Kuganiza mwakuya Maso anga adali kwa a Chitsi sindimadziwa kuti angapange Khomani!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!! Kunena zoona nthawi yatha tisamachedwe ndi kukokana
Mu dziko lino lapansi tili ndi soka lalikulu! We will surely die in the way zamasiku otsiliza... Ndilibe kanthu ndi munthu , ndili ndi kanthu ndi moyo wanga ndi onse akumvera chenjezo la Mulungu ndi kuyenda m'menemo! How would you say inu ndi Mulungu! Just worried of asking this such question
Manganya you are , a best actor , you impat knowledge and wisdom to Malawians.
Manganya mngochenjera angogwiritsa ntchito amzake😮 Poteteza mpando wake ilisi Sewero la Tikufelanji km La Tonse alliance
Ngati bodza
Full of sense, wisdom and knowledge.
Keep it up Guys ❤
Akuchimbukwa tulikwalolela naga akawe chalew^e... Khomani!!!❤❤
Good advice my VP
Manganya is good at this koma ku ndaleku aaaaa ndimaona kuti sakumasuka bhobho 😊
Vp inu one lkkkkkk munava mwambo
Mkazi samalawidwa kkkkk,Manganya mwaphunzitsatu
Kajambuleni kawiri we want the real tikuferanji not politics
😂😂😂😂 Ndaone mochedwa atakhala kale pa vice president. Anyway u perform well
Very nice point, Mr. Manganya like
😂😂😂😂 manganya anakonza nthawi Zina zimamveka zongosekesa chabe koma ayi ndithu zili ndi thandauzo
Kkkkk 😂 so ❤ zakwathu more nice 🇲🇼👊🤞
Manganya sewero labwn bwn wayamba kulowesa ndale
Watching from Johannesburg olifantsfontein
Bravo manganya utumbuka sungathe🎉🎉
Watching after he been made Vice President
You're coming old manganya just because muli m'boma
Kuganiza mwakuya Maso anga adali kwa a Chitsi sindimadziwa kuti angapange Khomani!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!! Kunena zoona nthawi yatha tisamachedwe ndi kukokana
watching from Capricorn Cape town
DR MANGA MY VP MUMAKANA
Manganya those were the days kale lathu 😂🎉
A Namalawa 😅😅😅 great piece of advice
Blees up sir👌
Ndale zoli apo manganya amatha kuyambila kale koma uwu unali msonkhano wa ndale
Paja nae alikomweko akudya nawo
Mlelemba akukwatanitsa Nkhwasala😂😂😂
Kkkķkkk mmakwana madolo inuyo more respect
Tinkawakonda amanganya km pano kkkkkkkkkk anatha analowa ndare opusa iwe manganya
Ulemu wanu avep
Ine pano supporting the vp🎉🎉❤
Inuyo zoti ndi a honourable sizimadziwika munthu odzichepetsa koopsa I 👍 you Dr manga
Achisi ndimangoti alankhula zosanveka.
😂😂😂Manganya ndigalu kwabasi
My best ever
My home boy
Palibe ndatola ky ndikuuma mutukwanga ky😂😂
Kakakakakakak ndaswekaa koma manganya kkkkkkk
Live Long sir usi
Kkkkkkkkkk mmmmm manganya wadiwonjeza mpaka akapa iwe tikumana tikalowesa zoma lathu ndilinawe ntchito
Manganya
Km manganya mmmm iwe anakoza
Zopusa basi ndare pa sewero
Manganya ipatseni moto
Manganya iweyo umakwana
Panotu akuti vp koma kkkkkkk
Manganya kumtima mbee...😂
Mumakwana inuyo ❤❤❤❤
Manga you're one
Zopusa izi ndale pasewelo
Ayambitsa nyimbo asa kudabwa2 ine
Kkkkk❤❤❤❤ more
Komano ndiye muzitipangirabe sewelo Dr Manga
😂😂😂😂 ndiye mwati knomani?😅😅😅😅😅
Ruth similar AKA make sikono
Mfumu kadzi ndawonatu ananyoni
Kdi ndye paulo atulukira liti😊
Anamalawaaaaaaaa!!!!!!!!!
Eeeeeee ziliko
Salute
Riiiiiiih khomani😂😂😂😂
Yomweyoooo 🎉
Come on Mr VP we proud of u not chakwera
Zopusa zeni zeni
Bring back ma sikono
Title ya njimboyo ndichan ine imandisangalatsa
timakusatani mwalowesa ndale😊
Ai zikomo
Abale Nyoo Ali kuti???
Manga umakwana 😂
kapeni for tonse
Akuluwo kd saima kuvuna nao aaaaa
🎉🎉
Waikamo zandale basi ingotsiyani amaganya
Munalowetsa ndale akulu inu
Ili sisewele la tikufelnji koma kuteteza udindo wanu nkulu mukuononga drama group ndi ma politics anuwo moya
"Munthawi yosiliza" 🤔
Kutsegula comment box kufuna kutitapa mkamwa😏🙄
Bamboo a sikono ajaa
Tikufelanji anasiya kubeba ndale too much
😂😂😂😂😂😂 koma
Mwazilowesa ndale
Ndipo kwabas ya week ino yalowa ndale zedi
@@user-ly6eg7zk1s ndipo sizinabebe taaa
🔥
Mmmm zalowa ndale
😂😂😂😂😂 tikuferanji kapena nsonkhano wa ndale
Ndimaganiza ngat nduwona ndekha
Msonkhano ndipo azathuwa sakuona vto poti akudya musavutikila ngat ife ife timagobola basi
Anali kale awa
Mukuononga mbili yanu chifukwa chandalama
Mbola
Ndale
Where is Mr nyo
😂😂😂
Mimba nkagunde chigololo salawa
Gindee
Alinse Ali ndi mutu wachewache achinyamata musamale
Boma losaopa Mulungu, zitheka bwanji kuti Ampingo alowererepo, kodi akanena chilungamo mungakhonze kuchimvera ? Atanena kuti Mulungu akuti president aime , chakwerayo angaime? Kumbukilani Mfumu Ahabu ... Adauzidwa ndi mneneri Mikaya zooona zake zomwe Mulungu wanena koma adasankha kusamvera , ndiye mundiuze inuyo kuti chidamuchitikira Mfumu Ahabu ndichiyani ! Adafa chifukwa chonyoza mau a Mulungu! Momwemo the current government will surely die 😢
Ndipo sikutiso angawavele apingowo ayi kma kuwasakaso kt awamange ati akutsutsana nawo iiii😢
Inu ndi mulungu?moti zinthu pano zikuvuta dziko lose simukudziwa?muziwerenga bible zamasiku otsiliza
Mu dziko lino lapansi tili ndi soka lalikulu! We will surely die in the way zamasiku otsiliza... Ndilibe kanthu ndi munthu , ndili ndi kanthu ndi moyo wanga ndi onse akumvera chenjezo la Mulungu ndi kuyenda m'menemo!
How would you say inu ndi Mulungu! Just worried of asking this such question
Koma Honourable Manganya
mangqdyq and mulemba don't talk nonsense musazitenge Malawi ndioupusa
Akudya bwino akalephele kusangalala😢
Ipatse motooooo
This is tikuferanji or politics??? Stop talking abt politics plz, sewero munaliyamba bwino koma mwalowetsanso ndale
Koma mikuluwiko ili umu eishií
bwana Michael usi ndi group yanu ai ai mumatha. ❤️❤️❤️❤️
watching from Capricorn Cape town
I think it's better to stop acting tikuferanji not boring like this.we don't need ndale tikufuna tikuferanji yachikale yokamba Za HIV and AIDS
You have just wasted my bundle with your boring drama. A drama full of politics asah
Why u open
My question
100 percent
I thought ndi Tikuferanji without knowing Kuti ndi Tonse alliance
I don't know why I always think of entertainment other than politics...I found it fun.😂