Koma chakwera aziziwa kt paziko pano palibe chosantha kubera chisankho sizitheka chifukwa tamuonerera kale asayese sitikuona panopo tekinolenji Ili palipose zimene akupangazo ndiziro pa 10 watching from Mozambique never give up bg brother timakunyadirani kwambir potiwululira zisisi zambavazi
We have been waiting for this very much we can now listening Dziko rilamulidwa with incompetent people Only Jesus Christ superstar will control with no corrupt thinking about.
Koma kukacha kumangodandaula chakwela Kodi iyeu wapambana bwanji mulungu amuone ndithu
Kodi kumuchosa athu akuopa iyeo
Ipondeni fadah ❤❤❤
Our trusted channel bakili TV only we love you big
Koma chakwera aziziwa kt paziko pano palibe chosantha kubera chisankho sizitheka chifukwa tamuonerera kale asayese sitikuona panopo tekinolenji Ili palipose zimene akupangazo ndiziro pa 10 watching from Mozambique never give up bg brother timakunyadirani kwambir potiwululira zisisi zambavazi
Following live from kakata phalombe kwa Nkhulambe. Keep fire burning Bakili muluzi tv
Best TV
Big up brother your number 1
Yalowa ndi misala anthu akumwera, maka maka Alomwe ndi Ayawo.
Umbuli inu
Ayi kungot anatipinda kusintha kwake ndikuononga and wakwanisadi
We love you bakili Muluzi tv channel 🎉❤🎉🎉❤❤
Chaka cha mawa tithyolanapo osati masewera
Ndipo kwambiri nkhondo ilipo yapachiweniwenindithutu😂
King 👑 wanthu mukwana bro mafiru ❤
Best TV ❤❤
Ukukakamira iwe chakwera ukufuna udzitiberabe ndiwe galu kwabas iwe chakwera😢
Zisankho sitizalorayi zoputsa ndipo a MEC akuyenera azakane kugwiritsa ntchito ma ID.
Without ID, how do you know the one voting is a Malawian? You guys are crazy. You think leadership has to be in the south always?
@@tasmania527 so how you vote seen 2004 ?
We back again #bakili muluzi tv mumakwana
Big Inu mumatha ulemu wanu
Best TV 📺
You are no 1 thanks
We have been waiting for this very much we can now listening
Dziko rilamulidwa with incompetent people Only Jesus Christ superstar will control with no corrupt thinking about.
if i were president i could make you my adviser
The biggest Channel ever, MCP out in 2025
Best tv keep it up bro timakunyadirani ulurani zonse
Big man
Timakunyadila man kwambiri ❤❤ ❤
Zoona! TA njewa, Lilongwe zikuchitika.
brother I love to watch bakili muluzi tv I give you five star ❤❤❤
❤
Ulemu wanu big ❤
Following sir
❤❤❤
He change everything as he said indeed but not the way as normal people think, He change other way around.
Izizi ndizoona kwa T/A Nkhongoni ana akulembetsa kuno 12,13,14 years akulembetsa ma ID
Ngat anthu akuzwa kt zikuchitika as Malawians what should we do?
Umakwana nkulu wanga
Mumakwana big
Tops
Dpp my vote
Bakili Muluzi TV ndi more
Wark up malawian
Komatu azitenge bwino kuzangot mcp yawina Ifetu sitizalola ata
Ndipo azakhaula tizapha MCP yonse wait n c
just on social media ,this information is strictly
Ndizawapha tokha akazangoti awina azadziwanso zedi
Exactly chakwera ndi galu kwabasi
Ndipo kwambiri tu mmm
Mmaso anga ndikuona nkhondo after Kulengeza kut Chakwera wawina. Nkhondoi izachitika chifukwa cha dziko kusavomeleza komaso kusakondwa kusankonda chakwerayu. Tipemphere kwambili kut za chinyengozi zisachitike. Dziko lilipamoto kuyambila mbuzi imeneyi inayamba kulamula. Mulungu wakumwamba amene mumalanga munthu wozunza ndiwoononga ndiwosalabada za wanthu. Wakuba wakupha wachinyengo. Chitanayen chakwela ndi onse alipambuyo pake. Daily nkhani ndi chakwela Chakwera Chakwera. 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
God is watching all these mess, soon will map way forward.
Hello Malawi
To hit the nail on the heard chakwela ndi mbuzi yamunthu akuona ngati amalawi sachedwa kuyiwala ngati iyeyo
Umakwana iweyo ❤❤❤
First comment
Muli bhoo man
We have too much people opita kumaula next year big
🙆🙆🙆
Am the first
Tell him truth Kuti zomwe akuchita aMalawi akuona
Ukaidi oyendera basi... Sugar mpaka 6 pin?... Iiiih!
kodi chifukwa chani ku Malawi ID yakwathu yimakhala ndi expired date while ku South Africa or other countries they don't have expired
Bwanji mumalimbani ndi zimenezi?
Ndikuziona izi season yo vota ino
TV iyiyi palibe chomwe ingachote or atalakhula chotani, One President at a time
Ma ID awowo chisankkho chake chikhala chakudambwe komweko
Nxt Yr yense woyambira dzaka 18 azavota bas kay Ali nd ID kapena ayi
Kod kumalawi ine ndizabwela ndi mfutitu ndipo chakwela akufunika la timke nawo bomba basi
Mbambande bakiri muluzi TV
Ndpo live even kwa chadza zikuchitika zimenez 😮
MCP kuwina ndikuti yabela, zithela zigogodo🤜🤛🦻
Inshort , lt Will happen here in MALAWl like happened in congo in 2025
Madela ambili sakulembesa chilungamoi
NAC please please don't try work with politics you will bring war in Malawi next year you will what is goner happened
Timakunyadiran kwambili inuyo a bakili muluzi Tv powatsuka anthu mmaso
Tizangomenyana muno
Tigawana zigawo asiyeni amenewa
Tawauzeni fadah komaso chinja magiya boma lopenga Malawi muno president wanthu ndi nyaupe yeni yeni😅
Musuta chiti Fadar?? 😊
Chakwela ndi mgalatiya without shame
Chakwera mmmm😢😢😢
LA 40 lizafika
Koma olo atagula ma votes wo kwa ana vote ili mmitima mwa anthu akhaula galu ameney
Dziko kuliinonga uku kuyambisa nkhondo
CDM TOUR and TRAVEL 🇲🇼
Inuyo opanga filimuyi muziwelenga Baibulo mofatsa kuti muli munthawi yanji yanyengo tadzifusani kuti Kodi mu asintha president chifukwa chani sichifuwa kunalimavuto kuyambila kale mavuto awa sazasintha mpaka ufumu wamulungu ubwele
Ulemu wanu big
katundu inuyo Bwana 6:34
Iweyo umakwanira bro
Chakwela galu kwabas 😢
Stupid president 🙄
Chakwela ndimuthu opanda chilungamo
Amalawi zofuna iziii
Malawi saibwino
Malawi samamva
Kuzangowina chakwela ndizamutumizila mphambe izamuswe bs
Ndakumbuka zisankho zapitazo. Dela linalake kum'mwela uko. Ankalembetsa ana. Mpaka MP wa DPP anamenya wa MEC. Atakana kulemba ana.
Litchuleni delaro tilidziwe nawo
Koma yaaaa
Your are not serious
BMTV umatha
Tiukhisanamo magazi sua sitizaloraso kuvotera nyasiz
A mcpakuona ngat sitikuona zomwe akupanga
Zisankho izi anthu tidzaphanapo Boma ili liribe chilungamo
Akumatumiza paka gule 😂😂😂
Kkkkkkkkkk 😅😅😅😅 opengadi awa
😂😂😂 Komatu a MCP athamanga misala ndi Peter Muntharika yu
Bakili muluzi ndi moto komanso imafukula zobisika
Nkhondo siyabwino,angokhala kut apulewa samaopa Mulungu,akanakhala ena akanatula pansi mwaulemu udindo
Chitsiru chamunthu .why not now to resign