MOSES KUNKUYU MUTU SUKUKOKA UKU KWANUNKHA UTSI

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 9 сен 2024

Комментарии • 96

  • @user-iv6iw1ck8s
    @user-iv6iw1ck8s Месяц назад +2

    Times 360 it's my best, Brian Banda and your Team pitilizani kutidziwitsa ndi kutivetsa kukoma, Brian Stanley Nowa, Capetown # from Monkey Bay chantulo

  • @gradsonmayira9336
    @gradsonmayira9336 Месяц назад +13

    Brian ntchito muyigwira🔥🔥

  • @BrianMaganga
    @BrianMaganga Месяц назад +1

    Mai chindevu mumakwana mwati Olira alile mwandisangalatsa

  • @LenoMvula
    @LenoMvula Месяц назад +7

    Times mmatha mmatiimilira kuno ku malawi nice job

  • @user-um2es1yp5y
    @user-um2es1yp5y Месяц назад +2

    Wonder chipongwe mzako akwatire 😅😅😅😅

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto Месяц назад +1

    Watching live fro RSA😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @PortiaMhlambi-y4g
    @PortiaMhlambi-y4g Месяц назад +4

    Brian Banda and ur team mumakwana

  • @annembepula
    @annembepula Месяц назад +6

    Omse okupha sadutsa munali buzy kupha,kumanga amzanu kuophyeza anthu muziwona zangoyambapo 2025 mulila munanyanyanya mmayesa mzamuyaya

  • @simonejose8925
    @simonejose8925 Месяц назад +2

    KUCHOKERS KUMOZAMBIKI A FELIX CATONHEZA TEMBO NSANJE SOUTH CONSITUENCY NSAMBA POLING CENTER PAMWAMBA A CHAKWERA 365TIMES

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf Месяц назад +8

    zigawenga za mcp pamenepo manyazi bwaa BICC chitukuko chandan inu 5yrs chitukuko chanu kupha mr chikangawa ndi umbava

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e Месяц назад +2

    Times mumandipangitsa ngati ndili komweko ❤❤❤

  • @mphatsosadiki4983
    @mphatsosadiki4983 Месяц назад +5

    Wamenya campaign yomwaza chuma chochuluka ndiye aluzeso eeeehhh timva ena atamwalira ndima BP sure

    • @Eric-gb9ms
      @Eric-gb9ms Месяц назад

      😂😂😂😂😂😂

  • @user-ko6kp7jl4d
    @user-ko6kp7jl4d Месяц назад +1

    Wishing mcp.all.the best.choose patriotic leaders please!!!

  • @user-ij1yz4ex2v
    @user-ij1yz4ex2v Месяц назад +1

    Eeee koma Brian ndi wonder ayi ndithu nkhawa zomaopa chikangawa munapachika

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r 24 дня назад +1

    Zisilu mcp kupha anthu apule chikangawa party

  • @TimothyKabumbuKendrix
    @TimothyKabumbuKendrix Месяц назад +1

    Mr Brian Banda zabwino zonse ndi timu yanu kumeneko, ndine Hendrix Timothy kuno ku Botswana

  • @user-ko6kp7jl4d
    @user-ko6kp7jl4d Месяц назад +1

    Well organised,convention kuyipasa moto viva mcp😮😮😅

  • @munashemoyo4190
    @munashemoyo4190 Месяц назад +1

    😂😂😂😂😂 kumkuyu wandiwaza zed ndinapemphera kut usawine ai 😂😂😂😂😂

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Месяц назад +2

    Onse okupha sakudusa kkkkkk

  • @MadalitsoGama
    @MadalitsoGama Месяц назад +1

    Zoledzera izi

  • @RichmanIssah
    @RichmanIssah Месяц назад +1

    😂ine Koma mayi chindevu😂

  • @RichardChirwa-em6qj
    @RichardChirwa-em6qj Месяц назад +4

    Agaluwo asakozele makoma kumeneko paja ndi khalidwe lawo lowononga

  • @BrianMaganga
    @BrianMaganga Месяц назад +1

    Wina athawà

  • @simonejose8925
    @simonejose8925 Месяц назад +1

    ABALE ANGA PANGANI CHILONGAMO POPANDA CHIWAWA DZIKO LOWOPA MLUNGU YEKHA NDIWAMKULU MLUNGU ALANGE OPANGA ZOIPA NAWONSO APANGE

  • @CassimCawanga
    @CassimCawanga Месяц назад +1

    Best television n plograms in malawi

  • @MichaelMbona-ch2kc
    @MichaelMbona-ch2kc 29 дней назад +1

    Chikangawa aut

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 Месяц назад +1

    Time group machine machine ❤

  • @ConeriasPhiri
    @ConeriasPhiri Месяц назад +1

    Times 360 mumatiimilira mumativesa kukoma zukachitika tivera kwa inu

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona Месяц назад +1

    " Pakuti Malamulo a Dziko lino amalora, choncho dzina langa likakatulukanso Ku Ballot, ine mkayimanso"
    Mr Lazarus Macathy Chikangawa ndinu munayankhula mawu amenewa pamaso pa yemwe munasayinira naye mgwirizano . Tulusani za kafukufuku wa ngozi ku Chikangawa simukutulusa.
    Pali ???????
    Munthu woyipa iwe,
    M'busa okuba ndi okupha. God Will judge you evil man 👹🔨⛏️⚒️🔨👹.
    Lero zisangalala koma Amalawi sangayiwale Kuti unapha kufuna zonse zikhale zako.

  • @honourablebanda1961
    @honourablebanda1961 Месяц назад +2

    Times 360 is the best.
    Allan Banda pritoria(RSA) #ing'aluleni azibambo

  • @johnkatumbu6846
    @johnkatumbu6846 Месяц назад +1

    Waitchela kale mwati kuluyo?🤣

  • @simonejose8925
    @simonejose8925 Месяц назад +1

    GWIRANI NTCHITO A TMS

  • @BlessingsSeleman
    @BlessingsSeleman Месяц назад +1

    Kod brian unayamba mwazifusa chifukwa chomwe asilikali Ena mwati safuna kuti camera yaonese

  • @DanielKatengeza
    @DanielKatengeza Месяц назад +1

    Times ilengezenso kuti Brian Banda president wa Malawi nzakoyo akhale Vice President I think dzikoli liyenda bwino popanda corruption

  • @SelinaGamaliyere-q8v
    @SelinaGamaliyere-q8v Месяц назад +1

    Onse omwe anapha chilima asawine anthu oyipa

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v Месяц назад +1

    Ubwino wake zomvota wochewa wokha wokha ndemukaluza muphanaso nokha nokha ma pb muzikomoka nawo zindalama mumamwaza zija

  • @pauljosephmakaula6835
    @pauljosephmakaula6835 Месяц назад +1

    Katundu Vitumbiko Mumba all the best...new political dimensions

  • @SelemanSimoni
    @SelemanSimoni Месяц назад +1

    Thomas chibade

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje Месяц назад +1

    Eeeee km times mukuigwila tchito yopambana

  • @user-ul1fb4yn5o
    @user-ul1fb4yn5o Месяц назад +1

    Times team mumakwanisa

  • @isaacgmc
    @isaacgmc Месяц назад +1

    Koma amalawi mukadali kuivotela MCP mmmmmm😂😂😂😂

  • @user-kh4qp1ji1i
    @user-kh4qp1ji1i Месяц назад +1

    Tea sitidya Brian 😂 timamwa!

  • @TriceGulani
    @TriceGulani Месяц назад +1

    Kkkkkkkkkkkk zavuta achimwene amosesi

  • @CatherineKamsare-cy3yo
    @CatherineKamsare-cy3yo Месяц назад +1

    Kwachema🤣🤣🤣🤣

  • @user-ww9rj2wx8d
    @user-ww9rj2wx8d Месяц назад +1

    Bolani asamupheso Brian Banda mtola nkhani mbambande

  • @KingsleySymon
    @KingsleySymon Месяц назад +1

    Nanga Nanu mtentha ndevuyo bwanj???? kkkkkkk am Kingsley Symon kusalima

  • @EnerstBanda-m4s
    @EnerstBanda-m4s Месяц назад +1

    President sanalakhule bwino sungadzudzule opeleka ndalama tsiku lovota ai pomwe Anthu ataononga kale ndalama zawo akanawauza nthawi yomwe amapanga kampeni kuti asagwiritse ntchito ndalama komaso akanauza omwe amaletsa enakuti asaime nawo chifukwa sanakhale mu chipani zaka ziwiri izi zapangitsa atidye nawo mong Dausi, Brown Mpinganjira,Uladi Mussa ndi Ken nsonda kuti asapeze nawo mwai opikisana nawo zomwe President akanatha kuzikhoza before not tsiku la master mansakho kumenekuku wapangira kampeni ena wichs not good

  • @zacchaeusbvumbwe391
    @zacchaeusbvumbwe391 Месяц назад +1

    Ntchito mwayigwira

  • @RichardChirwa-em6qj
    @RichardChirwa-em6qj Месяц назад +2

    Mkasa paja ankati sazatamandanso wa ndale waywala cruise 5 pa zodiac ndi joab, yedye

  • @NewtonSikwese
    @NewtonSikwese Месяц назад +1

    Koma kuyakhura chilungamo ndongotsolo lake likuyenda bwino koma mapeto ake Akala bwino

  • @MaggieKaufa
    @MaggieKaufa Месяц назад +2

    Koma kwachematu😅

  • @andiwochishadreck3753
    @andiwochishadreck3753 Месяц назад +1

    Ndalama zakuba zabwerera kwawo

  • @CatherineMakina-d5o
    @CatherineMakina-d5o Месяц назад +1

    Uncle b

  • @LikangaManuel-sk8yp
    @LikangaManuel-sk8yp Месяц назад +1

    Achewa okha okha kunva kamwamo ochewa weni weni 😂😂😂

  • @SolomonBewula
    @SolomonBewula Месяц назад +1

    Kunkuyu asowe

  • @annembepula
    @annembepula Месяц назад +1

    Komatu mkasa dyela uyu kwa Dad uli nkomko ukunsi eeeee

  • @HenryGoba-m7q
    @HenryGoba-m7q Месяц назад +1

    Anthu akuvotela zigawenga zachilendo ziphe manganyaa

  • @whatsonbanda4277
    @whatsonbanda4277 Месяц назад +1

    Mcp chipani Cha mtendele.

  • @EmmaMbewe-vg4td
    @EmmaMbewe-vg4td Месяц назад +1

    Onetsetsani kuti Mkaka asalowenso

  • @courageouslondo1986
    @courageouslondo1986 Месяц назад +1

    Mumatha mabwana

  • @RichardChirwa-em6qj
    @RichardChirwa-em6qj Месяц назад +1

    Mizimu anaononga ku chikangawa iwakanthe ndithu anthu akuphawo

  • @NedsonJosaya-pn1te
    @NedsonJosaya-pn1te Месяц назад +1

    Mwayedzeka kale?

  • @ZaithwaMatchado
    @ZaithwaMatchado Месяц назад +1

    Kukuyu 😂😂😂😂

  • @GiftPaulBrownBrown
    @GiftPaulBrownBrown Месяц назад +1

    Kwachema ku LL ine Gift Paul Brown from Mozambique

  • @user-zq3uf5bc8v
    @user-zq3uf5bc8v Месяц назад +3

    Issa manyaka ife tikulira biyeni wathu chauta Ave mapemphero amalawi kuti tidzadziwe chilungamo pokhapokha mcp itagwa muboma kuno ku katonga

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe Месяц назад

    Kkkk Amwe tea wa poison ndi zakudya za poison wa Achakwera..anthuwo asadye chakwera wakupha samalani naye angakudyeni

  • @user-lk8kj9zv6x
    @user-lk8kj9zv6x Месяц назад +1

    Inuyo guys ndi chuma cha boma ma pongolin athu

  • @user-ty1vq9lq6w
    @user-ty1vq9lq6w Месяц назад

    Chitukuko chao, ndikupha, kuba ndikuononga

  • @user-zw8ns7bk7s
    @user-zw8ns7bk7s Месяц назад +1

    Aichinja mozey

  • @Maliet-nh6kf
    @Maliet-nh6kf Месяц назад +1

    Panyo pachakwera kuno kuli holiday

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 Месяц назад +1

    Sopano zokudyaxo zokanganilana

  • @victorbanda9039
    @victorbanda9039 Месяц назад +1

    Achikhala a DPP akanakuswa brain muja umawanyozeramu a mcp wo aise Koma poti awa ndi anthu amtendere ukuyenda momasuka

    • @user-ww9rj2wx8d
      @user-ww9rj2wx8d Месяц назад

      Mwayiwala za kuchikangawa eti

    • @MzadziWanga
      @MzadziWanga Месяц назад

      Ku state house munamuthamangisiranji ngt muli a mtendere, osati ma vote akuzunguzan mkanamupheraso konko paja zaugawenga ndinu # 1

    • @uzaleuzale8603
      @uzaleuzale8603 Месяц назад +1

      Mwaiwara kt mwamuika mu list ya anthu ophedwa anthu akupha inu

  • @CathrineBizza
    @CathrineBizza Месяц назад

    Kwachema wina alira kuwononga ndrama zaziiiiii

  • @KingsleySymon
    @KingsleySymon Месяц назад +1

    Brain amatha kkkkkkk

  • @DesmondChavula
    @DesmondChavula Месяц назад +1

    Brain ntchito umatha

  • @KHWENGWEYAMAPEMBA-l4w
    @KHWENGWEYAMAPEMBA-l4w Месяц назад +1

    Kwayaka moto kumeneko

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np Месяц назад

    Wochakwera amafuna choncho basi kusogoza chilima...mwataya chipangano agalatiya.

  • @CynthiaLusubiroMwalwanda
    @CynthiaLusubiroMwalwanda Месяц назад +1

    2:16 am

  • @ChrispinJohnson-py5ie
    @ChrispinJohnson-py5ie Месяц назад +1

    kunkuyu dyela

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Месяц назад +1

    Kwachema

  • @hezekiayelemia
    @hezekiayelemia Месяц назад +1

    Brian Banda eiiish experience ikumuthawa

  • @peterkinsLekera
    @peterkinsLekera Месяц назад +1

    Kodi mec ndiyoyang'ana za chisankho cha chipani chimodzi ? Ndikudabwa

  • @user-gy8yn6qw2k
    @user-gy8yn6qw2k Месяц назад

    😂😂😂😂😂

  • @SebastiaoErnesto-mh6ec
    @SebastiaoErnesto-mh6ec Месяц назад +1

    🎉🎉🎉🎉😢😢

  • @peterkinsLekera
    @peterkinsLekera Месяц назад +1

    Kodi ndizololedwa kuti asirikali atenge nawo gawo ku conversation yachiani? Awapanga hire ngati chipani kapena angwiritsa ntchito misokho yathu

  • @user-ko6kp7jl4d
    @user-ko6kp7jl4d Месяц назад +1

    Palibenso chipani chingakututumuseni pitirizani.mfimdo.zanu.zotukula.dzikoli,linali mkamwa.mwa mimbulu more.fite

  • @BiliatMzungudala
    @BiliatMzungudala Месяц назад +1

    17:15 17:18 Ife sitigona a times tili nanu

  • @StevieChauluka-r4v
    @StevieChauluka-r4v Месяц назад +2

    Chithyola Banda adutsa pa SG basi, am Stevie Chauluka from area 25.

  • @thomasmilanzi6442
    @thomasmilanzi6442 Месяц назад +1

    Kunkuyu moto