KU BLANTYRE KWATENTHA 🔥 🔥 🙌 🙌 🙌 NDI BON KALINDO

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 23 окт 2024

Комментарии • 187

  • @HEROTHATNOBODYCANCELEBRATE
    @HEROTHATNOBODYCANCELEBRATE 2 месяца назад

    Malawi first the people's first!!!,we can find pure diamonds without friction,let's go under friction so that we can find pure diamonds!!!.World belongs to the clever and strong pipo,Malawians let's be strong and very courageous courageous!courageous!

  • @BlessingsMaloya
    @BlessingsMaloya 2 месяца назад

    We need people like you kalindo,only legends know that your doing a good job pachilungamo suzasuntha,ifeso tizafera flag imeneyi

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 2 месяца назад +4

    Malawi first ❤❤❤❤ big up brothers and sisters

  • @amadichembe4068
    @amadichembe4068 2 месяца назад +4

    Mulungu akudalitseni, kulila kwa amalawi mulungu akulandileni Ameen

  • @NoreenNaituri
    @NoreenNaituri 2 месяца назад +1

    Mademo anthu 4 basi zachibwana zokhazokha

    • @laurentbutao4084
      @laurentbutao4084 2 месяца назад

      Figure ya wanthu ilibe ntchito,koma uthenga omwe munthu wapereka

  • @PeterMwakihana
    @PeterMwakihana 2 месяца назад +1

    We want change things are not working to be honest. Kalindo wooooooeeeeeeeee 😂😂🔥🔥🔥🔥

  • @Ghama-k4i
    @Ghama-k4i 2 месяца назад +1

    Blantyre The most loved city in South Nyasaland

  • @Edoliwonde
    @Edoliwonde 2 месяца назад

    Mvuto lako kalindo zi2 za clious ukulowetsa drama😂😂😂

  • @PatriciaChiwerenga
    @PatriciaChiwerenga 2 месяца назад +1

    Koma winiko ngati ndi chamba chikuphweteka😂😂😂😂😂😂😂

  • @SueWahna
    @SueWahna 2 месяца назад +1

    More fire malawi first 💪💪 Kom Mai akuyimika mkonoyo akundiwaza 😂😂 akhale adzanga😅

  • @EmmanuelkpPraise
    @EmmanuelkpPraise 2 месяца назад

    Malawi first keep it up the good job❤❤

  • @IanAllstal
    @IanAllstal 2 месяца назад

    Zokongola Bwanji 💪👉🇲🇼🇲🇼

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 2 месяца назад

    Our own pangoline the DC ❤❤big up all demonstrators mwatiyimirira mtima umakhumba km tatalikira .

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 2 месяца назад +2

    Uyu koma anafa kale samaopa ayi olo atazunguliridwa ndi asilikari achakwera .samaopa ayi koma uyu ndichisuro chosapindika 😂.uyu ndi ddengourous child for sure .wangoyamba kununkhatu

    • @JafaliChiwimbi
      @JafaliChiwimbi 2 месяца назад

      Ndipo uyu ndee anamaliza macheza

  • @laurentbutao4084
    @laurentbutao4084 2 месяца назад

    beautiful drama

  • @estherkachingwe3605
    @estherkachingwe3605 2 месяца назад

    God have mercy on Malawi 🇲🇼 🙏

  • @KondwaniGumba
    @KondwaniGumba 2 месяца назад

    Koma anthu ndi zitsiru kkkkk, MOTi akukhara busy ndi zopusa . Taona ma demo ife osati zamowa izi .

  • @johnmponda9070
    @johnmponda9070 2 месяца назад

    This Malawi first fighting for real

  • @FebbieNjewa-g3k
    @FebbieNjewa-g3k 2 месяца назад +2

    Keep it up abro,,God to guide n protect yu wherever yu go n whatever yu do n also the blood of Jesus Christ to cover yu from head to bottom n the whole body ,,God to keep yu under HIS canopy in Jesus christ name

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 2 месяца назад

    Police akuiona ngati yamao, The DC booooooon kalindo mwana oopsa kwambiri 🎉🎉🎉

  • @ElijahMoto-t4m
    @ElijahMoto-t4m 2 месяца назад +1

    The Dc chibooooon kalindooooo🔥🔥🔥🔥🔥kuti buuu

  • @JafaliTenda
    @JafaliTenda 2 месяца назад

    ❤❤❤❤ADALA ABAMBO MUMAKWAKWANA INUYO MUMATIYIRILA THE DCEE

  • @MikeTangah
    @MikeTangah 2 месяца назад

    Well done malawi first indeed chakwela achoke

  • @FillanyaudaNyauda
    @FillanyaudaNyauda 2 месяца назад

    I love this 💗💗💗💗💗 chakwera akagwele uko

  • @Mrssamalanngwira
    @Mrssamalanngwira 2 месяца назад

    Good job more fire 🔥🔥🔥🔥

  • @ChifuniroSaulosi
    @ChifuniroSaulosi 2 месяца назад

    Mpaka winiko amakomoka 😂😂😂😂😂 Ndye.....

  • @ThivadoartistDyson
    @ThivadoartistDyson 2 месяца назад

    Mulungu akutetezele kalindo antill governments changes

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 2 месяца назад

    Ukali 😊😊😊

  • @SummyBøy-m9f
    @SummyBøy-m9f 2 месяца назад

    Mr Bon kalindo🎉🎉🎉🎉 never give up let's go💪💪💪💪💪💪💪👍👍👍👍

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 2 месяца назад

    Malawi first wooooooooye go komkoooooooo i like you guys

  • @DorothyMasamba-zm7rf
    @DorothyMasamba-zm7rf 2 месяца назад

    Ndizoonadi ife sitinalembesedi ndiye tivota bwanji

  • @Kagansa
    @Kagansa 2 месяца назад

    ❤❤❤❤😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 booooon kalindo more 🔥 fire

  • @RichardMatumbo
    @RichardMatumbo 2 месяца назад

    Bon umakwana pitiliza kutelo mpaka Malawi abwelele mchimake😂

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4sc 2 месяца назад

    Power to the people, amalawi tiyenela ti vote,olo lD palibe.malawi,wthu uyu.achekwela,2025achoke.

  • @EmmanuelNgambi-y6h
    @EmmanuelNgambi-y6h 2 месяца назад

    Nkhani ikhale yoti chakwera achoke coz mavuto onsewa ndi chakwera

  • @SaidiBaneti
    @SaidiBaneti 2 месяца назад +3

    umakwa DC booono kalindo ❤❤❤❤❤

  • @PeterChombo-f5r
    @PeterChombo-f5r 2 месяца назад

    Ifetu a kalindo tili pambuyo panu ndipo osalola kupasidwa ndalama amalawi ambiri akuzuzika kwambiri

  • @PeterMasud
    @PeterMasud 2 месяца назад

    We like you Mr Dc

  • @SueWahna
    @SueWahna 2 месяца назад

    Chaka ndi chaka kulira chimanga nacho chakwera for me 😅😅😅😅😅😅

  • @Blessingskanyinji-x7s
    @Blessingskanyinji-x7s 2 месяца назад

    Woooow zoona boma ili linaloweradi mademo lizachokaso chifukwa chaa mademo

  • @OliverYehuru
    @OliverYehuru 2 месяца назад

    Mkangoo the DC

  • @CorneliusSande
    @CorneliusSande 2 месяца назад

    Kkkkkkkkk. Akuti nchiyani? Ozolowera kulandira agalu awa

  • @MchachaGoodson
    @MchachaGoodson 2 месяца назад

    Keep fire burning ❤❤❤ Born Kalindo

  • @ISHAQADAWDI
    @ISHAQADAWDI 2 месяца назад

    Maine bando yanga ndimaona ngati ndiona ofesi ya NRB ikupsyatu,amalawi ndife abata ndimtendere zedi mlooo🎉

  • @MussaAndreQuenessi
    @MussaAndreQuenessi 2 месяца назад

    Kkkkkkkkkkkk the dc sazatheka😂😂😂😂

  • @davidbulla5128
    @davidbulla5128 2 месяца назад

    Rest in Peace Bwana Saulos 😢😢😢Tikulilabe

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 2 месяца назад

    Anthu kulibe a bon manyazi akugwireni

  • @BlessingsmadalitsoShumba
    @BlessingsmadalitsoShumba 2 месяца назад

    ❤️‍🔥 more fire 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @MariaDavison-i6y
    @MariaDavison-i6y 2 месяца назад +1

    Big up

  • @lyiemax
    @lyiemax 2 месяца назад

    Powerful 💪💪 ❤❤❤🔥🔥🔥🔥

  • @Sabina-hw4js
    @Sabina-hw4js 2 месяца назад

    May God bless

  • @JosephyMbizi-k1w
    @JosephyMbizi-k1w 2 месяца назад

    🤓🤓🤓🤓 ndizoona izo

  • @KajogoloDawa-s6z
    @KajogoloDawa-s6z 2 месяца назад

    DC ukukhwana tili pambuyo pako osafooka

  • @EmmanuelBanda-u8t
    @EmmanuelBanda-u8t 2 месяца назад

    God have mercy on us dziko siyili bho ili🥴🥴🥴

  • @JoyceLiwonde
    @JoyceLiwonde 2 месяца назад

    Osafooka 🎉❤️‍🔥❤️‍🔥❤️‍🔥❤️‍🔥❤️‍🔥

  • @masianobrighton
    @masianobrighton 2 месяца назад

    Mademo anthu osakwana 100 koma anthu amasowa zochita eti kodi malaeo first ilibe donor kuti aziwapasa ndalama azitipasa aphawife bwaaa

  • @YusufDyton
    @YusufDyton 2 месяца назад

    Bon kalindo more fire

  • @stevejizaremu3396
    @stevejizaremu3396 2 месяца назад

    The DC ndi moto

  • @HypeGallery-ur9xd
    @HypeGallery-ur9xd 2 месяца назад

    Application awa ng'alula akumuona live

  • @YeremiyaPhiri
    @YeremiyaPhiri 2 месяца назад

    Masewera achabe ndalama zachepa mademo sangathandize

  • @SumayaOsman-de2dn
    @SumayaOsman-de2dn 2 месяца назад

    Kwende kwende che kalindo ku mangochi chakachi?

  • @GeorgeTembo-v6i
    @GeorgeTembo-v6i 2 месяца назад

    Good job kalindo

  • @EmmanuelNgambi-y6h
    @EmmanuelNgambi-y6h 2 месяца назад

    Umakwana DC

  • @ChikondiPendame
    @ChikondiPendame 2 месяца назад

    Good job more fire 🔥🔥🔥 the Bon Kalindo

  • @MaxWell-d7o
    @MaxWell-d7o 2 месяца назад

    😂😂😂😂kma kalindooo

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 2 месяца назад +3

    MCP already gone with Chilima believe me

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 2 месяца назад

    Malawi first❤❤❤❤❤

  • @MelayiLindaChiumia
    @MelayiLindaChiumia 2 месяца назад

    Mwana woophsa kwambili

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju 2 месяца назад

    The DC🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @PeterMasud
    @PeterMasud 2 месяца назад

    We like you Mr Dc 😢

  • @AiameAdamo-su1nt
    @AiameAdamo-su1nt 2 месяца назад

    Umakwana a DC ulemu wanu from Mozambique.

  • @SprianoJeke
    @SprianoJeke 2 месяца назад

    Until government intervene our plee

  • @solobertkamunga2826
    @solobertkamunga2826 2 месяца назад

    Bwana DC mwadya chamba chachabe😂😂

  • @EdnahShantell
    @EdnahShantell 2 месяца назад

    😂😂😂😂😂😂more fireeeee😅😅

  • @ErickTym-u2m
    @ErickTym-u2m 2 месяца назад

    Winiko ndikugulira jombo ya Argentina Canada uzivala Popanga mademo kkkk iweyo umatiyimilira

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms 2 месяца назад

    Yonse bho big man ❤❤❤❤

  • @BesterSengeledo
    @BesterSengeledo 2 месяца назад

    Umakwana DC keep it up

  • @MustafaAbdullah-pb5zv
    @MustafaAbdullah-pb5zv 2 месяца назад

    😂😂😂😂 make Malawi first a party pls winiko

  • @SaleemEid-sr5ph
    @SaleemEid-sr5ph 2 месяца назад

    Osatopa boma ili rinawibila mademo tilichotsaso mademo

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 2 месяца назад

    🔥🔥🔥🔥🔥

  • @siphe_viola
    @siphe_viola 2 месяца назад

    The kalindo

  • @NatashaBema
    @NatashaBema 2 месяца назад

    Tikufunaso kuno mademo.omwewo Winiko

  • @YeremiyaPhiri
    @YeremiyaPhiri 2 месяца назад

    Chipani cha mcp chidzatopa chonkha kulamulira chifukwa anthu azindikira kuti akalindo akufuna anthu amenyere udindo basi

  • @DanMhone-iw6xg
    @DanMhone-iw6xg 2 месяца назад

    Izooooooo

  • @MelayiLindaChiumia
    @MelayiLindaChiumia 2 месяца назад

    Bornkalindo mulungu akuteteze ndi kukudalisa

  • @Gmtmphats124gy
    @Gmtmphats124gy 2 месяца назад +1

    Ulemu wanu big man bon kalindo

  • @sunganibaroni1077
    @sunganibaroni1077 2 месяца назад

    Malawi first 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 2 месяца назад

    Akuti zamtudzu 😅😅😅😅😅😂😂😂🎉

  • @amadichembe4068
    @amadichembe4068 2 месяца назад

    👍🙏👌🤩👋👋👋👍

  • @FloraMweza-u7y
    @FloraMweza-u7y 2 месяца назад

    🔥🔥🙏

  • @JamesChirwa-o1f
    @JamesChirwa-o1f 2 месяца назад

    How can follow muthu wa ku gwa

  • @Aisha-db6ds
    @Aisha-db6ds 2 месяца назад

    Winiko km ndi boma palokha

  • @HarrisonMakunda
    @HarrisonMakunda 2 месяца назад

    Mulungu wathu sangatisiye boma ili likupita

  • @KondwanDuwe
    @KondwanDuwe 2 месяца назад

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 4:57 Chokomoka Chiwiniko chotsilu chamunthu ichiiiiiiiiiii

  • @GiftSoko-w4h
    @GiftSoko-w4h 2 месяца назад

    Keep it up big

  • @MusaManati-ho4zf
    @MusaManati-ho4zf 2 месяца назад

    Ambwiyeeeeeeee che bon kalindoooo

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 2 месяца назад

    More fire Born Kalindo Malawi I follow you

  • @JoãoChirwa-n3l
    @JoãoChirwa-n3l 2 месяца назад

    More fire ❤❤❤❤ the DES

  • @swinibanda5412
    @swinibanda5412 2 месяца назад +1

    Kkkkkkkkklk anthu kuchitakuoneka kuti kulibe nkhwimbi laanthu kkkkkkkk kufuna kutamika basi akalindo

  • @LawrentChabinga
    @LawrentChabinga 2 месяца назад

    Zaziiiii