Woza Friday comrade ntanyiwa more fireeeeeee the spirit of Chilima still moving muyaluka anthu azipembezo chifukwa cha dyera shame Mulungu akulangeni nonse anthu opanda chisoni
You have nothing to tell Malawians apart from your empty vendetta. Kulibe izoooooooo. Forget about all those idiots you are mentioning. Failed politicians.
Tili Pano mdicholinga cha Yehova sangatisiye tikulira achitapo kathu ndithu amenewa alandire zilonda ndithu mabala osapora ayende maliseche azingobwebweta We love you Ntanyiwa ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Koma mizimu ya anthu 9 awa mmm itikantha ndithu pangachedwe maka Ambuye tipatseni vumbulutso ndi mzimu wachidziwitso. Its becoming more scarily especially with this issie involving the clergy eish my Mw serious??
Komatu MCP ifa ya chilima mupedza mayo soka mudzimatsa anthu ndalama cholinga wadzelu ndipamene akudxiwa kuti mwapha chilima kuti mupitilile 2025 KKKKK NUTSO ADZIBUTSA MAPHETSA MWANA NDIKUMAPITATSO KOKO PANO ALIYETSE AKUDZIWA KUTI KUKOKOMANA NDI FITI YAFITI CHAKWELA NDE AKAPATSIDWA NDALAMA MAFUMU MABUTSA KAYA ENA AKHALA NDANI KOM ZIWANI NDALAMA YAMAGADZI CHAKWELA 2025 CHAKE PALIBE
Ndipo kungoti dziko lathu transparency ma nkhani ngati izi imasowa. If we are to calculate imfa ya ngoziyi yapangitsa dziko to spend billions of kwacha right away from ndege which beyond repair, all those officers who were involved in to transfer dead bodies to where the Zambian plane collected and flew to LLs. All those press briefing, private mortuary charges, coffins/caskets, all those vehicles to Church, area 12, parliament, BNS and finally to Nsipe. Honestly guys even the venue ku Nsipe and other related processes.
Am not fear, am a citizen of Malawi, Malawi is my home country as am home soil i have right of freedom of expression , right to life, so no one can't threat me if am doing right thing, working professionally, same applying to nonsense president Chakwera if you know you're doing right things to Malawians, why most citizens of Malawi were not happy with you? Beware Chakwera, the blood of Chilima and others is on your head you never have a peace in life.
My fellow Malawians the problem we are currently facing is that we cannot differentiate between the righteous and the hypocrites in churches, mosques,politics,and in all human gatherings
Additionally the Germany clue, trabsport, hotel charges, daily operstions etc, yet we have trillions of unpaid debt, are we serious? Chenicheni a malawi fe tikufuna chani ngati dziko makamaka atsogoleri? Mulungu tipatseni mavumbulutso otherwise we are moving backward more faster than the opposite direction.
Ndi chinthu chowawa kwambiri mu dziko losauka kwambiri kumakhala kumagawa ndalama za misonkho yathu kwa anthu ochepa ngati chitseka pakamwa pamene mzika zambiri zikuvutika ndi kudula zinthu kwa zinthu mu dzikoli. Bwanji ma million akugawidwawa kupereka ku ma kampani kuti zinthu zisapitilire kukwera?
Ulemu wanu limpopo fm .now time has come MCP must go chakwera and his friends must be arrested all including wamkulu wa asilikari ndi wamkulu wa a police ndindunazao zonse
A Malawi tikugulitsa ufulu ndi ndalama imagine to the extent yoti mpaka mipingo nkumakalandira ndalama Kamba ka imfa ya munthu this is very shameful!!!!!!
May these innocent Souls of Late Right Honorable Dr Saulos Klaus Chilima and other 8 Malawians continue resting in eternal Peace
Munasowatu comrade,wina athawa state house akuifuna tipemphere kwambili anthu anapha aja azimubwelera onse kuchipinda kwa ndi a kasambara omwe
Jesus said clergies sit on Moses seat believe whatever they tell you but don't follow them because they are hypocrites Matthew 23
You❤❤❤ have to exactly for tell us poor people true god bless you 💕 end keep it up ❤
Mmapemphero anthu tisayiwale kupemphaMulungu kuti apengese misala azibusa ansembe ndi wina aliyense amene wadya ndalama kuti imfa ya aChilima isa wululike
I will join that fasting zikutipweteka
Ngozi yagalimoto anthu amanyenyeka koma ya ndege ai ndithu kungovula ma jacket bas ati afa bwino. Ai zikomo a MCP
Nkhani yokoma zedi fasting idziyamba nthawi yanji ndipo izintha nthawi yanji tipatseni program
We follow you Mr Ntanyiwa Lero simunayimbe nawo kanyimbo kaja mizimu 9 I were pamutu pake pa chalakwe😂😂😂
Woza Friday comrade ntanyiwa more fireeeeeee the spirit of Chilima still moving muyaluka anthu azipembezo chifukwa cha dyera shame Mulungu akulangeni nonse anthu opanda chisoni
Msamasowe a comrade timadalira inu pachilungamo
Tiuzeni ifeyo Comrade Ntanyiwa tili pambuyo panu ife tili kuno ku South Africa tithana naye akusaka moyo wanuyu
Zoona brother tiyeini tisale kudya choonadi chidziwike
Wosadandaula tizikupemphelela brother we love you so much ❤❤❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉❤❤❤❤❤❤❤
People's Power, Don't Take People For Granted
Am waiting for you my brother came with it more fire i ❤❤❤❤❤❤ it
You have nothing to tell Malawians apart from your empty vendetta. Kulibe izoooooooo. Forget about all those idiots you are mentioning. Failed politicians.
Msunuwako bhuti
You too , you got nothing to answer him
Honestly speaking, a Mtanyiwa mmatiimilira. Myoyo yaanthu ambili omwe tikulilira justice mitima yathu imakhala nchiyembekezo chifukwa cha inu. Keep the 🔥 burning
Tili Pano mdicholinga cha Yehova sangatisiye tikulira achitapo kathu ndithu amenewa alandire zilonda ndithu mabala osapora ayende maliseche azingobwebweta We love you Ntanyiwa ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Mvuto kumalawi timangolongolola nthawi nkumatha maiko anzathuwa sangwatero mphamvu zimakhala ndi anthu osati atsogoleri
Athu akuzuzika ku malawi plz tiyeni tisangoonerera
Osaiwala Amene tikusala kudya tisale ndinyumba momwe
Koma mizimu ya anthu 9 awa mmm itikantha ndithu pangachedwe maka Ambuye tipatseni vumbulutso ndi mzimu wachidziwitso. Its becoming more scarily especially with this issie involving the clergy eish my Mw serious??
Dokotalayonso ndopusa amudyesera azinena mawumboni abozawi ayaluka ili ndi dziko awakatha oansi pompano ndithu mulungu wathu ndi wa noyo
Tipemphelere kuti Chakwera akakhara pampando adziyabwidwa mpaka authawe
After Kenya Malawi get ready
Chakwera ndi amene a apha chilkma
Buddy Ntanyiwa ‼️
Ulemu wanu bwana
Keep doing the needful ♥️🔥
Ntanyiwa we're together from fasting, until something happen, Rip SKC and 8 others
Tiyeni tipempheledi awakantha mulungu awonekela poyela amene anachita chipongwecho ndithu
Naye bakili muluxi waying'alula tu ku
Kodi Ndege ikagwa kumakhalanso kuona nkhope??
Kkkkkk nanenso kudabwa😊
Awalanga ndipo asala pang'ono
Amene akudana ndiyinu mutu sukuyenda ukubebesa ayise
Mwati a mpingo so konko dollar?????????
If is rue shame to you Bishops ,,,,bloody money!,!
Komatu MCP ifa ya chilima mupedza mayo soka mudzimatsa anthu ndalama cholinga wadzelu ndipamene akudxiwa kuti mwapha chilima kuti mupitilile 2025 KKKKK NUTSO ADZIBUTSA MAPHETSA MWANA NDIKUMAPITATSO KOKO PANO ALIYETSE AKUDZIWA KUTI KUKOKOMANA NDI FITI YAFITI CHAKWELA NDE AKAPATSIDWA NDALAMA MAFUMU MABUTSA KAYA ENA AKHALA NDANI KOM ZIWANI NDALAMA YAMAGADZI CHAKWELA 2025 CHAKE PALIBE
Nanga y we didn't see Ring or helicopter took it 😅😅😅😅😅
Kod pa limpopo pano timafuna kudziwa kuti msilikali wa kamudzu balakisi unja zikuti bwanji alimoyo kapena kulibe
Ine ndayamba kale kutsala
Moti kunyumbaku sindikudya
" Atampachika pa Mtanda anagawana msalu zake napanga mayere" . Those evil men akudziwa komwe kuli tie,Msapato 😂😂😂😂
Lampopo tioseni zoona
Sabasaba uja bwanji?
Mangochi boys tanola kare zida apa tikungodikila pa 10 ndipo munverako
Nanga lamba wa trauzer ndege ndiyomwe inamasulasoooooo
Ndiolotse ndikakutafune( Gona mkuphe.
chakwera ndi chigawenga ma chende abambo ake ndithu mfiti satana
Ndipo live tisara kudya brother allah atiyankha so soon
Mulungu wathu sangatisiye tikulila chonchi zanyanya
Ife kuno ku Capetown tili nanu PA 10 pano
Chakwera atupe mutu
May God protect you sir!
Amen
Limpopo fm koma iwe wabweraso
Following mwachidwi always......
Salute bigy limpopo
😂😂😂😂Apengedi misala amenewa iyaaa
Kom imfa ya Chilima yosaiwalikatu😭😭 Rest well Legend
Ndpo zoopsa 😢
Ndipo comrade Ntanyiwa tionjezekepo pa ma prayer petitions po kuti: Mulungu akanthenso onse amene akulandira ndalama ndi cholinga chofuna kubisa chilungamo komanso kuwatseka pakamwa Mulungu wodziwa kubwezera (Psalm 94) atero mdithu.
Za mapemphero ndi kusala zakudya. comrade fotokozani bwino bwino nthawi yomasulira fasting imeneyi chifukwa mwangoti 5 days Mon-Fri
inetso zinandi khuzakwabili
Yose mmakwana
Mulungu atithandizedi pazimenezi
Mukugwira ntchito bwana
Ndipo kungoti dziko lathu transparency ma nkhani ngati izi imasowa. If we are to calculate imfa ya ngoziyi yapangitsa dziko to spend billions of kwacha right away from ndege which beyond repair, all those officers who were involved in to transfer dead bodies to where the Zambian plane collected and flew to LLs. All those press briefing, private mortuary charges, coffins/caskets, all those vehicles to Church, area 12, parliament, BNS and finally to Nsipe. Honestly guys even the venue ku Nsipe and other related processes.
Apingoaja kunoooo
Umatha tiuzeni zoona tiziwe
LIMPOPO UMAKWANA UNA MWELA
Am not fear, am a citizen of Malawi, Malawi is my home country as am home soil i have right of freedom of expression , right to life, so no one can't threat me if am doing right thing, working professionally, same applying to nonsense president Chakwera if you know you're doing right things to Malawians, why most citizens of Malawi were not happy with you? Beware Chakwera, the blood of Chilima and others is on your head you never have a peace in life.
2024😅 2:19
2024😅
2024😅
2024😅
My fellow Malawians the problem we are currently facing is that we cannot differentiate between the righteous and the hypocrites in churches, mosques,politics,and in all human gatherings
You have my support prayerß job already And God is revange continue to save the people dont sale your grace .God bless u
DPP ndi amzawo akatenga boma mtanyiwa ndi bakili muluzi tv guys"kalindo mmm awa tizawapase zochita""
I support😂😂😂❤❤
Bakili Muluzi adzakhala minister of finance😅😅😅😅
Ayii akuyenera kukhala komwe aliko kupangira pa mawa
Nkhanga izooo!!!!
Lipopo FM good
My everything radio ❤ watching from Israel 😂
A NEW THINKER WILL GOVERN OUR LAND AM GOING TO END ALL THIS NONSENSE GARBAGE FOOLISHNESS HAPPENING TO OUR BEAUTIFUL LAND
Eish tinakusowa welcome back 🙏
God bless you ntanyiwa We're following you
Apenga misala aboma
Additionally the Germany clue, trabsport, hotel charges, daily operstions etc, yet we have trillions of unpaid debt, are we serious? Chenicheni a malawi fe tikufuna chani ngati dziko makamaka atsogoleri? Mulungu tipatseni mavumbulutso otherwise we are moving backward more faster than the opposite direction.
Tikumva
Komanso kwa omwe akulandira ndalamazi chonde tiziganizile kuti imfa yi ikanatichitikira ife tingamamve bwanji kumva kuti ena akupezerapo cholowa?
Ndi chinthu chowawa kwambiri mu dziko losauka kwambiri kumakhala kumagawa ndalama za misonkho yathu kwa anthu ochepa ngati chitseka pakamwa pamene mzika zambiri zikuvutika ndi kudula zinthu kwa zinthu mu dzikoli. Bwanji ma million akugawidwawa kupereka ku ma kampani kuti zinthu zisapitilire kukwera?
Iwe Mtanyiwa ndikatundu kwambiri. Limpopo ndiyokha radio ya ife 🇲🇼 oxindikira😢😢😢😅
Munthu wamkulu inendikudabwa atsogoleli azipembezo ali chete kodi sakuona zikuchitikazi? Nanga akudikiranso chani poti panopo zinthu sizilibwino
Chilima anakakamiziwa ndi azipembezo omwewa lero waphedwa akuona.
Ulemu wanu limpopo fm .now time has come MCP must go chakwera and his friends must be arrested all including wamkulu wa asilikari ndi wamkulu wa a police ndindunazao zonse
A Malawi tikugulitsa ufulu ndi ndalama imagine to the extent yoti mpaka mipingo nkumakalandira ndalama Kamba ka imfa ya munthu this is very shameful!!!!!!
We proud of guys God bless you
Mr Mtanyiwa kunja kwacha chilungamo chimveke timadalira inu mwadzuka bwanji kumenekoooooooooo
We are ready brother and we are together
Good prayer points.😢😢
I love you Mr comrade go ahead
This is true radio number one
Do your job guy we are proud of you.
How are you comered I mess you
BIG ULEMU WANU ANTANYIWA TILI LIMODZI ,KODITU OLO OSAVOTA KOMA CHAKWERA AKUCHOKA NDIPAMATAKO PONUKHAPO
Osaopa, osafooka mpaka zofuna zathu zikwanilisidwe kumanga malawi 🇲🇼 wathu
Haaa kodi mmabishop omwe akudyya thupi la anthu amene adwalira pangozi ya ndege ku chikangawa ayibo koma ndi my dangerous
Takunyadilani Mr Mtanyiwa.... Mulungu wathu ndiwamoyo ndipo ndiwamayankho