Mai ife tikufuna economy yochita attract investment mdziko osati zogawa chimangazo.tikufuna ife a Malawi tidzidzathandizanso maiko ena ndi chimangacho.osati kumatiuza za zaulere
Unagulitsa ndege iwe nkusiya ndege yakutha yomwe inatiphera wathu uja.... Palibe chanzeru kumadzudzula MCP pakuti ukudya nayobe... Nkhani yopempha kuli mnzako Usi nayenso ati amatha kupempha... Anyway, you don't love Malawians... forget about becoming a president even in times of accidents...
❤❤❤❤ mashaalah kofunika ndithu
Aaaaaa zaziiiii mayi wopusa uyu za anagulitsa dege
Grece chimga anati kubwera chipani chamwazi mai njoice d chakwera buchillll
PP my Vote
Akabaza nde zichani so aaaaaaa aaa.
Just unite with UTM , forget about the past forward shall be gain by Malawians
Madam joice banda,bwanji summulangiza chakwera zinthu sizikuyenda iye angoyendayenda kumaononga ndrama anthu akuvutika
Ati funani wina, ine ndi ndani kuti ndikane, za ziiiii
Mai ofoyira uyu. Kugulisa ndege ya new one kusiya yokutha yomwe yatiphera abale athu😢😂
Hiyaa kangoneni mai kwanu munachita kapumeni
Mai oyipa mtima,kupha,kuba,kwa nthawi yochepa dziko linaonongeka
Mcp my vote 😂😂😂😂😂 mulirad chakwera mumuva kuwawa anthu aulesii inu alomwe 😂😂😂😂
Iwe galu ukuti ukusangalala
Ankakuvotereni ndani mfundo zake zimenezo?
Zilibwino kwambili mama😂😂😂😂
Mesa munari limodzi
Koma nyumba ndiye munamangadi mama to be honest may God bless you
Zoonadi munthu sakoma zonse kma Joyce mmm amaesesa than chikangawayi iiii
Zoona kuzitama kugwetsa kwacha? Bingu was agreat leader ever.
pp my vote 🗳 ❤❤❤
More fire 🔥 ❤❤😂😂
Chipani chokuba
Mai ife tikufuna economy yochita attract investment mdziko osati zogawa chimangazo.tikufuna ife a Malawi tidzidzathandizanso maiko ena ndi chimangacho.osati kumatiuza za zaulere
Oooooooooo0oo
Tisamveso kuti mwagwirizana ndi chikangawa pls yimirani panokha mai
Unite with DPP Malawi akuwawa uyu ee, zinthu zakwera, inu mama munakweza salary mwamphavu
Mesa kodi mumalamulira nonse
Azungu akuti! kkk
KOMA AMAI AWA MXIEWWWW
Mmmmmm anali limodzi ndi Chikangawa, anthu awa ndamene akuononga Malawi.
Kodi Mesa akuti nanga zotukwana ai? Kkkkk Mai uyu anamila basi
Pepani MAI JOYCE BANDA,Kodi dzumvekazi ndizoona?😞😞😞😞😞...
Fundo zabwino zedi
Akulankhula kwa oduka mitu anzake. Kuyamikira kugwetsa kwacha? Cash gate ija sakukambako bwa?
Koma amai mutsamakambe zakale takambani zapanopa chifukwa mukukhala ngati simukuwona bwanji inuyo ndi A MCP paja tisamale naye uyu guy
Tiwona zithu next year 😂😂
Koma kusisa marata osati kumagira athu
Palibe cha mzeru chomwe mungauze mtundu wamalawi mkuvera fundo zanu.Inunso ndi panja penipeni ndipo ndalama zomwe mwapangira msonkhano umenewo mwachita kupatsidwa kuchokera ku mcp.
Kkkkkk chilungamo ndi mwano
Ndipooo this country being ruled by mzimayi, forget about thatt, the Malawians can't do it again that mistake!!
Zapanga in ndi chakwera mm xandinyasa, pan ndikuyembekeza bpp utm ,afodi not pp
Chipani chokuba
😂😂 awaaa ndie ayi
Cash gate ina bweretsa mkw 1000 malawi akubaso inu ngati mcp
Kulimba mtima kokabanako ndalama CASH GATE
Unagulitsa ndege iwe nkusiya ndege yakutha yomwe inatiphera wathu uja....
Palibe chanzeru kumadzudzula MCP pakuti ukudya nayobe...
Nkhani yopempha kuli mnzako Usi nayenso ati amatha kupempha...
Anyway, you don't love Malawians... forget about becoming a president even in times of accidents...
Awa akufunika saport basi pawonkha sagawine
True.
Your speech seems like you're attacking Peter Munthalika,osamunena nzako amene akulamulira panoyu bwanji
Cash get tawonera paiwe simungawine or mutatani mesa unali kwachakwera sibasi mwabwerako
Anapitilako kukaphetsa Chilima
Osati mbutuma zinazi nkhalamba zikuwonekazi,tikufuna azimayi olimba mtima ngati ameneyu, amunanu tatopa nanu.
🤮🤮🤮🤮🤮
Mayiyu palibe chomwe angathandidze kudziko lamalawi she don't have economic wisdom ndipo she is fundoless
🤣🤣 Your speachh is full of emptyness!
Ndipo osamukhulupilira maiyu akungopusisa amalawi pp ndi MCP azagwilizana anthuwa kuvotera pp ndekuti wavotera MCP beware maguys
Mesa kodi mumalamulira nonse