Mukaona munthu akuti MCP my vote ameneyo ndi wa family ya chakwera mwina ndi ankolo ake kapena chakwera anakwatira pakwawo which means phindu la chakwera akuliwona ameneyo wachita zolozeka kwawoko
Skc ankafuna kutchoka after kusalemekdza mgwirizano omwe unalipo ndiyeno kutchoka it's a good move komano to agree with ndikutenga mnthu kunja that's wrong indeed
Yea that's very true and I see it ku utm utsogoleri unali wa chilima ena onsewa mavuto bola ku MCP komweko mudziwa bwanji mwina the death of chilima was planned with those who are on top blaming MCP for the death yets amafuna mpando wachilimawo why so early kutuluka mugwilizana without solid proof that is MCP guilty , ine unless pa social media muzabwerese real proof how you saw the killing happen that's when I will find them guilty
Nduna zomwe zikugawa ndalamazo akumatibera misonkho yathu yomweyi...ifetu maso athu tikuona ndipo tilankhula chaka cha m'ma chino....40million plus just for one meeting business yanji imene akupanga? Apapa zaonekeratu kuti andale amatibera pomwe anthu akufa ndi njala. Ambuye akukuonani ndithu
Mukaona munthu akuti MCP my vote ameneyo ndi wa family ya chakwera mwina ndi ankolo ake kapena chakwera anakwatira pakwawo which means phindu la chakwera akuliwona ameneyo wachita zolozeka kwawoko
Very wrong decision,the end of utm.chilima was the only leader with great vision and calmness, you can't make decision out of anger.
Kabambe afunampando ku utm koma autm samalanaeni mtsogoleli wanu autm sankhani kaliati ndiponso pamasankho adzawina anthu tilinae ndichikhupililo enawa tawaesa akanika
Ku utm kulibe mphungwe mpungwe
Winayo chipani chake ndi odya zake alibe mulandu
Nkhani ndiyomweyo mwamva bwino zikomo kwambiri pamibawa.. God bless you two guys... Mamakutu wava koma wopanda makutu mawa wazakuwawani
Anapha dala chilima cholinga anthu abalalike koma mulungu ndiwadongosolo a utm osafooka osatopa osaopa
Bakili Muluzi tv ndi katundu
Apa a UTM Mukapanda kumva zanu izo
Uku nde kuyankhula kopanga umodzi that's y ndimakukondani amibawa chifukwa mumayankhula chilungamo
vuto inu akulu mukukocha ndale mwachidule nanu mulikuseli kwa enaake
Khondo Yochita kutiponyera Mcp kumupanga usi
LET HIM BE THERE WILL MAKE CONVENTION SOON
Dpp moto❤❤❤
Aaa manganya ngati mutu mwake dziyendamo bwino ayi musiyeni ku MCP koko afela nayo limodzi
Yalakwa UTM kuchoka msanga ....awonesa umbuli kwambili
Ndipo usavage wa athu ophunzira umakhumudwisa
UTM motomoto osadandaula
MCP my vote ❤❤❤❤❤❤
Also me my vote
Njawala number one, kaluati number two be careful ndi anthu awiriwa ndi anthu oyipa mutima kwambiri
We love utm kwambiri koma isakhale ya munthu
Proper narration, big up guys ❤❤❤
Manganya iwetu wagulidwa ndichisilu chinzako
Inu nde munabwela kudzauza amalawi tchutchutchu osat akapilikon enawa ongokamba zinthu zopanda kumutu
Munthu uyu akunena zoona
Inu ngat mwin wake amafuna kusazika ndiye mukufuna omusatila atan
Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj
Zoona zake anganidze mofasa sure ❤❤❤❤❤
Kumupeza wina akuti mcp my vote
Amalawi ndichani
Ena si anthu....ndizinyalala tu.
Eti eti amwene mumune mcp yawonongera zinthu ndiye wina akut mcp my vote eeeesh
Anthu ena alibe mzimu... Kuti mwaoneso akuyankhulawo ali mbuuu
Kufuna kuzamva mkhwangwa ili mmutu
Mwawathandiza ulemu
Athu akuda ndife opanda nzeru
You to be specific
Ndibwino kt atengane okhaokah
Abwenza ndalamazi...eni ake akutuwa kusowa sopo...akuoneka a fumbi lokha lokha km ena akuononga mosaopa Mulungu...ayi tiona posachedwapa....nafe tikudikira
Probably the best program
Akumatibera zathu zomwezi zamisokho
Mulungu azikutete bro
Njawala ndi kaliati mutiwonongera chipani chathu ndakwiya Nanu heavy kuno kuntheu mutisamale awirinu
Koma selina 😂😂😂akut kod akabambe akulowela kut 😂😂😂😂
Don't lie to us.
You support MCP.
Skc ankafuna kutchoka after kusalemekdza mgwirizano omwe unalipo ndiyeno kutchoka it's a good move komano to agree with ndikutenga mnthu kunja that's wrong indeed
MCP 💥💥💥❣
Ma prophet watu koma atilankhilitsa pambali mxiiiiew
Mmmmm km mcp yaonjeza,zot amalawi akuvutika sakuganizako
Analysis yanzeru zozama koma imeneyo?
anthu atamalankhura ngati mmene ukuyankhulira lweyo anthu akhoza kumachitazinthu mwanzelu
Gwende u have fairly advised
🤣🤣🤣🤣 nkhani zake
Gwede is the best
Yea that's very true and I see it ku utm utsogoleri unali wa chilima ena onsewa mavuto bola ku MCP komweko mudziwa bwanji mwina the death of chilima was planned with those who are on top blaming MCP for the death yets amafuna mpando wachilimawo why so early kutuluka mugwilizana without solid proof that is MCP guilty , ine unless pa social media muzabwerese real proof how you saw the killing happen that's when I will find them guilty
Kkk😂😂😂😂😂😂😂😂 anzanga afumu owuka
First to comment
Pamaliro wandale athamangitsidwe
Mcp ya wina kale
😂😂😂😂😂😂😂 koma zinaz abale kkkkkkk kuthamangitsa masiket mudzi kkkk
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂Koma abale
😢😢😢😂 ozuka kumandao
Eeeeee kusokonezatu kkkkkkk
utm igawana zida zafikapa angonamizana
Usi ndi munthu yimodzi yomwe mwini wa UTM
Kuwechetamwangajimbilambali
Ndinu a Mcp chokani apa mukuyiwala kuti UTM idayamba yokha without mcp
vuto amalawi timasapota vitsilu kali ndi ........
Kma nkhani ya a pro andiseketsa bwanj😂😂
Nduna zomwe zikugawa ndalamazo akumatibera misonkho yathu yomweyi...ifetu maso athu tikuona ndipo tilankhula chaka cha m'ma chino....40million plus just for one meeting business yanji imene akupanga? Apapa zaonekeratu kuti andale amatibera pomwe anthu akufa ndi njala. Ambuye akukuonani ndithu
Aaaaa
Malawi
akuononga chipani cha utm ndi mai kaliati ndi azao filex njawala anthu awawa ndithu amaliza chipani cha utm samalani
Tafotokozani mmene akuwonongela ....
Kugawa ndalama Koma ma servants ndee ka salary ka mmanja
MCP 🔥🔥🔥🔥
Pathako pako 😂
Wabaya ase kkkkkk@@IshmaelIbrahim-s8c
Iwe fisi eti 😢😮
Mapazi ako nd mcp yomweyo
Njoka iwe fiti
Of course
Umakwana
As government I think abalalika ndithu
Ntchindi mulije mu utm
Zowona utm yisatenge munthu wakunja
Kodi ntchentche zikutanipo pamibawapo
Si ntchentche
😂😂😂😂😂
😂😂😂😂esh I think ndi lens
MCP ☑️
😂😂😂
😂😂😂😂😂😂
Ambuye mulungu daritsani chipani cha mcp 🇲🇼❤️
🙏🙏
Ndiwe opembedza mafano
Mulungu wa Abraham sangadalitse MCP...siwachisokonezo ngat Chakwera wakoyo...usamutchule Mulungu pachabe...ungaone tsoka
Ukunama ukadakhumudwa mcp chiyembekezo cha Malawi ambiri
@@user-px6kt8rx2p MCP chipani chafuko
Usatchule dzina lamulungu wako pachabe chome iwe
Mcp mooootooooooooo
Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj
Aaaaa
Malawi