Olo atapanga zotani palibe amudzutse chilima ndi athu 9 aja , waitaya garu iwe chakwela, garu bolaso garu , koma a malawi tiyeni pasewu uyu achoke abale ,chikutisangalatsa chani kodi anyamata, zoona tiziluza dziko ndikuwawitsidwa ndichakwela ngati iye ndi mulungu zoona
Pa sms yanu ndachedwapo mot sindimaivesa koman ndaivesa ,ndikanayakha zolakwika pomwe inu simunalakwe,yaa izodi ndizoona Malawi anali wa kaka ndi uchi koma pan mmm
Mbambande munyanane osavotela mcp nyasi kwambili 🎉🎉🎉🎉 timakunyadilani kwambili 💪🤝
LOMWE ULI BHOO KWAMBIRI LISTEN FROM NYODOLA SOUTHERN EAST AFRICA
mr president and vice president may God continue to protect and bless you
Panja ndi alamwanu? Ayi zikomo
Patumbo pako mwana wa hule iwe ndi Mr president akoo achikangawao
Yes God should continue bless them so that they can be able to see sufferings of poor malawian voters
Chitsiru china Ichi chokumwa mmadzi ometela ndevu.jb akuti mapwala ako
Olo atapanga zotani palibe amudzutse chilima ndi athu 9 aja , waitaya garu iwe chakwela, garu bolaso garu , koma a malawi tiyeni pasewu uyu achoke abale ,chikutisangalatsa chani kodi anyamata, zoona tiziluza dziko ndikuwawitsidwa ndichakwela ngati iye ndi mulungu zoona
Pa sms yanu ndachedwapo mot sindimaivesa koman ndaivesa ,ndikanayakha zolakwika pomwe inu simunalakwe,yaa izodi ndizoona Malawi anali wa kaka ndi uchi koma pan mmm
Ndipo ndemweyo Mc Cathy anadzamzembetsa nzake Ku South Africa wasatanic nzakei aluthera anthu limodzi😈😈😈😈chikangawa
Kuyipa kwachakwela chikangawa
Yemweyo wabweraso mnyanane tawajonjejonje kapena tawakazingekazinge andalewa😂😂🎉🎉🎉🎉
Uwasambwadze ,mapeto following u i❤❤❤❤❤
DJ this is good man
Following you DJ tinya nawe❤❤❤❤❤❤
Inudi Anya nanu.....🙌
Afa ndi chikumbumtima mr chikangawa
Mumakwana Mr
Ngongole yamagazi tiona zinthu kkkkkk
😂😂😂😂😂 uyu asaka ndithu kkkkkkkkk❤❤❤
Mumakwana man
😂😂😂😂😂😂😂😂
🎉🎉 🎉🎉🎉🎉❤❤❤❤ Rordiny
Ngati eeish ndingatukwane
Kkkkkkk wandibaya MCP ulipo yankhatu akuti mulungu wachitira Dara kugwesa Ndege kuti tione ngati Ndege imavura zovala anthu ... Palibe chisisi ....
Eti tipempherere gozi mukupanga nokha kkkk
Koma lero ndaseka !! Dziko la sataniki ili
Ndipo president uyu chakwela ndi ochimwisa kwambili
Kkkk😂😂😂
Munasowa dj
Iweyo ngati wokhudzidwa wathandizako ndani in your life? Tamusiyeni Ussi, mukungotaya nthawi Achimwene
Amenewa a MCP azayakha afune asafune pangatalike Chilango chilipo ndinthu
Too bad for that
❤❤❤❤💪💪💪💪💪💪💪💪💪💪
Niwolose mkakutafune party rest in peace SKS
Mr chikangawa akwawonesa anthu kwiyo kwambiri
Tukwana ase palibe vuto covid 19 ndiyonama imeneyija achibare nonse ndimbari imozi ya satanic imeneyija
Mcp ndiyokupha yasakho next year palibeso kulamura mcp chikangawa imeneija
Afiti aanthu amenewo.anthu osaganiza za amzawo
😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Komaso shabulika anapindika kale pano zachipembezo akumalowesa ndale nde asakhe chimozi ndale kapena zachipembezo
Dikila Madzi adutse you gonna see
Pepani
mutu wankhani ndi otani
Anakamutenga mzake wa satanic ki South Africa
MANGANYA ZIKUBWERA UDZALAKA LAKA KULOWA LANYERERE TINTEDI WAKOYO SUDZAKUMBUKILA KUVALA DIKILA
Kuyipa kwachakwela chikangawa