Abusa akuti vote yao atengapo anapanga mistake❎ 😂😂😂

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 2 июл 2024

Комментарии • 175

  • @augustMag
    @augustMag 24 дня назад +5

    Powerful words may God continue bless you Fr Mnthalika 🔥

  • @user-sv2vc7ie2m
    @user-sv2vc7ie2m 26 дней назад +6

    Anthu atengapotu phunzilo ndizovuta zomwe tikuziona chifukwa anthu amati akufuna kuona kusintha ndiye aonatu nyekhweeeeee

  • @GiftPhiri-tt7nn
    @GiftPhiri-tt7nn 26 дней назад +4

    Umenewu ndiye utsogoleri munthu wa Mulungu asamaope kuyankhula chilungamo , osati azibusa enawa kungowapatsa ndalama basi kusekelera zopusa , ana anjoka Inu Mulungu akulangani

  • @user-oc8nj3or6y
    @user-oc8nj3or6y 24 дня назад +2

    What a teaching ❤❤❤ impressed me so much waooooo❤❤❤

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 7 часов назад

    Eeee eeee Bon Kalindo siwamisalatu... Adanena kuti anthu akadzatopa adzalankhura m'modzi modz....
    God be with you ❤

  • @CathreenKadwala
    @CathreenKadwala 25 дней назад +3

    Father Inu Ambuye azikupasani moyo wautali simuwopa kuyankhula chilungamo

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 25 дней назад +2

    Amen abishop ndipo talira mokwana koma mulungu simunthu safulumira ndipo sachedwa one day is one day mulungu ayakha

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5o 26 дней назад +3

    you have spoken man of. God we. are listing God is God. does not. fail

  • @WilliamNhlane-fd9hi
    @WilliamNhlane-fd9hi 15 дней назад

    Amen , tangovomerezani bwana president tulani pansi udindo nokha mukuona kuti zakukanikani .

  • @MorrisMapiri-d6z
    @MorrisMapiri-d6z 24 дня назад +3

    Mlungu anamufunsa KAINI nati: alikuti m'bale wako Abele? Nde anati, taona mwazi wake ukundililira ine kunthaka. Zotsatira anali matembelero pa KAINI. Kukhetsa mwazi kumadzetsa tsoka.

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 29 дней назад +4

    Father mumakwanisa ulaliki wanu wabwino kwambiri

  • @ReginaKasambiza-ie2rp
    @ReginaKasambiza-ie2rp 26 дней назад +2

    Kumwamba kulande vote yanga
    Tsiku lina Mulungu wamva Pemphero lathu

  • @user-ir1lj8ir5t
    @user-ir1lj8ir5t 14 дней назад

    Amen and amen inenso ndipemphelo langa ambuye afute ma vote abale anga zoona zomwe timaziyembekezela sizimenezi ayi

  • @bysongeorge3243
    @bysongeorge3243 29 дней назад +4

    Chilungamo chokhachoka. Zokhumudwitsa wina tinamusankha anali M'busa..koma lero anasanduka ..

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p 29 дней назад +4

    True talking man of God

  • @EvelynLungu-lj8tp
    @EvelynLungu-lj8tp 26 дней назад +3

    Mwaputa nkhondo. Akatorika si anthu wamba. Wina atengapo thembelero

  • @JustinChinombo-dy6tp
    @JustinChinombo-dy6tp 26 дней назад +1

    Amen amen a bishop mulungu wathu salephera, Achilima anati mudima or ukule bwanji koma kuzacha ndithu ❤❤

  • @SueWahna
    @SueWahna День назад

    Amen ine ndagwirizana nanu atsogoleri

  • @user-wr1km2gh4g
    @user-wr1km2gh4g 25 дней назад +2

    Kuyankhula kwa mphavu,kopanda mantha,osaopa munthu,tiziopa mulungu

  • @MarkManyowa
    @MarkManyowa 21 день назад +1

    🤣🤣🤣🤣 Malawi ikakhala Nyekhwe nde taithamatu🤣🤣🤣🤣🇹🇿

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 23 дня назад +1

    Amen jone chilebwe

  • @user-te3ps3kf2t
    @user-te3ps3kf2t 26 дней назад +1

    Ali ndi khutu amve,powerful Massage.

  • @marthansaliwa7732
    @marthansaliwa7732 28 дней назад +1

    Amen! Father Ambuye azikutetezani.

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 29 дней назад +4

    Azisogoleli ameneqa onse alandile ma thembelelo kuyambila ana awo komanso zizukulu zawo za ana awo onse amene azadye ndalama zomwe akubasi za anath osauka alandile thembelelo ndibkhate mu zina la yesu....

  • @user-il8cn7ko9m
    @user-il8cn7ko9m 23 дня назад +1

    😂😂 eshi amen

  • @user-uf4db7im7d
    @user-uf4db7im7d 12 дней назад +1

    Mwaputa a katolika ndipo simunati muziona, campaign ali mmatchalichi

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 29 дней назад +12

    A Bishop mwalitha bomali, ndipo kumene ali Chakwera sakugona ndi m'mene mwatulukila ma Bishop. Chakwera ndi boma lake la MCP lalephera tatopanalo.

    • @MeckMdoma
      @MeckMdoma 25 дней назад

      Dpp nayo tinatopa nayo nkuona tinayithamangitsa. Mavuto ali mdziko muno solution si dpp. Awa adzawonjezera kusawuka kwa a Malawi kupsola apa. Malawi is going througheconomic problems because dpp mismanaged this country's economy.

    • @marryphili5419
      @marryphili5419 25 дней назад

      Borani DPP inali bwino fertilize wunali bwino anthu tinali ndi chakudya mapassport amapezeka palipose kuchoka ku mzuzu mupaka kumangochi ndalama sinali yotha mphamvu panopa wesi

    • @PrinceBlessings-bv5bs
      @PrinceBlessings-bv5bs 8 часов назад

      Kodi Dpp idalakwanji????

  • @user-ek6wf7bt7f
    @user-ek6wf7bt7f 26 дней назад +2

    Father mupitilize kumuthira fire chakwera,watikwana

  • @user-dy4gc2hr5e
    @user-dy4gc2hr5e 18 дней назад

    Powerful message Ambuye akutetezereni ntumiki

  • @user-xv3nr5kj2u
    @user-xv3nr5kj2u 16 дней назад +1

    Amen father

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z 29 дней назад +2

    Abusa awawa MULUNGU awapatse moyo wautali.imfa ya chilima akatolika sakugona ndipo akati apemphere amakhala serious mcp bro apule samalani

  • @user-wi8xw9qh7n
    @user-wi8xw9qh7n 17 дней назад

    Yes father God will help us

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636 26 дней назад +1

    Tiwemphelere atisiye anthu oipawa afe ndithu, mkhwiyo wa ambuye uwakwapule anthu akubawa

  • @user-gv2uu3cs3g
    @user-gv2uu3cs3g 26 дней назад +1

    Amen a Bishop.Amenewa Ndiye mau

  • @ThokozaniKaluluma-rj6rp
    @ThokozaniKaluluma-rj6rp 24 дня назад +1

    Koma muli ndi lawyer? Kkkk

  • @thatgirrroskrr3570
    @thatgirrroskrr3570 20 дней назад

    Powerful message

  • @user-vx5kv8dz3d
    @user-vx5kv8dz3d День назад

    Allah amutibule Farawo wathuyu

  • @NatashaBema
    @NatashaBema 29 дней назад +1

    Amen abusa inuyo mumatha

  • @lawrencemakina2882
    @lawrencemakina2882 26 дней назад +1

    Amen. Mulungu ndiye omenyera nkhondo ana ake

  • @MasausoMsiska-rz3id
    @MasausoMsiska-rz3id 22 дня назад

    Amen man of God

  • @AdamSteven-ne9hg
    @AdamSteven-ne9hg 18 дней назад

    Ulaliki ugwira mtima ndithu🔥

  • @AndersonChimwala-hz4so
    @AndersonChimwala-hz4so 29 дней назад +2

    Mau ogwila mtima zoona .

  • @user-dm2fs6hf1b
    @user-dm2fs6hf1b 29 дней назад +2

    Palibe zofuna kutchuka chilungamo chinenedwe achulewa a mcp anapha anthu pangoz ya ndege( chilima) ndi ena onse

  • @JamayakoJamayako-rv2he
    @JamayakoJamayako-rv2he 21 день назад

    Powerful massage
    Pipo shud listen carefully

  • @MestreMaday-fv7qo
    @MestreMaday-fv7qo 21 день назад

    IWE loya wachani IWE ndi m.malawi ukunva bwanji siya zimenezo

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r 26 дней назад +2

    Pano agula mifut malo mogula makhwala zipatalam

  • @CharlesChagudubuka-rm6bh
    @CharlesChagudubuka-rm6bh 26 дней назад +1

    Akuti apule chasanduka choseketsa 😂😂😂for

  • @user-qg4it7my9n
    @user-qg4it7my9n 26 дней назад

    Amen ambuye akudaliseni coz mwaonse azitumiki asakha kukhara cete ngati dziko likuyenda bwino koma mulungu azapeleka cilango coopsa kwa anthu amenewa

  • @elizasingano
    @elizasingano 29 дней назад

    Amen and amen mulungu atithandiza kumeneya nkhondo imeneyu

  • @user-hs4bm2yj8r
    @user-hs4bm2yj8r 23 дня назад

    Amen 🙏 father, Mulungu kutetezeni

  • @1kumilala1
    @1kumilala1 29 дней назад

    Mawu amalenga. Amen Father

  • @FazilahKazembe
    @FazilahKazembe 24 дня назад

    Amen wathu sameneyo ..

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 29 дней назад

    Ameen ameen abusa. Apa boma palibe koma chizuzo basi kuononga dziko uku. Koma apa pakufunika nkhondo ambuye atithandize.chifukwa ngati afika pomupha chilima ife ationa ngati ndani.koma nkhondo ndimeneyatsala basi

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 29 дней назад +3

    Munthu wamulungu walankhula apa

  • @LingsonMaida
    @LingsonMaida 29 дней назад +1

    Ifeso talanda bwana😂😂😂😂😂😂

  • @allansili-rc9gc
    @allansili-rc9gc 29 дней назад

    Wow this is charming

  • @MacreaChilingulo-ob9gb
    @MacreaChilingulo-ob9gb 26 дней назад

    You are the Greatest , Amen !

  • @deborahngwira724
    @deborahngwira724 23 дня назад

    Mkwiyowutu ukuchedwa. Ine nde ndikuufuna nsanga nsaname

  • @JosterNgalawa
    @JosterNgalawa 26 дней назад

    Amen bishop, ndipo pitilizani

  • @AndersonChimwala-hz4so
    @AndersonChimwala-hz4so 29 дней назад +1

    Anthu amulungu kugwa kwa munthu openphela amalandila nazo Themberelo.

  • @user-ve4zn2ne1k
    @user-ve4zn2ne1k 29 дней назад +2

    Alleluia Abosa naneso ndi banja Langa ndaitengako mulungu afufute ndithu!!!!

  • @DafterKhungwa
    @DafterKhungwa 23 дня назад

    Amen,nanenso ndayitengako

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 24 дня назад

    Amen Chakwela you mast go watikwana

  • @JamayakoJamayako-rv2he
    @JamayakoJamayako-rv2he 21 день назад

    Mateyu 18 vs 18
    Yomweyoo ikhake nyimbo ndi chitsogodzo kwa ife

  • @Allan-bk1
    @Allan-bk1 26 дней назад

    😂😂😂😂eeesh pastor

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 29 дней назад

    Amen mau awa agwile ntchito kwa woipayo kuti Malawi apulumuke

  • @ThokohPrescotKalonga
    @ThokohPrescotKalonga 29 дней назад +1

    Zowona ndithu, malawi akufunika ma demo kuti akozeke

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 29 дней назад

    God is speaking to the government of Malawi anayiwala kuti kunja kuno kuli Mulungu, akupembedza ndalama. Mulungu dzukani pa mpando wanu wachifumu mutimenyere nkhondoyi

  • @TiyanjaneMkwate-we8gu
    @TiyanjaneMkwate-we8gu 26 дней назад

    Mulungu alemekezeke, amalawi tikuzunzika kwambili, atithandize potiteteza kwa anthu a nkhanza ngati awa.Ft Mulungu akudaliseni pobwera ndi chilungamo.mwina liwu lanu linveka kwa MULUNGU.

  • @BestonMakochera-qk4sz
    @BestonMakochera-qk4sz 24 дня назад

    Sibas katolika waziwa chomwe chinachitik game yathapo yambani kulongeza 😢😢 anthu amene ziululika lero zayambik

  • @FredKanyerere
    @FredKanyerere 23 дня назад

    Bishop Amen

  • @user-uy8uk7so9d
    @user-uy8uk7so9d 10 дней назад

    God be with you

  • @munashemoyo4190
    @munashemoyo4190 29 дней назад

    Amen father Amen mau mau

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 28 дней назад

    Ulemu wanu Abusa ❤❤❤❤❤❤

  • @MzikaPhiri
    @MzikaPhiri 23 дня назад

    Yangaso ndatenga

  • @PeterChuma-yf1ps
    @PeterChuma-yf1ps 21 день назад

    Vote yanga naneso itengedwe

  • @ChilangoNdalama
    @ChilangoNdalama 28 дней назад

    Amen abshop

  • @sthoramexjrsa902
    @sthoramexjrsa902 29 дней назад

    Amen father 🙌🙌🙌

  • @HildaMachinjiri
    @HildaMachinjiri 11 дней назад

    Amen

  • @RachealHarawa-xc9gs
    @RachealHarawa-xc9gs 28 дней назад

    Chilichonse chili ndinthawi koma na apapa zafikapa Ambuye chitaponi kanthu mwasanga

  • @GeorgeKambwiri-xr9ri
    @GeorgeKambwiri-xr9ri 20 дней назад

    Koma yaa🤝 9:58

  • @PaxKinley
    @PaxKinley 23 дня назад

    Ndatenganso nane VOTE yanga

  • @MestreMaday-fv7qo
    @MestreMaday-fv7qo 21 день назад +1

    Chipan ali nacho ndi mulungu wathu

  • @B1Chitatata
    @B1Chitatata 22 дня назад

    Salute

  • @WilliamNhlane-fd9hi
    @WilliamNhlane-fd9hi 26 дней назад

    Amen God hear our prayers , rescue Malawi

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v 28 дней назад

    Amen 🙏

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 26 дней назад

    Pharaoh watsala pang'ono kuonetsedwa ukulu wa Mulumgu pompano aziona iyeyo kodi sakuona kuti ulemu wake unachoka Kale kale? President wanji omangotukwanidwa mgati chitsiru?

  • @BlessingsMakalani
    @BlessingsMakalani 29 дней назад

    Amen Amen

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 26 дней назад

    Tathokoza abusa ameneyu musasiye kumudzudzula pali mau amanena kuti :ONDIUZA ANALIPO KOMA KUSAMVELA KWANGA KWANDIPWETEKETSA

  • @KennethMchenga-j9c
    @KennethMchenga-j9c 23 дня назад

    Uthenga uwo siwamasewela mulungu akutetezelen ameni

  • @HassanJameskananjie
    @HassanJameskananjie 26 дней назад

    Kod amalaw mupepela mpaka liti lawyer nde kuti chan

  • @user-uy8uk7so9d
    @user-uy8uk7so9d 10 дней назад

    Munavotela zisilu kodi nanu

  • @gracekamzati
    @gracekamzati 26 дней назад

    Ameni abusa ine nde sinavotereko ndipoyamba pomwe ili siboma ayi koma kupha anthu

  • @williamchitonya
    @williamchitonya 14 дней назад

    Awa ndye mau

  • @tresawillicky
    @tresawillicky 29 дней назад +1

    Mau amphamvu zedi

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 22 дня назад +2

    Analowa mu Zina la ubusa 😢😢😢osaziwa satana watola joker eeeeee ai chakwela wapweteka Malawian 😭😭

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 29 дней назад

    Uthenga uwuwu ukamufika woipa chikumbu mtima chimugwile

  • @user-wd5tw1mz8h
    @user-wd5tw1mz8h 26 дней назад

    Wakutumani ndimulungu lankhulan mosaopa chifukwa malawi waonongeka ndi chakwela

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 29 дней назад

    Tikufuna anthu olimba mtima kumalawi kuno ngati fazzala awaa

  • @SpearChikwapulo
    @SpearChikwapulo 20 дней назад

    Wakatolika