This man was my best ..even ndigone osadya but kungovela nyimbo zake ndimakhiluta ....like I wasn't having a stress for the food....may his soul rest in peace 😢
Basi moyo ndi choncho, iwo kudwala kupitisidwa ku south Africa, president waku south Africa kudwala kupitisidwa ku Kenya or UK, waku UK kudwala kupitisidwa ku Japan 😮😮😮😮😮
My my my my best best ❤musician in malawi is thomas chidade not astanic awa ena iyaaz .. miss
Mwana uyuyu ineyo ndimamufira heavy ❤❤❤,🔥🔥
Ine ngat Pali nyimbo zalokolo zomwe ndimavera ndiza Thomas chibade ndipo sindizasiya kuvera paka ndizapite koko
Nice music brother I love you❤
Thank you very much. I have been looking for this song
The best of the very best Mr Chibade the Legend
Compose a song like Thomas Chibade did and Lucius did these were speaking for Malawians through music, legends never die
Koma mwati satuma zigawenga zikamugwile chibade kumanda komweko😅😅😅😅
Akhoza kukamufukula ndikumusiya pantundatu
Kkkkkkkk eti
ngati kuli nyimbo zomwe ndimazikonda kwambiri moti everyday ndimatha kumvera×5 ndi big man amenewa koma dziko lapansi RIP my king
My Legend and my friend continue Rest in peace
May his soul continue resting in peace. He was one of my favorite artists in Malawi.
My best musician ever may his soul rest in peace
Best song indeed
Always you was in sweet sound Chibade❤❤❤❤❤
The best song T chibade rest well
Madala hit munapha iyiyi heavy size kukan my his soul rest in peace until we meet again on other side
Rip Thomas 😭😭
Very strong messages from our late musician Thomas chibade May his soul rest in peace
Chibade unali mutu oganiza ❤❤❤❤❤
My best musician ever forgettable continue rest in peace bro
Best song composer Malawi ever had,RIP Legend
Zimatilisa zoterezi
We shall never have him again,, Legend
Beautiful song RIP
Very nice song
The best song like this one
Nice song from the lost talented musician.
This man was my best ..even ndigone osadya but kungovela nyimbo zake ndimakhiluta ....like I wasn't having a stress for the food....may his soul rest in peace 😢
Nice song
Best artist
Chibade was a prophet. And sees from far..!.
Just that He was attacked by a Satan blindly, and lost the way.
Exactly bro and u saw it in real
He was gone with his talent and wise 😭😭😭😭😭😭
Eishh koma Thomas eishh ayi ndithu imfayi eee ai ine ndikusowa chonena may your rest in peace
Plz ngati mulinazo tumaniko zinandi plz nyimbo zake uyu
Was my favorite iwe imfa 💔
Nice song
Rest in peace
Good massage
Eish chibade continue rest in peace . Ndipo tiika pa repeat
Awa anali atate pamayimbidwe ur soul may continue rest in internal peace 🕊️
Uyuyu anali captain ndipo mpaka kalekale dziko tidzamukumbukira ,anabwera kuzalankhula chilungamo munyimbo zake R.I.P
😢😢😢😢😢 koma infa kutenga anthu otilankhulila😭😭😭😭😭rip legend
Please nyimbo imeneyi taito yake ndi Chan please
The gap is too huge to be filled..........
Oweyz loving you chinkumba rip
Title please nduisake ku Vidmate
Ulendo wa pa ndege mwaononga ndlama zingat
Nice song ❤❤❤❤❤
❤❤❤❤❤❤❤❤
Nyimbotu Koma izi osati achina Zeze ndi a jetu ndi ena otero
Basi moyo ndi choncho, iwo kudwala kupitisidwa ku south Africa, president waku south Africa kudwala kupitisidwa ku Kenya or UK, waku UK kudwala kupitisidwa ku Japan 😮😮😮😮😮
Respect Thomas chibade
Pakanakhalatu mwayi omavota kuti ena amene anafa abwelerenso uyuyu ndikanamuvotera azadzudzulebe komanso Matafale ndikanamuponyera vote. Osati ena amayimba zachamba aja
Eeeee ayaaa mamamama haha
dolo kwambil
Anapitad km uthenga ndiomwe anatisiyira CHIBANDE again rest in peace 😭😭😭😭😭
👍
Anali mwana oganiza bho kwmbr km yifaa mulungu yekha
Aimvere chakwera
Luso lanu lizavuta kuiwara Rip Chibade
Legend
❤
Power 💪💪💪
Real men never dies
Uyu analikatundu pa compose
Uyu anali katundu ndipo dzumuwake uziwusa mutendere 😢
Kod zikutibwanji kumeneko chibade wamwarira aa 😭😭😭😭😭😭
Chibade tizakulila pakana kale
Uyu Anali freedom fighter wachinsinsi guys mzimu wake uwuse muntendere ndithu
akanakhal moyo akanamumangstu😂😂
RIP chibade
Chibade chibade 😢😢😢
Uyu anali oyimba zinangotivuta
Rest well
Continue Rest well ❤️🩹 legend 🎉😢
Wa bwino sakhalisa pa dziko
rip lengend
Ndaikonda kwambiri nyimboyi....otsutsa boma simungatiuze zochitanso ai, munali mommo koma matama too much, ndalama munkangowana nokha nokha kukudzudzulani simunkamva. Adad anu aja munawakhumbatira ndipo simunawalole kuti adzimva kulira kwa anthu ena popeza anali adad anu okha lero bwa? Ndiye inunso amene mukulamulira lero mukumatilankhula ngati pamipandopo munadziikapo nokha dikirani muone zomwe zichitike next year, mutiliratu inu. Ife timaika atumiki pa mipando komanso kuwathotholapo akamatitenga ngati ife ma zoba...Pano muli busy kumatiopseza dikirani muone zomwe tikupangeni 2025. Tikkapo ena omwe alibe mifunda ndithu...
koma umu munali chilungamo chanyoooo eee rip 😭😭😭😭😭😭😭😭
Abwino sakhalitsadi mzimu wake uwuse mumtendele
Rest piece my legend
Yoooooooooo
RlP dolo💔😭
Continue rest in peace Legend 🩸
😢😢😢😢
It's true
Crip chenkhuma
Nzimu wa Thomas R,I,P
Rest peace bro
abwino sakhalitsa pa dziko MYSRIP
😭😭😭😭😭 RIP CHIBADE
😢😢
IFA sithawika gulani makhwala muike mzipatala
Anali akatundu awawo ndithu
Very sad
RIP MR CHIBADE
Muli uthenga
Ulemu wanu Achibade zoonadi uthengawu ndiwazoodi big
Daily tikumaluza anzathu a luso eish...
ANTHU A LUSO ANALI OMWEWA NDITHU
Zoona boss nt ati gibo lantos ndiye ndaniso kaya
Iyi nde ipite kwa pule
R lp
Rip
Ngati zatero kurira kwanga kosarekeza
Ndi
Palibe amayikidwa kumwamba tonse timayikidwa nthaka
Mawu akulu awa ndithu, anali wachikulire chibade
Nice song