Ndege munthu ndiyomwe inachita iziiiii Anthuwatu akuona ngati amalawi tikadali ntulo sakudziwa kuti tinachangamukaaa Muzionaa ndipo muyankha mafuso onsewa kwa amalawi and to the whole world Mfiti Chakwera
Ndikangolowa pa RUclips choyambilila ndi mafuna ndi mvele Limpopo fm koma ka melody mumaikaka kamatalika kwambiri musanayambe kulankhula ofcourse ndika bwino koma kasamatalike kwambiri nthawi Zina timakhala tili pachangu nde kamatipangisa kuti tisamalize kuvela
That’s true Vs president he was going for funeral with suit and tie now he body is nicked so how take out his clothes is look like something that does happen, am very sorry what happened to him and died like thief and Chikwara he is proud like nothing happened
Inetu ndi mathokoza kwambiri a Limpopo FM ndipo ndadziwa ndale chifukwa cha Limpopo FM pitirizani kutipatsira nkhani zonse mulungu adzikudalitsani bambo muthwanyiwa
The best fm ,,, listening from Botswana I can't wait ❤❤❤❤
Munthu amene amadana ndilimpopo ameneyo ndifiti
My best ❤ Limpopo FM radio
I can't believe it that our brother is gone just like that No No
Limpopo following 🙏
SKC and others who died Rest in Eternal Peace 😢😢😢
Were in Zambia but our hearts our bleeding
Masowela aaah yoooo timbwela from Zambia
Congratulation Mr mtanyiwa gp🎉❤❤❤
Ntanyiwa komaso bakili muluzi these guys i salute 💪
Mulungu akukuteni kut onyansa mtima awa osowa umunthuwa
Asamakufikireni komano big tawakumbuseni a DPP Asiya uchetewawu adzuke
Listening from cosmo city, just here malibongwe drive south Africa ❤❤❤❤❤🎉🎉🎉🎉🎉 Comrade!!! tili limodzi apa✅✅✅🇲🇼💪💯
Ntanyiwa katundu owopsa zedi ❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Ndege munthu ndiyomwe inachita iziiiii
Anthuwatu akuona ngati amalawi tikadali ntulo sakudziwa kuti tinachangamukaaa
Muzionaa ndipo muyankha mafuso onsewa kwa amalawi and to the whole world Mfiti Chakwera
Inuyo ndi one ndpo sindmafuna pazidusa one hour tisanakumven mau nice big man
Chairman ndinga pange bwanji ndizikutumizilani khani
Comrade Ntanyiwa .God bless you,protect you,guide you and entire family.
SKC soul im sure ukukuyanganilani Comrade ,and the entire Limpopo DJ's🙏🙏.
Nkhanga zikungoyenela ziziona👀👀👀👁️.
Uku tikusala kudya ndi kupemphela ,chilungamo chioneke ndithu.
Limpopo 🎉🎉🎉🔥🔥🔥🔥🔥 moto kuti buu !!!!, 🔥🔥🔥
Listening 🎧 from springs
A Ntanyiwa chifuwa SI chipha osatekeseka..imwani madzi ochuluka
Limpopo FM 💪💪
Pheee,pano pa limpopo ndi comrade mtanyiwa
Dzoooona osamalimbana nawo inu pangani ubwedzi ndmlungu osati munthu odzuza thupi ndyesu yekha oteteza lnuyo antanyiwa❤❤❤❤
The best Limpopo FM radio station is the one 🔥🔥🔥🔥
Thanks for your update Big Baba
Limpopo to the world 🌍
Bwana timakukondani ndipo timakunyadirani chifukwa mumatidziwitsa chirichose
Hehehehehe yomweyo galu iwe awuzeneni amvese comred ntanyiwa
Timakunyadirani alimpopo fm
Tikusatira mwachidwi ndinthu ndipo alimpopo mukat musatumize uthenga ndinadandaula kobas andi bon kalindoso ulemu wanu pitizan kuima pachilungamo mulungu alinanu nonse mudzina layesu mulungu wamoyo
Ndiponso chigwada chake chimakhala chosinja kale😂😂😂 Mr ntanyiwa mumayidziwanso Randburg????😂😂 I love u Mr mumakwana Enawa ndi Ana awa❤❤❤🎉🎉🎉
A chair man
RIP SKC, kodi nanga anthu 8 enawo imfa zawo zinali zotani? Pamenepa sipakumalongosoredwa
Mukhale ndi moyo wautali comrade ntanyiwa anthuwo angodana nanu akusowa zochita chifukwa mumanena chilungamo
Ngati chilima anaphedwa ndiye kut onse anaphedwa , kaya ndingozi ndiye kut onse ngozi eeeeetu
Iwe ulingati m,zimayi mabodza umangoduladula nkhani osayimaliza kuchita kudziwika kuti ndiwe wamabodza iwendiwe galu wachabechabe nakutuluka
Akutimenyera nkhondo anyamata awa amphawife😭😭😭😭😭😭😭
Listening from randburg..
Same to me
Mmatiimirira bwana
Congratulation mr mtanyiwa❤❤❤
limpopo fm ft bakili muluzi tv 🔥🔥🔥🔥
God pleasease,, protect ntanyiwa Abeg 🙏
Limpopo FM❤❤
Ma demo akanapanga pa 20 coz ana pa 10 akhalabe akulemba mayeso
Ntanyiwa sing'anga amuka drip yamadzi atapita kukathamangitsa mizimu mwaterooo😂😂😂😂
Nthanyiwa umakwana timakunyadila MCP ndiyamagazi mmaja kuyambira kale
TAnyiwa we are defending Malawi
Bwana Mtanyiwa gwirani ntchito Basi osalimbana ndizinazi zikuiwalitsani zochita
Limpopo tiziwiseni munthu ama munkhapa chilimayo timuziwe
I ❤ Limpompo fm
Yes anawavula ndani?? Poti ndege ilibe manja 😅
Kkkkkkkkkkkk yochita zonsezi ndege yomweyo? 😂😂😂😂❤❤🇲🇼🇲🇼🇲🇼
The problem is that ayesetsa kuti akuchiteni chipongwe koma alephera anthuwa Comrade ndiye nzeru zatha
More fire
We can't 10 July come one come all their see
Demonstrations a kulu timbwela better there tell us🌟 the 😭 truth why there killed our brother
Ndipo inuyo munasowa😂😂😂😂
Limpopo ndi namber one
Eeeeee imfa iyi ikupweteka ukailingalira, Ambuye kumwambako mumadziwa zonse😢😢
Mzimu wa Chilima itipatsanso hope ina mayooooooo ine A Chilimaaaaa😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
We are not young GOD is watching
Mbambande mtanyiwa❤
Ndikangolowa pa RUclips choyambilila ndi mafuna ndi mvele Limpopo fm koma ka melody mumaikaka kamatalika kwambiri musanayambe kulankhula ofcourse ndika bwino koma kasamatalike kwambiri nthawi Zina timakhala tili pachangu nde kamatipangisa kuti tisamalize kuvela
Vgg🎉
Ndipo mulungu azikudalisani
This is sad for sure
That’s true Vs president he was going for funeral with suit and tie now he body is nicked so how take out his clothes is look like something that does happen, am very sorry what happened to him and died like thief and Chikwara he is proud like nothing happened
Umatha ase
Kkkkkkkkkkk koma zidyamula nandolo
Tizapindula
Iweyo Ntanyiwa ndi number one ndipo ndimamva nawe kukoma zed. Ndipo timamva zenizeni
Koma nde Apengedi misala mwinanso anachita kuyitanidwa kuti atsekedwe pakamwa nkona adzibusa Mafumu ndi ena azipembezo zosiyana siyana akukhala phe kumangoyang, anila dziko likungowonongeka chifukwa chodya chibanzi Mulungu akulangeni nonse amene mukungolandila ndalama koma chilungamo mukuchidziwa
Koma nde okapanga kidnap wo adzafera konkotu
Oyenela kupepesedwa ndi akubanja km chakwela anapepesa ndi 5milioni ndizovesa chison kt chakwela akugawa ndalama kwa anthu omwe malilo sakuwakhuza tichedwepo pamenepa
NTANYIWA MBAMBANDE , KOMA VUTO NDI ROTI MAFUMU NDI ANTHU ADYERA KOMASO MA BISHOP MITUYAO SIGWIRA NTCHITO, NDIPO MAFUMUWA AKUFUNIKA KUWAGWIRA PAKHOSI KOMASO MA BISHOP NDI ANTHU OTI SANGATHANDIZE DZIKO CHIFUKWA MWAIWO U MULUNGU MULIBE MWSIO MEADZAZA NDI DYERA MALO MIYANG'ANA DZIKO MOMWE LIKUYENDERA NAONSO.TIWAPANGIRA MADEMO NGATI SAKUDZIWA ASATIONONGERE DZIKO CHIFUKWA CHADYERS LAO IYAAAAAA
Inetu ndi mathokoza kwambiri a Limpopo FM ndipo ndadziwa ndale chifukwa cha Limpopo FM pitirizani kutipatsira nkhani zonse mulungu adzikudalitsani bambo muthwanyiwa
Siziwona
Khumbo la apolisi anthu komanso a army, ma doctors,amphuzitsi....its just better life not to be rich
Ku Randburg ndinapezako mbewa ndi ngumbi
Mbambande Limpopo
Limpopo mumakwana from Cape Town
Apatsa Ambuyache mafiti opephera km mulungu awayendele
Hand mistake sorry I want to press like ❤😂
Chobisika chili chose timavera kuchokera kwa limpopo FM kuchokera kwa khomuredi Ntanyiwa mumati vesa kukoma kwambili ndpo timaku pephelerani kwambili ndpo oyipayo sangaku kwaniseni kt akupangeni chipogwe ndpo mulungu apitilize kukutetezani mix born kalindo mulungu apitilize kukusungani ndimoyo wautari pa libe radio iliyose yomwe ingatiuze zoona zokha zokha ndi limpopo yokha bas mulungu apitilize kukumenyerani khondo nose
Rip our vp
Missing dear ❤
Our last hope Limpopo fm
Following ine zanga phee mix lawyer ndilibe kkkkkk
A Ntanyiwa mumatha
Limpopo ndekuti chani
Uyu ndi machine owopsa zedi Ntanyiwa❤❤❤❤❤❤❤
Akufuna ma vote a chakwela kuti mafumuwo akalimbikitse anthu awo akati tiyeni timvotele MCP
Ayelekeze kupanga kidnap anawo awone zomwe zichitike mmanyumba mwawo asatana amenewa 👺👹👿☻
Koma Limpopo ikubwera boh
Galu iwe mesa paja umapepha ndalama kuti network Yako ikuvuta kkk koma iwe eti
Ndipo tisaladi kudyako chilungamo chioneke basi
Nkhani zodabwitsatuu iziiii
Kodi photo ya a chilima yogwira kolona alipo angandionese?
Mumakwana inuyo big
🙏🙏🙏🙏
Chimene akufunira kuti apange kidnap ana athu mchiyani?, ana alakwa chiyani?, even omenyera ufulu athu a genuine mmalawi muno alakwa chiyani?, tiwonensanaa ,
Limbikilani
Mukhala aboza sitizikukhulupirirani. Kamaulusani nkhani zoona
Zamphavu ntanyiwa
Katundu omanga ndizisulo
Kkkkkkkk ndiwe galu kwambili eti
Siwe munthu wamba adha umakwana
😅