Mbiri ya Kell Kay_chiyambi chake_moyo wake Oimba ndi chuma chake

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 20 сен 2024

Комментарии • 38

  • @MosesMatupi
    @MosesMatupi 21 день назад

    Zeze..ndavomera

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson1443 Год назад

    Always on point bro .... Bravo bravo Mr sam mukubwela nyatwa mn

  • @AlbertKabaghe
    @AlbertKabaghe 6 месяцев назад

    Ndalama zachepa sangakhale ndi 17 million

  • @JonathanMulimba
    @JonathanMulimba Год назад

    Mbiri yaketu ndy mwadumpha zambiri eeeee!! Kkk

  • @victoriasululu7563
    @victoriasululu7563 Год назад +1

    Mpesa ndi number one

  • @thomasgamah764
    @thomasgamah764 Год назад +1

    Very analysed story big up sam

  • @Thoccokavalo
    @Thoccokavalo 5 месяцев назад

    My favorite ❤

  • @Allieshaibu8612
    @Allieshaibu8612 Год назад +2

    All the way we together

  • @hucklyrajabu7137
    @hucklyrajabu7137 Год назад

    Kodi akulu skeffa chimoto wawina ma award angati chiyambireni kuimba

  • @StanfordBanda-f6f
    @StanfordBanda-f6f 9 месяцев назад

    Koma tiyiziwe ntchito yinayo kupatura kuyimba mwafotokoza zonse mulephele job yake

  • @GZONEZAMUMTIMA
    @GZONEZAMUMTIMA 4 дня назад

    Amatha

  • @gracianbinali2272
    @gracianbinali2272 Год назад

    Nde Ma Sister Akewo Ma Ina Ao ATI Ndi Ati
    Cuz Cross Ndi Imeneyo Tiwafuxe Ma Pahe Muuu

  • @BusyBlain-yv1ci
    @BusyBlain-yv1ci 6 месяцев назад

    Sukuyizwa mbili yake

  • @hucklyrajabu7137
    @hucklyrajabu7137 Год назад +1

    Ma a ward amenewo ndiogura kkkkkkkk kma abale Kelly k mpaka kuwina amaziwanso kuimba

  • @HaliJana
    @HaliJana Месяц назад

    CHAKWERA MACHEDE WAKO CHILIMA KUKUYIKA PA MPANDO IWE NDIKUMUPHA UMAGANIZA BWANJI MBUZI YAMUNTHU PANYO PA MAKO WAVA CHAKWERA NDIPO SITIKUKUFUNASO AI IWE MCP YATHELA KU CHIKANGAWA

  • @PreciousDube-ze7wc
    @PreciousDube-ze7wc Год назад

    Exactly do something special

  • @gifahumphrex2454
    @gifahumphrex2454 Год назад

    Inu amabodza khan za Matse Nd kell kay zodanazo nde kusokonezako

  • @EmmieEmmie-y2f
    @EmmieEmmie-y2f Год назад

    Nymbo zake szmandgwra mtima bolanso za Matse

  • @danielkhinguirossejuliasse6106

    Zachepa kwambili ndarama zo ka
    Kumalawiko zinthu ndizovutadi eti?

  • @christopherbottoman9131
    @christopherbottoman9131 Год назад

    Oyimba akumalawi ndiye mwati alindindalama zingati ayi anyway 🤦🤦🤦💐💐

  • @petermasenti2084
    @petermasenti2084 Год назад

    Zilibwino big koma ngati kotheka mutipasireko mbiri ya thomas chibade

  • @Kassamajibu
    @Kassamajibu Год назад

    😂😂😂zosangalatsa ndithu koma za Ndalamazo ndaletse coz mukhodza kudziwa zomwe zili pa public zokha

  • @MEATV-qb4zi
    @MEATV-qb4zi Год назад

    Wawa

  • @justinedamson8862
    @justinedamson8862 Год назад

    Zili bwin ndipo pitilizan kutiberesela zabwn

  • @stevenkananji8509
    @stevenkananji8509 Год назад

    Izizi ndimaloto ndithu koma ndakhala ndikukutsata ndipo ndinapeza kuti iwe umakhala mbali ya namadingo koma maganizo amalawi salingati ako let him come out and see what malawi will say nthawi yamavote ikadzakwana, asamale tindalama taketo koma musamupusitse za ndale mudzangomusautsa mwana

  • @emmamolande8193
    @emmamolande8193 Год назад

    17 million ndizaboza people with 17m they look poor than him try to find out his netwoth

  • @alickkachepa3801
    @alickkachepa3801 Год назад

    Ukunena chulungamo.....

  • @youngestincharge5390
    @youngestincharge5390 11 месяцев назад +1

    Alongo status not awiri

  • @ronaldchirwa253
    @ronaldchirwa253 Год назад

    Ndi dolo

  • @Rafique948
    @Rafique948 Год назад

    All the way we together ❤