Wa pa kaliyala akuyimba belu; Don't take malawians for granted.

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 5 окт 2024

Комментарии • 158

  • @shideshidex5679
    @shideshidex5679 4 месяца назад +15

    Apeze Ntchito Kwaamkuno Mbuz Yobhibhira Muchimbudz Iyi Gwape

  • @moyo77777
    @moyo77777 4 месяца назад +5

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣zaziwika Kuti chakwera ndichilima ndimbava zopanda zelu out we don't need them again mbava

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 4 месяца назад +2

    Bakili muluzi tv God bless you ❤❤❤

  • @MalakamMillie
    @MalakamMillie 4 месяца назад +6

    Bakili muluzi umakwanila balewanga God ahead u

  • @sweeneykamwendo6251
    @sweeneykamwendo6251 4 месяца назад +8

    This government has been extremely unsuccessful.

  • @MaliGomani-z4k
    @MaliGomani-z4k 4 месяца назад +8

    😢malawi ifeyotu kukhanzikaku Koyenda sikufuna

  • @ZaidJafar-kk9be
    @ZaidJafar-kk9be 4 месяца назад +2

    kod tima sound tanuti munati tenga kt bigyy timandi waza kwabass🔥🔥🔥🔥 makamaka kena kaja kamandi vetsa kukoma hevyy my best tv 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🙏

    • @GiboTakondwa
      @GiboTakondwa 4 месяца назад

      Anayimba nyimboyi ndi a millenium sound checks zinavuta nchala cha 2000

  • @Vincentmandota
    @Vincentmandota 4 месяца назад +6

    Best TV ever

  • @innocentbwanali7546
    @innocentbwanali7546 4 месяца назад +3

    chilima is genius whether one's like it or not

    • @JohnmarkNazombe-hi9xd
      @JohnmarkNazombe-hi9xd 4 месяца назад +3

      Because of that mentality that why we are poor......

    • @DouglasDazuKamwendo
      @DouglasDazuKamwendo 4 месяца назад +1

      Innocent bwanali ndiwe wopembedza mafano kape

    • @actuarialscience2283
      @actuarialscience2283 4 месяца назад

      Aksnakhala genius sakanaputsitsidwa ndi MCP. Manifesto amenewa anabera Silvio Berlusconi wa ku Itally. Anachita kukupera ndendende.

    • @BenjaminKamanga-p8w
      @BenjaminKamanga-p8w 4 месяца назад +1

      Mutu wako sukuyenda bwino, go visit the doctor immediately

  • @chimajrbhahat2334
    @chimajrbhahat2334 4 месяца назад

    Keep informing us bro. Asatana akulamulawa ngolephera

  • @NoelKhwimba-bh3ts
    @NoelKhwimba-bh3ts 4 месяца назад +1

    Amene amalandira 35k 2019 amalandira ndalama zambiri kuposa amene alulandira 120k 2024 😢😢

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 4 месяца назад +2

    Ndisamvenso kt mukumusaka wa bakiri muluzi TV mukumva kubomako

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 4 месяца назад +1

    The grade of MCP government is "Undoubted Failure"=="E".

  • @IshmaelAbdulHakeem
    @IshmaelAbdulHakeem 4 месяца назад +1

    Samadziwa zomwe amayankhula achina chakwerawa amangoziyankhulira🤜👨

  • @innocentnjoka7014
    @innocentnjoka7014 4 месяца назад +1

    Keep it up brother mmakwana❤

  • @GiftHaward
    @GiftHaward 4 месяца назад +2

    Mbuzi ya president

  • @powercharios2087
    @powercharios2087 4 месяца назад +1

    Chitsilu ichi akuti chakwerayi akangokambapo atakhuta nsima yomwe imapezeka tikugula fetereza otchipa muthawi ya Peter osati zalerozi ulamulilo wausi one million Job or Jocks

  • @MustafaMausen
    @MustafaMausen 4 месяца назад +1

    Zowona kutinamidza ife akumangochi

  • @JannatuyaseenmwangaMwanga
    @JannatuyaseenmwangaMwanga 4 месяца назад +1

    😂😂 eeee ayi ndithu
    Ulemu wanu brother ❤

  • @BrownMainje-sh7hj
    @BrownMainje-sh7hj 4 месяца назад +1

    This is great staff

  • @JohnGavinara
    @JohnGavinara 4 месяца назад +1

    Kkkkk chilungamo ndi mwano m,darayu walepela

  • @robertthawie3334
    @robertthawie3334 4 месяца назад +1

    Malawi sazatheka and we lost our hope

  • @KalongaKachipi
    @KalongaKachipi 4 месяца назад +1

    First watch

  • @chifundolipenga270
    @chifundolipenga270 4 месяца назад

    😂😂😂😂😂Malawi ngokoma
    Odi ine ndipichire kwazizira

  • @AustinManes-m3w
    @AustinManes-m3w 4 месяца назад +1

    Kuno timangwila ntchito yosatifusa ma pepala aku school

  • @HassanSinoya-wl3vl
    @HassanSinoya-wl3vl 4 месяца назад

    Ndimomwemo alephela achoke bas ameneyo 😂😂

  • @JoiceStanley
    @JoiceStanley 4 месяца назад +2

    Wakuba ameneyo

  • @chimajrbhahat2334
    @chimajrbhahat2334 4 месяца назад

    Anthu ankati ayi m'busa apanga chilungamo!! Mbava yeniyeni

  • @SadamBito
    @SadamBito 4 месяца назад

    Chisilu cha president

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 4 месяца назад

    Chikomekome cha nkhuyu mukati Muli Nyerere usogoreli alibe anthu Awa ndi akuba okhaokha

  • @JoeMuhamadi
    @JoeMuhamadi 4 месяца назад

    Bg brother mokupemba tatifufuzileni za hamas ndi israili plz

  • @VitumbikoKumwenda-sd1uo
    @VitumbikoKumwenda-sd1uo 4 месяца назад

    Best Tv

  • @User_n6-8n
    @User_n6-8n 4 месяца назад

    Mulungu wakumwamba akhululukire amalawi tonse chifukwa cha nsanje zomwe tilinazo chifukwa boma lomwe linalipo lija anthu munadana naro opanda chifukwa chokwanira lero tili ndizifukwa zonse zofika pamaso pa Mulungu nkugonja tinachimwa

  • @JacksonMoyo-tm8dv
    @JacksonMoyo-tm8dv 4 месяца назад

    The fact is that onsewa alephera a UTM ndi a MCP

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 4 месяца назад

    Olikonda dziko la Malawi asavitere achakwera ndi achilima ,anthu awa asaukisa malawi kwambiri,asayese ngat omwe alikumaiko akunjawo sikuti mkufuna ayi koma kunganiza ndimomwe zithu zilili kuno ku Malawi

  • @rexphiri7242
    @rexphiri7242 4 месяца назад

    Wakuba nd m'bale wake m'busa 😅😅😅😅😅 koma Malawi

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 4 месяца назад +1

    phwala lako iwe chakwera ndi chilimayo zitsiru zanthu

  • @Amgwagwa
    @Amgwagwa 4 месяца назад +1

    Kwankuno

  • @Aubreysekeyah
    @Aubreysekeyah 4 месяца назад

    Kkkk kwankuno😂😂😂 koma yaa that's why anasokoneza system yapassport

  • @QassimuKatsobola
    @QassimuKatsobola 4 месяца назад +1

    Atitopetsa atose agulu kobass

  • @FelistasNkasalaMakumbo
    @FelistasNkasalaMakumbo 4 месяца назад +1

    Mmmm

  • @HarryKandani
    @HarryKandani 4 месяца назад

    Aaah nyau alliance zolonjeza thoooo koma yeah abusa a ku bagamoyo

  • @abisalomchunga6695
    @abisalomchunga6695 4 месяца назад

    Good work big

  • @PatsonFundi-ie2fm
    @PatsonFundi-ie2fm 4 месяца назад

    Big up

  • @IliyasaYusuf
    @IliyasaYusuf 4 месяца назад

    Don't give up bakili muluzi

  • @Oscarzebron
    @Oscarzebron 4 месяца назад

    Zintchito lembani anu ndi abale anu ife ndi ana adadi bas palibe zobiza zanuzo zatikwana ife 😂😂😂😂

  • @JoshuaMhango-tf2kh
    @JoshuaMhango-tf2kh 4 месяца назад

    Iwe ndi 1 ase. Sanakugwirebe?

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 4 месяца назад

    Airport mamanga ndiiti imodzi yokha, olo half ya Airport

  • @FreddieMatuta
    @FreddieMatuta 4 месяца назад

    Kodi abale Chakwerayu amagwa khunyu kapena?

  • @GeorgeMphale-n8q
    @GeorgeMphale-n8q 4 месяца назад

    Every presence has problem

  • @sanlakedickson6780
    @sanlakedickson6780 4 месяца назад +1

    mphamva izi anyapala anjala awa

  • @RichardSauti-n8p
    @RichardSauti-n8p 4 месяца назад

    Mmakwana brother ❤❤❤❤

  • @WysonAdamu
    @WysonAdamu 4 месяца назад

    Anthu away mbuzi dzaanthu asiyeni mulungu atimenyela nkhondo

  • @EnerstManess
    @EnerstManess 4 месяца назад

    Wayambaso kunama chakwera

  • @lusolawo73
    @lusolawo73 4 месяца назад +1

    Mi konda u bakili Muluzi TV

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 4 месяца назад

    A Chilima ndi mayi Kaliati akuti ndi a ecclesia catholic kolona dii PAKHOSI ayi zikomo

  • @Jermah51kennias
    @Jermah51kennias 4 месяца назад

    Awa liyawo ndithu🤣🤣

  • @JEFFERYJUMA
    @JEFFERYJUMA 4 месяца назад +1

    DPP woye not much better ApM

  • @KennethKadawati-jc1el
    @KennethKadawati-jc1el 4 месяца назад

    Wabodza kwambiri Lazalo

  • @MathewMandutu
    @MathewMandutu 4 месяца назад

    Mapulani amenewa ozachita liti ameneyu kkkkkkkkk

  • @ashikalam8616
    @ashikalam8616 4 месяца назад

    Yonse alliance yonse mbuzi za wanthu .

  • @mrsmoseskita9180
    @mrsmoseskita9180 4 месяца назад

    Nyau yoputsa galu weniweni chakwera ndiwe mbuzi ya president moyenda bagamoyo watikwana

  • @SyilesChebomba
    @SyilesChebomba 4 месяца назад

    Mapwara anuoo

  • @prayphiri3184
    @prayphiri3184 4 месяца назад

    Instead to create job for Malawian he is busy giving his family and friends high position and get them government contacts

  • @jameschibisa1433
    @jameschibisa1433 4 месяца назад

    Guys apapa Pali mawu a bakili muluzi tv??? Let's be serious mawu awo agaluwa akuwapweteka okha and because of manyazi they turn in kulimbana ndi anthu aphee tivomerezedi kuti tili mu one party regime

  • @giftmasenti5732
    @giftmasenti5732 4 месяца назад

    International Airport Ku Nyika😂😂😂

  • @ThomasShuga
    @ThomasShuga 4 месяца назад

    Pa mtumbo pake chakwera ndi chilima wakeyo

  • @OusmanDavie
    @OusmanDavie 4 месяца назад

    Kodi inu muzalangidwa ndi yehova yemweyu analenga ifeyu kapena wina?
    Eish anthu inuyo kma mulungu akukhululukireni

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 4 месяца назад

    Most lovely TV in malawi and Malawian government the want to arrest the guy but why? Because he talks the truth about your corporations government

  • @HedgensChisale
    @HedgensChisale 4 месяца назад

    Koma iweyo chakwela aaaa unatinamizadi feteleza 4000 ndi khathu ai ambuye alowelelepo

  • @fumbomumba5016
    @fumbomumba5016 4 месяца назад

    Chakwera ndiwe muzi kwabasi mutu wake uwo ungange ntchito iwe?

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 4 месяца назад

    Vise president alibe mphavu, don't hate vise president

  • @andrewmtendere3167
    @andrewmtendere3167 4 месяца назад

    Chakwela kod sangasamuke awone kolowela iya

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 4 месяца назад

    Chakwela walephela

  • @rashidsaid2232
    @rashidsaid2232 4 месяца назад

    R u still remembering these kind of promises mr president and and his vice president mr Chilima?

  • @SimonBanda-b1f
    @SimonBanda-b1f 4 месяца назад

    President wake kuyankhula modekha ngati zenizeni koma zinazi

  • @petrokagona1708
    @petrokagona1708 4 месяца назад

    They are accountable

  • @BFWCPHIRI1978
    @BFWCPHIRI1978 4 месяца назад

    Chitsilu cha president,,, up to date still blinding Malawians but why chakwela? 1million jobs in what ways yet you gone through 4yrs and what you archive is kuba

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 4 месяца назад

    Kkkkk maloto malemba athu 2 million wo

  • @EvansNaphazi
    @EvansNaphazi 4 месяца назад

    Mwalephela inu chanu palib

  • @AndrewNgwira-d9p
    @AndrewNgwira-d9p 4 месяца назад

    Koma ndale siungaivese please mupaseni mupata chilima

  • @OusmanDavie
    @OusmanDavie 4 месяца назад

    Apa ndipomwe ndimadziwa kuti kumwamba kulibe satana kma ali pansi pano shaaa. Ndizadina kulowa m'manda kma sizapanga mistake yosapota Munthu wandale ayi

  • @BiyolaMwashithu
    @BiyolaMwashithu 4 месяца назад

    Malawi. 2020 😂😂😂

  • @tisuhmakhwah7085
    @tisuhmakhwah7085 4 месяца назад

    Asatitukwanise galu ameneyi

  • @EnockSaiwa
    @EnockSaiwa 4 месяца назад

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 4 месяца назад

    Best TV

  • @LangfordMabaso-z7u
    @LangfordMabaso-z7u 4 месяца назад

    chakwela ndiwe galu

  • @PromiseKhenzo
    @PromiseKhenzo 4 месяца назад

    Koma Malawi 🎉😂🎉😂

  • @xxxrepair
    @xxxrepair 4 месяца назад

    Tikayamba kumanga, airport, tikakhala ndi MA factory, too much promises

  • @alfredpindani9045
    @alfredpindani9045 4 месяца назад

    Nyani okuda kumaso

  • @JafarAnusa-s9g
    @JafarAnusa-s9g 4 месяца назад

    Kkkkkkkkk 😂 ndekwa nkunodi basi mwalephera kapumeni

  • @EmmanuelGordon-q9s
    @EmmanuelGordon-q9s 4 месяца назад

    🎉🎉

  • @feehasaidid.r.d
    @feehasaidid.r.d 4 месяца назад

    Chimbalangondo cha president ichi

  • @DanielZitande-y1d
    @DanielZitande-y1d 4 месяца назад

    Zonza abwana🙊🙊🙊

  • @HamzaAyame-ch3et
    @HamzaAyame-ch3et 4 месяца назад

    Manyaka

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w 4 месяца назад

    Mulungu akukhulukileni ndithu athu oipa inu kutengela boma phuzo mulungu adzakulangani chifukwa mau amanena kuti mulomo.wabodza sudzapuluka chilango

  • @DonaldPonda-p2q
    @DonaldPonda-p2q 4 месяца назад

    Chakwera pakamwa nkhati chimbudzi chofulasha chilima imvi nkhati mphaka

  • @LaddinShaibu
    @LaddinShaibu 4 месяца назад

    Too late bwana president next year your fired

  • @GiftChitsulo
    @GiftChitsulo 4 месяца назад

    Kodi achilimawa ATI m,chiyani munthu oyipauyu

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 4 месяца назад

    Mkuluyu ndiwabodza kwambiri pano akunhoba ndalama zamisonkho zathu