The Malawian voted for you to do better than DPP so what is happening now Malawian they don't have freedom to express their concerns overwise they end up in JAILED Sshame on you MCP.
Kunkuyu mukusangala chifukwa mukuba ndalama Za Malawi eti muzanya mu2025 muzaona mkwiyo wa amalawi osamanena Kuti dziko likuyenda bwino ndipo nrhawi ya Dpp zinthu zinali bwino kusiyana ndi boma la chakwera out no matter what
Kodi DPP ikulamula zinafika apa? Akunkuyu fertilizer amkavuta ngati momwe zinachitikilamu?
Akumkuyu mwabaiba mwatopa munganene chani choti ife tingamve ingovomelezani zakuvutani basi👐
Koma timakwanisa kugura
We will not remain silent
mosez mkukuyu uli ndi umuthu koma mapwala ako wava
Ndie ngati likubwereranso ku ulamuliro wa chipani chimodzi iwowo monga chipani chachikulu chotsutsa chikupangapo chani mmalo moti adzuke ndikutsutsana nazo zimenezo koma ai ndie pano zaka 4 zatha
Zitsilu za anthu ango ziwa kulubwa lubwa but i believe any time any day any week any month from now anyamata azuka ngati ku Kenya 🇰🇪
@@innocentmusuli7380
Otsutsa akanadzukadi now kumayakhula kumaletsa olo kuyambitsa mademo aja koma ayi kuli ziiii 😂😂😂
Kunkuyu uku ndikupenga tsopano metsa mumati mukufuna mukonze zinthu kodi 😂😂😂
Iwe kukuyu ukunama
😢ussi achokeko Ku UTM ki osamvotera ameneyo mdya kuwiri
Astana awa,anaoha wittika ndi kunkuyu koma kuli ziii
A Chaponda siajawa awa?
Kunkuyu nzeru mulibe
inu mukukamba za njanji osakamba za president bwanji akuba kwambili ndi anthu omuzungulila bwanji
Kunkuyu sangayankhule anthu ndikumumva let's wait for 2025 awona panali Gospel kadzakotu pamenepo samala
Ndiye kunkuyu wapangapo chani 4 years dziko mwalipitisa kubakamoyo
Anthu a Dadzi ndinkaona ngati ndiamzeru, ayi ndithu amaganizila pamimba
ena ndi anzeru kmana uyu kunkuyu uyu sitikuziwa kuti amaganiza chan
Mmmm timadya amaba awa koma dollar imatifikira tikasaka saka ife tikusangalala ina ayi akuvutika
Kunkuyu ka phwala kako wamva udzatipeza
Moses kumkuyu ndiwe ngalu pamodzi ndi agogo ako komatu Musamale nosenu mudzakhwezedwe pazomwe mukuchitazi azanu olamula ndi amene akuluza panopa
Iwetu kunkuyu iwe mulungu amukanthe wamva?
Kodi a police abale awo sakuvutika KU midzi kwawo?
Komanso mwina a police wo NDI a chigawo chapakati poti mukuti achewa Ali 14 000 000
Za ziiiiiiiii Who's Chaponda? Katangale mwayiwala Muja munkaberamu
Mcp sitikuifuna ikagona basi no fetereza ochipa
Machende ako kukuyu bamva
Moses ndi mfiti yamunthu
Kunkuyu amayankhula ngati mwana sindidziwa kuti amayankhula ngati wamwa mowa Ambuye amukhululukire
The Malawian voted for you to do better than DPP so what is happening now Malawian they don't have freedom to express their concerns overwise they end up in JAILED Sshame on you MCP.
Kumkuyu pa chakut Pako usankhe wekha
Kukuyu mulungu adzakulangani ndi boma lako la usatana tsiku likubwela
Chimanga cha admac nawenso ubweze, sumanva chisoni ukamaona anthu akuvutika? Njala ukunenayo chimanga mesa unadya wekha ndie ukufuna uzabenso
Kumkuyu azalila day one lomwe tizapange mademo anyoo tifika kunyumba kwa Kumkuyu koko tizaotcha zathu zomwe waba
Kunkuyu you will see Kenya soon
Chikangawa sinzaiwala basi😢😢😢😢😢
Nanga chimanga chija
Kumkuyu ndiwamisala kwambili
Iwe kunkuyu ndiwe mbalame yeniyeni
Kunkuyu witika akuvutisa
Kunkuyu asanamepo apa, nthawi ya ulamulilo wa DPP zinthi sizimavuta chonchi, Chakwera ndi boma lake la MCP alephera. Chaponda akunena chilungamo.
Ma passport amkavuta chonchi?
Km boma la achakwera ndi loputsa
Iwe kunkuyu ndiwe Galu kwabasi
Kodi kunkuyu pali zina akhoza kuyankhula zabwino zokomela amalawi chinachirichonse chimene amafotokoza ndi chotsutsa mtundu wa Malawi bwanji kunkuyu.
Kumkuyu udzivere chisonii
Uyuyu kunkuyu ndi chisilu cha munthu
...unapha allan witika iwe
...tsogolo lako palibe
Kukuyu ndiamene akuononga dziko lathu machende Ake
Awiri onse
Kunkuyu matako ako ndiithu
Kumkuyu nthawi mkachitsilu uziyankhula modziwa kuti Malawi siyako ndi chakwera i
Kunkuyu hes talking nonses now
Kumkuyu, Kodi ukuyesa ife dzitsiru? You will smell Malawian anger very very 🔜👀👀👀😎😎
Mkukuyu umunthu mulibe ndithu... Sakuganizirapo chilichose chokhuza amphawi kumudzi.,. Mwatikwana koma mukadatula pansi udindo wanu
Kumkuyu ndi mbudzi ya munthu
Kodi akunkuyu ife Malawi time ziti sopano pompano mwakhala mukuyimba nyimbo ya kovidi mwayambanso yamkhondo yakurasha mwaimbanso yanamondwe😢 zonsezi ndizimene mumati zatibwelesela mavuto mudzikomuno APA tikudabwanso mukubwela ndinyimbo Ina yoti a dpp ndiamene apangisa mavuto Mudzikoli ife tikudabwa Kodi a dpp panoalulamulilabe dzikoli Kodi muja ankati tivoteleni Kuti tizakutheseleni mavuto alipowa Iwo Amati mavuto amene akufuna kuzathesawo ndiati apatu kunkuyu tikuwona Ngati mzimu wawitika wayamba kumuyenda Mutu make tsopano
Chaponda wakuna chimanga iwe
Nkukuyu pamasinda pako ku dpp kunalibe izi inu a mcp pukupha athu chipani chanu ichi ndichamagazi inu a mcp
Kumkuyu ndi achisilu uyu umunthu aibe
Moses ndionama kwambiri iweyo ukamayakhula uzidziwa kuti tsiku lina suzakhala ulipompo,aaaa koma moses tatiuze omwe adakhapa anthu kwasundwe ndinani mpaka pano kuliziii or modzi sadagwidwe zonyasa zomwe zikuchitika mum'boma lanu iweyo ungayakhule zoipa kpn zabwino kuti ukome koma choona chake tikudziwa bwino khanza zomwe chikuchita chipani cha mcp chimodzimodzi kale lija
Kunkuyu mukusangala chifukwa mukuba ndalama Za Malawi eti muzanya mu2025 muzaona mkwiyo wa amalawi osamanena Kuti dziko likuyenda bwino ndipo nrhawi ya Dpp zinthu zinali bwino kusiyana ndi boma la chakwera out no matter what
Mose kunkuyu you are talking nonsense.
Akukuyu komwe muliko Bola mukanamwalira mwatikwana ndiboza lanu galu iwe
Monses kunkuyu ndiwe oputsa kwambili zakatangalezo ? Bwanji mukususana chilungamo ? Njala thawi ya DPP kudali be mukutisausat posafuna kuvomereza MCP kumalawi PALIBE chikuyenda ukamat ulamulilo walazalo Uli BWINO ,ulibwino kwamako osat ife amalawi
Akumkuyu machende ako
Ndiye ingakonze mavuto a DPP ndi DPP yomweyo inu mwalephera vomerezani chilichonse osamachinkha mwa ndale kumkuyu
Chakwera nkhanza alibedi chifukwa ndi mbava yinzako mmesa.
Akhala bwanji wankhanza Chakwera poti nonse ndinu akupha.
Mmesa unapha Witika ndiwe Kunkuyu chifukwa Cha uhule MOTi siukumangidwa chifukwa CHOTI nonse ndinu dzigawenga
Zimene ukunena ndi zimene mukupanga panopa mboli yako
Amkukuyu akunana sangabvomereze pazakulephera kwa boma la MCP chifukwa iwonso ndi amene akuthandizira nawo kuononga ziko lamalawi
akunkuyu pena dzinthu kumavomeledza chifukwa mukavomeledza simupusa ayi koma china chilichose inu mumakana chabwino dzimene anena achaponda dzija ndizoona chifukwa boma lanulo anthu akanena mmene mukubela ndalama anthu mukuwamanga ndiye sopano achaponda akunena kut tikubwelela ulamulilo umodzi inu ndiye mukuti ayi kudi akunkuyu inu mumapephela inu
Nkukuyu bole yamako munthu wako.uugwira ntchito
Amozesi inu mapwala anu akulu
Kunkuyu mbuzi yamuthu iwe machende ako
Nkukuyu nyini yamako mbuzi iwe
Akukunyu machende ako galuiwe mu dpp sinalisosika muona 2025 agalu you go
Iwe mkukuyu mboli yamako wamva
kumkuyu mutu wa bambo ako ndi Chakwera wakoyo
Zavuta vumelezani akulu
Nayenso Kumkuyu ndi mbuzi ya munthu kwambiri kodi ndi chifukwa chani nthawi zonse amakamba zopusa ngati sali ku Malawi komwe kuno bwanji kodi iyeyu amakhala ukuyankhulira dziko la Malawi kapena amayankhulira mbuzi nzakeyo Chilima chifukwa nthawi zonse amakhala ku mbuyo kwa Chilima ndi chipani cha MCP koma asamayankhule ngati kuti zawo zili pa bwino ai ndimamva chisoni ndi momwe amayankhulira a Moses Kumkuyu. Chifukwa DPP inachoka pano patha zaka 4 ndie ndichifukwa chani amangoloza dzala chipani choti pano chili kunja?? Apa zimangowonekera2 kuti awa ndi olephera.
Kunkuyu machende ako mu ulamuliro wa dpp unayamba wasinthapo 1r to 123
Useless government spokes person
Akukuyu ndi agalu wa MCP nthawi ya DPP KWACHA INATHA CHOMWECHI AAAA IWE MBUDZI YA MUNTHU
Koma kunkuyu mutu wako umagwira bwino ntchito? Kapena mwanzi was witika ukukusowesa mtendere.kapena kuchikangawa kuja eti.bashop
Kunkuyu chamba eti
ok inu akunkuyu ndikufuseni kuti nanga inu boma lanu chitengeleni mwapanga chani pamene mumatenga boma la Malawi kuchokela ku dpp dziko ndalama inali ya mphamvu chimanga chimapezeka zakudya zinali zoship nanga inu mukutani bomamu pachitengeleni akulu akulu ifa ikubwela kunama kwanu muzavomela siku lolowa manda anthu aboma mwatiojeza Kwambili anthu akuvutika kwambili chifukwa cha boma lanu munalowa boma koma mulube dzelu komaso munali osauka Kwambili simungatukule dziko lamalawi munali osauka muvomeleze
Wabodza uyu ndi satana uyu pajatu satana amatsutaa zili zonse ndi pomwe yafika DPP Ngati kuli boma lomwe lawononga dziko lino ndi DPP mu ulamulolo wa a Peter munthalika Chita manyazi chaponda ndipo wawuponda simudzawina inu ayi 😅😅😅😅
Kumkuyu pamtumbo PA mako galu
I iiiii bwana wanga mwawojedza kutukwana chonde
@@amonfrancisautotune2073 sitifuna kutukwana ayi koma anthu Ena ndiwotukwanitsa ngati Mkuyu yu iyah, akukondwa ndani lero ndi mbava zimenezi? Kuma watukwana kumene kuti azidziwa m'mene anthu talusira pano ndi MCP yawoyo.