Anasemphanitsa Ma Waya | Nkulu Wina Waululanso | Koma Nkhanizi Mukuziona Bwa?

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 14 июн 2024
  • #chilima #skc #utm #mcp #news #malawi #trending #viral

Комментарии • 126

  • @emmammatsa1284
    @emmammatsa1284 13 дней назад +24

    Chomwe ndikudabwa ine ndichakuti, the searching was discontinued and Anthu ofufuza ndege tsiku lomwe idasowa they were being directed to wrong directions pamene ozitsatawo amadziwa the right direction komwe kunali ndege so they could finish their evil mission like hiding their cell phones and also that there shouldn't be any victim left alive. May God vindicate them in broad daylight

    • @user-vu4cz1mt4f
      @user-vu4cz1mt4f 11 дней назад

      Sichokhachonso akuti pafupi ndipomwe ndege idakwera pali tower ya TNM ndipo mulonda anaona zonse koma anauzidwa kuti asaulule chifkwa chan tinene sanaone ? Ngt munthu amamva tswatswa wakuyenda kwagalu nde phokoso landege angalimve motan ?
      Ngt mulondayo sanamve phokosolo nde akutanipo akulondelapo zichan pot ilo linali phokoso lalikulu than tswatswa wamunthu

  • @MemoryChikakuda
    @MemoryChikakuda 13 дней назад +9

    Yehova Mulungu akukanthen nonse omwe mwatengapo mbali paimfa ya anthu amenewa.

    • @KeishaFeston
      @KeishaFeston 8 дней назад

      Palibe watengako mbali inu only God knows what happened

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 13 дней назад +4

    I wonder this guy called chakwera kod amamva bwanji akamachita zithu zoipa motere athu mkumadandaula za iye

  • @RonaldtonyMnenula
    @RonaldtonyMnenula 13 дней назад +3

    😢❤koma ayi anthu amadziwa kuipa kuposa satana

  • @OFG-th3st
    @OFG-th3st 13 дней назад +10

    Even Macbeth was manipulated by three witches 😢😢😢😢😢😢

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 13 дней назад +4

    Koma abale inu Saulos Chilima wafa imfa yowawa amene apanga zimenezi wo achotsedwe ndithu kupha mzanu ngati chinyama Mulungu akulangeni ndithu anthu nonse amene mwapanga chiwembu chopha anthuwa

  • @ElonBlack1999
    @ElonBlack1999 13 дней назад +4

    Keep up the good work brother

  • @alexmkolongo3089
    @alexmkolongo3089 13 дней назад +3

    Mkaka amayakhula manyi kwambiriso mumuuzako panyelo pake

  • @LeendaDeborah2005
    @LeendaDeborah2005 13 дней назад +1

    Chakwerayu amandikumbutsa za character wamu book yomwe adalemba William Shakespeare wotchedwa Macbeth. Adapha azinzake chifukwa chokakamila ufumu koma kumapeto adaphedwa ndi adani

  • @louismagongwa
    @louismagongwa 12 дней назад +1

    ife tikudabwa akut ndekhe inasowa 10 am kuyamba kufufusa 4pm mkudzaimaso aaaa akuluwa they are sleeping on duty komaso komas opandapo wa mcp onse a UTM mwasamba mwazi abusa muziona😂😂😂

  • @malvinhusted6245
    @malvinhusted6245 13 дней назад +2

    Watamba masana chakwera wayaluka

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 13 дней назад +2

    Kuchita chopuntha alibe chisoni anthuwa😢😢😢

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 13 дней назад +3

    Kodi ndimayetsa amawawudza anthu kuti otsawopa lelo nde anthu adziwopa nsono aaaa uchisilu wa MCP umenewo apa mwayaluka mwapha olakwika chakwela aCHOKE BASI NDI GALU KWABASI

    • @BeatGondwa
      @BeatGondwa 13 дней назад

      Kom ndip inu achokedi

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 13 дней назад +7

    Musakaikile , chakwela ali momwemo , komanso nduna zitatu mwatchula zija zilichomcho , komanso pali commander of MDF komanso wamkulu wa Malawi police ali momwemo ,
    Inshort , all cabinet are involved on this accident

    • @SameKaposa
      @SameKaposa 13 дней назад +1

      Including chakwera

  • @user-vu4cz1mt4f
    @user-vu4cz1mt4f 11 дней назад

    Ambuye mwapase anthu akufa chiusiro chosatha ndipo kuyera kosatha kuwalise maso awo ndipo awuse mumtendere amen

  • @leonardjika2100
    @leonardjika2100 13 дней назад +5

    A NEW THINKER WISE WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD

  • @FlechaChipeta
    @FlechaChipeta 13 дней назад +3

    Chakwera wapha chilima iyo wakuziziwa chakwera please naye mupheni ameneyo

  • @peter..nyirenda4780
    @peter..nyirenda4780 13 дней назад +2

    Kodi pilot sanaone kuti ndege ilindivuto?

  • @RobertLifestyle-eo1sj
    @RobertLifestyle-eo1sj 13 дней назад +5

    Brutal truth I can't denie

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 13 дней назад

    Good Messnge Chakwela you mast go

  • @mariamahamadu8402
    @mariamahamadu8402 13 дней назад +1

    Ndiakumpadi away😭😭😭😭😭

  • @HanifaIshmael
    @HanifaIshmael 13 дней назад +2

    Mcp ya khadzaaaa zidangochitika

  • @Allan-bk1
    @Allan-bk1 13 дней назад +3

    Anthu oipa awa

  • @user-kz3py3rn5e
    @user-kz3py3rn5e 13 дней назад +3

    Plus mkaka

  • @raheemngoma1151
    @raheemngoma1151 13 дней назад +4

    Koma ziliko

  • @AllanChabwela
    @AllanChabwela 13 дней назад +2

    Zachibwana zokhazokha uyu sakuyenera kupitiliza kulamula dziko

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b 13 дней назад +1

    Upresidernt sikupha koma kugwira ntchito mokomera anthu magwiridwe achakwera ndizokomera iyeyo ndi nduna zake ndiye anthu tinkafuna kuyikapo chilima cholinga apange mokomera tonse inu mwapha koma mwanya

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 13 дней назад +2

    Eeeee koma ziliko!

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb 13 дней назад +2

    M cp has done again.

  • @AlfredNazombe-me2ly
    @AlfredNazombe-me2ly 13 дней назад +4

    Vuto lakusamva achinyamata mwaphesa Chilima chifukwa cha vote mumauzidya MCP ndiyoipa kusamva mumati muone zina we are in democracy ndi izi

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 13 дней назад +6

    Komaso chakwera amapha anthu kuti azikwela azikazi awo muone dza sadick mia pano akukwera mkazi wao

  • @user-ev4or2kg4z
    @user-ev4or2kg4z 13 дней назад +1

    Ndipo ndiona a president mwayaluka kwambiri chifukwa mukufuna kulamula mpaka 2030

  • @sungananitoto-5955
    @sungananitoto-5955 13 дней назад +1

    Mhuuu 😢😢

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope День назад

    Kuyankula kwa nzeru ankolo

  • @4ourcusworldwide426
    @4ourcusworldwide426 13 дней назад +2

    Mzimu wa chilima ukathe aliyese yemwe watengapo mbali. Ndipo achite misala

    • @messiii1018
      @messiii1018 13 дней назад +1

      He was a Christian ✝️

    • @gladyschisomo4324
      @gladyschisomo4324 11 дней назад

      Ndipo i agree mpaka nawoso adzikhweze

    • @gladyschisomo4324
      @gladyschisomo4324 11 дней назад

      Ndipo ine nnanena kale kuti ndege ya asilikali imakhala very safe kuposa zose zatheka bwanji kuti ya asilikali athuwa ikhale ndi mavuto bodza ili Zina kambu Zina leku chilipo chilipo ndipo i wish nzimu waanthu awa utawazuza anthu amene ali involved mpaka adzabwele poyela okha 😢😢

  • @user-yw3sy2wp4d
    @user-yw3sy2wp4d 4 дня назад

    That's is true

  • @susanjolly6710
    @susanjolly6710 12 дней назад

    Ambuye lowelelanipo,Aliese amene watengapo mbali mukantheni,afe nawo imfa yonyasa

  • @OFG-th3st
    @OFG-th3st 13 дней назад +3

    Osama bin laden 🚁

  • @user-ky8eq5ek1p
    @user-ky8eq5ek1p 13 дней назад +2

    Zoonadi Brother

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim 13 дней назад +1

    Balibeso mafunso chakwera ndiamene wapha

  • @malawigeneralguide1646
    @malawigeneralguide1646 13 дней назад +1

    Mhhhhh😢

  • @user-ym4kf9it2d
    @user-ym4kf9it2d 13 дней назад

    Ine ndikufa kuti siku lirilose president waku malawi amwalireso ngati mumena aphera azizake ndi galu kwabasi president waku malawi

  • @fundoniccoo-fk4ld
    @fundoniccoo-fk4ld 13 дней назад +3

    Chakwera tayakhanitu apa black box unasunga uziona tu waputa olakwika

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim 13 дней назад

    Ngati makhoti athu ndi janji athu ali achilungamo ngatiso sali bussness chimwendo mosese henly wasilikali onse akaikidwa chilima onse ku ndende ,bwanji anthu sadakwere nawo denge

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 13 дней назад +1

    Ndalama ena azisadza sua chaka chake chin

  • @NOKIAMalawi
    @NOKIAMalawi 6 дней назад

    Ziululika zonse mulungu ndi oopsya

  • @emiliaumali8360
    @emiliaumali8360 11 дней назад

    Mmmmmmm no mercy anthu oipa 😢 mizimu yawo isautse onse achita zimenezi

  • @mirriamchiwaula3862
    @mirriamchiwaula3862 10 дней назад

    Ndipo iwe chakwela ndiiwe muthu oyipa kwambili padziko pano fisi wamuthu iwe 😢😢

  • @mariamahamadu8402
    @mariamahamadu8402 13 дней назад +1

    Mmmmmm msambi

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 6 дней назад

    A mcp anapenga misala asiyen athana okha posachedwapa

  • @homeremedys3748
    @homeremedys3748 10 дней назад

    Chakwela Taimanso Tione ngati utamalize, chifukwa Mwamupha chilima uja nzimu wake ndiokwiya ifenso ndi okwiya

  • @GilbertMbvundula
    @GilbertMbvundula 11 дней назад

    Kuephanitsa zingwe ndenge singayende

  • @YOMALO.
    @YOMALO. 10 дней назад

    Osayankhula kwambiri, ife tikufuna tione umboni. Mukayankhula kwambiri your words shall be used against you.

  • @RobertmussaRobert
    @RobertmussaRobert 13 дней назад

    Saulos chilima andiwawa kwambili akadawina u prenzident malawi akadapita pasogolo

  • @kangungufoundation2020
    @kangungufoundation2020 12 дней назад

    Ndege si sienta yoti angasinthanise Mawaya amalawi tiyeni tikhale ndi nzeru Pena pake osati kumangobweresa umbuli pa internet mukuchitisa manyazi

  • @ThokozaniKaluluma-rj6rp
    @ThokozaniKaluluma-rj6rp 12 дней назад

    MCP VP and Tonse alliance VP onse apita why Malawi? Term imodzi?

  • @kasupeowenpaul
    @kasupeowenpaul 13 дней назад +1

    😢😢

  • @MosesNyalugwe-ll8hh
    @MosesNyalugwe-ll8hh 10 дней назад

    Agogo anga amkandiuza za MCP ndimkaona ngat bodza 😢😢

  • @SavicoJastin-vj7pt
    @SavicoJastin-vj7pt 12 дней назад

    Tithokoze kuti Santana tikumuwona ndi maso anthu omwe afa mboma la chiromboco eeeeeeeeeee kumanda yah

  • @vicshyma5644
    @vicshyma5644 13 дней назад +1

    Monster 👻 👽 Chakwera

  • @KeishaFeston
    @KeishaFeston 8 дней назад

    Koma ndaseka atimankhwala 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 iwowo analibe makwala ochosela ?😂😂

  • @alfredbanda1693
    @alfredbanda1693 13 дней назад +3

    Ku Malawi palibe amafa chifukwa choti moyo umatha. Aliyense akafa ndekuti wina wamupha. Ngozi, malaria,cholera kwathu kuno kulibe

  • @asiyatujuma5507
    @asiyatujuma5507 13 дней назад +1

    😭😭😭😭😭😭

  • @JMB804
    @JMB804 12 дней назад

    Dziko lapansi 🙌🏾😭

  • @davidkadyakapita8836
    @davidkadyakapita8836 8 дней назад

    Chakwera munthu oipa komanso wadyera kwambiri.

  • @user-nw6ie3xx8b
    @user-nw6ie3xx8b 13 дней назад +1

    That's propaganda

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 13 дней назад +2

    Zikhale ng'oma, chakwera, moses kumkuyu nose ofunika muona zakuda Magazi amunthu ndioopsa kwabasi 😭

  • @wysonkomela8223
    @wysonkomela8223 12 дней назад

    Dzikuveka nditu alongosoled bwino filimiyi sanayikite bwino ayi akanafuna njila ina

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v 13 дней назад +3

    Komaso. Chakwera asamale ndi anthu omwewo athaso kuzakuphani inu nomwe chakwera anthu amenewo mukupanga nawo chiwembuwo

  • @DesiderioLuis
    @DesiderioLuis 13 дней назад +1

    😭😭😭😭

  • @MasterHeadson-ki7ji
    @MasterHeadson-ki7ji 2 дня назад

    📌

  • @Ranwellmwaupighu
    @Ranwellmwaupighu 13 дней назад +1

    Koma

  • @ThandieGwayi
    @ThandieGwayi 13 дней назад

    zonvesa chisini eeeh mwana wayini ake ndithu wafa mmm

  • @frankbanda4074
    @frankbanda4074 13 дней назад

    Why speculate? Life comes and goes, agree people! Each one of us will die.

  • @SiphoPeterMachamo-fb5gd
    @SiphoPeterMachamo-fb5gd 10 дней назад

    Za ziiii umbuli ndi nthendadi eti😂

  • @user-tn4xm2dc2n
    @user-tn4xm2dc2n 9 дней назад

    Ifeyo tive ziti makamaka??

  • @JimmyIsaac-xd4ef
    @JimmyIsaac-xd4ef 13 дней назад +1

    😭😭😭

  • @LevisChimombo-om2th
    @LevisChimombo-om2th 7 дней назад

    Chakwera nd mfiti yosekerela

  • @Penjanichirwa
    @Penjanichirwa 13 дней назад +1

    😢😢😢😢😢

  • @dianelikhucha5546
    @dianelikhucha5546 13 дней назад

    yoombela ijaso mwaithyola mwaona kuti us not making sense?

  • @BillyNkhma
    @BillyNkhma 13 дней назад

    Ifeyo tivezit kod

  • @KhalideNerve-mu1eq
    @KhalideNerve-mu1eq 13 дней назад +1

    😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @ClintonMoffati
    @ClintonMoffati 13 дней назад

    MCP ufiti sidzaleka ndichipani chamagazi okhaokha

  • @user-io2uw2me9f
    @user-io2uw2me9f 7 дней назад

    Ineso ndimadabwa kut ma fn awo alikut anthu onsewo pot uku kunali kuntchire kunalibeko anthu oti angatole ma fnwo

  • @eliasnyilongo4865
    @eliasnyilongo4865 13 дней назад +1

    wamuphad mzake

  • @mafukenimasangwi5487
    @mafukenimasangwi5487 13 дней назад

    Chakwela ndi mwana pa ndale atupele adanena kumangomva kut anthu amapanga dinkamu lero ndiizo ayaluka nazo

  • @user-sk3ld2ss7s
    @user-sk3ld2ss7s 13 дней назад +1

    Muziphuzira, kulemekeza atsogoleri adzikolanu, ndinu cibebe, chopanda kanthu, chosokosa...

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 6 дней назад

    Anayiwala kuti mulungu.amaona zose

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z 6 дней назад

    So sad

  • @alexmkolongo3089
    @alexmkolongo3089 13 дней назад +1

    Azibusa a fk

  • @user-xc1gk6bw6m
    @user-xc1gk6bw6m 13 дней назад

    Mulungu amuwone munthu oipa amenei chakwera

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r 13 дней назад

    Abuye tengen

  • @BeatGondwa
    @BeatGondwa 13 дней назад

    Ndiwakuphadi uyu eeee waopsatu

  • @user-zg8rt3tz9g
    @user-zg8rt3tz9g 13 дней назад

    Ndipo ichi mukuti chachakwere ntchizereza chomene ndipo chikuninyasa 😡😡

  • @PreciuseMBinga
    @PreciuseMBinga 7 дней назад

    Ndikumati kut lelo kukubwera athu ochook ku Germany

  • @mathewsosman7313
    @mathewsosman7313 11 дней назад

    Maopsyo

  • @bernardbanda7821
    @bernardbanda7821 7 дней назад

    Mbuz

  • @stanleylemanichimwaza755
    @stanleylemanichimwaza755 13 дней назад +1

    Zoopisaa Iziii ndiwe mbuli

  • @NastonVickta
    @NastonVickta 13 дней назад

    Zikuveka

  • @Patie324
    @Patie324 13 дней назад

    Chakwera is a murder