BRIAN BANDA KUFUNSA MAFUNSO PAMAPERO PA CONVENTION

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 26 окт 2024

Комментарии • 135

  • @IvyMkhura
    @IvyMkhura 2 месяца назад +3

    Peter Mutharika is so genius, amene anamuchalira kuti abweranso ku convention kachiwiri wauponda.

  • @PetroKachingwe-jf7dh
    @PetroKachingwe-jf7dh 2 месяца назад +3

    Nkhalamba zokhazokha osasiyila achinyamata bwanji
    Mbava izi
    Uyu George Chaponda anaba chimanga chonse ndalama za Admark
    Mbava iyi asakudziwa ndani
    Admark inatha chifukwa cha Anthu awa

  • @ishmaelsiffah9900
    @ishmaelsiffah9900 2 месяца назад +1

    Peter muthalika ndiochenjera guys,kuteroku ndiye kuti oyedzeka anzao aja anamuchalilira lero auponda iye sanabwere 😂😂😂

  • @WhiteRichard-cw2fo
    @WhiteRichard-cw2fo 2 месяца назад +12

    Muthu waluza musamukwezi tima ayi musiyeni wafotokoza bwino kwambiri

    • @JustinLipipa
      @JustinLipipa 2 месяца назад

      Kkkkkkkkk ndizakuchipani izi.

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj 2 месяца назад +6

    Ndiwayankhile ine a Chaponda kukula komwe akula sizikutanthauza kut akhale pansi ai..azakhala pansi ntchito yao ikazatha pa Dziko lino..this is why we have a Old testament qnd new testament..

  • @MauriceMukona
    @MauriceMukona 2 месяца назад +1

    Nonse amene mukunena zokalambazo mbolo zanu ndi nyini zanu mxiiiii.manamvapo kuti ukalamba ndimatenda?

  • @FatimaUmali-pc8sy
    @FatimaUmali-pc8sy 2 месяца назад

    Zoona zake ndi ZImenezo kuti a nawona adani ake alipafupi ndi munthu wankulu Peter akaona patali genius Peter ❤❤❤ mphechempheche mea njovu Salita awiri

  • @mayachikadewa7551
    @mayachikadewa7551 2 месяца назад +2

    Zitheka bwanji Kuti president asapezeke potseka convention?

    • @JohnsonMaulana
      @JohnsonMaulana 2 месяца назад +1

      Adani achuluka amaionela patali mkuluyu wachita bwin😊

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 2 месяца назад +7

    Koma Briane ukufuna kukweza BP munthu wachikulileyo Kodi komanso zakhala bwino akula azigwila ndi anyamata ntchito

  • @LewisJumbe
    @LewisJumbe 2 месяца назад

    Conversation yayenda bullet,mafunso Anu,sapindula kanthu.lets look forward.

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju 2 месяца назад

    Age is just a number indeed...DPP my vote

  • @MadalitsoBokosi-j3u
    @MadalitsoBokosi-j3u 2 месяца назад +3

    Akulu ndi dambo mozimira moto ... Anyamata azikathamanga pa ground akolo azilangizi

  • @Chikwina
    @Chikwina 2 месяца назад +2

    Chaponda waledzera ndipo mutharika akupuma after ukalamba azigonagona

  • @stalickkafera3454
    @stalickkafera3454 2 месяца назад +2

    Mutalika wantha mukumukakamza kugwirabe ntchito😂😂
    Osamusiya apume bwanji
    Adzaferatu pa msokhano😂

    • @thomaswyson-e2q
      @thomaswyson-e2q 2 месяца назад

      Iwe namachende asanafe peter ayambe kufa ndiabambo ako

  • @AlickChima
    @AlickChima 2 месяца назад

    Maharaja nde mwawapanikizatu onyamata inu 😅😅😅 mpaka chibwibwi kudzitamandira ati Leader of opposition ndi power 😅😅😅😅

  • @MisheckKamwendo-w9n
    @MisheckKamwendo-w9n 2 месяца назад +4

    Koma Brian ndi azako muthu waluza koma mafuso ameneo muthu atha kukomoka

  • @charleskazembe5728
    @charleskazembe5728 2 месяца назад

    Brayan thanks you always make program sacessfull 😅😅😅

  • @christopherkamphinga
    @christopherkamphinga 2 месяца назад +2

    Zayambika uku. Azizathawanso mu office ndi ukalamba.

  • @UchizieFMtemela
    @UchizieFMtemela 2 месяца назад

    A chair mwayankha bwino 😂😂alekeni chabe😂😂

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 2 месяца назад

    Profe sikape guys ... , munthu uja amayiwelenga

  • @VenançioZocueza
    @VenançioZocueza 2 месяца назад

    Iwe Brian peter amaopa kuphedwa ndi dzigawenga dza mcp

  • @AlihIbrahim-s7v
    @AlihIbrahim-s7v 2 месяца назад +2

    Koma inusotu Chanel chanuchi ndiye gaga weniwenotu Madera bwanji ingoduka basi chimphwetelele

  • @tasmania527
    @tasmania527 2 месяца назад

    Iwe Namalomba, njala inabwera chifukwa ma leaders anu ammbuyo sanapange za irrigation kuphatikiza ndi ng'amba ya Southern Africa. Mwakhala mukunena kuti achina Mutharika ndipatali, nanga anayika madziko anji mu nthawi ya ulamuliro wawo kuti ku Malawi kusakhale njala ? Mulibe fundo koma kunama ndi kupusitsa anthu.

  • @PreciousPhiri-l8w
    @PreciousPhiri-l8w 2 месяца назад

    Koma chi peter chija osazachiphwekes chochenjera ❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @Apostolic.faith7044
    @Apostolic.faith7044 2 месяца назад

    These are elders supposed to rest for sure. Old to a point where they can't function to bring change in Malawi. People must accept they are old and tired, not even able to close a convention. They can't even see the difference of frail health on P. Mutarika. He did his best part in the past but must retire all these who are not able to see that they a madalas

  • @Blessings-b7h
    @Blessings-b7h 2 месяца назад +1

    Kodi Brian bwanji ukuwavutitsa anthu dpp?
    Munthu wamkulu akuphunzitsa ana ntchito.

  • @AnnastanziaMhango
    @AnnastanziaMhango Месяц назад

    😂😂😂😂😂 Kusakhalapo pa musokha umenewo zikuoneka kulemphera kuti sazalowaso mu boma

  • @BrianMaganga
    @BrianMaganga 2 месяца назад

    Adad akuyendani pansi, muona kuti mutani 😂😂

  • @MaxwellChiwaya-i8q
    @MaxwellChiwaya-i8q 2 месяца назад +1

    Kkkkkkk koma anamalomba ndi achina Brian kkkkk

  • @BrianAmos-s2k
    @BrianAmos-s2k 2 месяца назад

    Zomwe akuyankhulazo ndidziwona chomwe chinachititsa kuti msonkhano uwonjezeledwe matsiku Malo motha tsiku le ileni ndichani?which means adani amakonz a chiwembu.President adachita bwino kungolemba note yotsekela msonkhano wawo basi

  • @FanizoKawindula
    @FanizoKawindula 2 месяца назад +1

    Kodi Hon Mchacha alipo?

  • @CleverlyKanthyos-ds5sg
    @CleverlyKanthyos-ds5sg 2 месяца назад +1

    DPP khalamba zokhazokha
    Zoyha mano

  • @GreyMwanyimbo
    @GreyMwanyimbo 2 месяца назад

    Koma zitithandiza??????

  • @husseinjabu8866
    @husseinjabu8866 2 месяца назад

    Poor quality of coverage improve guys

  • @KenAipa-r3r
    @KenAipa-r3r 2 месяца назад +2

    Kkkkkkkk Kuchita kubwereza kuti Kodi aluza ????

  • @thomphalavi5027
    @thomphalavi5027 2 месяца назад +2

    Dpp yatsakha bwino mipando komaso mukutipasilanu mukulemphera

  • @beinhardkausiwa7107
    @beinhardkausiwa7107 2 месяца назад +1

    The question is unprofessional

  • @AnnastanziaMhango
    @AnnastanziaMhango Месяц назад

    Chaponda tinamutopela ife anthu a Malawi sitikufuna olo ngati sakuziwa umunthu alibe

  • @JohnBanda-ux9fy
    @JohnBanda-ux9fy 2 месяца назад +2

    Munthu wamkulu APM anachoka lero mmawa chifukwa anadziwa Kuti Ku dpp kulibe kukhapana ngati achita chikangawa party..anachezera convenshon .. Koma kurephera kukayang,ana ndege Ku chikangawa 😂😂

  • @EmmanuelChirwa-z3n
    @EmmanuelChirwa-z3n 2 месяца назад

    Chokani mwakalamba oba chimanga inu🤣🤣🤣

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli 2 месяца назад

    Munthalika ndi dolo Mesa anthu amachachila kuti amupange zina ndi zina ndiye iyeyo wabanduka ndi dolo

  • @GladsonBanda-m3e
    @GladsonBanda-m3e 2 месяца назад

    Nkumati tiyendetsa Boma pumani mwakula kukanika kukatseka msonkhano ngakhare campaign idzawavuta

  • @AnnastanziaMhango
    @AnnastanziaMhango Месяц назад

    Wakalele waka adzukulu nakuonera mbuzi muchiwaya kumudzi fundo mulije ndipo akalamba basi

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 2 месяца назад

    Muthalika ndiwochenjela wayenda kwambili uja ndiwozindikila

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi 2 месяца назад

    Sakumwa akutero ma ujeniwa 😂😂

  • @KingsleyKunneno
    @KingsleyKunneno 2 месяца назад

    Koma nkhalamba izi nazo 😂

  • @83kwak
    @83kwak 2 месяца назад +3

    I love Malawi,let's keep praying to Lord,Jesus Christ ...........

  • @leonardmalirana7423
    @leonardmalirana7423 2 месяца назад

    Brian osatero, osamuyankhulitsa chibwibwi munthu, Muthalika watopa akapumule

  • @hassammaulana4529
    @hassammaulana4529 2 месяца назад +1

    Koma guys akuti alipomwepana ali kubuyoko

  • @EnerstBanda-m4s
    @EnerstBanda-m4s 2 месяца назад

    Please abale athu a Dpp tamumverani chisoni Gogo wakula munthu sangakwanitse kulamulira dzikoli ndi munthu okalamba kwambiri his a good President sibodza but tasakhani munthu weniweni wamoyo osati izizi Please mukulimbana ndi chipani choti chili m'boma kale woke up Malawians we can't continue ruled by old person 85yrs or muli serious

  • @johnchicoti
    @johnchicoti 2 месяца назад

    Peter wadwalika ndichifukwa chake sanabweleso

  • @JusticeKawilira
    @JusticeKawilira 2 месяца назад +3

    Munthu wankulu posakhalapopo sanafune zopalana pakamwazo

  • @EmmieChikuseKoreya
    @EmmieChikuseKoreya 2 месяца назад

    Zokalamvazo ndiye usanene iweso osakalamba iwe unkhoza kufa kumusiya okalambayo komaso kukalambako ayamba ndi mai ako ndi bambo ako

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh 2 месяца назад

    Peter wakula sangakwanitse kulamulira azalamulira ndi getrude ndi chisale yawo ija

  • @AnnastanziaMhango
    @AnnastanziaMhango Месяц назад

    Sazalowaso mu boma awa nanji iwowa chaponda nde never mpaka yesu wize

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward 2 месяца назад

    Iwetu brain Banda ndikuwona umadana ndi dausi

  • @MahallaMinistries-fv1hw
    @MahallaMinistries-fv1hw 2 месяца назад +3

    Atolankhani athu suffers from a certain condition

  • @ConradccjSokoSoko
    @ConradccjSokoSoko 2 месяца назад

    Wadwalika ndi kutopa gogoyu.
    Siyirani anyamata. Alipo ambiri anyamatakumeneko.
    Milandu ya malibino yinathera pati, atatchulidwa ku kothi pamodzi ndi Ntaba

  • @RonnexNyezule
    @RonnexNyezule 2 месяца назад

    Brian ati get away tu😂 atero George 😂

  • @douglaskayira8362
    @douglaskayira8362 2 месяца назад

    Nice

  • @GiftBonomali
    @GiftBonomali 2 месяца назад

    😂😂😂😂😂 koma Brian amanditsangalatsa❤❤

  • @violetkamvanthupi2443
    @violetkamvanthupi2443 2 месяца назад

    UTM my vote

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda 2 месяца назад

    This old party, with old experience

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 2 месяца назад

    Chapond sakuyankh funso mwaluz ndiy muzit ndil ndigalimot ndiy kt chiyan anthu akukanan

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj 2 месяца назад +2

    Nothing is was wrong Muthalika posamaliza nawo zochitika..bola alemba babawo zoyankhula zawo

  • @RabeccaMkandawire-i9j
    @RabeccaMkandawire-i9j 2 месяца назад

    Akapume amenewa ndi amene anayambitsa quota system

  • @OwenDubbyflitz
    @OwenDubbyflitz 2 месяца назад

    Mbwerera zeni zeni

  • @MphatsoZintambila
    @MphatsoZintambila 2 месяца назад

    Mbuzi izi

  • @DavieChiwale
    @DavieChiwale 2 месяца назад

    Brain uzioona mikoko yogona iwe

  • @RABSONSIKELO
    @RABSONSIKELO 2 месяца назад

    Mr Maize gate ur wounded

  • @AlihIbrahim-s7v
    @AlihIbrahim-s7v 2 месяца назад +3

    Dpp yasankha bwino mipando yawo

    • @RiteRoderick
      @RiteRoderick 2 месяца назад

      Ndipo koopsa zed bro❤❤❤

  • @DjKingXuluMtenje
    @DjKingXuluMtenje 2 месяца назад

    Kumangoduladula mau zobowa

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 2 месяца назад +2

    Nice conversation

  • @MoreenSemu
    @MoreenSemu 2 месяца назад +1

    Akudwala Peter akungu mukakamiza

  • @VictoriaKumwenda-k6o
    @VictoriaKumwenda-k6o 2 месяца назад +5

    Kukalamba munthu uja ndi nkhamba

    • @MzadziWanga
      @MzadziWanga 2 месяца назад

      Kagwere uko pedegu iwe 😂😂😂 age is just a number

    • @HarrisonMwanga-xy4sc
      @HarrisonMwanga-xy4sc 2 месяца назад

      😂😂😂😂😂😂😂 kodi 😅😅😅😅

    • @patrickmoffat9609
      @patrickmoffat9609 2 месяца назад

      Iwe suzakula

    • @DalitsoDjimo
      @DalitsoDjimo 2 месяца назад

      Zoona a mwene suti a piter niwoyipa ayi koma akamba nchito yi sangayikwanitse.

  • @StanfordMNthali
    @StanfordMNthali 2 месяца назад

    Chaka chino tiona maroza akariyati akupanga ubale ndi dpp ayiwala dpp amunyoza Chirima ndiposo kariyati kumbukirani mumene dpp yinamphela banja raTambala ku Lilongwe kariyati uribe Kodi Chirima anakhala kuti arimoyo mukanapita kumeko Mai opanda manyezi iwe

  • @PreciousDzonzie
    @PreciousDzonzie 2 месяца назад +1

    Agogo agogo agogo 2025 kotsutsa boma woooooo

  • @LightonKamwana
    @LightonKamwana 2 месяца назад

    Abanda muziva chisoni ndi agogo.

  • @JacklineNiwahereza-ni3pm
    @JacklineNiwahereza-ni3pm 2 месяца назад

    Kkkkkk koma nde mwamuwonjeza chaponda kkkkkkk

  • @MaikNkhoma
    @MaikNkhoma 2 месяца назад

    Kkkkkkk yadwala nkhalamba ija

  • @RabiaNotes-ql8cf
    @RabiaNotes-ql8cf 2 месяца назад

    😂😂😂😂Dr George Chaponda

  • @peterwhite3782
    @peterwhite3782 2 месяца назад +1

    ❤❤❤❤ Dpp

  • @YusufMapata
    @YusufMapata 2 месяца назад +1

    amuthalika akuchita kukakamizidwa kuti ayime koma munthu uja mafupa atopa popeza mtima sukalamba

    • @thomaswyson-e2q
      @thomaswyson-e2q 2 месяца назад

      Mafupa akalamba ndiabamboako kapeonyozamakoloako iwe mboliyakonso

  • @Lingstone-r3z
    @Lingstone-r3z 2 месяца назад

    Brain that is issue to close covetion,

  • @ConlardNkhoma
    @ConlardNkhoma 2 месяца назад

    Chipani chamagogo kkkkkk

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 2 месяца назад

    Sindin wadpp kom ndakondw kwambir pomuchots chapond

  • @ishmaelimani3779
    @ishmaelimani3779 2 месяца назад

    Khangati mitu sikugwila amalawi chomwe timachifuna sitimachidziwa

  • @charitykalulu
    @charitykalulu 2 месяца назад

    Kusakhalapo osati chifukwa chokula kapena

  • @MaxwellChiwaya-i8q
    @MaxwellChiwaya-i8q 2 месяца назад

    Kkkkkkkk Brian Banda usadzafe udzangosowa

  • @omicloans
    @omicloans 2 месяца назад

    Use proper internet

  • @gradsonmayira9336
    @gradsonmayira9336 2 месяца назад

    Brian banda😂😂😂😂😂

  • @GavanaradagarasiDagarasi-bu6le
    @GavanaradagarasiDagarasi-bu6le 2 месяца назад

    Wakomoka amenewuja akudwala

  • @GiftJulius-ro9ev
    @GiftJulius-ro9ev 2 месяца назад +1

    Kkkkkkkkkkk koma yah😅😅😅😅

  • @solobertkamunga2826
    @solobertkamunga2826 2 месяца назад

    Next time Dont post video yot ikuduladulA, azungu azititseka

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh 2 месяца назад

    Tizakalamba koma ngati tizizakakamila mpando

  • @JamesMpinda
    @JamesMpinda 2 месяца назад

    wakulu uyu avomeleze

  • @LydiaManzy
    @LydiaManzy 2 месяца назад

    Sokhano watha bhooo what's wrong sanabweere iyaa nawe

  • @GreyMwanyimbo
    @GreyMwanyimbo 2 месяца назад

    Madala team

  • @DumisanPhiri
    @DumisanPhiri 2 месяца назад

    Wakalamba uyu

  • @JonesManyeka
    @JonesManyeka 2 месяца назад +1

    Iiiii musiyeni munthu akagone