Ndiwayankhile ine a Chaponda kukula komwe akula sizikutanthauza kut akhale pansi ai..azakhala pansi ntchito yao ikazatha pa Dziko lino..this is why we have a Old testament qnd new testament..
Zoona zake ndi ZImenezo kuti a nawona adani ake alipafupi ndi munthu wankulu Peter akaona patali genius Peter ❤❤❤ mphechempheche mea njovu Salita awiri
Iwe Namalomba, njala inabwera chifukwa ma leaders anu ammbuyo sanapange za irrigation kuphatikiza ndi ng'amba ya Southern Africa. Mwakhala mukunena kuti achina Mutharika ndipatali, nanga anayika madziko anji mu nthawi ya ulamuliro wawo kuti ku Malawi kusakhale njala ? Mulibe fundo koma kunama ndi kupusitsa anthu.
These are elders supposed to rest for sure. Old to a point where they can't function to bring change in Malawi. People must accept they are old and tired, not even able to close a convention. They can't even see the difference of frail health on P. Mutarika. He did his best part in the past but must retire all these who are not able to see that they a madalas
Please abale athu a Dpp tamumverani chisoni Gogo wakula munthu sangakwanitse kulamulira dzikoli ndi munthu okalamba kwambiri his a good President sibodza but tasakhani munthu weniweni wamoyo osati izizi Please mukulimbana ndi chipani choti chili m'boma kale woke up Malawians we can't continue ruled by old person 85yrs or muli serious
Wadwalika ndi kutopa gogoyu. Siyirani anyamata. Alipo ambiri anyamatakumeneko. Milandu ya malibino yinathera pati, atatchulidwa ku kothi pamodzi ndi Ntaba
Peter Mutharika is so genius, amene anamuchalira kuti abweranso ku convention kachiwiri wauponda.
Adatopa ndi achikulire
Nkhalamba zokhazokha osasiyila achinyamata bwanji
Mbava izi
Uyu George Chaponda anaba chimanga chonse ndalama za Admark
Mbava iyi asakudziwa ndani
Admark inatha chifukwa cha Anthu awa
Mpakana Osayila kkkk
Peter muthalika ndiochenjera guys,kuteroku ndiye kuti oyedzeka anzao aja anamuchalilira lero auponda iye sanabwere 😂😂😂
Muthu waluza musamukwezi tima ayi musiyeni wafotokoza bwino kwambiri
Kkkkkkkkk ndizakuchipani izi.
Ndiwayankhile ine a Chaponda kukula komwe akula sizikutanthauza kut akhale pansi ai..azakhala pansi ntchito yao ikazatha pa Dziko lino..this is why we have a Old testament qnd new testament..
Nonse amene mukunena zokalambazo mbolo zanu ndi nyini zanu mxiiiii.manamvapo kuti ukalamba ndimatenda?
Zoona zake ndi ZImenezo kuti a nawona adani ake alipafupi ndi munthu wankulu Peter akaona patali genius Peter ❤❤❤ mphechempheche mea njovu Salita awiri
Zitheka bwanji Kuti president asapezeke potseka convention?
Adani achuluka amaionela patali mkuluyu wachita bwin😊
Koma Briane ukufuna kukweza BP munthu wachikulileyo Kodi komanso zakhala bwino akula azigwila ndi anyamata ntchito
Conversation yayenda bullet,mafunso Anu,sapindula kanthu.lets look forward.
Age is just a number indeed...DPP my vote
Akulu ndi dambo mozimira moto ... Anyamata azikathamanga pa ground akolo azilangizi
Chaponda waledzera ndipo mutharika akupuma after ukalamba azigonagona
Mutalika wantha mukumukakamza kugwirabe ntchito😂😂
Osamusiya apume bwanji
Adzaferatu pa msokhano😂
Iwe namachende asanafe peter ayambe kufa ndiabambo ako
Maharaja nde mwawapanikizatu onyamata inu 😅😅😅 mpaka chibwibwi kudzitamandira ati Leader of opposition ndi power 😅😅😅😅
Koma Brian ndi azako muthu waluza koma mafuso ameneo muthu atha kukomoka
Brayan thanks you always make program sacessfull 😅😅😅
Zayambika uku. Azizathawanso mu office ndi ukalamba.
Malawi muno tupusitsana kobas
A chair mwayankha bwino 😂😂alekeni chabe😂😂
Profe sikape guys ... , munthu uja amayiwelenga
Iwe Brian peter amaopa kuphedwa ndi dzigawenga dza mcp
Koma inusotu Chanel chanuchi ndiye gaga weniwenotu Madera bwanji ingoduka basi chimphwetelele
Iwe chikangawa choka ap tulutsani report basi
Iwe Namalomba, njala inabwera chifukwa ma leaders anu ammbuyo sanapange za irrigation kuphatikiza ndi ng'amba ya Southern Africa. Mwakhala mukunena kuti achina Mutharika ndipatali, nanga anayika madziko anji mu nthawi ya ulamuliro wawo kuti ku Malawi kusakhale njala ? Mulibe fundo koma kunama ndi kupusitsa anthu.
Koma chi peter chija osazachiphwekes chochenjera ❤❤❤❤❤❤❤❤❤
These are elders supposed to rest for sure. Old to a point where they can't function to bring change in Malawi. People must accept they are old and tired, not even able to close a convention. They can't even see the difference of frail health on P. Mutarika. He did his best part in the past but must retire all these who are not able to see that they a madalas
Kodi Brian bwanji ukuwavutitsa anthu dpp?
Munthu wamkulu akuphunzitsa ana ntchito.
😂😂😂😂😂 Kusakhalapo pa musokha umenewo zikuoneka kulemphera kuti sazalowaso mu boma
Adad akuyendani pansi, muona kuti mutani 😂😂
Kkkkkkk koma anamalomba ndi achina Brian kkkkk
Zomwe akuyankhulazo ndidziwona chomwe chinachititsa kuti msonkhano uwonjezeledwe matsiku Malo motha tsiku le ileni ndichani?which means adani amakonz a chiwembu.President adachita bwino kungolemba note yotsekela msonkhano wawo basi
Kodi Hon Mchacha alipo?
DPP khalamba zokhazokha
Zoyha mano
Koma zitithandiza??????
Poor quality of coverage improve guys
Kkkkkkkk Kuchita kubwereza kuti Kodi aluza ????
Dpp yatsakha bwino mipando komaso mukutipasilanu mukulemphera
The question is unprofessional
Chaponda tinamutopela ife anthu a Malawi sitikufuna olo ngati sakuziwa umunthu alibe
Munthu wamkulu APM anachoka lero mmawa chifukwa anadziwa Kuti Ku dpp kulibe kukhapana ngati achita chikangawa party..anachezera convenshon .. Koma kurephera kukayang,ana ndege Ku chikangawa 😂😂
Chokani mwakalamba oba chimanga inu🤣🤣🤣
Munthalika ndi dolo Mesa anthu amachachila kuti amupange zina ndi zina ndiye iyeyo wabanduka ndi dolo
Nkumati tiyendetsa Boma pumani mwakula kukanika kukatseka msonkhano ngakhare campaign idzawavuta
Wakalele waka adzukulu nakuonera mbuzi muchiwaya kumudzi fundo mulije ndipo akalamba basi
Muthalika ndiwochenjela wayenda kwambili uja ndiwozindikila
Sakumwa akutero ma ujeniwa 😂😂
Koma nkhalamba izi nazo 😂
I love Malawi,let's keep praying to Lord,Jesus Christ ...........
Ukakamira nkhalamba.
Brian osatero, osamuyankhulitsa chibwibwi munthu, Muthalika watopa akapumule
Koma guys akuti alipomwepana ali kubuyoko
Please abale athu a Dpp tamumverani chisoni Gogo wakula munthu sangakwanitse kulamulira dzikoli ndi munthu okalamba kwambiri his a good President sibodza but tasakhani munthu weniweni wamoyo osati izizi Please mukulimbana ndi chipani choti chili m'boma kale woke up Malawians we can't continue ruled by old person 85yrs or muli serious
Peter wadwalika ndichifukwa chake sanabweleso
Munthu wankulu posakhalapopo sanafune zopalana pakamwazo
❤you Peter
Zokalamvazo ndiye usanene iweso osakalamba iwe unkhoza kufa kumusiya okalambayo komaso kukalambako ayamba ndi mai ako ndi bambo ako
Peter wakula sangakwanitse kulamulira azalamulira ndi getrude ndi chisale yawo ija
Sazalowaso mu boma awa nanji iwowa chaponda nde never mpaka yesu wize
Iwetu brain Banda ndikuwona umadana ndi dausi
Atolankhani athu suffers from a certain condition
Wadwalika ndi kutopa gogoyu.
Siyirani anyamata. Alipo ambiri anyamatakumeneko.
Milandu ya malibino yinathera pati, atatchulidwa ku kothi pamodzi ndi Ntaba
Brian ati get away tu😂 atero George 😂
You are dreaming
Nice
😂😂😂😂😂 koma Brian amanditsangalatsa❤❤
UTM my vote
This old party, with old experience
Chapond sakuyankh funso mwaluz ndiy muzit ndil ndigalimot ndiy kt chiyan anthu akukanan
Nothing is was wrong Muthalika posamaliza nawo zochitika..bola alemba babawo zoyankhula zawo
Akapume amenewa ndi amene anayambitsa quota system
Mbwerera zeni zeni
Mbuzi izi
Brain uzioona mikoko yogona iwe
Mr Maize gate ur wounded
Dpp yasankha bwino mipando yawo
Ndipo koopsa zed bro❤❤❤
Kumangoduladula mau zobowa
Nice conversation
Akudwala Peter akungu mukakamiza
Kukalamba munthu uja ndi nkhamba
Kagwere uko pedegu iwe 😂😂😂 age is just a number
😂😂😂😂😂😂😂 kodi 😅😅😅😅
Iwe suzakula
Zoona a mwene suti a piter niwoyipa ayi koma akamba nchito yi sangayikwanitse.
Chaka chino tiona maroza akariyati akupanga ubale ndi dpp ayiwala dpp amunyoza Chirima ndiposo kariyati kumbukirani mumene dpp yinamphela banja raTambala ku Lilongwe kariyati uribe Kodi Chirima anakhala kuti arimoyo mukanapita kumeko Mai opanda manyezi iwe
Agogo agogo agogo 2025 kotsutsa boma woooooo
Ndipo nkhalamba izi
Abanda muziva chisoni ndi agogo.
Kkkkkk koma nde mwamuwonjeza chaponda kkkkkkk
Kkkkkkk yadwala nkhalamba ija
😂😂😂😂Dr George Chaponda
❤❤❤❤ Dpp
amuthalika akuchita kukakamizidwa kuti ayime koma munthu uja mafupa atopa popeza mtima sukalamba
Mafupa akalamba ndiabamboako kapeonyozamakoloako iwe mboliyakonso
Brain that is issue to close covetion,
Chipani chamagogo kkkkkk
Sindin wadpp kom ndakondw kwambir pomuchots chapond
Khangati mitu sikugwila amalawi chomwe timachifuna sitimachidziwa
Kusakhalapo osati chifukwa chokula kapena
Kkkkkkkk Brian Banda usadzafe udzangosowa
Use proper internet
Brian banda😂😂😂😂😂
Wakomoka amenewuja akudwala
Kkkkkkkkkkk koma yah😅😅😅😅
Next time Dont post video yot ikuduladulA, azungu azititseka
Tizakalamba koma ngati tizizakakamila mpando
wakulu uyu avomeleze
Sokhano watha bhooo what's wrong sanabweere iyaa nawe
Madala team
Wakalamba uyu
Iiiii musiyeni munthu akagone