Utumiki wa a Twaibu - kufotokoza za kuzima kwa magetsi ndi nthawi yomwe tiri komanso komwe tikupita
HTML-код
- Опубликовано: 18 сен 2024
- Mu utumikiwu, a Twaibu akufotokoza za vuto la magetsi mogwirizana ndi nthawi yomwe tiri ndi komwe tikupita. Mkati mwa izi, afotokozanso zina zambiri zoti okhulupilira tidziwe.
Amen
Thank you for opening our eyes so that we should be really ready for Jesus is really coming, may living God bless you and your family
Amém 🙏. Deus nos proteja para ganharmos a vida eterna
Thanks mtumiki Twaibu
Ziphunzitso zanu zolamitsa
Pitilizani kutiphunzitsa
Amen
Yesu abwela posachedwa
Amen abusa
A twaib ine ndiye ndimachita kuchalira each and every subject yanyuwani ina iliyose koma ndimakuoemphani kuti zina zomwe munangotilonjeza muziizpitiliza
Ai zikomo brother twaibu
One phe kuverera nichidwi, kuyembekezeraso maenje 8 amene anasala nde Pali kii ya gate muulendo was chikhristu chonde mtumiki was Mulungu tikumbukireni.
Ndifuna kukufunsani Inu mtumiki Twaibu Ahmidu kuti,Kodi nkhani ya kukhwimira munthu kukhala ndondocha abathwa ndikumawagwiritsa ntchito zosiyanasiyana,ndiye timamva kuti amangotitengera munthu uja mwamatsenga chimene timakaika ndi china chachabe olo Chanthochi,ndiye ndiye tatambasulani mtumiki kuti Kodi zimayenda bwanji kwenikweni,Kodi anthu aja akumatulukira pambuyo poti wakhala kumanda Kwa zaka Kodi akubwera aja ndi anthu Eni Eni kapena zifanifani kapena ziwanda za Satana tithandizeni mtumiki please
Mtumiki pitilridzan ku phunzitsa za thawi yakumapeto, panonso tayamba kumva za ulenje wa anthu omwe akumagula Tiana ta nkhuku uku akugula anthu
Following
Mulungu wakumwamba apitilize kukudalisani ndikutiululila zobisikaxo kt ife tiziwe za izo zili kuza.
yosamaliza tu iyi😑
maliizani za maenje16