Chitsilu ichi akuti chakwerayi akangokambapo atakhuta nsima yomwe imapezeka tikugula fetereza otchipa muthawi ya Peter osati zalerozi ulamulilo wausi one million Job or Jocks
Guys apapa Pali mawu a bakili muluzi tv??? Let's be serious mawu awo agaluwa akuwapweteka okha and because of manyazi they turn in kulimbana ndi anthu aphee tivomerezedi kuti tili mu one party regime
Chitsilu cha president,,, up to date still blinding Malawians but why chakwela? 1million jobs in what ways yet you gone through 4yrs and what you archive is kuba
Apeze Ntchito Kwaamkuno Mbuz Yobhibhira Muchimbudz Iyi Gwape
🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣zaziwika Kuti chakwera ndichilima ndimbava zopanda zelu out we don't need them again mbava
Bakili muluzi tv God bless you ❤❤❤
Bakili muluzi umakwanila balewanga God ahead u
This government has been extremely unsuccessful.
Exactly
😢malawi ifeyotu kukhanzikaku Koyenda sikufuna
kod tima sound tanuti munati tenga kt bigyy timandi waza kwabass🔥🔥🔥🔥 makamaka kena kaja kamandi vetsa kukoma hevyy my best tv 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🙏
Anayimba nyimboyi ndi a millenium sound checks zinavuta nchala cha 2000
Best TV ever
chilima is genius whether one's like it or not
Because of that mentality that why we are poor......
Innocent bwanali ndiwe wopembedza mafano kape
Aksnakhala genius sakanaputsitsidwa ndi MCP. Manifesto amenewa anabera Silvio Berlusconi wa ku Itally. Anachita kukupera ndendende.
Mutu wako sukuyenda bwino, go visit the doctor immediately
Keep informing us bro. Asatana akulamulawa ngolephera
Amene amalandira 35k 2019 amalandira ndalama zambiri kuposa amene alulandira 120k 2024 😢😢
Ndisamvenso kt mukumusaka wa bakiri muluzi TV mukumva kubomako
The grade of MCP government is "Undoubted Failure"=="E".
Samadziwa zomwe amayankhula achina chakwerawa amangoziyankhulira🤜👨
Keep it up brother mmakwana❤
Mbuzi ya president
Chitsilu ichi akuti chakwerayi akangokambapo atakhuta nsima yomwe imapezeka tikugula fetereza otchipa muthawi ya Peter osati zalerozi ulamulilo wausi one million Job or Jocks
Zowona kutinamidza ife akumangochi
😂😂 eeee ayi ndithu
Ulemu wanu brother ❤
This is great staff
Kkkkk chilungamo ndi mwano m,darayu walepela
Malawi sazatheka and we lost our hope
First watch
😂😂😂😂😂Malawi ngokoma
Odi ine ndipichire kwazizira
Kuno timangwila ntchito yosatifusa ma pepala aku school
Ndimomwemo alephela achoke bas ameneyo 😂😂
Wakuba ameneyo
Anthu ankati ayi m'busa apanga chilungamo!! Mbava yeniyeni
Chisilu cha president
Chikomekome cha nkhuyu mukati Muli Nyerere usogoreli alibe anthu Awa ndi akuba okhaokha
Bg brother mokupemba tatifufuzileni za hamas ndi israili plz
Best Tv
Mulungu wakumwamba akhululukire amalawi tonse chifukwa cha nsanje zomwe tilinazo chifukwa boma lomwe linalipo lija anthu munadana naro opanda chifukwa chokwanira lero tili ndizifukwa zonse zofika pamaso pa Mulungu nkugonja tinachimwa
The fact is that onsewa alephera a UTM ndi a MCP
Olikonda dziko la Malawi asavitere achakwera ndi achilima ,anthu awa asaukisa malawi kwambiri,asayese ngat omwe alikumaiko akunjawo sikuti mkufuna ayi koma kunganiza ndimomwe zithu zilili kuno ku Malawi
Wakuba nd m'bale wake m'busa 😅😅😅😅😅 koma Malawi
phwala lako iwe chakwera ndi chilimayo zitsiru zanthu
Kwankuno
Kkkk kwankuno😂😂😂 koma yaa that's why anasokoneza system yapassport
Atitopetsa atose agulu kobass
Mmmm
Aaah nyau alliance zolonjeza thoooo koma yeah abusa a ku bagamoyo
Good work big
Big up
Don't give up bakili muluzi
Zintchito lembani anu ndi abale anu ife ndi ana adadi bas palibe zobiza zanuzo zatikwana ife 😂😂😂😂
Iwe ndi 1 ase. Sanakugwirebe?
Airport mamanga ndiiti imodzi yokha, olo half ya Airport
Kodi abale Chakwerayu amagwa khunyu kapena?
Every presence has problem
mphamva izi anyapala anjala awa
Mmakwana brother ❤❤❤❤
Anthu away mbuzi dzaanthu asiyeni mulungu atimenyela nkhondo
Wayambaso kunama chakwera
Mi konda u bakili Muluzi TV
A Chilima ndi mayi Kaliati akuti ndi a ecclesia catholic kolona dii PAKHOSI ayi zikomo
Awa liyawo ndithu🤣🤣
DPP woye not much better ApM
Wabodza kwambiri Lazalo
Mapulani amenewa ozachita liti ameneyu kkkkkkkkk
Yonse alliance yonse mbuzi za wanthu .
Nyau yoputsa galu weniweni chakwera ndiwe mbuzi ya president moyenda bagamoyo watikwana
Mapwara anuoo
Instead to create job for Malawian he is busy giving his family and friends high position and get them government contacts
Guys apapa Pali mawu a bakili muluzi tv??? Let's be serious mawu awo agaluwa akuwapweteka okha and because of manyazi they turn in kulimbana ndi anthu aphee tivomerezedi kuti tili mu one party regime
International Airport Ku Nyika😂😂😂
Pa mtumbo pake chakwera ndi chilima wakeyo
Kodi inu muzalangidwa ndi yehova yemweyu analenga ifeyu kapena wina?
Eish anthu inuyo kma mulungu akukhululukireni
Most lovely TV in malawi and Malawian government the want to arrest the guy but why? Because he talks the truth about your corporations government
Koma iweyo chakwela aaaa unatinamizadi feteleza 4000 ndi khathu ai ambuye alowelelepo
Chakwera ndiwe muzi kwabasi mutu wake uwo ungange ntchito iwe?
Vise president alibe mphavu, don't hate vise president
Chakwela kod sangasamuke awone kolowela iya
Chakwela walephela
R u still remembering these kind of promises mr president and and his vice president mr Chilima?
President wake kuyankhula modekha ngati zenizeni koma zinazi
They are accountable
Chitsilu cha president,,, up to date still blinding Malawians but why chakwela? 1million jobs in what ways yet you gone through 4yrs and what you archive is kuba
Kkkkk maloto malemba athu 2 million wo
Mwalephela inu chanu palib
Koma ndale siungaivese please mupaseni mupata chilima
Apa ndipomwe ndimadziwa kuti kumwamba kulibe satana kma ali pansi pano shaaa. Ndizadina kulowa m'manda kma sizapanga mistake yosapota Munthu wandale ayi
Malawi. 2020 😂😂😂
Asatitukwanise galu ameneyi
❤
Best TV
chakwela ndiwe galu
Koma Malawi 🎉😂🎉😂
Tikayamba kumanga, airport, tikakhala ndi MA factory, too much promises
Nyani okuda kumaso
Kkkkkkkkk 😂 ndekwa nkunodi basi mwalephera kapumeni
🎉🎉
Chimbalangondo cha president ichi
Zonza abwana🙊🙊🙊
Manyaka
Mulungu akukhulukileni ndithu athu oipa inu kutengela boma phuzo mulungu adzakulangani chifukwa mau amanena kuti mulomo.wabodza sudzapuluka chilango
Chakwera pakamwa nkhati chimbudzi chofulasha chilima imvi nkhati mphaka
Too late bwana president next year your fired
Kodi achilimawa ATI m,chiyani munthu oyipauyu
Mkuluyu ndiwabodza kwambiri pano akunhoba ndalama zamisonkho zathu