BRIAN BANDA KUPHAPHALITSA ZIMAFUSO -🤔🤔🙌🙌21 July 2024

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 14 окт 2024

Комментарии • 55

  • @JumaGadaff
    @JumaGadaff 2 месяца назад +15

    Akayamba choncho dziwani kuti mulungu wamakamu ayamba kuwakantha inu mulungu awavula zovala onse akuimila MCP ife chete ndi umasiye wanthu amen 🙏🙏

    • @moosasinoya3307
      @moosasinoya3307 2 месяца назад

      May Soul Rest In Peace SKC😭🔥💪

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 2 месяца назад +1

    Mtsukuluzi simunampatse mpata kwambiri ngati mmene munachitira ndi Ndebvu za mwayi. Muzipanga balance a Brian Banda. Mwaonetsa tsankho

  • @MervinMwambinga
    @MervinMwambinga 2 месяца назад +1

    He can be a youth, well educated, good passions and visions but our constitution does not give power to Vp to decide and implement ideas. We have evidence, our lovely late VP SKC. He was our only hope for this country and no one else. Tiye tizinamizana chonchi basi.

  • @IssaJohn-cb8vn
    @IssaJohn-cb8vn 2 месяца назад +4

    Skeffa chimoto wathadi eti mpaka afika apa kkkkk

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 2 месяца назад

    Big up brother man!!

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 2 месяца назад +7

    Mcp ndiyakupha

  • @NelsonMarley-m6p
    @NelsonMarley-m6p 2 месяца назад

    Zimayi opusa chinkhope ngati mtengo wamulambe mxiew

  • @AisherKhaalid
    @AisherKhaalid 2 месяца назад +1

    Mayi Chikata my neba from Mzuzu

  • @PriscillaKhumbanyiwa-i1d
    @PriscillaKhumbanyiwa-i1d 2 месяца назад +3

    Satana amayenda ndi asatana azake amalawi wosazindikila kumasapota anthu akumpha amcp

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 2 месяца назад

    AAAAAAAAA nthawi Yotani monse muja??? Mumba ndi chakwera amabera limodzi agalu amenewa shupitiiiii

  • @HarrietMtenje
    @HarrietMtenje 2 месяца назад

    Dzitukuko dzompha anthudzo alamulira inuyo

  • @macmsiska2937
    @macmsiska2937 2 месяца назад +3

    Mbava yayikulu iyo yikamayankhula m'maso muli gwaa

  • @PriscillaKhumbanyiwa-i1d
    @PriscillaKhumbanyiwa-i1d 2 месяца назад +1

    Anthu andale makonda kumuchula mulungu pafupipafupi mulungu akukantheni bava za mcp

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di 2 месяца назад +1

    Botolo la madzi okumwa muziliika kusogolo kwanu a Brian osati ku mbuyo or ku mohepete kwanu muziliona or mulibuzy

  • @LloydMkula
    @LloydMkula 2 месяца назад

    Akufuna kutumikila a chakwera not a Malawi ma delegates mazimvelatu

  • @CathrineBizza
    @CathrineBizza 2 месяца назад

    Ziyezekanani ku mcpkp uyaaa

  • @joeljere4385
    @joeljere4385 2 месяца назад

    Onse aku North okhaokha

  • @UseniMailosi
    @UseniMailosi 2 месяца назад +3

    Koma siteniwe muganise bwino sachakwela muiwale

  • @EnerstManess
    @EnerstManess 2 месяца назад +2

    N'gona zen zen

  • @CrispineBetha
    @CrispineBetha 2 месяца назад

    Akunama amayiwotu 2025 mcp mulibepo😂

  • @GiboTakondwa
    @GiboTakondwa 2 месяца назад

    Mwamvatu nokha akuti eyeyu akufuna azizatimikila achakwela osati amalawi

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 2 месяца назад +1

    Mukupikisana kwambiri because you are in government now,, fact osati zinazo aaaaaah. We have also heads to reason.

  • @stevemtambalika
    @stevemtambalika 2 месяца назад

    Chikangawayu watha basi kkkkk

  • @FaheemChipojola
    @FaheemChipojola 2 месяца назад

    Amai awa nzeru alibe ndithu

  • @NthambiInvestment
    @NthambiInvestment 2 месяца назад +1

    Ngati mukunamizana zowinaso muiwale,, vote ya 2025 tikavotela kuchikangawa ,, MCP Pachilani muzipita ,,,,,
    Nanunso a skeffa ndi a mlaka plz plz ziyalondolelani anthu koyenela pl

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 2 месяца назад +1

    😂😂😂 thiraspot paka 1 mita

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 2 месяца назад +2

    Nyero yako mzimai iwe ndithu

  • @Betty-fe9ql
    @Betty-fe9ql 2 месяца назад +1

    Koma ma comment a Brian mpake pena amankhoma 😅

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr 2 месяца назад

    A Brian ndi a ndevu apatu tikudabwatu leroli kwabookatu Ku MCP money kkkkkk.eeeeee koma abaleeeee.

  • @DavieMoyo-pe8vn
    @DavieMoyo-pe8vn 2 месяца назад

    😂😂😂😂 nyamata WA vinyo Ku MCP Malawi ngosangaratsa

  • @DanielZitande-y1d
    @DanielZitande-y1d 2 месяца назад

    Abambo idzoo za ku chipani kwanu siii zotandidza a Malawi

  • @EDGARMPIKAMEZO
    @EDGARMPIKAMEZO 2 месяца назад

    A Mumba is very controversial, kudzikundikira too much. Ubwino wako amaudziwa ndi ena. Zikuonetsa kuti atasemphana nawo mwayi uwu atha kuukira chipani . He is too confident. He is not bigger than the party.

  • @alomuddin8801
    @alomuddin8801 2 месяца назад

    Mcp ya khanza yabweletsa njala mu dziko la Malawi chilichonse chinakwera mtengo,

  • @EnerstManess
    @EnerstManess 2 месяца назад +2

    Mbava

  • @andrewBwanaisa
    @andrewBwanaisa 2 месяца назад

    Mwagwa nayo nonse a mcp

  • @lupakishomalangaelix6606
    @lupakishomalangaelix6606 2 месяца назад

    Usi sakaimila uku?

  • @jamesmsonkho4830
    @jamesmsonkho4830 2 месяца назад

    Kkkkkkkkkkkkkkk

  • @LowanMasiye
    @LowanMasiye 2 месяца назад +1

    Boma ndilomweli

  • @giftmakoyo1441
    @giftmakoyo1441 2 месяца назад

    Amayi inu mmmm😢

  • @kingnavitcha6243
    @kingnavitcha6243 2 месяца назад

    Angalephere kuchitsa chipani choti ndi chake

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 2 месяца назад

    Kamat uku sizitha bwino uku mungot phee

  • @tisuhmakhwah7085
    @tisuhmakhwah7085 2 месяца назад

    Woiphonya ati akufuna kutumikila chakwela not malawians.

  • @mussamapira801
    @mussamapira801 2 месяца назад

    Akuba okha okha

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 2 месяца назад

    Zaziii

  • @ChimwemweChiwawa-g5o
    @ChimwemweChiwawa-g5o 2 месяца назад

    Amayi opusa

  • @KondwaniLungu-x5l
    @KondwaniLungu-x5l 2 месяца назад

    Anthu akewa sizothandiza ziko

  • @samuelosman3215
    @samuelosman3215 2 месяца назад

    Aaaa simulaka uyu?

  • @hopembendela
    @hopembendela 2 месяца назад

    iwe wakhutatu kondole eti

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw 2 месяца назад +1

    paja iwe dxina lako ndani

  • @IssaJohn-cb8vn
    @IssaJohn-cb8vn 2 месяца назад +1

    Kkkkkkk oyimba akumalawi

  • @michaelzuze6516
    @michaelzuze6516 2 месяца назад +1

    I regret watching this shit

  • @MarriamBakalie
    @MarriamBakalie 2 месяца назад

    Ndiwe galu pamodzi ndi akwanu ose stupid guy gud man for nothing.