Go on Guy's we wait to see the changes in Malawi eeeee from Bakili muluzi up to know am in RSA because of politics of Malawi throwing as away not thinking of coming back to home eeeeeeeeesh
Alot of people re in marriages that ended a long time ago but due to kids u re forced to still living together that's what I think was the case of SKC&usi.
Mcp ivutika chifukwa isanalowe m'boma amalawi ankaopa nkhanza za mbiri yawo Lero in their 4yrs rule patuluka nkhanza. Do you think they can reign???????????
ngati bola Allience latha ndibwino kukhala opanda president cs chakwela polowa m boma unali mgwilizano maka utm inali ndimavoti ambiri kuposa mcp we must have emergency presidental election
Go on Guy's we wait to see the changes in Malawi eeeee from Bakili muluzi up to know am in RSA because of politics of Malawi throwing as away not thinking of coming back to home eeeeeeeeesh
Manganya ndi mcp anapha chilima.
Guys keep it like this ,this is Hot current we know from those days congratulations
Chilima was assassinated that's the truth what more do u want to hear?
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💯💯
Usi si wa UTM. Munamuwona muja amarandira udindo muja? UTM yachita bwino kuwaturuka.
Kkkkk akut ipondeni fadha
🤩
Ngozi ija singozi ngozi ,,komanso yonse taona ndimafinso
Briefcase parties end just like that.
Alot of people re in marriages that ended a long time ago but due to kids u re forced to still living together that's what I think was the case of SKC&usi.
Well spoken guy's adzimva akawalalawa
Apa ndiye mwabwelatu chilungamo chimenecho
Sitizalola report. Wonder you are very Intelligent than pankukuyo
Osamayakhura ngat akupatsani za lent kung'alura basi ukuva iwe ndevuzamwayi !!
Dziko nkumasawukaaaaah!!!!!!!
Usi atha ngati nankhumwa sure, olo kuthesako akufuna kukhaulisa manganya coz anamuziwa kuti uyu sitili limozi ndi wa mcp.
Masapota a UTM tonse tatuluka ku mgwirizano Chifukwa tinkasapota Chilima.Usi alibe masapota.
Times muziwe kuti chilima agwila bwanji ntchito ndi chakwela mu 4years
Akuti mbwexe😅😅😅😅😅😂😂😂
Walephera Chakwera kulamulira kuchedwa 4yrs ndipo akhala akungodandaula DPP mmalo mopanga ziganizo msanga
😂😂😂😂😂 chaka chino ndi CHONG'ALURA
Mtsukuluzi ukulankhula mopusa, kufooka kwa Ussi kunayamba Chilima alimoyo. Ndipo. Chilimma anali atamuzindikila Kale Ussi ukathyali wake.
Chakwera so asamale zomwe wawona Nzake wa kwa merica zija zichitikanso kuno.
How many meetings manganya has been attending?? Can he allow to apart from the alliance coz it's obvious manganya it's won't allow
Salute u guys 😂
Mbwelera zokha zokha za mcp kkkkkkk koma pankuku!!!!!!
President osaziwachomwe akuchita he is so relaxing President President uyu ndi bubu shatapu zake
MCP yayambitsa nkhondo yoopsa yokha amalawi sangasangalale nazo izi
Zotsatila results zangozi kuli ziiiii mpaka pano what do you do
Changucho chiyambile pa kafukufuku wa ndege inapha chilima kenako the public ikhala ndi changu
Sizachilendo olo pa ngozi ya ndege ija anachedwanso kukafufuza ayambe kuchotsa ameneo onwe amaenera kukafufuza za ngozi ya ndege
😂😂😂😂😂 anyamata inu mwandisangalatsatu chikufunika ndichimenechi osanyangerera kulankhula chilungamo kubandaluka basi sizoopaso ayi
Keep it up Guy's ife ndalama tidya koma sitidzawavotela talira kokwana sife opusaso pano
Ipitilile ndiyabwino coz ikulakhula mosatenga bali
Fiti ndifiti basi awa sangaulule chilingamo kwao ndikunama basi koma ife chilingamo tinachipeza kale
Inu ussi siwa UTM 😂😂😂😂ameneuja ngawa MCP
Masapota ake ati omwe atsatire Usi ku MCP. Musanamizane palibe yemwe angavotere MCP true member wa UTM
Wakulu andevu zamwayi amayankhura Chichewa cha boo
Akuchedwa Nd pule yomweyo😂😂😂😂😂
Eni ake a UTM ndifeyo ovotafe Tatupu ndife awowo dyela Paolo asaleko tilibe nawo film
Koma ma guys inuo hahaha munatopa nalo dzikoli simufunaso zachikape
Akuyambisa kuchedwa ndi achakwela ndipo ife tinalakwisa kumuika munthu onamizila ubusa Ngati uyu pa mpando
Manganya ndi wa mcp not utm
Kuchokela pa ifa ya VP chilima kufikila pasiku la mavoti UTM ILI PA TOP ONE. or Dpp ndi mcp ita phatikizana. UTM IKUTENGA BOMA TIZAIPEPESA NDI VOTE.
Exactly Wonder bambo wanzelu amakonza mavuto amu nyumba mwake not kutuluka nkumakadandaula panja or kubwalo kuti mnyumba mwanga sitikudya ana anga sakuvala bwino, sitikudya bwino! Nde ana Inu muzivala bwino, muzidya bwino, ukuganiza kuti anawo azitenga kuti?
Koma makosana inu MMM mwanditha keen on on our behalf
Dziko ndilathu osaonesa kutopa azibambo ipondeni thawi ino palibe kuopa ng,alulani basi ng,ambani
Mcp ivutika chifukwa isanalowe m'boma amalawi ankaopa nkhanza za mbiri yawo
Lero in their 4yrs rule patuluka nkhanza.
Do you think they can reign???????????
Uyakhura za chidodoyo ndiye ili mbudzi yoyambisa chakwera samasata zinthu that’s y anyamata ake angomisewera basi.
Gyz mmmatha
Eeeeeee yankhulani guys ❤
Very true wonder and jona, a PULE akuchedwaa
Inu a times muyang'ane mgwirizanou kuchokela mmbuyo inunomwe mumaunikira mgwirizanou mmene umayendela chilima asanamwalile asiyeni ausi ali ndigululawo odya zake alibe mulandu
Tamusiyani maganya abakhala komweko adzatiuza zenizeni abawatola zifukwa adzapange sewelo mutu wake chakwera anapha zake chifukwa chaudindo
A Usi si president wanthu,,munthu mkazi wake tamuziwa polumbilitsa mkumazitama kuti ine sindinayendepo ndi mkazi wanga,,muthuyu angayendese chipani
ngati bola Allience latha ndibwino kukhala opanda president cs chakwela polowa m boma unali mgwilizano maka utm inali ndimavoti ambiri kuposa mcp we must have emergency presidental election
Mumakwana mabigi
A mcp chipani chokupha
Pa nkhani yochedwetsa chitukuko, tingomuchotsa next year basi, sali fit Chakwera to be a President.
Chakwela azuzula bwanji pomwe iyeyo anaphaso muzake
You guys u don't share kamba here really keep it up guys kkkkkkkkk
Lero munabweratu a jonah kkk wonder akuti back to sender eee Chakwera dzimvere mumtolo
Osawopa ayi a malawi ambiri tikuyang'anira inu kut muziyakhura mosawopa apa
Did. Mcp ask Afford
Anaphedwa ku Mwanza aja ndiochepa.pano ayesetsetsa kupha ambiri.athakati sadzasintha.Malawi Congress of Perishers
Iwe pankuku osamayakhura mowopa apa
Inuyo munabwera ngati coming 🔥
Aganizq bwanji mwakuya kuposa anthu zosatheka ubongo unatha chifukwa ankadya zopasidwa Za chaulele
Kaya DPP kaya ilibe ndalama iwinabe 2025
Emusipi ofunika isale yokha. Anthu woipa awa
Nkhaniyo ndiyoona, a President akugona kwambiri pachiongolero, dziko silingatukuke ai
Asiyeni atuiuka chifukwa chake achakwera apha chirima ndipo ndizoona
Musamamuzile zochita president, yekha samawona???
President wake uti
Ma comments 100 wa MCP yekha .chita manyazi😅😅
MCP ndi Yakupha
Ng'alula iwe
🤣🤣🤣 iponden fadah kkk
Decisiveness palibepo
A pule ayamba kupemphera ku CCAP kamutu kataya
Ofufuza ngozi akuti, khoswe akakhala pakhate sapheka
Osamayiwala ku mudzi kaamba kokomedwa ndi maidyaidya chifukwa tsiku Lina amadzakusandutsa mtsamiro wa mfumu ikadzamwalira.
Ndipo inuyo kumeneko mumaitha 😂😂😂 akuchedwesa ndi chakwera
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
You. are. wrong. it. Is. People. at. the. grassroots. who matters not individuals
Anthu ake ndi chimwendo banda,howeh mkaka,zikhaleng'oma ndiomwe akuyenela kuchoka
Eeh 😂
😂😂😂 President wake utiyo mukudikira kuti azuzuleyo
agaluwa alilimosi ndi chachera
Mumatiimilira big hands for you
Kod amaphang’ombe ali kut😂😂
Ine dakalira malemu za chipani tizitaye uko aaa
Koma Wonder Ati kukura mtima 😂😂😂😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥uyatseni basi ng'alulani basi
A kaliati ndi a njawala nzokonza izi, akufuna apange handpick Kabambe, can't you read between the lines? Typical of atsogoleri a dyela.
Chakwera ndiwofoka koma kumagaanthu chimenecho ndiye chitukuko.chake
Mumakwana mabigi