ULENDO AMALAWI TIVOTELA SATANA WABWINO ........ BRIAN BANDA NDI ANZAKE AKUTI ONSEWA PALIBE M'NGELO
HTML-код
- Опубликовано: 18 сен 2024
- ULENDO AMALAWI TIVOTELA SATANA WABWINO ........ BRIAN BANDA NDI ANZAKE AKUTI ONSEWA PALIBE M'NGELO
Welcome to our channel, where we dive deep into the intricate and evolving world of Malawi’s politics. From the rise of powerful political parties like the Democratic Progressive Party (DPP) and Malawi Congress Party (MCP) to the powerful impact of the UTM Party, we bring you insightful analysis on the key players shaping the nation. Explore the journeys of leaders like Lazarus Chakwera, Saulos Chilima, and the influential activist Bon Kalindo as they navigate the challenges of governance, power struggles, and the quest for a better future.
Our channel is dedicated to unraveling the complexities of Malawi’s political landscape, offering you detailed breakdowns of alliances, rivalries, and the significant events that continue to define the country’s destiny. Whether you're interested in historical perspectives or current political dynamics, we provide in-depth coverage and engaging content that keeps you informed and inspired.
Subscribe to stay updated on the latest developments, and join us as we explore the fascinating stories that shape Malawi’s political narrative.
#MalawiPolitics #PoliticalAnalysis #DPP #MCP #UTM #LazarusChakwera #SaulosChilima #BonKalindo #AfricaPolitics #PoliticalActivism #petermutharika
Times sikondera chipani chilichonse ngati aja Ali ku mibawa ndi mbc
Mulungu apitilire kukudalitsani
Better devil yemweyo
Ine makosana inu mumakwana ngati Pali program yoveka nde ndinu madoda
😂😂😂 eshi
Bravo guys mukuchita ntchito yayikulu Ku unikila a Malawi, ngati pali Boma lingayamike ndi la Tonse munalimenyela nkhondo ndinu achina Brian ndi gulu lanu.
Boma ili munthu wolimbikira awona kusintha guys osamadikira zopasidwa at tiyen kumunda Tikalime basi
Man anthu akulimbikila km zinthu sizikuyenda
Mizwanya yosatenga mbali polankhula,ndiye tiyeni tizionere tokha.
Koma Satana uyu wa chikangawa ndiwausilu,amadicha ndalama zambili Ku asogoleri osiyana siyana ,pamafunika Kuti Nagari wadicha ndalama alandile Koma asamuvere agwile ntchito mwachulingamo
😂😂😂 koma mjedo wakoma ma guys.
Komadi tsongoleri akakhala wakudya utsi onse omusatira amakhala okudya utsi.zoona Wanda.
Nkhaniyo ndiyoonadi tikavota basi tichose satanic yi
Chakwera ndi galu
Apopo mkunena zowona koma ngakhale zovuta Zina kuno kumuzi fetelezayo ndiyet tikumatha kgula kwambiri NDipo zinthu zolimidwa ziyende chocho 3 yrs ikubwelay miyoyo ya anthu amene amalimbika ntchito awona kusintha eytu
🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉😂😂😂
😂😂😂 koma mjedo wakoma ma guys.