KU CHIKANGAWA NDIYE KWACHEMA UKU / ZINTHU ZAKE ZOVUTA🙌🙌

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 28 авг 2024

Комментарии • 396

  • @RiannahKaliat
    @RiannahKaliat Месяц назад +30

    Pempho langa ndilakut ngat chilima anaphedwa ndi anthu ndikut mzimu wake uwakathe ndipo asowe mtendere mpaka kare uwakathe

  • @RiannahKaliat
    @RiannahKaliat Месяц назад +36

    Imfa ya chilima mpaka lero ikumandivetsa mutu 😢Rip legend

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r Месяц назад +64

    The problem with Comrade Timothy Mtambo is that He's after Money so He has nothing to do with the development of this Country. He started as an Activist while His aim was to benefit something.

    • @sithandanechirwa6376
      @sithandanechirwa6376 Месяц назад +8

      I also don't trust Timothy but if I overthink about the dearth of SKC makes me think that maybe Timothy lost direction because of the ruling gvnt. His mouth was shut by other elites who takes Malawi to their own hands

    • @HamiltonwaNamuwah
      @HamiltonwaNamuwah Месяц назад +5

      Ndi galu kwabasi ameneyi Timothy Mtambo

    • @MarthaJafali
      @MarthaJafali Месяц назад +3

      Timothy mtambo is a betray cos he was betrayed the who malawians some years ago I really don't like this gu

    • @user-nw6ie3xx8b
      @user-nw6ie3xx8b Месяц назад +2

      I love this brother but dyela

    • @user-zk7jw9up6m
      @user-zk7jw9up6m Месяц назад

      Zikomo mtambo

  • @emmanuelmukondia3568
    @emmanuelmukondia3568 Месяц назад +16

    THE best way is you to prepare yourself with God. So that you are right with God.

    • @jamesgondwe6669
      @jamesgondwe6669 Месяц назад

      God, how many times have we consulted God? How come that God fearless countries are more progressive than Malawi? Do you think we really survive death to claim heaven?

  • @HarlodAndrewbanda-vf2rd
    @HarlodAndrewbanda-vf2rd Месяц назад +11

    We're still crawling to get there!! Rest in peace Dr SKC, UTM is a movement

  • @jogechawa6192
    @jogechawa6192 Месяц назад +7

    For the first time I agree with Mtambo .Sitimayenela kusangalala 6th July. Palibe chikukoma

  • @mishecksipolo7153
    @mishecksipolo7153 Месяц назад +13

    That's too bad,and it's evident kuti chilima anachita kuphedwa,it just needs the youth to clean up this mess

    • @AbelSinoya
      @AbelSinoya Месяц назад +1

      Khala chete God knows ungatenge tsoka😂😂

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 Месяц назад +5

    SKC forever in our hearts 💔🔥 powerful words Comrade Mtambo Osafooka kms Osaopa Dziko ndi lanthu ife kuno Ku Ntcheu tili mbali yanu...

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx Месяц назад +12

    Mtambo thanks for the vital words.
    We now needs actions against these idiots in the government

    • @rexphiri6951
      @rexphiri6951 Месяц назад +1

      powerful words Mr Mtambo

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 Месяц назад

      Only stupid people with commend the selfish and greedy Timothy Mtambo

  • @EdoJohn46
    @EdoJohn46 Месяц назад +17

    Antambo 😂😂😂 ndikukutengeni ngati ndinu amene mudasongezera dzikuni dzamoto kuti tipse Malawi muno ndiwe galu kwabasi

    • @ThomasShuga
      @ThomasShuga Месяц назад

      Very true 😢😢

    • @MatiasMbaula
      @MatiasMbaula Месяц назад

      Very true

    • @MaggieCement
      @MaggieCement Месяц назад

      Ndipo Inu alibe umuthu uyu za ziiii mesa iye emweyi ndiamene anapangitsa kuti tilowe mudima akuonapanowo galu zedi

    • @wakisamsukwa9918
      @wakisamsukwa9918 Месяц назад

      No matter how long you have gone the wrong road, turn back.
      Turning back isn't an offence

  • @JohnSingano-f1p
    @JohnSingano-f1p Месяц назад +2

    The voice of a lion always brings confusions

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Месяц назад +10

    Amtambo...ngat mukufuna kut ife tikukhululukireni ...pitani ku mademo mutibwenzere dziko lathu...anthu akuopa mademo chifukwa alibe support...mabungwe onse chakwera adasiya abale ake mmaudindo

    • @LOKAMJ
      @LOKAMJ Месяц назад

      Exactly

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 Месяц назад +1

      DPP could have finished us . He did the right thing to rescue some of us from DPP. It was oppressing us

    • @InnocentMmanga
      @InnocentMmanga Месяц назад

      😂😂😂

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Месяц назад +1

      @@ancientnkhata1137 oooooh ...May the curse of Almighty befall who is a lier...and make them the wood of hell fire

    • @ShabaniKuswere
      @ShabaniKuswere Месяц назад

      ​@@ancientnkhata1137aaa chimakhala chilichani, ufiti kapena??? Iwe ukundiuza Kuti mmene zinalili nthawi imeneija DPP ikulamulira ndipano bola Pati??? Oppression yake iti tiuzeni yomwe ikuposa panopa????

  • @user-ub1mw7ce5p
    @user-ub1mw7ce5p Месяц назад +4

    Well spoken, comrade Mtambo.

    • @KondananiNjakwa
      @KondananiNjakwa Месяц назад +1

      He has missed the trail. Uyu watha. Ndipo akamati ngati wina amawona ngati wayimisa agenda, atanthawuza kuti munthu wina anachita kuphedwa? Kulankhula kopanda nzeru

    • @KondananiNjakwa
      @KondananiNjakwa Месяц назад

      Nanga munthu angati anyamata oganiza bwino akumanena wena Lwarwa aaaah guys Mtambo anaganiza bwanji?

  • @user-zf9xs3zj9b
    @user-zf9xs3zj9b Месяц назад +4

    Wakuba mtambo akutiona ngati amalawi ndife galu anthu mwa sandutsa ndale ndi maliro a Dr saulos chilima 😂😂😂

  • @user-ro1pl7rv7z
    @user-ro1pl7rv7z Месяц назад +1

    Sometimes I wish Bakili Muluzi to come back again....
    Ligongo apano indu yayi itupile Draft kwabasi. 😅😅 Yangajenda Ata panondi

  • @user-te4ii6sz2v
    @user-te4ii6sz2v Месяц назад +5

    We quote more political speeches than prayers. This was not a political rally

    • @JosephHill-fy1bb
      @JosephHill-fy1bb Месяц назад

      Ntambo is not a pastor.... Just watch pastor's preaching time...

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 Месяц назад

    Well spoken comrade mtambo criticism singalephere as Malawian we were born like that, keep it up comrade

  • @YohanePatrick-lc2lq
    @YohanePatrick-lc2lq Месяц назад +4

    Man ife amalawi tikufuna dpp enawa abodza ngati iweyo Timothy anakuchosa ku mcp chifukwa cha katangale

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj Месяц назад +5

    Mtanbo akuyakhula za ndale zikugwilizana bwanji ndi mwambowu

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 Месяц назад +9

    Ndikakumbukila ifa yaathu amenewa mtima umawawa

  • @user-bq5ev7de1l
    @user-bq5ev7de1l Месяц назад +4

    Apm my vote ✊

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Месяц назад +9

    More fire mtambo chakwera machende ako😂

  • @dhaoudhiabedinegomaseko2363
    @dhaoudhiabedinegomaseko2363 Месяц назад +1

    Mtambo mseu wa Rumphi Nyika Chitipa munawukana mesa munkaguba nkumaphwanya zinthu kuti musinthe utsogoleri

  • @emmanuelmukondia3568
    @emmanuelmukondia3568 Месяц назад +11

    Idol worship

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Месяц назад +3

    That's true they is nothing to celebrate 60 years, it's like we help chakwera, kumkuyu ndi zikhale ng'oma kudya mitsonkho yanthu. Ayi momwemo 😂

  • @AndrewLanken-v3u
    @AndrewLanken-v3u Месяц назад +1

    He has got nothing to give malawians never

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf Месяц назад +8

    mtambo walankhula za mzeru kuposa namachende chakwera

  • @surgeon1621
    @surgeon1621 Месяц назад

    Malawi has become a very sad country. Everyone is just fighting for their own stomach. A person like Mtambo shouldnt be applauded like that as if he wasnt a minister in this government. What achievement can he show malawians to prove he is a better man for malawians. A lot of people want to use Chilimas death to gain points for themselves and yet they have no substance themselves. Too much sentimentalism without constructive knowledge

  • @ConfidenceBanda-g8k
    @ConfidenceBanda-g8k Месяц назад +4

    Koma ndipo poletsa kupepherapo ndie nduchitsiludi,mobwereza amene amaletsa kupepherayo nchitsiru

  • @EdwinMakwangwala
    @EdwinMakwangwala Месяц назад +1

    Only God is our rest not this politicians. God help Malawi

  • @user-nb2uf5rp7j
    @user-nb2uf5rp7j Месяц назад +1

    Mtambo you can't be the President of Malawi....

  • @DannielOnions-fy3dc
    @DannielOnions-fy3dc Месяц назад

    Thanks so much 🙏 keep it up please we need people like 👍 u

  • @ChiletsoChembe
    @ChiletsoChembe Месяц назад +1

    Amalawi please! Let's pray to God forgive us and punish those who mudder saulos chilima

  • @RitaKainga
    @RitaKainga Месяц назад

    Zikomo Inu nonse amene mwalimbabe mtima kupanga mwambo uwu though asatana akutchinga,Mulungu wathu ndwabwino,sanalepherepo,imfa iyi ndyovuta kuiiwala

  • @LulezLele
    @LulezLele Месяц назад +2

    Kapolo uyu guyz akulubwa chani, mesa udapanganso ufitiwo at dat time kape

  • @WisdomMaseko-fi5sv
    @WisdomMaseko-fi5sv Месяц назад +9

    Koma tizikukhulupirirani ndithu a Timothy???

    • @DeliaKaduya
      @DeliaKaduya Месяц назад

      My question too 😢😢

  • @arthurmanyozo1289
    @arthurmanyozo1289 Месяц назад +2

    Give your life to Jesus.The owner of your soul is Jesus

  • @SakanjiraRose
    @SakanjiraRose Месяц назад +1

    I'm getting confused, he is the man who mobilized people to fight a government that was to me far much better than the this one he helped to form.

  • @SteveKumwenda-t3d
    @SteveKumwenda-t3d Месяц назад +2

    Chitsiru ichi, ndiponso uku sikumapemphero

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 Месяц назад +2

    A ndale ndabodza kumene. Ndi chifukwa chake olo akuba ndalama zambiri-mbiri akavala amangokhala ngati avala chithumba chaku chigayo

  • @jonathanmalanda7742
    @jonathanmalanda7742 Месяц назад +1

    A Mtambo ikani za mapemphero kuti mzimu wa skc uuse mumtendere

  • @LloydLuwis
    @LloydLuwis Месяц назад +4

    Keep morefire mr tman

  • @LunnahMtambo
    @LunnahMtambo Месяц назад

    More fire bro ,love from ccter namtambo cp

  • @kamangamathias2001
    @kamangamathias2001 Месяц назад +2

    What's the reason of kuwaletsa anthu ku phiri. Kiphiri kuli chani?

  • @TnmMpamba
    @TnmMpamba Месяц назад +1

    Watching live from Salima, Khombedza

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 Месяц назад +2

    LUWALA ANGASINTHE CHANI MBAVA YA MNTHU

  • @AbdulKhan-j2h
    @AbdulKhan-j2h Месяц назад +1

    Mpava iyi atidye bawo bwanji Sumatuluka uli nduna pano abakuchosa ukufuna kodwela amalawi timaiwala

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi Месяц назад +1

    Antambo vuto chinthu chimozi mumafuna ndalama Chonde muzikhala ngati Born Kalindo chifukwa amati pavute pasavute asayimira amalawi ndipo akuti imila amangidwa amangidwanso pomwe enanu mumatifuna pomwe zakuvutani tikukukuwerenganitu INEYO NDIKUCHALENJA zoti wina aliyese aime payekha kuyambira Apita. Tupele. Raz. Nankhumwa. Shahana. Osati Chakwera Amayi Joyce banda ndi phulezdent Kalindo. Ndiye tikavote masankho mawa mwachilungamo mopanda kubela angawine ndi Kalindo chifukwa ndi amene akuoneka kuti angatithandize osati Ena inu 😁😁😁😁😁😁😁😁😁

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 Месяц назад

      Inuyo

    • @user-ww4ei5fb7d
      @user-ww4ei5fb7d Месяц назад

      Kalindo ndiolimba mtima, ofunika kumuvotera. 😂

    • @JohnAsendi
      @JohnAsendi Месяц назад

      @@user-ww4ei5fb7d zoonadi sister osati enawa akuoneka ngati akuti konda koma mmitima mulibe chikondi

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 Месяц назад +1

    Osaoopa ai......ku Malawi kulibe president

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso Месяц назад +1

    Ndipo ngati chilima anachita kuphedwa ndi anthu adzakhala osowa ntendere mpaka Ndipo ngati mizimu imakantha yakanthe anthu amenewa

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws Месяц назад +2

    Vote yanga yikupita kwa afford

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Месяц назад +1

    Akulesa bwanji ma pephelo akuopa chani tiyeni nazo pephelo ndi chida

  • @MagretIdimu-u7w
    @MagretIdimu-u7w Месяц назад

    We're heart broken 💔 SKC still remains in our hearts 😢😢😢

  • @PianoChimpeni
    @PianoChimpeni Месяц назад

    Kodi iye adali nduna adapangapo chani pa unduna wakewo vuto mukumayankhula ndale pa Malo poti tikukumbukira malemu SKC may his soul rest in internal peace

  • @JosephJosab
    @JosephJosab Месяц назад +4

    Mtambo ndi kape

  • @AustinBornface
    @AustinBornface Месяц назад +1

    Malawi timakhala ngati tili pa stage tupanga drama kma ayi ndithu ndi action

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 Месяц назад

    Shame on you MCP kuwalesa amupingo Kuti asamapange mapemphelo Pali tu Pali thekenya Pali biiii Pali minga

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x Месяц назад +16

    APM my vote ❤❤❤❤

    • @user-zc4zb6gf9u
      @user-zc4zb6gf9u Месяц назад +1

      Kagwere uko ndi APM wakoyo.atithandiza chani?

    • @EllahChikwatu
      @EllahChikwatu Месяц назад

      Apm my vote kumene ​@@user-zc4zb6gf9u

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x Месяц назад

      @@user-zc4zb6gf9u APM for ever ♥️♥️

    • @spargomw
      @spargomw Месяц назад +1

      200% Peter my vote❤❤❤

    • @LOKAMJ
      @LOKAMJ Месяц назад

      Hahaha yabaya tu,,, ​@@user-zc4zb6gf9u

  • @user-oc8nj3or6y
    @user-oc8nj3or6y Месяц назад

    But we needs people who can at least change something in this country 😢😢apart from this government that we have now😢😢

  • @MorrisMapiri-d6z
    @MorrisMapiri-d6z Месяц назад

    It's not over until it's over. We shall shut up when we will be satisfied.

  • @user-ev3hl4hv4e
    @user-ev3hl4hv4e Месяц назад +1

    Akutitu ndi afana osata ngini mwana wapa Chitipa .moooooo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @SaeedHurzrut
    @SaeedHurzrut Месяц назад

    chilima wakuba ngati amwalira sangakhale wabwino Ife tonse tikuziwa zimenezo aphana pa gwilozano wawo

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 Месяц назад

    Exactly Andale akale achoke boma achinyamata alamulire dziko nkhalamba ndi mfiti komaso ndiankhaza

  • @ChilangoNdalama
    @ChilangoNdalama Месяц назад +2

    Big mtambo timakunyadiran

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Месяц назад

    Good Messnge Mr Mutambo

  • @yowasschitsosa5348
    @yowasschitsosa5348 Месяц назад +6

    A chitsilu a mtambo iwo ali after ndalama basi,

    • @chesterphiri7523
      @chesterphiri7523 Месяц назад

      In politics everyone is after money.
      There is none and absolutely nobody who is there to serve the people.

    • @user-fz3gu2ez1o
      @user-fz3gu2ez1o Месяц назад

      Ayitu...mukadzacheza naye you will understand better...

    • @wizmalota2438
      @wizmalota2438 Месяц назад

      Achitsiru ndambuyako garu iwe

    • @yowasschitsosa5348
      @yowasschitsosa5348 Месяц назад

      Mukuona ngat anthu muwapusitsaso, mumapanga busness m'dzina la ma demo achitsilu a mtambo alibe zochita awa

  • @LimbikaniMakwandu
    @LimbikaniMakwandu Месяц назад

    Only chilima not you mtambo RIP CHILIMA

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 Месяц назад +1

    Dziko la Malawi likuyenda cham'mbuyo

  • @VincentAndrew-jz2gf
    @VincentAndrew-jz2gf Месяц назад +1

    Atambo ,Ulibe Zelu unaphetsa Athu Ambili

  • @user-wz1or9ud9i
    @user-wz1or9ud9i Месяц назад

    Mzimu wa chilima awasowetse mtendere anthuwa mpaka anfe amene anapha chilima.

  • @Anordchatha
    @Anordchatha Месяц назад +1

    Apm my vote

  • @YahayaUndiya
    @YahayaUndiya Месяц назад +1

    Mpira amauona ndi akunja big bolani osaiwala zimene mukuyankhulazi antambo

  • @YasinAmidu-b7b
    @YasinAmidu-b7b Месяц назад

    The problem with us is that we are the ones that took evil to lead us

  • @markjames-v1f
    @markjames-v1f Месяц назад

    Chomwe mkukanikila kutiyimilira ndichan boss wanga

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 Месяц назад +1

    Nanunsotu mukutichitsa manyazi, 60 eyes ndekuti chani?

  • @Josehimba
    @Josehimba Месяц назад

    More fire comrade

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 Месяц назад +1

    Mzimu wachilima is moving

  • @limbanikamanga7514
    @limbanikamanga7514 Месяц назад

    A Minister of National Unity aja

  • @taombeedward5026
    @taombeedward5026 Месяц назад +1

    The biggest problem mtamboyu

  • @WiscotDzombe
    @WiscotDzombe Месяц назад

    Uku ngat kunari kumapemphelo ngat uyu anari compain amtambowatu safuna Bata Malawi koma kusokoneza

  • @AminaDaudi-jk9tb
    @AminaDaudi-jk9tb Месяц назад +1

    Comrade he is true son and patriotic

  • @PeterThomas-lw3io
    @PeterThomas-lw3io Месяц назад

    Rest in peace 🕊️ chilima anagwira chito yaikulu DPP mu
    2014 ikanafela giya komano chilima anapanga zotheka kuti Peter akhale tsogoleri muchomwechotso mu 2020 wayigwira ntchito yathangata kumuyika Crazy Chakwera akulamulila koma njilu ndikupanga mission plane yakumupha yooohhh Chakwera ngoyipa

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q Месяц назад +1

    Mtambo is fighting for injustice we need a president from north enough is enough Malawi is for all even from north.

  • @user-qs2tx7wt6g
    @user-qs2tx7wt6g Месяц назад

    Achinyamata ake ati angavele iweyo pathako Pako iweyo unakakhala wa mzelu unakakana undunaaa

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso Месяц назад

    Mtambo mtima wake ndi wadyera mmene wachoka ku MCP akufuna apeze not adzidyera kudzera kwachihanna ndiye in leronso asabwere ndimabodza ake ofuna podyera watipwetekesa ngati dzikoli Lili pamoto nfichifukwa Cha iyeyu ndi galu kwabasi

  • @GibsonBakha
    @GibsonBakha Месяц назад

    Andale inu musamatiwawitsemutu muma gofuna ndalama agalu inu

  • @WilliamTemboh
    @WilliamTemboh Месяц назад +2

    Km tkukhulupilileniso amtambo kapena mukufuna tindalama plz tell me coz munatpweteketsa

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Месяц назад

      Apitenso pansewu atibwenzere dziko lathu...ndiyemweyu adatipereka

    • @DeliaKaduya
      @DeliaKaduya Месяц назад +1

      Ndipo ndi yemweyu analisiya dziko ku anthu otamba akewa, apa angotibwenzerapo dziko lathu lakale lomwelija

  • @user-ie5pc4ox8i
    @user-ie5pc4ox8i Месяц назад

    Ada awawa bwenz Ali MUNTHU wapamwamba kwambir kma Anapanga zausiru ngat akufuna timukhulukire ayambise mademo

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 Месяц назад

    Politics will never transform Malawi. I suggest,all party presidents,some traditional and religious leaders should jointly accost the H E and matters of philanthropy and patriotism concerning current national teasers.Neither invective nor censure wll bring democratic solidarity in our beloved nation.There is need for deliberation with the HE and his Vice President.Avoid self centredness,power hunger, political chauvinism and cupidity.We are no longer ease!

  • @AllanaChiphazi
    @AllanaChiphazi Месяц назад

    A Mntambo akunena zimenezi chifukwa anawachotsa pa Unduna awa, anali m'boma momo palibe chimene anachita hiyaaa

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso Месяц назад

    Imfa yachilima ine sinfidzaiwala mpaka pano ndikulirabe ngati kuti anali bambo wanga amene anabereka ine koma sichoncho Ndipo mzimu wachilima ukuyendayendabe pakati pathu mzimu wachilima ambuye muulandire kumpando wanu wakumparadise

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 Месяц назад

    Amtambo naye ine ndinakhumudwa naye ndipo ndinataya chikhulupiriro mwaino mwatulukirano nthawi yonseyi munali momwemotu mu Timbaland wakudayo ndiye pano mukutinamizaso chani apaa iyaaa😊

  • @WilliamChopika
    @WilliamChopika Месяц назад

    God is our side nthawi zonse

  • @YamikanAbubakary-my4ie
    @YamikanAbubakary-my4ie Месяц назад

    Bvuto ife a Malawi timangokhutila ndi mau opunsa ngati amenewa
    A Tambo panyipano mwamva chifukwa iweyo namene unapangitsa kuti a chakwera alowe m'boma mu 2020
    Koma atangoti akuchotsani unduna nayamba kulubwa lubwa
    tsopano ukufuna ku watengela kuti a Malawi garu iwe 😂😂😂😂 sadzakupatsaso unduna ukhaulla
    Ndiwe garu kwabas wamva kkkk
    Pali anthu awilli
    Oyamba iweyo wachiwilli ndi Born kalindo amafuna so unduna kwambili km bvuto nthawi yanu yokhala PA unduna sinafike
    M-C-P 2025🔥🔥🔥🔥🔥100%🇲🇼✍️😂😂😂😂

  • @stevenchirwa5028
    @stevenchirwa5028 Месяц назад

    Unatinamiza ndiwe tuu kut MCP 2019

  • @LunnahMtambo
    @LunnahMtambo Месяц назад

    Osamulekerera chakwera angazolowere ,ndipo keep the fire burning ,osatopa ,osaopa

  • @georgenundwe
    @georgenundwe Месяц назад

    Why do we choose kusadziwa pamene everybody knows pretty well kut kuli global crisis ya economy.....and one expects milakuli that we do best than the lest ....lets.be the champion of telling Malawians the.truth

  • @ChancyJere-pz5sv
    @ChancyJere-pz5sv Месяц назад

    Choyamba Malawi uyu ndiwanthu osaopa osa fowoka kulibeso Malawi wina sitikukuopani mwava MCP machende anu mwava

  • @nafejonga972
    @nafejonga972 Месяц назад

    Rest in peace, my president .. we are still fighting

  • @josephmsyali
    @josephmsyali Месяц назад

    Mtambo is the man