Ndipo wina ayaluka pa ground chifukwa ndi Mfundo zomwe alibe amawakwapulira Mfundo ndiye anamutafunira ku CHIKANGAWA. Chi........te cha President kudzolowera kuphyodza Magazi ndi mikodzo . Ngakhale Ku ma MP MCP ilira . Tilipano kuonera. Keep moving forward the DC Bon Kalindo
Nthata zanjala zikuyamwa mazi wa amalawi modetsa nkhawa,DCamanena zoona pamodzi ndi amnzake aja.Mayi akutitakata.Nthawi inu a opposition mukugona tulo chenjerani.These are turning up every stone not leaving any stone unturned.
Malawi Sali bwino dziko anthuwa aliwononga 1 rand panopa ikusinthidwa pa 183 kwacha for the very first time in malawi history but am sure ifika 200 soon
Ndimanena nthawi zonse kuti maboma a mbuyomu amaba inde koma timadya komanso dzinthu dzimayenda bwino osati idzidzi kuba kopanda plan ndichifukwa tikuti APM abwelele
Bon kalindo woyeeeee! Mumatiyimilira inuyo mulungu azikudalisani pamene mungayende ndi pamene mungakhale keep it up
Umakwana here from Capetown God bless you ❤
Ndipo wina ayaluka pa ground chifukwa ndi Mfundo zomwe alibe amawakwapulira Mfundo ndiye anamutafunira ku CHIKANGAWA. Chi........te cha President kudzolowera kuphyodza Magazi ndi mikodzo .
Ngakhale Ku ma MP MCP ilira .
Tilipano kuonera.
Keep moving forward the DC Bon Kalindo
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥 more more more more more fire fire mr God bless you nd protect you
Amen 🙏🙏🙏 God bless you the DC everything for you amen 🙏🙏🙏
Listening from Capetown more fire Kalindo I'm behind you. ❤
Ipaseni Moto lfe pambuyo panu bass💥💥💥💥💥🔥👍👍
Booon Kalindo the DC 🔥🔥💪💪 mwana wachabe kwambili
The best one brother Bon Kalindo 🔥🔥🔥🔥
Viva the DC viva we want peace in our country not peaces 😢
The DC may God bless you and protect you ❤❤❤
The DC mumakwana❤❤
Big up the DC forward ever backwards never,,,God bless you
We are in democracy.I wish to suggest national re-registration of voters.First, form Government of Unity for free and fair Sept. tripartite polls.
Mwana owopsaaaaaaa kwambiri ❤❤❤❤
Bon kalindo God bless you all the time am with you
i will always pray for you, may the GOOD GOD CONTINUE TO PROTECT YOU 🙏🙏😅
bon kalindo ❤from Cape Town mitchells plain town centre
The Dc❤❤❤❤
The DC❤❤❤
the DC akatundu 🔥🔥💪 chesaopa
Umatimilira The Dc
The dc ❤️❤️
The DC the President of the less privileged people in Malawi.
You represent Us
Born kalindo more fire atikwana amenewa😮😮😮😮
Big ulemu wanu 😂😂
The DC🎉🎉
Dc🎉🎉🎉
THE DC🎉🎉🎉,mumakwana bigeeee
Long live legend ❤❤
You are the one Bon kalindo
The DC 🔥🔥🔥🔥
Osafoka DC ❤❤
The DC♥️♥️♥️😊
😅😅😅😅 koma the DC umakwana more 🔥 am coming 🎉🎉🎉🎉
Yes Yes
Kkkkkkkk akulakula matako eti ali abambo koma akulakula matako ngat azimayi 😂😂😂😂
Viva Kalindo Viva!!!!!!!
Mwana woooooooopsa kwambili ❤❤❤❤❤
Mcp ndaona makape koma mcp kuli makape thawi sikuyima kkkkkkkk olo mungone ikuyenda😂zitsiru
Thanks Born Kalindo mwainu tikondwera
Uyu mkatundu omanga ndimawaya tiyenaooooo,😮😮😮😮😮😮❤❤❤❤❤🎉
Awe
Mmakwana akalindo
But you Bon Kalindo, 😅😅😅😅,you are someone ..😂😂
Mwana owopsa kwambiri
Fire Mr born kalindo timadara inuyo
DC UMATIYIMILILA IFE OSAWUKA TILI PAMBUYO PANU
The DC❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Eya ku Dpp-ku eeeh sikunali bwino, koma ngati Mulungu angawapase mmpata akuenela ku zasintha basi .
Nthata zanjala zikuyamwa mazi wa amalawi modetsa nkhawa,DCamanena zoona pamodzi ndi amnzake aja.Mayi akutitakata.Nthawi inu a opposition mukugona tulo chenjerani.These are turning up every stone not leaving any stone unturned.
Ndimakuziwa Dc sumawopa
Umakwana the DC
Dc munabwela osafooka💪💪
😂😂😂 DC 🎉🎉🎉
The DC 🎉🎉🎉
Yes muthu wakulu never give up 🏃♂️🏃♂️🤸♂️
The DC......❤
The Dc ❤😂😂😂
Tatulusani ndodozo the DC plz
Inuyo ndimachine🎉🎉🎉❤❤Dc❤
Machine 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Ayelekeze kukumanga ife tikachezela pa area 30 po ndizibwana zimenezo
Mumukumbukenge skc pa campaign imwe wa mcp
Katswiri,🔥
I love you boss
The DC ❤❤❤❤❤❤❤❤❤😂😂😂😂
kalindo yes yes kkkkk minatha
Kalindo is a culprit!
Pango lini
Dpp sinalakwe, unapangisa ndiyiweyo kalindo Ntambo chilima kaliyati, anthu inuyo ndamene munaika amalawi pamoto
Amayendera chiungamo DPP imalakwisanso. Musiyeni ali ndi chilungamo. Amanena momwe zilili
😂😂😂😂Dc
Uyu akuti chimwendo Banda matako kutalika mpaka kufika mu nsana koma mimba kuchita kuyambila ku khosi abale. Tamadyani bwino ndalamazi. Savage
Boncalindo mulungu azikutetezerani timadalila inuyo bro
😂😂😂😂😂 ATI ine sindi manyengelera nd mangonena eeeee DC sadzatheka 😂😂😂😂
Ati ndingobwera ndekha kapena 🤣🤣🤣🤣🤣
a opposition azang'wempha adzatuluka mamina MPHUNO MKAMWA NDI MMAKUTU kuzimva kwambiri
The DCCCCC❤❤❤❤❤❤❤
Solution yomupha chilima kunali kuganiza mwaumbuli kwa MCP Chifukwa chilima anali mmalawi and it was agreed kuti mulamulila 5 yrs winanso 5yrs, Achakwela ngati mumapemphela mumangotaya nthawi yanu
❤❤❤❤
Yaa
Mumatiimilila bwana, mumanena chilungamo
DC mwana wachabe kkkkkkkk
Viva kalindo
Iwe wati nthata zanjala 😂😂😂😂😂😂 zoona
Auzeni zenizeni a DPP ankameraso mapiko kwabasi kuiwala kuti Malawi amaona Ndipo asinthe adzapoze mabala tilinawowa
Malawi Sali bwino dziko anthuwa aliwononga 1 rand panopa ikusinthidwa pa 183 kwacha for the very first time in malawi history but am sure ifika 200 soon
The DC mwana wakwathu kumulanje
Iwe ndidolo
Viva kalindo DC
The DC
Vuto anthuwa safuna kt azatese mavuto km azigwadilidwa ngati mulungu vuto Malawi tilibe umozi tidakali ntulo kukonda ndale mwalo molikonda ziko lathu
ruclips.net/video/o0g35X9MOE0/видео.htmlfeature=shared
Mphamvu the dc
Umakwana
M'banga weni weni
Big Big umatiyimilatu
Koma pa mumba ndiye ukunyika kwambiri
😂😂😂😂komaa kupereka phone number kodi
Ndimanena nthawi zonse kuti maboma a mbuyomu amaba inde koma timadya komanso dzinthu dzimayenda bwino osati idzidzi kuba kopanda plan ndichifukwa tikuti APM abwelele
Ngat mumange kalindo Ineso mundimange
😂😂😂😂 eti inu munthu mmodzi koma a police mbwelele apapa
Tribalism a DPP ndi quarter system mbola
MCP mfiti
Mr DC tili pa mbuyo panu
Ndipo live ❤❤❤