Limpopo iiiih! ma demo ajatu kwabwela anthu akunja kudzaletsa atapangidwa hayala Ntanyiwa waulura

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 4 июл 2024

Комментарии • 99

  • @ShaolinThomas-ow8yn
    @ShaolinThomas-ow8yn 12 дней назад +7

    Inuyo mulungu adzingokuonjexelani moyo wautali basi ,chifukwa mukutimvetsa kukoma

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b 12 дней назад +13

    We won't fear anything even as Zambian s were coming in Malawi guys to fight that evil man chakwela

  • @mellipherjohn7158
    @mellipherjohn7158 10 дней назад +1

    umakwana mtanyiwa tikuziwa zambili amalawi ambuye azikupasani moyo wautali 🎉🎉🎉🎉

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 11 дней назад +2

    Akulu akulu mukulankhula koma sitikumva 😢

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba 11 дней назад +3

    Koma iweyo pokhapa pot awagwila ndakuimikila manja mwamba athuo agwidwad

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 12 дней назад +3

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa.

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 11 дней назад +2

    Asilikari anthu ntchito yao ndi kuchinda mahule mutchesi umu😂😂

  • @PeterMphanza
    @PeterMphanza 6 дней назад

    Nice job comred mwana wa amama kuno ku Zambia

  • @UsenLashid
    @UsenLashid 11 дней назад +2

    Komaso Mr ntanyiwa musalore Kuti anthu 8 amene agwidwawo asatuluke Ayi kufikila chakwela atule pansi udindo komaso dziko la South Africa asawapange rilizi Ayi kufikila lamampho atamuzenga mulandu chakwela

  • @WatsonNtchito
    @WatsonNtchito 10 дней назад +1

    Mademo akayambire kumamfumu hotel komweko tiyeni tonse tikasokhane popo pa mfumu hotel ku ma room achulidwawo osaopa

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda 11 дней назад +2

    Akatula udindo chakwerayo, azibale ake onse azachotsedwe ntchto. Galu watitopetsa

  • @user-ht7vs3dp2u
    @user-ht7vs3dp2u 12 дней назад +2

    Ntanyiwa iweyo ndi number one radio yako timainyadira kom athu athawa ziko lili rawo kom kumeneko moto kuti buuuuu mumtimamo angokhuta mphuma lokhalokha km mulimba Ntanyiwa woyeee

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 11 дней назад +1

    Asilikali a ku Malawi ndi ogona tulo zitsilu zimalimbana ndi anthu wamba usayelekeze kuvala kabudula wa makaka ndiye amaonesa mphamvu zawo ati wavala unform yawo mbudzi

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 11 дней назад +2

    Koma chakwera wandikwana one day ndi kupedza people they call gringo

  • @Hassankazembe-d3o
    @Hassankazembe-d3o 11 дней назад +1

    May God bless you comrade Ntanyiwa

  • @BitonFred
    @BitonFred 9 дней назад

    Anthu akumalawi umbuli, anachotsa peter, ati wabwino chakwera, pano akufuna peter yemwe uja, mmalawi wanzeru sakuyenera kupeleka vote ku president yemwe analephera kale, votelani atsopano osati apeter muthalika

  • @CadTafa2
    @CadTafa2 12 дней назад +3

    Apolici a malawi a kuzishipisa

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 12 дней назад +3

    Pano malawi ndi North Korea 😭😭😭

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi 11 дней назад

    Apapa ndatanganidwa kuwerenga nkunvesera😂😂

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal 11 дней назад +1

    Anthu nonse amene mukudana ndi nthanyiwa mitungati zoswera malambe inu zikukusangalasani mmene akuyendesela dzikoli gule wanuyi achoke alibe phindu

  • @BrunoChakukuma
    @BrunoChakukuma 10 дней назад

    Ntanyiwa woyeeeee

  • @misoMoyo
    @misoMoyo 11 дней назад

    Limpopo FM ineyo ndimachedwa Ku ntchito kuti ndimvere basi nkhani ZANU mumandidalitsa ine ndi m,ngoni weni weni more fire inuyo a Mr Ntanyiwa

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 11 дней назад

    Ankolo ku malawi kulibe a silikali akanakhala kuti alipo zikuchita galu ameneyo mukumuti chokwerayu atamukhazika kale pansi, koma nawo asankha kugwirantchito ndi chipani ayiwala makamulo awo ndi mbuzi za silikali za manu pansi ndi mbuyao chakwerayo tionana chaka cha mawa onse amene akupha ndi chakwera tikhaulitsa boma ili lapita olo ataopseza motani zosatheka

  • @blacksonpeshes5057
    @blacksonpeshes5057 11 дней назад

    kom mukutivetsa kukoma ndikapanda kuva uthenga kuchokela kwainu sindipuma bwino kod mudarikuti mosemunja

  • @PartsonMdeza
    @PartsonMdeza 10 дней назад

    nkhanga zaonaaa

  • @DuntumaziyaDuntumaziya
    @DuntumaziyaDuntumaziya 11 дней назад +1

    following you sir

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 11 дней назад

    Kuti muone ku mcp kuli anthu osaoneka bwino okhaokha pamaso ndionyasa ndi mtima momwe

  • @JaneLikome
    @JaneLikome 11 дней назад

    Nice mr ntanyiwa

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 11 дней назад

    Ndipo chakwera tidzachita kuotcha pamoto chifukwa chankhanza akuchitazi

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 11 дней назад

    Comredy mtanyiwa tikufuna number yanu tizipephela Nanu mulungu azikudalisani kwambili ndipo azikutetezani kulikose komwe mukuyenda

  • @JamesIsaac-zi4kb
    @JamesIsaac-zi4kb 11 дней назад

    Chakwela ofuna adibwe kanyenya basi

  • @MikeMerecah
    @MikeMerecah 11 дней назад

    Ma activists athu musakhare chete kunoko akumangidwa mwachisisi mudziwe zimenezi, anthu osatchuka panopa Ali ku area 30 guyz,

  • @NisharChibisa
    @NisharChibisa 12 дней назад +1

    Mumakwana

  • @AjibuTwalibu
    @AjibuTwalibu 11 дней назад

    Umakwana ya mtanyiwa tili nawenawe my brother

  • @AugustineIshmael
    @AugustineIshmael 10 дней назад

    Zachamba basi dikilani 2025 vote yanu ndiye nuclear power osati zabibi zanuzi

  • @Bonisiwentamo
    @Bonisiwentamo 12 дней назад

    ❤Zowona acc muthu ameneyu AChoke

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 11 дней назад

    Chakwela ndikanankhala kuti ndimatha ufiti ndinakamchosa ineyo manyi akee anthu

    • @EllenPhiri-xt8pt
      @EllenPhiri-xt8pt 11 дней назад

      Chitsilu chichakwela ndi family yake yonse ambuye tichotseleni munthuyi😊

  • @maluli5691
    @maluli5691 11 дней назад

    Asilikali Aku malawi ndi asilikadzi.west Africa asilikali sakunyengelela kulanda boma

  • @YONA-v5o
    @YONA-v5o 12 дней назад

    Anthu amenewo ngat agwidwa aphedwe ndinthu cifukwa iwowo anabwela kuzapha

  • @stanleychisasa4343
    @stanleychisasa4343 11 дней назад

    Boss mbuyomu munatiuza kuti athu aku German ofufuza ndege aja anali okonza miseu lero muti ndi aku butcher which is which
    Big man?

  • @user-vu4cz1mt4f
    @user-vu4cz1mt4f 11 дней назад

    Tisayembekezere kuti tingamve munthu wakuphayo kuti ndine ndapha mayz ?
    Munona kt wakupha kufufuza chifkwa chomwe wina wafera koma atapha ndiyeyo ?
    Mayankho ndiomwewa omwe tikumayankhulawa coz action ikuchitatu kuoneka yokha ndipo mwachindunji monga kumangidwa anthu then kulowesa zigawenga nde ngt akusakidwa anthuwa kuti aphedwe nde nkumat ena omwe adafa aja anafera zina ?

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 12 дней назад

    M C P -- Malawi Congress Party
    M C P = Malawi Chikangawa Party 👹👹👹🔨⚒️⛏️

  • @GetrudeBanda-sd1yf
    @GetrudeBanda-sd1yf 12 дней назад

    Zoonad amalawi azimai tizingoyang'anira nyasizi bvuto azimai timatengrka ndi kathu kochepa

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 11 дней назад

    mademo mpanga komweko ku lilongwe ayi mkanya

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 11 дней назад

    zinamizanani pano pa limpopo kwachwera ali pheee kukozanyasi zomwe inapanga dpp . alikuti anthu omwe agidwa aaa opusi mtanyiwa

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon 11 дней назад

      Iwe mutuwako suyenda ngati akutuma a mcp anthu akufinya ndi chakwera wakoyo ngati akupasa ndalama ulibe manyazi wekha otsutsa pano aaaaaaaa ona kolowera

  • @jangiya03
    @jangiya03 11 дней назад

    Ambuye tithandizeni Malawi waipa

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 12 дней назад

    Hahaha AAA, Malawi poison party, Wanthu anawa votera dala, bolani ife tiri kutali zina ukamva zina Leku kamba anga mwala.

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 11 дней назад

    Limpopo FM ndi 1

  • @IssahAluba
    @IssahAluba 11 дней назад

    Chonde AMalawi asatiphimbe maso BOMA ilili osalivera tiyeni pansewu week yamawa osaopa gayz 💪💪🛶🛶🏹🏹⚒️⛏️

  • @BitonFred
    @BitonFred 9 дней назад

    😂😂😂😂

  • @walesbanda4959
    @walesbanda4959 10 дней назад

    😂😂😂

  • @SeephyMfaume
    @SeephyMfaume 11 дней назад

    MCP Pamtumbo pawo ndithu

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o 11 дней назад

    Nde inu mukuganiza kut olo patabwera peteryo zinthu zingasinthe foundation ya Malawi kuvuta konseko ndi chipani Cha udf olo mutatani Malawi sazasintha

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq 12 дней назад

    Asilikira akumalawi ndi wopusa.

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq 12 дней назад

    Koma chakwera anthawa wauyouyo mbwiyache.

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o 11 дней назад

    Ukanakhala kut mwina ukutiwuza munthu wozamuvotera koma nawenso ukumpangila peter kampen choti uziwe peter nayenso atatitopesa kale sitikunfunanso

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 11 дней назад

    😂😂😂😂😂 zabwino zonse wachita bwino wagwidwa tiakonzere konkuno

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri1799 11 дней назад

    If what comrade is saying is the truth,then Chakwera must be the worst president in Southern Africa.

  • @HappyMaolid
    @HappyMaolid 11 дней назад

    It's time to figh now,osagona

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 12 дней назад

    Chakwela ndigalu kwabasi

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 12 дней назад

    Koma Malawi walowa chibwana chakwera anapita ku sukulu koma?pano akusekedwa ndi anthu akunja omwe

  • @ThokohPrescotKalonga
    @ThokohPrescotKalonga 12 дней назад

    Malawian kuwopa too much that’s why amakonda kulepheresa mademo so don’t tell us ngati muziwona zoti sizingatheke zochita mademo! Aaa why amakonda kulepheresa mademo

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE 12 дней назад

    Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe

  • @user-xi2vo4gc4u
    @user-xi2vo4gc4u 12 дней назад

    Ku Malawi aku shooter ma movie rekani amenyane

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 11 дней назад

    Mcp mukali kuyalukirayalukiratu

  • @PaulineKamwana
    @PaulineKamwana 11 дней назад

    8:30 musova mcp ,mulithawa dziko mukulifuna

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 12 дней назад

    😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @CharlesMateya
    @CharlesMateya 11 дней назад

    Following

  • @user-td6qe4gr6w
    @user-td6qe4gr6w 11 дней назад

    Chopweteka kwambiri ndi choti ndalama za nkhani nkhani zikuthela kulipira anthu a kunja amene zomwe akuchita mudziko lathu phindu lake opindula ndi ochepa

  • @UsenLashid
    @UsenLashid 11 дней назад

    Kodi inu apolice ndi asilikali ntchito yanu ndi chiyani kumalawiko? Kodi mukuyang'anila zika Zanu zikuphedwa Kodi inu ndinu apolice opanda ntchito pamodzi ndi iwe wa mkulu wa asilikali utule Pasi udindo coz your usiless man dammit asilikali inu achilungamo menyani nkhondo please

  • @dorisbutao4227
    @dorisbutao4227 11 дней назад

    Mmmh

  • @FrankMulela-qt1wi
    @FrankMulela-qt1wi 12 дней назад

    Number yotumizila zinthu kwantanyiwa plz

  • @mipeacemakermw9501
    @mipeacemakermw9501 9 дней назад

    Mwatukwana president 🤣🤣🤣🤣ruclips.net/video/WRDkQ8s_34k/видео.htmlsi=PkGoYsuJRKSW0v4p

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 12 дней назад

    Atanyiwa pathako pako

    • @ShentrycChinoko
      @ShentrycChinoko 12 дней назад

      Yess

    • @ShentrycChinoko
      @ShentrycChinoko 12 дней назад

      Zowonadi mchutsuludi chimenechi

    • @user-yc3ik9dq3x
      @user-yc3ik9dq3x 11 дней назад

      Inu amenewo mungodziyankha nokha muli phee kugwiritsidwa ntchito ndi agaluwo 🥺mxieuw

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer 12 дней назад

    Am waiting good news not bad news 😔😔😔😔😔

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 12 дней назад

    Chakwera atha ngati Idi amin sizimuthera bwino ndithu.

  • @user-tm3zh5zk4t
    @user-tm3zh5zk4t 11 дней назад

    Paja ninakuwuza kale kuti upite kumalawi mabodza akowo mtanyiwa yiweyo niamene ukumasokoneza anthu infe timapeleka ulemu kwa boni kalindo osati mbuziyiweyo ayi

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 12 дней назад +1

    Ndikut mambodza akowa Pali ine no comment ndizopusa zakozo tithana phwanga galimoto uma user ija nditha kukutumizira komaso pachikwangwani umakonda kucheza paj okay

    • @victorauwana7258
      @victorauwana7258 12 дней назад +1

      Mwapemphedwa kutu mupange comment?

    • @NizigiyimanaChantal-c2p
      @NizigiyimanaChantal-c2p 12 дней назад

      😢

    • @SoundmasterElectrical
      @SoundmasterElectrical 12 дней назад

      Mbudzi iwe uthana ndindani usawone ngat ndife ogona wamva panyo pako

    • @MaryNyirenda-nq3mh
      @MaryNyirenda-nq3mh 12 дней назад

      Chigawenga iwe chimunthu chopanda phindu chitsilu ulibe manyazi mulungu akukanthan

    • @LukaThawe
      @LukaThawe 11 дней назад

      Anthu achoka Kuti iwe nawendimbuzi kwambiri ukukofuna kusokoneza amalawi ,chifukwa amalawi ndiopepera kale ndiye azikuvera nyasi zako sata yako

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 12 дней назад

    Muyiyambe muwone utsi ntanyawa Ali kunja athawa ataba mbuzi kumalawi

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 12 дней назад

    Chikamabodza chabwela zotani kukamwa ngati manyi

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 11 дней назад

    Achakwera vomelezani😂

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE 12 дней назад

    Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe