FRIDAY SPECIAL ON LIMPOPO FM NDI COMRADE NTANYIWA 28 JUNE 2025

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 1 окт 2024

Комментарии • 174

  • @PETERSINKADZIWA
    @PETERSINKADZIWA 3 месяца назад +8

    May these innocent Souls of Late Right Honorable Dr Saulos Klaus Chilima and other 8 Malawians continue resting in eternal Peace

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 3 месяца назад +5

    Munasowatu comrade,wina athawa state house akuifuna tipemphere kwambili anthu anapha aja azimubwelera onse kuchipinda kwa ndi a kasambara omwe

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 3 месяца назад +4

    Jesus said clergies sit on Moses seat believe whatever they tell you but don't follow them because they are hypocrites Matthew 23

  • @RiyemaDomybusiness
    @RiyemaDomybusiness 3 месяца назад +4

    You❤❤❤ have to exactly for tell us poor people true god bless you 💕 end keep it up ❤

  • @LiamTennessee
    @LiamTennessee 3 месяца назад +3

    Mmapemphero anthu tisayiwale kupemphaMulungu kuti apengese misala azibusa ansembe ndi wina aliyense amene wadya ndalama kuti imfa ya aChilima isa wululike

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 3 месяца назад +4

    I will join that fasting zikutipweteka

  • @EvanceJimmy-e6c
    @EvanceJimmy-e6c 3 месяца назад +3

    Ngozi yagalimoto anthu amanyenyeka koma ya ndege ai ndithu kungovula ma jacket bas ati afa bwino. Ai zikomo a MCP

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 3 месяца назад +3

    Nkhani yokoma zedi fasting idziyamba nthawi yanji ndipo izintha nthawi yanji tipatseni program

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 3 месяца назад +3

    We follow you Mr Ntanyiwa Lero simunayimbe nawo kanyimbo kaja mizimu 9 I were pamutu pake pa chalakwe😂😂😂

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 месяца назад +3

    Woza Friday comrade ntanyiwa more fireeeeeee the spirit of Chilima still moving muyaluka anthu azipembezo chifukwa cha dyera shame Mulungu akulangeni nonse anthu opanda chisoni

  • @ShiraKasekaNyirenda
    @ShiraKasekaNyirenda 3 месяца назад +3

    Msamasowe a comrade timadalira inu pachilungamo

  • @aligrayjeo1071
    @aligrayjeo1071 3 месяца назад +3

    Tiuzeni ifeyo Comrade Ntanyiwa tili pambuyo panu ife tili kuno ku South Africa tithana naye akusaka moyo wanuyu

  • @MaxwellMbesa
    @MaxwellMbesa 3 месяца назад +2

    Zoona brother tiyeini tisale kudya choonadi chidziwike

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 3 месяца назад +2

    Wosadandaula tizikupemphelela brother we love you so much ❤❤❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉❤❤❤❤❤❤❤

  • @masterchitabwino898
    @masterchitabwino898 3 месяца назад +2

    People's Power, Don't Take People For Granted

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 3 месяца назад +2

    Am waiting for you my brother came with it more fire i ❤❤❤❤❤❤ it

  • @GrivinSauka
    @GrivinSauka 3 месяца назад +2

    You have nothing to tell Malawians apart from your empty vendetta. Kulibe izoooooooo. Forget about all those idiots you are mentioning. Failed politicians.

  • @JohnChiwaya-ym5me
    @JohnChiwaya-ym5me 3 месяца назад +2

    Honestly speaking, a Mtanyiwa mmatiimilira. Myoyo yaanthu ambili omwe tikulilira justice mitima yathu imakhala nchiyembekezo chifukwa cha inu. Keep the 🔥 burning

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 3 месяца назад +2

    Tili Pano mdicholinga cha Yehova sangatisiye tikulira achitapo kathu ndithu amenewa alandire zilonda ndithu mabala osapora ayende maliseche azingobwebweta We love you Ntanyiwa ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @shuraimuwamama2349
    @shuraimuwamama2349 3 месяца назад +2

    Mvuto kumalawi timangolongolola nthawi nkumatha maiko anzathuwa sangwatero mphamvu zimakhala ndi anthu osati atsogoleri

  • @MphatsoMwale-it4xd
    @MphatsoMwale-it4xd 3 месяца назад +2

    Athu akuzuzika ku malawi plz tiyeni tisangoonerera

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 3 месяца назад +2

    Osaiwala Amene tikusala kudya tisale ndinyumba momwe

  • @RhoxinahMalamba
    @RhoxinahMalamba 3 месяца назад +1

    Koma mizimu ya anthu 9 awa mmm itikantha ndithu pangachedwe maka Ambuye tipatseni vumbulutso ndi mzimu wachidziwitso. Its becoming more scarily especially with this issie involving the clergy eish my Mw serious??

  • @YankhoGuza
    @YankhoGuza 3 месяца назад +2

    Dokotalayonso ndopusa amudyesera azinena mawumboni abozawi ayaluka ili ndi dziko awakatha oansi pompano ndithu mulungu wathu ndi wa noyo

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 месяца назад +2

    Tipemphelere kuti Chakwera akakhara pampando adziyabwidwa mpaka authawe

  • @johnmpatama1461
    @johnmpatama1461 3 месяца назад +2

    After Kenya Malawi get ready

  • @LazaroSinerioSineiro
    @LazaroSinerioSineiro 3 месяца назад +1

    Chakwera ndi amene a apha chilkma

  • @DaveDambo
    @DaveDambo 3 месяца назад +2

    Buddy Ntanyiwa ‼️
    Ulemu wanu bwana
    Keep doing the needful ♥️🔥

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em 3 месяца назад +1

    Ntanyiwa we're together from fasting, until something happen, Rip SKC and 8 others

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 3 месяца назад +2

    Tiyeni tipempheledi awakantha mulungu awonekela poyela amene anachita chipongwecho ndithu

  • @JamesMadina-uv6xe
    @JamesMadina-uv6xe 3 месяца назад +1

    Naye bakili muluxi waying'alula tu ku

  • @WezzieChimuzi-ek7bk
    @WezzieChimuzi-ek7bk 3 месяца назад +2

    Kodi Ndege ikagwa kumakhalanso kuona nkhope??

    • @BrightZionga
      @BrightZionga 3 месяца назад +1

      Kkkkkk nanenso kudabwa😊

  • @mensuremegrem8330
    @mensuremegrem8330 3 месяца назад +2

    Awalanga ndipo asala pang'ono

  • @CorencPromise
    @CorencPromise 3 месяца назад +2

    Amene akudana ndiyinu mutu sukuyenda ukubebesa ayise

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 3 месяца назад +2

    Mwati a mpingo so konko dollar?????????

  • @mariezorgen7735
    @mariezorgen7735 3 месяца назад +1

    If is rue shame to you Bishops ,,,,bloody money!,!

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 3 месяца назад +1

    Komatu MCP ifa ya chilima mupedza mayo soka mudzimatsa anthu ndalama cholinga wadzelu ndipamene akudxiwa kuti mwapha chilima kuti mupitilile 2025 KKKKK NUTSO ADZIBUTSA MAPHETSA MWANA NDIKUMAPITATSO KOKO PANO ALIYETSE AKUDZIWA KUTI KUKOKOMANA NDI FITI YAFITI CHAKWELA NDE AKAPATSIDWA NDALAMA MAFUMU MABUTSA KAYA ENA AKHALA NDANI KOM ZIWANI NDALAMA YAMAGADZI CHAKWELA 2025 CHAKE PALIBE

  • @IjilanMwalija
    @IjilanMwalija 3 месяца назад +1

    Nanga y we didn't see Ring or helicopter took it 😅😅😅😅😅

  • @StephanonachipoMakawa
    @StephanonachipoMakawa 3 месяца назад +1

    Kod pa limpopo pano timafuna kudziwa kuti msilikali wa kamudzu balakisi unja zikuti bwanji alimoyo kapena kulibe

  • @KimDexonAdamson
    @KimDexonAdamson 3 месяца назад +1

    Ine ndayamba kale kutsala
    Moti kunyumbaku sindikudya

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 3 месяца назад +1

    " Atampachika pa Mtanda anagawana msalu zake napanga mayere" . Those evil men akudziwa komwe kuli tie,Msapato 😂😂😂😂

  • @SamamaMagone
    @SamamaMagone 3 месяца назад +2

    Lampopo tioseni zoona

  • @sylviachisama3829
    @sylviachisama3829 3 месяца назад +2

    Sabasaba uja bwanji?

  • @SalemFund
    @SalemFund 3 месяца назад +1

    Mangochi boys tanola kare zida apa tikungodikila pa 10 ndipo munverako

  • @GiftPhiri-tt7nn
    @GiftPhiri-tt7nn 3 месяца назад +1

    Nanga lamba wa trauzer ndege ndiyomwe inamasulasoooooo

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 3 месяца назад

    Ndiolotse ndikakutafune( Gona mkuphe.

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 3 месяца назад +1

    chakwera ndi chigawenga ma chende abambo ake ndithu mfiti satana

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 3 месяца назад +1

    Ndipo live tisara kudya brother allah atiyankha so soon

  • @reginakamaliza8414
    @reginakamaliza8414 3 месяца назад +1

    Mulungu wathu sangatisiye tikulila chonchi zanyanya

  • @FloridaMakwinja-eq2ek
    @FloridaMakwinja-eq2ek 3 месяца назад +1

    Ife kuno ku Capetown tili nanu PA 10 pano
    Chakwera atupe mutu

  • @AiameAdamo-su1nt
    @AiameAdamo-su1nt 3 месяца назад +1

    May God protect you sir!

  • @AyandaJanga-fe7wp
    @AyandaJanga-fe7wp 3 месяца назад +1

    Amen

  • @NastonVickta
    @NastonVickta 3 месяца назад +1

    Limpopo fm koma iwe wabweraso

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 3 месяца назад +1

    Following mwachidwi always......

  • @GiftManuel-er7yh
    @GiftManuel-er7yh 3 месяца назад +1

    Salute bigy limpopo

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 месяца назад +1

    😂😂😂😂Apengedi misala amenewa iyaaa

  • @YamzyNedson
    @YamzyNedson 3 месяца назад +2

    Kom imfa ya Chilima yosaiwalikatu😭😭 Rest well Legend

    • @mthawisakaunda
      @mthawisakaunda 3 месяца назад

      Ndpo zoopsa 😢

    • @RhoxinahMalamba
      @RhoxinahMalamba 3 месяца назад

      Ndipo comrade Ntanyiwa tionjezekepo pa ma prayer petitions po kuti: Mulungu akanthenso onse amene akulandira ndalama ndi cholinga chofuna kubisa chilungamo komanso kuwatseka pakamwa Mulungu wodziwa kubwezera (Psalm 94) atero mdithu.

    • @RhoxinahMalamba
      @RhoxinahMalamba 3 месяца назад

      Za mapemphero ndi kusala zakudya. comrade fotokozani bwino bwino nthawi yomasulira fasting imeneyi chifukwa mwangoti 5 days Mon-Fri

  • @PreciousLuwis
    @PreciousLuwis 3 месяца назад

    inetso zinandi khuzakwabili

  • @Bonisiwentamo
    @Bonisiwentamo 3 месяца назад +1

    Yose mmakwana

  • @ElasonAimon
    @ElasonAimon 3 месяца назад +1

    Mulungu atithandizedi pazimenezi

  • @KelvinMangwengwe
    @KelvinMangwengwe 3 месяца назад +1

    Mukugwira ntchito bwana

  • @RhoxinahMalamba
    @RhoxinahMalamba 3 месяца назад

    Ndipo kungoti dziko lathu transparency ma nkhani ngati izi imasowa. If we are to calculate imfa ya ngoziyi yapangitsa dziko to spend billions of kwacha right away from ndege which beyond repair, all those officers who were involved in to transfer dead bodies to where the Zambian plane collected and flew to LLs. All those press briefing, private mortuary charges, coffins/caskets, all those vehicles to Church, area 12, parliament, BNS and finally to Nsipe. Honestly guys even the venue ku Nsipe and other related processes.

  • @HassanMufase
    @HassanMufase 3 месяца назад +1

    Apingoaja kunoooo

  • @MussahMalidadi
    @MussahMalidadi 3 месяца назад +1

    Umatha tiuzeni zoona tiziwe

  • @PreciousLuwis
    @PreciousLuwis 3 месяца назад

    LIMPOPO UMAKWANA UNA MWELA

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 3 месяца назад

    Am not fear, am a citizen of Malawi, Malawi is my home country as am home soil i have right of freedom of expression , right to life, so no one can't threat me if am doing right thing, working professionally, same applying to nonsense president Chakwera if you know you're doing right things to Malawians, why most citizens of Malawi were not happy with you? Beware Chakwera, the blood of Chilima and others is on your head you never have a peace in life.

  • @JonathanHeadson
    @JonathanHeadson 3 месяца назад +1

    2024😅 2:19

  • @JonathanHeadson
    @JonathanHeadson 3 месяца назад +1

    2024😅

  • @JonathanHeadson
    @JonathanHeadson 3 месяца назад +1

    2024😅

  • @JonathanHeadson
    @JonathanHeadson 3 месяца назад +1

    2024😅

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 3 месяца назад

    My fellow Malawians the problem we are currently facing is that we cannot differentiate between the righteous and the hypocrites in churches, mosques,politics,and in all human gatherings

  • @ProphetessEzinass-qu4ir
    @ProphetessEzinass-qu4ir 3 месяца назад

    You have my support prayerß job already And God is revange continue to save the people dont sale your grace .God bless u

  • @Dellingsmunthali
    @Dellingsmunthali 3 месяца назад +1

    DPP ndi amzawo akatenga boma mtanyiwa ndi bakili muluzi tv guys"kalindo mmm awa tizawapase zochita""

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus 3 месяца назад

      I support😂😂😂❤❤

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus 3 месяца назад

      Bakili Muluzi adzakhala minister of finance😅😅😅😅

    • @SalemFund
      @SalemFund 3 месяца назад

      Ayii akuyenera kukhala komwe aliko kupangira pa mawa

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 3 месяца назад +1

    Nkhanga izooo!!!!

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 3 месяца назад +1

    Lipopo FM good

  • @RoseChiphiri-ts8jx
    @RoseChiphiri-ts8jx 3 месяца назад

    My everything radio ❤ watching from Israel 😂

  • @leonardjika2100
    @leonardjika2100 3 месяца назад

    A NEW THINKER WILL GOVERN OUR LAND AM GOING TO END ALL THIS NONSENSE GARBAGE FOOLISHNESS HAPPENING TO OUR BEAUTIFUL LAND

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 месяца назад

    Eish tinakusowa welcome back 🙏

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 3 месяца назад

    God bless you ntanyiwa We're following you

  • @nellikkmwenda7087
    @nellikkmwenda7087 3 месяца назад +3

    Apenga misala aboma

  • @RhoxinahMalamba
    @RhoxinahMalamba 3 месяца назад

    Additionally the Germany clue, trabsport, hotel charges, daily operstions etc, yet we have trillions of unpaid debt, are we serious? Chenicheni a malawi fe tikufuna chani ngati dziko makamaka atsogoleri? Mulungu tipatseni mavumbulutso otherwise we are moving backward more faster than the opposite direction.

  • @Jamesmwale-iz4ri
    @Jamesmwale-iz4ri 3 месяца назад +1

    Tikumva

  • @RhoxinahMalamba
    @RhoxinahMalamba 3 месяца назад

    Komanso kwa omwe akulandira ndalamazi chonde tiziganizile kuti imfa yi ikanatichitikira ife tingamamve bwanji kumva kuti ena akupezerapo cholowa?

  • @RhoxinahMalamba
    @RhoxinahMalamba 3 месяца назад

    Ndi chinthu chowawa kwambiri mu dziko losauka kwambiri kumakhala kumagawa ndalama za misonkho yathu kwa anthu ochepa ngati chitseka pakamwa pamene mzika zambiri zikuvutika ndi kudula zinthu kwa zinthu mu dzikoli. Bwanji ma million akugawidwawa kupereka ku ma kampani kuti zinthu zisapitilire kukwera?

  • @TressLuka
    @TressLuka 3 месяца назад

    Iwe Mtanyiwa ndikatundu kwambiri. Limpopo ndiyokha radio ya ife 🇲🇼 oxindikira😢😢😢😅

  • @highcallingglobalministries
    @highcallingglobalministries 3 месяца назад

    Munthu wamkulu inendikudabwa atsogoleli azipembezo ali chete kodi sakuona zikuchitikazi? Nanga akudikiranso chani poti panopo zinthu sizilibwino
    Chilima anakakamiziwa ndi azipembezo omwewa lero waphedwa akuona.

  • @OssmanAbubaker-st7pu
    @OssmanAbubaker-st7pu 3 месяца назад

    Ulemu wanu limpopo fm .now time has come MCP must go chakwera and his friends must be arrested all including wamkulu wa asilikari ndi wamkulu wa a police ndindunazao zonse

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 3 месяца назад

    A Malawi tikugulitsa ufulu ndi ndalama imagine to the extent yoti mpaka mipingo nkumakalandira ndalama Kamba ka imfa ya munthu this is very shameful!!!!!!

  • @MosesTangwe
    @MosesTangwe 3 месяца назад

    We proud of guys God bless you

  • @MerryWayson
    @MerryWayson 3 месяца назад

    Mr Mtanyiwa kunja kwacha chilungamo chimveke timadalira inu mwadzuka bwanji kumenekoooooooooo

  • @AyandaJanga-fe7wp
    @AyandaJanga-fe7wp 3 месяца назад

    We are ready brother and we are together

  • @crosbyphiri1745
    @crosbyphiri1745 3 месяца назад

    Good prayer points.😢😢

  • @MAFUNSOMOLESI
    @MAFUNSOMOLESI 3 месяца назад

    I love you Mr comrade go ahead

  • @SmartJumbe
    @SmartJumbe 3 месяца назад

    This is true radio number one

  • @ZondoChirwa
    @ZondoChirwa 3 месяца назад

    Do your job guy we are proud of you.

  • @IbrahimLibwalo-kz1ip
    @IbrahimLibwalo-kz1ip 3 месяца назад

    How are you comered I mess you

  • @HaliJana
    @HaliJana 3 месяца назад

    BIG ULEMU WANU ANTANYIWA TILI LIMODZI ,KODITU OLO OSAVOTA KOMA CHAKWERA AKUCHOKA NDIPAMATAKO PONUKHAPO

  • @HarryNtanga
    @HarryNtanga 3 месяца назад

    Osaopa, osafooka mpaka zofuna zathu zikwanilisidwe kumanga malawi 🇲🇼 wathu

  • @OmarMkwela
    @OmarMkwela 3 месяца назад

    Haaa kodi mmabishop omwe akudyya thupi la anthu amene adwalira pangozi ya ndege ku chikangawa ayibo koma ndi my dangerous

  • @WezzieChimuzi-ek7bk
    @WezzieChimuzi-ek7bk 3 месяца назад

    Takunyadilani Mr Mtanyiwa.... Mulungu wathu ndiwamoyo ndipo ndiwamayankho