Apolisi, ngati munali musanafufuze za mulandu wa a Kaliyati nde mmamumangilangi, Patu mwamulakwira chiire, coz it's already more that 48 hours now, Malawi Why? Our police, why,
Ndiye akanapanga Kaye kafukfuku kenaka ndikumanga munthu because her rights are also violated as we know kuti anayenera kukawonekela ku Court pasanathe 24hrs.
Muyamike kuti mulungu anasiya kuulula kwa aneneri ngati ngati kale mukanaona inu, kafunseni mfumu David inapha uriya muhithi pomuika pa malo pathina nkhondo kenako anaona ngati plot yatheka koma mulungu anamuuza zonse anapanga, themberero kwa oyandikana ndi oipayo mwazi wa chilima
Manganya Chakwera ndi nduna zake athu awa ndiakhaza chifukwa cha ndale kumumanga muthu basi koma thawi ndi nyengo ikubwera pompano musamatenge ngati dziko ndi rakwanu nonse a mcp thawi ndi nyengo ikubwera Osaopa osatopa osafooka Allah alipo
Which one is which ?investigation before or after arrest? Mukuwuzana a mcp nokhanokha or the Nation ,that communication is useless,trying to fool Malawians
Zacbibwana, why arresting someone without finalizing type of case committed. Zanuzo musatiuze our parents used to tell us that MCP ndi yankhanza koma kusamva kwathu.
A chakwera musaduse mbali mesa ku state House koko, asanavuvuzidwe za ngozi ya ndege chakwera ayankhe yemwe anamuuza kuti ndege inafika ku mzuzu ndipo anaibweza ndani, anamuuza chakwera kuti inaomba Phiri ndiyani, kenako mkulu wa asilikali anamuuza kuti ndege sinafike ku mzuzu ndani ndipo inagwera kuwilira moti asilikali sanakafike, Mr mkukuyu Black box la munatiuza kuti mwalisunga liri kuti nankha lipoti la ku Germany akuti munalibe Black box, pali wamkulu Ali ku mwamba akuona zonse ndipo akuyalusani, thanks bakili muluzi popanga kafukufuku wa a China gadama ndi ma friends ake inalibe chinyengo ndipo Malawi anakhutira, Zikomo Joyce banda pa kafukufuku wa malemu bingu a libe chinyengo koma izi ai sipazakhalabe chilungamo, choona chitadziwika chakwera ndi mcp members akazatuluka boma
Mozadusa mmbali chakwera ndi Big suspect ndipo anamupha chilima ndipo mwini wake chilima Ali ndi umboni
Ananenatu Kalindo Antanyiwa kuti Athu Ambili amangidwa mix Akaliyati chakwela angofuna kuphimba khani yandege iye ndiamene ana pha chilima
That's indeed good idea I support it
Apolisi, ngati munali musanafufuze za mulandu wa a Kaliyati nde mmamumangilangi, Patu mwamulakwira chiire, coz it's already more that 48 hours now, Malawi Why? Our police, why,
Mcp ndiyakupha yankhanza si chipani chakuti mpaka kumachisekelera fokof
Kuti aphedwe Chilima adatsekula khomo kuti akuphawo abwere munyumbamo ndi Manganya bambo a sikono koma thawi yamuthela
Mapwalaakeameameneyo
Am Pastor Yona ,its good to live the political party members out in team because it must be neutral
Ndiye akanapanga Kaye kafukfuku kenaka ndikumanga munthu because her rights are also violated as we know kuti anayenera kukawonekela ku Court pasanathe 24hrs.
Munthu akamumanga pamafunika anene chomwe alakwa nde azikhara asoziwa chomwe alakwa😢😢😢😢
Asalemelapakati
Chifukwa chiani a police amatamangila kumanga munthu asanafufuze zomwe munthu wapalamula.? Malawi yikuluza ndalama zambiri za boma, for nothing. Zitsilu!
Ubulutu
Muthu anapha munthu nzake ndi futi koma osamangidwa koma akunanga munthu oganizilidwa kuti amafuna apalamule, no sense
Sizithauza kathu zimenezo ayakhula akubaj
What kind of the case is this? Arresting some then investigating?
Kaya mwina malamulo adziko anasintha mmmmhu
Komano ndikanandano kuti mnyamata wapatawa ya MTN uja akumane Naya akamapanga kafukufuku coz zikuoneka kuti iyeyo ndi eye witness
Akuyenera akhaulisidwe pakafukufuku wadege chifukwa akudziwapo kanthu
Chakwela sindinafune kutulutsa mau awa, panyini pamkazi munthu oipa kwambiri iwe.
Aku banja a kwa Chilima akhalepo pa zakafukufuku.
Mcp mukungotayapo mavoti apa, yachikangawa siinathe mwayambanso iyi?
Kalaya ndi chakwera mapwala anu nonse
Mmm zchisoni chipani chooipa zedii
Mbole zanu a police a mcp ndi president wanuyo chakwela
Km zoona mutasowa zochita kumugwila zimai kumakamuzuza Ku ndende mulandu musanaupeze zoona mmmmm mudziwe yesu ndiophuzila ake
Ndikanakonda mukomitiyi mukhale munthu umozi wa kubanja popanga kafukufukuyo
Achakwela amwalali😂😂
Akutanthauza chan ma pioneers a chakwera wa, si apolisi a ife amalawi koma ndia chakwera.
Muyamike kuti mulungu anasiya kuulula kwa aneneri ngati ngati kale mukanaona inu, kafunseni mfumu David inapha uriya muhithi pomuika pa malo pathina nkhondo kenako anaona ngati plot yatheka koma mulungu anamuuza zonse anapanga, themberero kwa oyandikana ndi oipayo mwazi wa chilima
Amen
No sense, an professional mcp police why can't you arrest chakwera who killed 9 people including vice president.
Mulando waboodza ,kubvutitsa basi.Police ypo manga munthu pali be umboni wa mulandu,Mulungu akulsngeni kubviutitsava opposition,nrhawo yanu izafika.
Umbuni sungapezeke pokhapokh a independent
Akupha awa MCP kwathandidza kulowa boma mistake ya UTM
I COULD BE HAPPY IF ONE FAMILY MEMBER WAS INCLUDED IN THIS COMMISSION OF INQUIRY, EVEN ONE MEMBER OF uUTM
Apolice mukanangosiya kupemphera kumwamba chanu kulibe mwatanganidwa ndi za dziko
Ndipo live
This is not independent body in Malawi.
Mcp ndichipani chomvetsa kwambiri
Tawelengani chichewa ife zikukanika kuno 😢😢😢
Pakhalabwaji chilukgano pamene mugulumo mulioipaokhaokha
Akalaya machende anu chomwe mumuzuzira kaliat nchani
Angosankhana okhaokha a mcp bwanji osatengako akubanja pali chinyengo apa
Kodi mukamangobwereza bwereza , adzuka , ? Poti aliyese Ali ndi ifa yake ,
Kodi a police amadziwa malamulo pa ufulu wamunthu?Kapena akuyendela malamulo akamunzu.?
aaaaa agulu akupa inu apolice anthu osachita bwino
Koma ndale zaku malawiiiii
Komatu mukuzichotsera ma vote ok tieni Nazo Ngati Ndinu ma Doro osathesa mavuto tirinawo mziko Muno
Zoona nkhuni ina ija ya aromwe amati usi ndiwakupha ndiwakuphadi 😢😢😢😢😢😢😢😢
Yes it suppose to be like that akanema nawo azikajambura live
chonde a Peter chimalaya musamugwirire mzimayiyo kumeneko a Peter chimalaya
Why not to put his wife so that she can have some pictures
Amaiwala kuti kunali anzawo kunjaku alikuti?kuchita kulitenga dziko ngati lambuyawo.
Police State!!!! Ikadakhala mbewu,tikanakazinga yonse kuti ana athu mbewu imeneyi asazaioneso,coz it's not Police service
Exactly
Simon nyasulu rumphi tifunan tiziwe ife
Akubanja palibe bwanji?
Mbuzi zawanthu inu apolisi
Kodi madokotala aku central aja anawawuza chani akubanjawo
Iwe chakwela tamutuluseni dzimaiyo bwanji kodi chamba eti
Zazi ndale zaumbuli 😂😂😂😂
Manganya
Chakwera ndi nduna zake athu awa ndiakhaza chifukwa cha ndale kumumanga muthu basi koma thawi ndi nyengo ikubwera pompano musamatenge ngati dziko ndi rakwanu nonse a mcp thawi ndi nyengo ikubwera
Osaopa osatopa osafooka Allah alipo
Plan yamanganya iyi mothandizidwa ndi chikangawa
Tili pompano ndipo tidzaonana
Which one is which ?investigation before or after arrest? Mukuwuzana a mcp nokhanokha or the Nation ,that communication is useless,trying to fool Malawians
I a good idea azijambula chilichomnse zithandiza kuulura choonadi
Ine,kanakonda wakubanja mozi akhalemo mukomitiyo
Ambuye, musamayankhule ngati mkazi kapena ngati ndinu mwana, these guys arrested her without evidence hence just wanted to punish her...
Zacbibwana, why arresting someone without finalizing type of case committed. Zanuzo musatiuze our parents used to tell us that MCP ndi yankhanza koma kusamva kwathu.
Namia ndiufulu wanu msapiteko ntchito yomenyera ufulu yikukwanila kokalumbira mukadyako chibazi
Panyapanu inu musiyeni kaliyatiyo
Koma police yaku Lilongwe yachukatu pita chimalaya ndianzake umbuli ulipo
Ngati sanapalamule amafuna kupalamula nde mwamumangila kut amafuna apalamule? That is nonsense
Kodi wandale akalakwa asamamangidwe? Kwachuluka ma saveg
3day without charges malawi police useless
Wathuyo akangodwala olo kungodula moyo wake muzatimva
A chakwera musaduse mbali mesa ku state House koko, asanavuvuzidwe za ngozi ya ndege chakwera ayankhe yemwe anamuuza kuti ndege inafika ku mzuzu ndipo anaibweza ndani, anamuuza chakwera kuti inaomba Phiri ndiyani, kenako mkulu wa asilikali anamuuza kuti ndege sinafike ku mzuzu ndani ndipo inagwera kuwilira moti asilikali sanakafike, Mr mkukuyu Black box la munatiuza kuti mwalisunga liri kuti nankha lipoti la ku Germany akuti munalibe Black box, pali wamkulu Ali ku mwamba akuona zonse ndipo akuyalusani, thanks bakili muluzi popanga kafukufuku wa a China gadama ndi ma friends ake inalibe chinyengo ndipo Malawi anakhutira, Zikomo Joyce banda pa kafukufuku wa malemu bingu a libe chinyengo koma izi ai sipazakhalabe chilungamo, choona chitadziwika chakwera ndi mcp members akazatuluka boma
Ndale it's a dirty game.
wishing u (Akweni) all the best
Davil is a liar!!
Poor government
Aaaaa kma ndipo kwanukhaditu
Koma ine sindipeza Iwo ngat orakwa pazimene arankhurapozi
zoona yudasi usi osalankhulapo kanthu
Aboma akakamizika ndiye mzovuta kuwa va
Zauchiziru
Ndichifukwa chani anamanga mayi patrisha kaliati akuziwa kuti kafukufuku wa ndege akhalanso akuchitika konseku ndikubvunganyiza
Akweni atuluke akapange mavoti awo
Sakufuna kuti amayiwa akapikisane nawo pa convention ya utm
Kma ndye bora iri ndronukha bwanj
Olo mumusunge mpaka kufa kwanu, kuti mutchuke.
Mfumu inailiyose imasapota president
Aaaa ndale dzabodza idzi
Dziko linoo linamvuta ndinthu
Mulandu ulipo tidikire court Monday
A Limpompo Bakili Muluzi TV ananena musatiputsise
Monday Ndikuti ndizaboza mukupekela milandu yaboza
Ndale si tipangila maliro
Vuto longothamangira kumanga munthu pasanapezeke umboni weniweni munthu asanamangidwe
Mwamuzumza munthu wa mai kulakwa
Zomwe akunena avarerazo tagwirazana nazo zikhara pa air
Samalani ndi namiwa sikukbwela chilungamo uku
Hmmmmmm bt why guys
😢😢😢😢
Its so sad
Zufuna pajatu akweni amamutamandila chikangawa ndiye lelo asamadandawule
Police ndinchito Yao yomanga anthu ngat kaliyat musamutae ameneyo galu wamunthu
Malawi wanunkha uyu