Azisogoleli ameneqa onse alandile ma thembelelo kuyambila ana awo komanso zizukulu zawo za ana awo onse amene azadye ndalama zomwe akubasi za anath osauka alandile thembelelo ndibkhate mu zina la yesu....
Dpp nayo tinatopa nayo nkuona tinayithamangitsa. Mavuto ali mdziko muno solution si dpp. Awa adzawonjezera kusawuka kwa a Malawi kupsola apa. Malawi is going througheconomic problems because dpp mismanaged this country's economy.
Ameen ameen abusa. Apa boma palibe koma chizuzo basi kuononga dziko uku. Koma apa pakufunika nkhondo ambuye atithandize.chifukwa ngati afika pomupha chilima ife ationa ngati ndani.koma nkhondo ndimeneyatsala basi
God is speaking to the government of Malawi anayiwala kuti kunja kuno kuli Mulungu, akupembedza ndalama. Mulungu dzukani pa mpando wanu wachifumu mutimenyere nkhondoyi
Powerful words may God continue bless you Fr Mnthalika 🔥
Anthu atengapotu phunzilo ndizovuta zomwe tikuziona chifukwa anthu amati akufuna kuona kusintha ndiye aonatu nyekhweeeeee
Umenewu ndiye utsogoleri munthu wa Mulungu asamaope kuyankhula chilungamo , osati azibusa enawa kungowapatsa ndalama basi kusekelera zopusa , ana anjoka Inu Mulungu akulangani
What a teaching ❤❤❤ impressed me so much waooooo❤❤❤
Eeee eeee Bon Kalindo siwamisalatu... Adanena kuti anthu akadzatopa adzalankhura m'modzi modz....
God be with you ❤
Father Inu Ambuye azikupasani moyo wautali simuwopa kuyankhula chilungamo
Amen abishop ndipo talira mokwana koma mulungu simunthu safulumira ndipo sachedwa one day is one day mulungu ayakha
you have spoken man of. God we. are listing God is God. does not. fail
Amen , tangovomerezani bwana president tulani pansi udindo nokha mukuona kuti zakukanikani .
Mlungu anamufunsa KAINI nati: alikuti m'bale wako Abele? Nde anati, taona mwazi wake ukundililira ine kunthaka. Zotsatira anali matembelero pa KAINI. Kukhetsa mwazi kumadzetsa tsoka.
Father mumakwanisa ulaliki wanu wabwino kwambiri
Kumwamba kulande vote yanga
Tsiku lina Mulungu wamva Pemphero lathu
Amen and amen inenso ndipemphelo langa ambuye afute ma vote abale anga zoona zomwe timaziyembekezela sizimenezi ayi
Chilungamo chokhachoka. Zokhumudwitsa wina tinamusankha anali M'busa..koma lero anasanduka ..
True talking man of God
@@user-mj2te7vl6p Kung'alula
Mwaputa nkhondo. Akatorika si anthu wamba. Wina atengapo thembelero
Amen amen a bishop mulungu wathu salephera, Achilima anati mudima or ukule bwanji koma kuzacha ndithu ❤❤
Amen ine ndagwirizana nanu atsogoleri
Kuyankhula kwa mphavu,kopanda mantha,osaopa munthu,tiziopa mulungu
🤣🤣🤣🤣 Malawi ikakhala Nyekhwe nde taithamatu🤣🤣🤣🤣🇹🇿
Amen jone chilebwe
Ali ndi khutu amve,powerful Massage.
Amen! Father Ambuye azikutetezani.
Azisogoleli ameneqa onse alandile ma thembelelo kuyambila ana awo komanso zizukulu zawo za ana awo onse amene azadye ndalama zomwe akubasi za anath osauka alandile thembelelo ndibkhate mu zina la yesu....
Amen
Amen Amen
😂😂 eshi amen
Mwaputa a katolika ndipo simunati muziona, campaign ali mmatchalichi
A Bishop mwalitha bomali, ndipo kumene ali Chakwera sakugona ndi m'mene mwatulukila ma Bishop. Chakwera ndi boma lake la MCP lalephera tatopanalo.
Dpp nayo tinatopa nayo nkuona tinayithamangitsa. Mavuto ali mdziko muno solution si dpp. Awa adzawonjezera kusawuka kwa a Malawi kupsola apa. Malawi is going througheconomic problems because dpp mismanaged this country's economy.
Borani DPP inali bwino fertilize wunali bwino anthu tinali ndi chakudya mapassport amapezeka palipose kuchoka ku mzuzu mupaka kumangochi ndalama sinali yotha mphamvu panopa wesi
Kodi Dpp idalakwanji????
Father mupitilize kumuthira fire chakwera,watikwana
Powerful message Ambuye akutetezereni ntumiki
Amen father
Abusa awawa MULUNGU awapatse moyo wautali.imfa ya chilima akatolika sakugona ndipo akati apemphere amakhala serious mcp bro apule samalani
Yes father God will help us
Tiwemphelere atisiye anthu oipawa afe ndithu, mkhwiyo wa ambuye uwakwapule anthu akubawa
Amen a Bishop.Amenewa Ndiye mau
Koma muli ndi lawyer? Kkkk
Powerful message
Allah amutibule Farawo wathuyu
Amen abusa inuyo mumatha
Amen. Mulungu ndiye omenyera nkhondo ana ake
Amen man of God
Ulaliki ugwira mtima ndithu🔥
Mau ogwila mtima zoona .
Palibe zofuna kutchuka chilungamo chinenedwe achulewa a mcp anapha anthu pangoz ya ndege( chilima) ndi ena onse
Powerful massage
Pipo shud listen carefully
IWE loya wachani IWE ndi m.malawi ukunva bwanji siya zimenezo
Pano agula mifut malo mogula makhwala zipatalam
Akuti apule chasanduka choseketsa 😂😂😂for
Amen ambuye akudaliseni coz mwaonse azitumiki asakha kukhara cete ngati dziko likuyenda bwino koma mulungu azapeleka cilango coopsa kwa anthu amenewa
Amen and amen mulungu atithandiza kumeneya nkhondo imeneyu
Amen 🙏 father, Mulungu kutetezeni
Mawu amalenga. Amen Father
Amen wathu sameneyo ..
Ameen ameen abusa. Apa boma palibe koma chizuzo basi kuononga dziko uku. Koma apa pakufunika nkhondo ambuye atithandize.chifukwa ngati afika pomupha chilima ife ationa ngati ndani.koma nkhondo ndimeneyatsala basi
Munthu wamulungu walankhula apa
@@WilliamBandaWili Kung'alula
Ifeso talanda bwana😂😂😂😂😂😂
Wow this is charming
You are the Greatest , Amen !
Mkwiyowutu ukuchedwa. Ine nde ndikuufuna nsanga nsaname
Amen bishop, ndipo pitilizani
Anthu amulungu kugwa kwa munthu openphela amalandila nazo Themberelo.
Alleluia Abosa naneso ndi banja Langa ndaitengako mulungu afufute ndithu!!!!
Amen,nanenso ndayitengako
Amen Chakwela you mast go watikwana
Mateyu 18 vs 18
Yomweyoo ikhake nyimbo ndi chitsogodzo kwa ife
😂😂😂😂eeesh pastor
Amen mau awa agwile ntchito kwa woipayo kuti Malawi apulumuke
Zowona ndithu, malawi akufunika ma demo kuti akozeke
God is speaking to the government of Malawi anayiwala kuti kunja kuno kuli Mulungu, akupembedza ndalama. Mulungu dzukani pa mpando wanu wachifumu mutimenyere nkhondoyi
Mulungu alemekezeke, amalawi tikuzunzika kwambili, atithandize potiteteza kwa anthu a nkhanza ngati awa.Ft Mulungu akudaliseni pobwera ndi chilungamo.mwina liwu lanu linveka kwa MULUNGU.
Sibas katolika waziwa chomwe chinachitik game yathapo yambani kulongeza 😢😢 anthu amene ziululika lero zayambik
Bishop Amen
God be with you
Amen father Amen mau mau
Ulemu wanu Abusa ❤❤❤❤❤❤
Yangaso ndatenga
Vote yanga naneso itengedwe
Amen abshop
Amen father 🙌🙌🙌
Amen
Chilichonse chili ndinthawi koma na apapa zafikapa Ambuye chitaponi kanthu mwasanga
Koma yaa🤝 9:58
Ndatenganso nane VOTE yanga
Chipan ali nacho ndi mulungu wathu
Salute
Amen God hear our prayers , rescue Malawi
Amen 🙏
Pharaoh watsala pang'ono kuonetsedwa ukulu wa Mulumgu pompano aziona iyeyo kodi sakuona kuti ulemu wake unachoka Kale kale? President wanji omangotukwanidwa mgati chitsiru?
Amen Amen
Tathokoza abusa ameneyu musasiye kumudzudzula pali mau amanena kuti :ONDIUZA ANALIPO KOMA KUSAMVELA KWANGA KWANDIPWETEKETSA
Uthenga uwo siwamasewela mulungu akutetezelen ameni
Kod amalaw mupepela mpaka liti lawyer nde kuti chan
Munavotela zisilu kodi nanu
Ameni abusa ine nde sinavotereko ndipoyamba pomwe ili siboma ayi koma kupha anthu
Awa ndye mau
Mau amphamvu zedi
Analowa mu Zina la ubusa 😢😢😢osaziwa satana watola joker eeeeee ai chakwela wapweteka Malawian 😭😭
Uthenga uwuwu ukamufika woipa chikumbu mtima chimugwile
Wakutumani ndimulungu lankhulan mosaopa chifukwa malawi waonongeka ndi chakwela
Tikufuna anthu olimba mtima kumalawi kuno ngati fazzala awaa
Wakatolika