HOT CURRENT ON TIMES TV 19/05/2024--CHAKWELA AVOMELEZA KUTI ZAMUVUTA TIVOTE LERO LOMWE

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 18 май 2024
  • #numeroyapastorntambabazi0788554028 #malawipolitics #news #duet #march2019 #bongotv #zodiaktv #humour #aford #31march
    watch ZODIAk CRUISE 5 WITH MLAKA Malilo part 2 here
    • ZODIAK CRUISE 5 NDI ML...
  • РазвлеченияРазвлечения

Комментарии • 14

  • @FosterChakanga
    @FosterChakanga 23 дня назад +3

    Amandiwaza makosanawa akati aseke😂😂ngati nkhosa zikulira mu khola😅😅😅😅😅

  • @YusufuKaifa-fr4wt
    @YusufuKaifa-fr4wt 23 дня назад +1

    Very nice conversation in this part I like you guys keep up helping malawian people's lives

  • @user-nk5mj5ws8v
    @user-nk5mj5ws8v 23 дня назад +2

    kodi atati amenyedwa a mcp achakwela angamango yang'ana achipani awo akumenyedwa

  • @aliwillardkundaje1083
    @aliwillardkundaje1083 23 дня назад +1

    Are they Malawians

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 20 дней назад

    Made in malawi always very expensive ,

  • @QualitySamuel-oz2uh
    @QualitySamuel-oz2uh 23 дня назад

    aaaaa inu chokani apa mitu youmayo ndinu mbuzi za mcp asakuziwani ndani

  • @user-rf4br1fv2z
    @user-rf4br1fv2z 23 дня назад

    Ndangwiliza nowe kodi chakwera akhoza kutuma anthu mukawateme mmmm ndizosatheka pena kodi amalakhulile kalindo munja ndili mu lilongwe muno ine sindimaopa ndine mwano oopsa amafuna anthu a mu lilongwe atani

  • @fredrickkhebozy6683
    @fredrickkhebozy6683 23 дня назад

    Eish

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d 23 дня назад

    Mmm

  • @user-rf4br1fv2z
    @user-rf4br1fv2z 23 дня назад

    Mukhalitsa kwa mcp basi kodi ku kamuzu stadium anthu ankaimba achoke ankafuna otsatila mcp atani bwanji osakambapo imeneyi dpp idali ndi msonkhano kodi a mcp adapita nkumakaimba agogo agogo kodi musamakondele timadziwa ndinu a south nonse ndi anthu ozizindikila kuposa madela ena kodi tizitukuko tikuchitikati bwanji osamauzapo amalawi madzi mangetsi pano bolani

  • @user-bi6pb5gc8t
    @user-bi6pb5gc8t 23 дня назад

    Zimenezo ndizimene ife tikufuna wina asanayambe ntchitoyo muziyamba kukawonamo Kuti asoyamo chani ndichani tatopa ndinyimbo yoti mboma tinapezamo mulibe chilichonse zimenezo ife zikutinyansa

  • @PhilipMatolino
    @PhilipMatolino 23 дня назад +1

    Guys to be honest chakwera walephera and palibe amene angasangalale kut chakwera azakhalenso pampando we r tired

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 23 дня назад

    Kodi atola nkhani inu why are you lying to Malawians? President amanena mobwelezabweleza kuti he doesn’t condone violence.
    Vuto ndi anthufe we need to take responsibility mtsogoleri sangalondere anthu 20 million tonsefe. Tisinthe tonse pathoka

    • @gamammwenye
      @gamammwenye 23 дня назад

      its in nature of humanism to be reluctant, thus laws are put in place to control the society. European countries and America have stiff Laws to maintain order. However MPs and OPC are our policy makers, so if there is no order in a society we blame the policy makers.