 8 дней назад

    A Malawi kukonda mabodza, that's cheap politics, tiyeni tipeze zochita zina, much as things are not supposed to want them be, economically, socially, and every aspect of live, but we can not allow people in the name of activism push us to and from.
    We are grown up persons and come elections will do the needful!

  • @Halima-i4x
    @Halima-i4x 8 дней назад

    😂😂😂🎉🎉🎉 koma Tanyiwa ayi wati bwanji apa ngangnanganganga zaona koma ayi dzikomo iweyo 😅😅😅😅

  • @StalnLossan
    @StalnLossan 9 дней назад +4

    Mulungu azikutetedzani mwati segura mutu

  • @Tulihj
    @Tulihj 9 дней назад +1

    ❤❤

  • @OnexAliMwale
    @OnexAliMwale 8 дней назад

    Koma Amalawi ndinu opeperadi 😂😂 Tiyeni tizingonamizana

  • @FreddieKanyerere-u2z
    @FreddieKanyerere-u2z 8 дней назад

    Comrade more fire

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 8 дней назад

    More fire mtanyiwa inuyo ndi one AGALU awawa a MCP atikwana afiti opemphera

  • @EmilyKanyika
    @EmilyKanyika 9 дней назад

    🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 9 дней назад +1

    Chakwela akuona ngati amalawi tonse ndife mbuli zoti tizingoti boma ndilomweli , waiwalakuti mbuli ziliku mcp kokha .

  • @geofreykandabongomani4715
    @geofreykandabongomani4715 9 дней назад +1

    Agalu amenewa akufuna abweletse nkhondo Malawi muno serious kumalawi pa 17 September kukesedwa mwadzi munzandikumbuka mau anga

  • @moyowrobert3331
    @moyowrobert3331 8 дней назад

    😂😂😂koma ndiye asovakkkkkkkk

  • @EmiryMaponya
    @EmiryMaponya 8 дней назад

    Mtanyiwa machine bambo

  • @LuciusScott-q7o
    @LuciusScott-q7o 9 дней назад

    Welcome back

  • @FytonRichard-t3w
    @FytonRichard-t3w 8 дней назад

    Mbambande 🔥🔥🤣

  • @JenniferKameza
    @JenniferKameza 9 дней назад

    All comrades ,God bless you all ,long live

  • @HarryMakwale
    @HarryMakwale 9 дней назад +3

    Ulemu wanu basi mr ❤❤❤❤❤

  • @DicksonKamwendo
    @DicksonKamwendo 9 дней назад +1

    Eish Tamia bola ukanango pakulitsa pang'ono kuti nkhani isapte patali uptatu iwe

  • @ErnestMatick
    @ErnestMatick 9 дней назад +1

    Moto kt buuuuu

  • @isaiahbanda4590
    @isaiahbanda4590 8 дней назад

    Comrade Ntanyiwa iweyo umakwana

  • @WysonSawasawa
    @WysonSawasawa 6 дней назад

    Tanyiwa umativesa kukoma

  • @lilianprince661
    @lilianprince661 8 дней назад

    Ku statehouse kwasanduka beerhall ndi lesthouse kobelekera ana mwinaso tingot kumatenity hospital kkkkkk chikangawa woyeeeeeeeeeeeeee

  • @ElizabethPhiri-m4e
    @ElizabethPhiri-m4e 8 дней назад

    Oh God save us from this crocodile party

  • @geofreykandabongomani4715
    @geofreykandabongomani4715 9 дней назад +1

    Ulemu wanu Mr mtanyiwa

  • @idris6597
    @idris6597 9 дней назад

    Allah azikutetezerani bwana comrade ntanyiwa

  • @ChimwemweGphiri
    @ChimwemweGphiri 9 дней назад +2

    Osamayiwala clff

  • @KamotoManex
    @KamotoManex 8 дней назад

    Bg up

  • @AndrewZakeyo-p8t
    @AndrewZakeyo-p8t 8 дней назад

    😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @HajieMtenje
    @HajieMtenje 9 дней назад +1

    Nkhangaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaaa zaona😂😂😂😂😂!!

    • @Halima-i4x
      @Halima-i4x 8 дней назад

      😂😂😂😂😂😂😂 inezotu ndasekatu ati ngaaaaaaaaaa 😅😅😅😅 mavuto

  • @JoyceMoyo-mp3de
    @JoyceMoyo-mp3de 9 дней назад

    Comrade ntanyiwa your a fire 🔥

  • @joempesi
    @joempesi 9 дней назад

    Long live mtanyiwa

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 9 дней назад

    😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😂😂😂😂yomweyo Chikangawa party koma mulimba 😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😂😂😂😂😂🎉🎉🎉😂😂😂

  • @SueWahna-y8m
    @SueWahna-y8m 9 дней назад +1

    Kkkkk kom abale khan zake 😂😂😂

  • @lilianprince661
    @lilianprince661 8 дней назад

    Koma inudi ndi ntanyiwa zibwerani nazo zambiri kut ife amalawi tipulumukeee

  • @FatimaAyami
    @FatimaAyami 8 дней назад +1

    Nanuso tamqtipatsani ma feedback abwana osati kumaonjezela zina zoti sizinachitike mutisokoneza mutu anthuwa ambiri amakupangani follow up so tiwuzeni zoona zinaso ayi

  • @AlicePondani
    @AlicePondani 8 дней назад

    Machine

  • @JumahIshmael
    @JumahIshmael 8 дней назад

    Kod jb alikuti abale muuzeni fast fast mamvete

  • @Felie-p7l
    @Felie-p7l 9 дней назад

    A comrade munasowatu inu ife matha kuti chakuchitikilani ndichiyan

  • @KassimKanyenga
    @KassimKanyenga 9 дней назад +1

    Moniwo kwa ben longwe bwa

  • @Hamusa-j3p
    @Hamusa-j3p 8 дней назад

    𝕋𝕒𝕞𝕚𝕪 𝕪𝕠𝕞𝕨𝕖𝕪𝕠

  • @laurentbutao4084
    @laurentbutao4084 9 дней назад

    Ine ndimadabwatu kuti chifukwa chomumangilacho mchosakwanira..Personal issues ndi zimene zavuta

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 9 дней назад

    🎉

  • @JosephyHarry
    @JosephyHarry 9 дней назад +1

    Bro munasowatu.koma Malawi ndichani dzikoli nkhani yake izingokhala yazigololo basi izi ndiye zatikwana.koma kuti azaonekere ng'amba nkazi wina azangomucheka pang'ono wina wogundika ndi azimayi nziko muno.azimayiwa tiziwapatsa ulemu.

  • @Dellingsmunthali
    @Dellingsmunthali 9 дней назад +3

    Apooooooooo😂😂 ndipamene timaziwa kut wabwera mtanyiwa akat nkhaaaangaaaazaoonaaa😂😂😂😂

  • @NeliaGlaciano
    @NeliaGlaciano 8 дней назад

    Mupole moto a mcp

  • @fet-joeabbuh7016
    @fet-joeabbuh7016 9 дней назад

    Tsono ife ayiniyake a fone ndikugula ma data moni sitimamufuna??

  • @FatimaMisheck
    @FatimaMisheck 8 дней назад

    Ndi makunyadila ntanyiwa

  • @ManyengoJnr
    @ManyengoJnr 8 дней назад

    Inenso ndipatsen moni

  • @AishaMuhammad-v8m
    @AishaMuhammad-v8m 8 дней назад

    Koma

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal 9 дней назад

    Mm koma chikangawa party ayi ndithu

  • @EmmanuelDanken-h9d
    @EmmanuelDanken-h9d 9 дней назад

    Kod wapolis anawombera mai said mukandu wake uli litilo?

  • @rodrickwiskes
    @rodrickwiskes 9 дней назад

    😂😂😂ok

  • @MustafRajab
    @MustafRajab 9 дней назад

    Kodi ndichifukwa chiyani sankagula atangolowa mmboma akugula akufuna kupanga zisakho?

  • @Faston-d2p
    @Faston-d2p 9 дней назад

    Go for manual

  • @LalaNkhoma-h1s
    @LalaNkhoma-h1s 8 дней назад

    Mulungu tiyendeleni Satan akuyenda maliseche

  • @AbdulJohn-t7l
    @AbdulJohn-t7l 9 дней назад

    Tamiya akanalola kenako ndikunena kuti andigwilila kuti azengedwe milandu ntchito itatha iwe Tamiya ukavumbulukako uku ukulila kuti andigwilila chifukwa ku chipatala amakayeza ndiye akayeza azapeze kuti akumbwindadi akanalipila komaso ndi kumangidwa komwe

    • @HawaHussein-o5k
      @HawaHussein-o5k 9 дней назад +1

      Zikomo moni talandila bomali lichokedi ambuye atithandize

    • @HaroonSaidi-jv3ek
      @HaroonSaidi-jv3ek 8 дней назад

      Paja amatha kuwaopsyesa ma dotolo kuti asanene chilungamo like za amayi saidi zija zinazimva bwanji kuti anene ngamo kuopa kuzima

    • @AbdulJohn-t7l
      @AbdulJohn-t7l 8 дней назад

      @HaroonSaidi-jv3ek kumapita ku za private zikulu zikulu

    • @RachealHarawa-xc9gs
      @RachealHarawa-xc9gs 8 дней назад

      Anachita bwino kukana akanangomupasapo matenda basi anthuwatu anavunda kale

  • @HADIJAZAMBIA
    @HADIJAZAMBIA 9 дней назад +2

    😂😂😂😂😂

  • @Virdimir
    @Virdimir 9 дней назад

    Kufuna kuthila mazi pambwanda yamwana kkkk kuthila mazi pakayera, paimaso, pachimbamba, paimaso ,panyemba penipenipo bac

  • @Sabina-hw4js
    @Sabina-hw4js 9 дней назад

    Pathetic government

  • @paulyohane3197
    @paulyohane3197 9 дней назад

    🧑‍💻

  • @ChriOffice
    @ChriOffice 9 дней назад +1

    PA manual po game ili bho man

  • @ElizabethKalonga
    @ElizabethKalonga 9 дней назад

    Moni

  • @MphatsoChepetsani
    @MphatsoChepetsani 9 дней назад

    Koma ya ziriko

  • @YusufAlidi
    @YusufAlidi 8 дней назад +1

    More fire ntanyiwa

  • @bellsnampanda
    @bellsnampanda 9 дней назад

    It's to childish

  • @crosbeygondwe5403
    @crosbeygondwe5403 9 дней назад +1

    Following from 2nd road Hyde Park Sandton

  • @JackAmoss-zg2zw
    @JackAmoss-zg2zw 9 дней назад

    Kkkkk

  • @MariaJaya-s9b
    @MariaJaya-s9b 8 дней назад

    ❤❤❤❤❤

  • @CostableowenKusesiwe
    @CostableowenKusesiwe 7 дней назад

    Inu zomwe mumakamba

  • @MustafRajab
    @MustafRajab 9 дней назад

    Kodi ndichifukwa chiyani sankagula atangolowa mmboma akugula akufuna kupanga zisakho?

  • @TimexKaufa
    @TimexKaufa 8 дней назад

    ❤❤❤❤❤