Ndipo ndizoonadi tilipo ambiri tinachokako ku Malawiko khani kulibe ndalama pano tili ndi zaka 7 panopa mu Botswana timafuna kubwera kumeneko koma kwacha yakeyo 😂😂
Abon kalindo.....point of correction;Chilimatu sanali munthu wabwino ndipo balibe chabwino chomwe anachitira amalawi...km a malawi akuonetsa kut ali kumbuyo kwake chifukwa cha mmene adaphedwera ndi MCP..Km musanene kut akanasintha zinthu...he was the worst
Kudziva ndi kudzikuzi ndi kulalatila ena chifukwa cha ntchito yomwe umagwila zimangosonyeza umbuli Pa ntchito yakoyo, uyembekezele zinthu ziwili pa ntchito yakoyo kuchotsedwa kapena kufa,,,
Powerful speech and strong advice from our beloved president, the Dddddd Cccccc ❤❤❤
Good speech mr kalindo❤❤❤.but chakwera vuto ndi mphawi Ndiye akuona ngati kuti akatula pansi udindo asauka.Sinanga umphawi unamphweteka kwambiri.
Good advice... 🔥
The D.C BORN KALINDO!!!!!!!!! ZAMBIA HERE LUSAKA
Achinyamata anzanga tiyeni tisegule maso ,osamaimbira mmanja zisilu let's be wise and open our eyes 👀
Aaaaaa kodi mtsikana iwe kalindo ulipo uasatisokosere mutu wokhala Ngati mbinawo galu 😅
Power massage and power unity
More 🔥.
Strong voice
nanga mmene zililimu palichifukwa chovootera muthalikaa?
Boooorn kalindo
Mr boni kalindo tikudalira inu
Ndipo ndizoonadi tilipo ambiri tinachokako ku Malawiko khani kulibe ndalama pano tili ndi zaka 7 panopa mu Botswana timafuna kubwera kumeneko koma kwacha yakeyo 😂😂
Ndipo zoonad sukunama the DC woyeeeee
Iweyo ndiwa mfundo kuposa manganya sure
Ndimalondola khani za bon kalindo nkhani zimandingila mtima koma video ndiimozi naimozi?
Munyamata opusa ndi amene akulandila 2000 ndikuononga chilungamo wachinyamata opusa ndi amene akusangalala ndi ngongole yomwe singamupindulire . Tachinyamata sitikufuna kupita kumaiko akunja tikufuna ziko lanthu mukhale ntchito tizigwira muziko mwanthu tiyeni tizuke . Opposition wamphavu kumalawi ndi DC tantiwa bakili TV kalua game changer munyanyiwa . Anthu inu muyambise chipani kumalawi kuzasintha simukufuna kubera amalawi komaso mumayima pa chilungamo. Osagulidwa ndi ndalama ngati ena.kuti president wako wamwalira mosaziwika bwino iwe 7 days ndikulandira udindo pali zeru
Manganya alindinzeru chisilu cha munthu chimenechi chopanda mfundo fotseki
Uthenga wachilimbikitso ndipo watisegula maso
Viva kalindooooo
Abon kalindo.....point of correction;Chilimatu sanali munthu wabwino ndipo balibe chabwino chomwe anachitira amalawi...km a malawi akuonetsa kut ali kumbuyo kwake chifukwa cha mmene adaphedwera ndi MCP..Km musanene kut akanasintha zinthu...he was the worst
IWE NDAGWIRIZANA NAWE
The DC please kapangeni mademo lero kumangochi chifukwa chakwera walawila lero kumeneko akut akuyendara mmafamu kumeneko Ky akufuna chani😂😂😂😂Ife ctikufuna the DC ndipo pelekelani micro foni kumeneko mutiuuze zosatila💪💪💪
The Dc bon kalindo good Messnge ❤
Bravo No Retreat No Surrender
Kudziva ndi kudzikuzi ndi kulalatila ena chifukwa cha ntchito yomwe umagwila zimangosonyeza umbuli
Pa ntchito yakoyo, uyembekezele zinthu ziwili pa ntchito yakoyo kuchotsedwa kapena kufa,,,
Perfect talk the DC.
Let's open our eyes guyz
Apo walankhula mosaopa
The DC...💓
Dolo kwambiri
❤❤
Zoonadi Amfumu
T̈ḧë DC
K̈ẅb̈r̈ l̈ïv̈ë
Zoliboh
The deceeee