Mkumabisala mu Dzina la Mtumiki wa Mulungu Koma zochita zake Nyansi zeni zeni. Mulungu akuyendere iwe Woyipawe ndipo uwone ukulu wa Mulungu. Brother Mtanyiwa keep it up. God bless and guide you in this evil World.
Vuto laife timasankha anthu okwaver koma onena analipo kuyambira Andale analankhurapo koma sitinawaver winaso Mr twaibu analankhuraso nkhan imenei koma timaona ngat akulankhura zogona lelo bwanji makosana but almighty Allah forgive us
We thank you as malawains who resides in south africa do be fear we hear you day and night we give you powers we thank you very much with the information for the plane. From Jawadu Majidu
A Malawi tili ngati mbuzi sitimamva ndipo timakhulupilira titavulala Onena analipo ndipo si munthu mmodzi Olo former president Dr Bakili Muluzi ankanena msonkhano wina ulionse kulikonse kuti a Malawi olo patavuta bwanji musazavotere chipani cha MCP mudzalodzedwa chokupha, cha nkhanza komanso cha sankho ndikumakumbusatso zintchito zake kumatchula onse anaphedwa mwa nkhanza Koma ata lero si izi zidathera mu nsinje wa tinkanena kusamva iiiii ayi ndithu
To honest this guy say one truth kwinaku amakhala maboza chifukwa kwinaku amongopembembeza anthu open your eyes malawians kwina imakhala camghpain be mindful
Azitsogoleri anthu ali paubale ndi akumidima tiyeni tilimbikire kupemphara mu dzina la yesu kuti mulungu atichotsere anthu oipa ku parliament pachisankho chikubwerachi.
Ok ok nichifukwa chake bushiri anathawa ku joni ndekuti kujoni bushiri amapha anthu basi taziwa kuti bushiri nisataniki ni chakwera ose nimasataniki ndipo kwabeba kumalawi ni usataniki mwava
Ine ndi mboni ya zimenezi kuti nzoona chifukwa anadzandichita attack koma analephera ,nzambiri zomwe ndinganene, komanso ndichenjeze Inu a Mtanyiwa khalani mukudziwa chomwe mukudziwa
What comes around , goes around ,
No secret under the sun , may ALLAH bless our country MALAWl for ever .
Mkumabisala mu Dzina la Mtumiki wa Mulungu Koma zochita zake Nyansi zeni zeni.
Mulungu akuyendere iwe Woyipawe ndipo uwone ukulu wa Mulungu.
Brother Mtanyiwa keep it up.
God bless and guide you in this evil World.
Ndiye choncho wina ndi uchitsiru wake aziti Chakwera 2025 Boma zoonaaaaaaaa???????
@@VeronicaChirwa-ct4osndipo anthu alibe manyaz amwene, ambiriwa ndi okupha
Koma abare inuyo aaaaa atimalizatu
Vuto laife timasankha anthu okwaver koma onena analipo kuyambira Andale analankhurapo koma sitinawaver winaso Mr twaibu analankhuraso nkhan imenei koma timaona ngat akulankhura zogona lelo bwanji makosana but almighty Allah forgive us
The evil spirit is moving, eishhhhhh my Malawi where are you going. Our God who at in heaven please hear our cry
Comrade Antanyiwa pls Malawi ipange strike kuti bushiri azipita ku South Africa amange
Kmanso Chakwera akatuluka dziko zimachitikira zambiri
Inu dziko sapangira mademo kuti utenge ai
@@MahometAli-e8weti eti
Inudi ndi 1 and ndikugwilizana nanu♥︎♥︎♥︎♥︎
Mufufuzeni bwino mwana ochedwa bushiri yo , akudziwana bwino ndi chakwela awononga dziko athu amenewo, musakaike bushiri chakwela mai joice banda
We thank you as malawains who resides in south africa do be fear we hear you day and night we give you powers we thank you very much with the information for the plane. From Jawadu Majidu
This is what Grace Chinga said about it only God knows
At this time we need more Grace
The,s no secret on earth , we are Ander the clouds , GoD protect you from these killers,
We will meet on judge Ment day am swear for God
Bushiri be aware choonde please choonde please choka mwamtendere ma Malawi 🇲🇼
That's why Peter amamukanatu bushii eshiii Koma osavotera mcp
Lipopo FM number one
Mumakwana guys ndi maumboni yoooo
The world belongs to the most high nothing is hidden the bible talked about this already 😢😢😢
God should protect our country Malawi
Comrade Ntanyiwa with Lipompo fm 🎉
God never fails
Bushiri mutumizgani kuno wazakhare mundende chakwera tangomuyikani mu bini musekepo kwambiri
Thanks my brother ntanyiwa ❤❤❤❤❤❤❤
Koma mr ntanyiwa mulungu apiririze kukusungirani moyo wautali kuti mupitilize kutisegura maso😮😮
Km Pete muthalika amamukana kulowa kumalaw
MANGANYA ALI BUSY KUDYA CHAKULAMBA 😂😂😂😂 MISALA YENI YENI NDITHU
Kodi azitsogokeli apenga
Eti eti Ngozi paliponse bushiri ndi wausiru eshii bodza Ngozi zikuonjeza
zoona zake. Mukunena zi athanyiwa Ambuye atithandize ndithu Ambuye azikudalisani inuyo athanyiwa
Bushiri ndi Joyce banda samala
Pambuyo panu AComrade 🙏
Pa dziko lapansi palibe chinsisi Mulungu kubvumbulutsa kumeneku
Mmmm ndiye wapenga misala tu chakwerayu ndi zake wakudya mma restruant 😂😂😂😂😂😂
Kumalawiko ndizabwera boma liri panoli likazachoka....
🔥🔥aululeni
Mchifukwa chake mmayi uja anaphedwa Grace chinga esh akanaulula zambiri mu nyimbo muja esh
Ambuye tagwada maondo pansi tiunikileni nyali yanu ikhale yowala kwa ife ana anu
Same like bakili tv 📺 kuthoka ngamo
Choyankhula chandisowa mmmm
Ambuye atithandize tiyeni tipephere😢😢😢
Mulungu ndiy aziwa bas
There is no secret under the sun
GUYS BUSHIRI ABWELELE KOMWE ANALI KU SOUTH AFRICA PLEASE
Apite kwina kuno aphedwako mmene akumfuniramo
Abwele amako mboliyako galu iwe
Ndipo mau, akachiphere komweko ishiii
Zoonadi mr ntanyiwa Zoonadi zimene mukunena
A Malawi tili ngati mbuzi sitimamva ndipo timakhulupilira titavulala
Onena analipo ndipo si munthu mmodzi
Olo former president Dr Bakili Muluzi ankanena msonkhano wina ulionse kulikonse kuti a Malawi olo patavuta bwanji musazavotere chipani cha MCP mudzalodzedwa chokupha, cha nkhanza komanso cha sankho ndikumakumbusatso zintchito zake kumatchula onse anaphedwa mwa nkhanza
Koma ata lero si izi zidathera mu nsinje wa tinkanena kusamva iiiii ayi ndithu
To honest this guy say one truth kwinaku amakhala maboza chifukwa kwinaku amongopembembeza anthu open your eyes malawians kwina imakhala camghpain be mindful
Let's pray hard for our country again bad evil spirit
Mr Ntanyiwa please pray hard ndi nkhondotu iyiyi..please
Boma likangosintha 2025 bushili athamangitsidwe chakwera aphedwe chimwendo Banda mundende moyo wache onse mozes kumkuyu zikhale ngoma mdi ambiri amcp onse mundemde zanyanya
Ndichifukwa chake Peter amamukana
Peter uja ama pephera
Anaziwa
Amkaziwa ndithu ambuye chitanipo kathu
💔💔💔💔💔 chonena ndilibe ine
Enanso kuno azimai akumalawi aku joina satanic kuno Ku Johannesburg azimai opusa ngati chakwera
Bushiri u should be careful don't just think that God he is not watching u
Satanism is really very high in this country, sizikukhala bwino
Mcp manyaka enieni basi bagamoyo
Nanga ku SA kwachitika zingati ngozi , wa satanic ndi iweyo ntanyiwa
Jesus name is the only way ❤❤
Zovuta kwambiri koma Allah atiteteza ndithu
Muwawuze zoona machende alinawo achakwera ,bushiri ndi mayi joice banda naye nyini yochotsera mwana alinayo asawononge m'mtundu wa anthu anyani amenewa fiti achoke m'malawi muno.
Azipha ana awo alinawo osati ana azawo
Mbuzi zathu
Number one nice man
Tingolimba ndikupephela amaliwi tigonjese mizimu yoipayi
Chakwera ndiye gwero la mavuto onsewa chifukwa pomuthawisa bushiri anali akudziwa chimene chingachitike,now abwerere bushiri adzamalize milandu yake ndipo chakwera atule pansi udindo
Malawi ndi Munda WA azungu otiakafuna magazi,or chinachilichosechimene Iwo akufuna amadzipeza kumalawi,chifukwa audindo athu ndiowewo achitaizi
Koma guys mmmmmmmm
Mlungu atithandize atitumile mzimu oyera utifungatile ayikumbukile
Cipani cinawina 2019 ndi DPP
ndizona zake atanyiwa athuwa ndiwoipa kwambili chakwela ndichikangawadi
Eeeee Limpopo ndi one ndipo anayankhuladi grace asanamwalire koma lero si iziii zikulumikizana kwathunthu
😂😂😂 angokwera njinga ampanga withdraw kaganizidwe 😅
mercy Lord🤦🤦
Mbambande big man ❤❤❤❤❤
Ndimanena kut bushili nzakudya akugawazi nzitha athu mwaona izi, achikangawa mukutitha plz, tisiyeni
ANtanyiwa Ambuye azikupasani moyo wautali, mupitilize kutitsekula maso
Atimaliza agaluwa Achoke bas
Mumuuze kuti machende apotatoo
Pa dziko lapansi palibe chisisi ndakhulupilira ndithu koma zonse zizatha ambuye ndiwavhifundo khani ndiyoti tilimbike kupephela ambuye azatiyakha tisalimbane ndi kumenyana
Lero madzulo omwe ano pa standard bank ku limbe
Satanic wakula eeee ayi🙌🙌🙌 chabwino mwawina ndinu
Ambuye MULUNGU atichosele chonyasachi
Osamapeleka ana awo bwanji
Tithatu kuno ku Malawi amwene 😱 chifukwa tinayamba ndi namondwe Zina ndi izi anthu angofa ngozi zimene zikuchitikazi haaaa😫😭😫😭😭😿
Koma sakusaka iweyo mtanyiwa😂
Bwana mthanyiwa nkhanga zaona limpompo fm mukunena zoona zinazi zikudabwisa kwambili komanso usogoleri omwe ulipo ukulekelera bushir kuti azitipha ife ngakhale mphepo yomwe inachitika kumalawi yamvula sizinachitikepo komanso amalawi tiyeni tisiye kulandila zinthu za ulele zochokela kwa mtumuki ameneyu atimaliza
Ntanyiwa ntapangani zonteka bushili abwelele ku South Africa 🇿🇦 kuno
So sad !!!
Azitsogoleri anthu ali paubale ndi akumidima tiyeni tilimbikire kupemphara mu dzina la yesu kuti mulungu atichotsere anthu oipa ku parliament pachisankho chikubwerachi.
Problem ndi DPP nkhani ya satanic akufuna ndalama zochitila campaign
Zitukuko za Ku Lilongwe ndi dowa ndie ndziko lonse mwatha basi
Asilamu inu tangokhalani chete this is not a time for Muhamadi its a time for jesus.
😂😂😂😂 koma adah
Amenewo ndiye manyi kod mmaonangati asilamu amapanganawo zamanyizo. Kungokula ndi umbuli basi muziona simunati Mesa inunso mulimommo zaumbulizanuzo ife ayi.
Okupha alubino linali boma la DPP musaname inu
Ok ok nichifukwa chake bushiri anathawa ku joni ndekuti kujoni bushiri amapha anthu basi taziwa kuti bushiri nisataniki ni chakwera ose nimasataniki ndipo kwabeba kumalawi ni usataniki mwava
Mtanyiwa iponyera kwakuya, ng'alulani basi, Ambuye azikudalitsani kale kunalibe izi sitimadziwa zomwe zinsinsi zina zadziko muno panopa nthawi yatha satana ayaluke basi
Makape a DPP mwayambapo kupanga ma fake report video imeneyi tipanga report sipezekanso apa for the next few hours
Santhe ndi kasungu osati mchinji
Ndare za panyasaland chilichose chalowa ndare sorry!
Stanic iyi
Yemweyo Chikangawa zakumidima zizaururika
Tsoka ntunda ndi nyanja pakuti oyipa watsikila ku malawi 👿👿👿
Ine ndi mboni ya zimenezi kuti nzoona chifukwa anadzandichita attack koma analephera ,nzambiri zomwe ndinganene, komanso ndichenjeze Inu a Mtanyiwa khalani mukudziwa chomwe mukudziwa
Pa mtengo wanthenganso bus ya captain yagwa costor nso pompo zomvetsa chisoni kwambiri
Dziko la umphawi basi nkhani zake zopusa basi kosowa zochita
Kulichapwa Mr mtanyiwa kkkkkkkkk
Iweyo iweyo mr chikangawa chakwera
AGALU AMENEWO amaonjeza ndipo amandibowa basi chilichose mupaka ayikepo umbuli zazii, popeza anatiphera chilima ifeyo nde akuzitenga kut ndiophuzira iya akhalike agalu amenewo achina mr chikangawa chakwera fiti za anthu
Kkkk kuvina uli maliseche, koma ndalama
Thanks big man we proud of you ❤❤❤❤❤❤❤.
Bushiri ndi munthu oyipa kwambiri satana ndithu
bolani ali ndi ndalama amathandizanso amalawi omweo nanga iwe ndi ine
@@jennyx6914 inuso kwanu mukuenela mumatamba
@@jennyx6914kudalila zolandila zamagaz
Ndipo sukunama oterewa amakhala anazama muufiti cos munthu wa normal sungamabakile zopusazi boss!.mxiew
masiku otsiliza