Ambuye akudalitseni chifukwa ndi ochepa amene akumaona patali mu uzimu, ambiri ali komweko chifukwa anabadwila momwemo kapena makolo awo anawasiya mzikiti omwe anamanga, ambuye akuthandizeni in everything especially moyo wanu wa uzimu
Alhamdulillah kuti ndine Msilamu. Ma videos ngati awa adzipezeka ndithu pa RUclips. In so doing zithandizira uthenga wa Allah kufikira ena omwe ali kutali mosavuta
Hohn 14 v 6, Yesu anati ine ndine njira choonadi ndi moyo. palibe munthu adza kwa atate koma mwa ine. Most of theses things brings conflicts among peoople, Palibe mpikitsano pa mawu a mulungu
I am proud to be a muslim , Komafunso langandiloti , Ndichifukwachani Muhammad timamupemphela chikhululuko komanso madaliso kwa mulungu ? Kodi Muhammad ndi azibale athu omwe anamwalila oyenela kuwafunila zabwino kwa mulungu ndindani ?
Dzina la mtumiki Muhammed likatchulidwa timanena kuti swalalah alaih wasalamah,( meaning , mtendere ndi madalitso amulungu apite kwa iye). Zimenezi even zimachitikaso kwa Azitumiki ena onse . Issah(Yesu) ndiye timati Alaih Salam Wasalatuh(Meaning, madalitso amulungu apite kwa iye). Nde zimenezi zimanenedwa kwa mtumiki winaaliyese akatchulidwa dzina.
Mwenyezi Mungu, hapana mungu ila Yeye, Aliye hai, Msimamizi wa milele, Amekuteremshieni Kitabu kwa haki, kinachosadikisha yaliyokuwa kabla yake, na ameteremsha Taurati na Injili kabla yake kuwa ni uwongofu kwa watu. Na akateremsha upambanuzi: Hakika walio kufuru Ishara za Mwenyezi Mungu watapata adhabu kali, na Mwenyezi Mungu ni Mwenye nguvu, Mwenye kulipiza kisasi wewe katika Mwingi wa rehema, vipi hakuna mungu ila yeye ni mpendwa, Mwenye hikima ni yule aliyeteremshiwa kwako Ama waliomo nyoyoni mwao wanafuatwa Hawakusema kuwa kila mmoja Kwa Mola wetu Mlezi. na hawakumbuki ila wenye akili, tusipotoke nyoyo zetu baada ya kutuongoza bila shaka Mwenyezi Mungu hatavunja ahadi yake, mojawapo ya makusudio ya surah. Kudumu katika Uislamu baada ya ukamilifu na ubainifu wake, na kukanusha shaka za Watu wa Kitabu, hususan Wakristo Ni surah ya Madina iliitwa Surah Al Imran kwa sababu familia ya Imran imetajwa ndani yake katika aya ya surah. Herufi hizi zilizotengana zimemtangulia mwenzao katika Sura Al-Baqarah, na zinaonyesha kutoweza kwa Waarabu kutoa Qur’ani kama hiyo ingawa inaundwa na herufi ambazo Sura ilianza nazo, na kutoka kwao wanatunga hotuba yao. Mwenyezi Mungu ndiye ambaye hana mungu wa kuabudiwa kwa haki isipokuwa Yeye pekee na hakuna mwingine aliye hai ni maisha makamilifu yasiyo na kifo au upungufu.
I once met this Saidi Zambia for almost 8 hrs. Anafika pokwiya titamufotokozera zinthu zomwe iye samadziwa za chiyambi chachisilamu ndipo anakwiya heavy. Amene mumamudziwa ask him za anyamata omwe anakumana nawo usiku mnyumba ina ku mangochi. He ended up a failure on that meeting.
Where is the other part of Seventh Day part? Let's PRAY that each one of us here on Earth meets GOD's Grace and know the truth, I Pray for you my muslim brothers. Amen
I am proud from Christian to be Muslim ☪️ ❤❤❤
Mashallh
Am proud to be a Muslim,Allah is great
Allah bless you professor mashalah❤❤❤
I am proud to be a Muslim
Allah akbar
Ndinali msilamu koma ndinasiya Chisilamu nditazindikira kuti YESU ndiye njira yowonadi.
Mulungu akudalitseni kwambiri, munapanga chisankho chabwino.
munali msilamu koma Osazindikila kungopitako poti makolo Anu amkapita kumeneko
Ambuye akudalitseni chifukwa ndi ochepa amene akumaona patali mu uzimu, ambiri ali komweko chifukwa anabadwila momwemo kapena makolo awo anawasiya mzikiti omwe anamanga,
ambuye akuthandizeni in everything especially moyo wanu wa uzimu
Nthawi yatha amsilamu inu musasokoneze choonadi
Akusokoneza ndi chani amenepo mmm
Asokonesa pati 😂😂😂
Chilungamo chakufika mutima mwako
Alhamdulillah kuti ndine Msilamu.
Ma videos ngati awa adzipezeka ndithu pa RUclips.
In so doing zithandizira uthenga wa Allah kufikira ena omwe ali kutali mosavuta
❤❤❤
Alhamdulillah am proud to be Muslim. May Allah guide me and protect me In shaa Allah.
In sha Allah
Hohn 14 v 6, Yesu anati ine ndine njira choonadi ndi moyo.
palibe munthu adza kwa atate koma mwa ine.
Most of theses things brings conflicts among peoople, Palibe mpikitsano pa mawu a mulungu
Zamasiku otsiliza amenewa ndiwo omkana yesu aja zimene munthu udakhazikikamo sikopheka kukusutha amenewa simungawauze za mzimu oyela sangave ndiwo umaulula umazindikilitsa umaphuzitsa ngat ulibe mzimu oyela ungalive baibulo ukamaliva kuthupi mzimenezo zovetsa chison ambuye akuzindikilitsen amen
Kumva chichewa umafunikira kukhala ndi Zimu oyera kod?
Ine anthu inu mmandiwaza apapa
Kumva language yako yomwe zufunaso nzimu oyela??
Kukuuza kut iyo ndi kapu yomwela madzi, sumva coz ulibe nzimu oyera??
This thing of nzimu oyera, koma mmaudziwa, mungaufotokoze ndi malemba maumboni??
Concept iyiyi eeeeti eeeeeeish mumadyera guys 🤣🤣🤣🤣🤣
Mzimu oyelawo anaulenga ndan??? 😂😂😂
@@tauhidtimbakayatu 😂
Mmm baba moti ma verse akupereka muthuyu si amu bible
Afarisi a lero ndamenewa ntchito yao nkuphwekesa Yesu basi
Alhamdu lillah proud to be one hu follows Allah's submission
Im proud to b Muslim, mpaka imfa idzanditenge ndili msilamu
Allah akudaliseni ma sheikh nonse
Ma sha Allah may Allah bless u sheikh SAID HASSAN ZAMBIA
Mashallaah Sheikh mulungu akudalitseni ❤.
Aaaaaaa ine saidi Zambia nakhala nayepo ndi tambwali uyu
Masha Allah may Allah Grant him jannat firdaus
Alihamudulilahi kwaine mpakana kwa asilamu ose pano pa dhunia mashaalhaa
Allihamdulilah to be a Muslim my dad please protect pokhala slamu paka ifa
Mashah allah ❤ ♥ 🙏
I'm proud to be a Muslim
❤❤❤❤
❤❤❤
My lecture Said Zambia you miss me long time no hear you
Mashallah
Mashalla Allah ndi silamu ndipo tikuphemba kwa Allah ndizafe ndi silamu
Alhamdulillah for choosing me to be a Muslim❤
Proud to be a Muslim Alhamdulilah ❤
Am proud to be a Muslim ❤
Kwamuthu yemwe sawerenga ndikutsata za zipembedzo adupha nkhani zonse ndikumangosankha momwe akufuna pokwanilitsa zolinga zanu koma choonadi mukuchidziwa
Pelekan lemba nanu
Pelekani zomwe mmawelenga inuzooo
Ndanga izi zikuchoka mmitu mwao ngat?? 🤣🤣🤣🤣🤣
Minika ❤❤❤❤
I am proud to be a muslim ,
Komafunso langandiloti ,
Ndichifukwachani Muhammad timamupemphela chikhululuko komanso madaliso kwa mulungu ?
Kodi Muhammad ndi azibale athu omwe anamwalila oyenela kuwafunila zabwino kwa mulungu ndindani ?
Dzina la mtumiki Muhammed likatchulidwa timanena kuti swalalah alaih wasalamah,( meaning , mtendere ndi madalitso amulungu apite kwa iye).
Zimenezi even zimachitikaso kwa Azitumiki ena onse . Issah(Yesu) ndiye timati Alaih Salam Wasalatuh(Meaning, madalitso amulungu apite kwa iye).
Nde zimenezi zimanenedwa kwa mtumiki winaaliyese akatchulidwa dzina.
@@JohnstoneMwandira ok , ndichifukwa chani okhala atumiki a mulungu timawafunila mtendele ndi madaliso , chikhalilenicho anapanga ntchitoya mulungu .
@@rashidadan2533 Zimenezi akulamula ndi Mulungu akuti mfunireni zabwino mtumiki wanu. Nde Ife ndindani kukanira.
Iweso sisilamu tachoka apa
Ndizomwe timadikilira,go ahead
Allahu Akbar. Ma sha Allah. Na am ❤❤😂
Mashaalla
Alhamudulillah to be a Muslim
Devil's deception 😢😢 beware my fellow Christian this is one of the last events
Aim of this ceremony is to contradict your faith keep watching 😢😢
Proud to be a Muslim
Kodi simungayike apapa dawa yonse please tikuyifuna
Mposo abaleee, nanga kwinako tikakupezera kutiko sono
Manshaallah brother
Mwenyezi Mungu, hapana mungu ila Yeye, Aliye hai, Msimamizi wa milele, Amekuteremshieni Kitabu kwa haki, kinachosadikisha yaliyokuwa kabla yake, na ameteremsha Taurati na Injili kabla yake kuwa ni uwongofu kwa watu. Na akateremsha upambanuzi: Hakika walio kufuru Ishara za Mwenyezi Mungu watapata adhabu kali, na Mwenyezi Mungu ni Mwenye nguvu, Mwenye kulipiza kisasi wewe katika Mwingi wa rehema, vipi hakuna mungu ila yeye ni mpendwa, Mwenye hikima ni yule aliyeteremshiwa kwako Ama waliomo nyoyoni mwao wanafuatwa Hawakusema kuwa kila mmoja Kwa Mola wetu Mlezi. na hawakumbuki ila wenye akili, tusipotoke nyoyo zetu baada ya kutuongoza bila shaka Mwenyezi Mungu hatavunja ahadi yake, mojawapo ya makusudio ya surah.
Kudumu katika Uislamu baada ya ukamilifu na ubainifu wake, na kukanusha shaka za Watu wa Kitabu, hususan Wakristo
Ni surah ya Madina iliitwa Surah Al Imran kwa sababu familia ya Imran imetajwa ndani yake katika aya ya surah.
Herufi hizi zilizotengana zimemtangulia mwenzao katika Sura Al-Baqarah, na zinaonyesha kutoweza kwa Waarabu kutoa Qur’ani kama hiyo ingawa inaundwa na herufi ambazo Sura ilianza nazo, na kutoka kwao wanatunga hotuba yao.
Mwenyezi Mungu ndiye ambaye hana mungu wa kuabudiwa kwa haki isipokuwa Yeye pekee na hakuna mwingine aliye hai ni maisha makamilifu yasiyo na kifo au upungufu.
Proud to be Muslim
Chiweluzo chidzapelkedwa chifukwa Cha zintchito zarhu osati proud to be a Moslem or proud to be a chriastian nzopanda pake
Evidence please !!!!
Masha Allah pondipanga kukhara msilam ❤
Ma sha Allah❤
MAA SHAA ALLAH
Mr Hassan munaphunzira koma ndinu mbuli yothelatu kuuzimu ndichifukwa chake mukupembedza wovumbulutsa Quran naganiza ndikukhulupilila kuti mukupembedza Mulungu wamoyo, chonsecho ndiSATANA weniweni adamunamidza muhammad kuti ndiiyeyo adili kuvumbulitsila aneneneli amuBible
❤Mashallah
❤Ma shaaAllah
Mashah allah sheikh awuzen ndithu❤❤❤
Ameen thummah Ameen
Mashallah, please upload some more
Ma Sha AllAh Amee
Jazakum llah khaira
I'm proud to be a musilim
Allahmdulillah ❤❤❤❤❤❤
MULUNGU AKUONJEZELENI MASIKU AMOYO WANU ADALISESO MU MZELU ZANU
ان الدين عند الله الإسلام
🕋🕋🕋🕋🕋☝️☝️
MASHA ALLAH MASHA ALLAH MASHA ALLAH
Ma shaallah
Dawa koma imeneyo osati zakuti Achibeketi adali mfiti adakuphera agogo ako muzichita Dawa yolimbana ndi amene Sali Asilam timakunyadiran big kep it up
Anayankhulapo choncho iyeyu?
Mashaa Allah sheikh ❤❤
We need you here at ntonda in ntcheu
Ma shaa Allah
Ma sha Allah ❤❤
Anthu timasokoneza pakati pa Mulungu ndi Alla, palitu kusiyana kwakukulu, ndipo mudzadzindikira koma mochedwa kusiyana kwa awiriwa
Tiyeni tafunile zabwino zonse makolo athu omwe anayima pakati pachowonadi chisilamu omwe alimoyo mpakana omwe anasogolera kale kumanda mulungu awapatse jan'na please
Allihamdulillah pokhala msilam chonde Allah muzanditenge ndili msilam
Aaaaa Sheik openga uyu kanundu akumupweteka,, mutuwo kukulako ukumulemera
Kung'alula zomwe mmazidutsa kutchalitchikoka nde mwadabwa nazotu??
Akutenga zammutu kapena??
Else likunama ndi Bible lotu pamenepoo 😂😂😂😂
Minika!!!
Maashallah
Mashaah Allah
Asilamu olambila mwala wa ku arabia saudi dzipumi biii ngati zoona
Masha Allah ❤
Macha hallah ❤❤
Pakut ngat wakhungu alondole njira akukhungu onse awili azagwa mmbuna....mukazaziwa choona choona chizakumasulani
Inu chilungamo munachiona bwanji
Allah akbr
Alihamudulilah❤
MBULI ZA ANTHU NDIPO PALIBE CHIMENE MMADZIWA
Masha Allah
MashaAllah ❤❤
Allah Akbar
Mulungu wamoyo wovumbulutsa Uthenga wamuBible akuchitileni chifundo kuti mumudziwe.
Komano kunena chilungamo Alhamdulillah asilamu mulungu anawapasa mzelu ndithu
Ameen
Mashaa llah
I once met this Saidi Zambia for almost 8 hrs.
Anafika pokwiya titamufotokozera zinthu zomwe iye samadziwa za chiyambi chachisilamu ndipo anakwiya heavy.
Amene mumamudziwa ask him za anyamata omwe anakumana nawo usiku mnyumba ina ku mangochi.
He ended up a failure on that meeting.
Chinayamba bwanji tiziwe nao
Machalawu
Asilamu nonse ndi ma judger ndekha nonse moto ma vindictivist shupiti
1 muslim
Alhamdulillah
Masha Allah Allah Akibari
MaShaallah
Masha Allah shelk
Alihamdulilahi
Where is the other part of Seventh Day part? Let's PRAY that each one of us here on Earth meets GOD's Grace and know the truth, I Pray for you my muslim brothers. Amen
Kulowa kumoto kulipo ndiiithu 😂😂😂😂
Mashaallah
Ndikudziwa chimene ndikunenachi and i Challenge you
Mashaalah
❤❤❤❤❤❤
Ndipepha Allah kut ndidzamwalire kanali silam